< Luka 12 >

1 Nthawi yomweyo, anthu miyandamiyanda atasonkhana, ndi kumapondanapondana, Yesu anayamba kuyankhula poyamba kwa ophunzira ake, nati, “Chenjereni ndi yisiti wa Afarisi, amene ndi chinyengo.
Mipui isâng tamtak, inkhat le inkhat insirpolin Jisua an bôma. Jisua'n a ruoisingei kôma, “Pharisee asarotholngei chol renga singthei roi.
2 Palibe chinthu chophimbika chimene sichidzawululika, kapena chobisika chimene sichidzadziwika.
Jâttin ihîpa om la phong nîng a tih, a ipa om khom la phuongsuok nîng a tih.
3 Chimene mwanena mu mdima chidzamveka dzuwa likuwala, ndipo zimene mwanongʼona mʼkhutu mʼchipinda chamʼkati, zidzayankhulidwa pa denga la nyumba.
Masikin, ajînga nin ti ngei hah sûn khovâra lân phuong nîng a ta, khâltan sûnga kuor kunga nin ti ngei hah inchunga chuongin tânghâi la nîng a tih,” a tipe ngeia.
4 “Ine ndikuwuzani, abwenzi anga, musachite mantha ndi amene amapha thupi chifukwa akatero sangachitenso kanthu.
Ka malngei nangni ki ril, ei takpum that suonûka, ite mi lo thei khâiloi chu chi no roi.
5 Koma Ine ndidzakuonetsani amene muyenera kumuopa: Wopani Iye, amene pambuyo pakupha thupi, ali ndi mphamvu yakukuponyani ku gehena. Inde, Ine ndikuwuzani, muopeni Iye. (Geenna g1067)
Tumo nin chiruo nangni ril ki tih. Thi nûk khoma, dûkmuna nangni pai theina rachamnei ani sikin, Pathien chi roi, ani, nangni ki ti, Ama vai chi roi. (Geenna g1067)
6 Kodi atimba asanu samagulidwa ndi ndalama ziwiri? Ngakhale zili chomwecho palibe imodzi ya izo imene imayiwalika ndi Mulungu.
Invate rangnga poisa nikin an juor ngâi ni mak mo? Ania, Pathien'n chu inkhat te luo hah mingil ngâi mak.
7 Ndithudi, tsitsi lonse la mʼmutu mwanu ndi lowerengedwa. Musachite mantha; inu ndi oposa kwambiri mpheta zambiri.
Nin lu chunga nin samngei tena khom itelvar kêng. Masikin, chi no roi, invate tamtak nêkin nin lut uol.
8 “Ine ndikukuwuza kuti, aliyense amene avomereza Ine pamaso pa anthu, Mwana wa Munthu adzamuvomerezanso pamaso pa angelo a Mulungu.
“Nangni ki ril, tutu lôko rieta ni thop kai chu, Miriem Nâipasal khomin Pathien vântîrtonngei makunga thop a tih.
9 Koma iye amene andikana Ine pamaso pa anthu adzakanidwanso pamaso pa angelo a Mulungu.
Tutu lôko rieta ni hengpai kaichu, Miriem Nâipasal khomin vântîrtonngei makunga hengpai a tih.
10 Ndipo aliyense amene ayankhulira Mwana wa Munthu mawu oyipa adzakhululukidwa, koma iye wochitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa.
Tutu Miriem Nâipasal rilsiet chu ngâidam nîng a ta, Ratha Inthieng rilsiet chu ngâidam nino nih.”
11 “Akadzakutengerani ku masunagoge pamaso pa oweruza ndi a maulamuliro, musadere nkhawa mmene mudzadzitchinjirizire nokha kapena chimene mudzayankhule,
“Hanchu, nin roi jêk rangin synagog mo, governor makunga mo, roijêkpungei makunga mo, nangni an tuong tikin, inmo ki thuon rang, imo ki ti rang, tiin nin mulung min jîng no roi.
12 pakuti Mzimu Woyera nthawi imeneyo adzakuphunzitsani zoyenera kunena.”
Nin ti rang chu a zora tika Ratha Inthiengin nangni ril a tih.”
13 Munthu wina mʼgulu la anthu anati kwa Iye, “Aphunzitsi, muwuzeni mʼbale wanga andigawireko chuma chamasiye.”
Mipui lâia mi inkhatin Jisua kôma, “Minchupu, Ka lâibungpa kôm, kin pa rochon mi mâk pe mi sem rangin tipe roh,” a tia.
14 Yesu anayankha kuti, “Munthu iwe, ndani anandiyika Ine kukhala woweruza kapena wogawa chuma pakati panu?”
Jisua'n a thuona, “Mala, nangni inik chungroi jêk rang le nin rochon sem rangin tumo roineina mi pêk?” a tia.
15 Kenaka Iye anawawuza kuti, “Chenjerani! Khalani tcheru ndi makhalidwe onse adyera; moyo wa munthu sukhala chifukwa cha kuchuluka kwa zimene ali nazo.”
Hanchu, an rênga kôma, “Singthei roi, ôinangei murdi renga indîn thei roi, asikchu, rochon, neinangei hih miriem ringna abitak nimak, idôr khom nei resea,” a tipe ngei.
16 Ndipo Iye anawawuza fanizo ili, “Munda wa munthu wina wachuma unabereka kwambiri.
Male, Jisua'n hi chongmintêk hih a ril ngeia, “Mi aneipa inkhat hin a loia chimu tamtak a minvânga,
17 Iye anaganiza kuti, ‘Ndichite chiyani? Ndilibe malo osungiramo mbewu zanga.’
Inmo ko tho rang ani zoi, o, ka bu le bâl darna rang dôn khâi mu-ung hi,” tiin a mindona.
18 “Ndipo Iye anati, ichi ndi chimene ndidzachite: Ndidzaphwasula nkhokwe zanga zonse ndi kumanga zokulirapo, ndipo ndidzasungira mʼmenemo mbewu ndi katundu.
Hi anghin tho ki tih, ka sasier set ka ta, anêka lien uol sin ki tih, mahan ke neinun murdi dar ki tih.
19 Ndipo ndidzawuza moyo wanga kuti, ‘Uli nazo zinthu zabwino zambiri zimene zikhalepo zaka zambiri, usapupulume; idya, imwa ndi kukondwera.’”
Maleh, ka ratha kôma, “Ratha, kum tamtak rang neinun sa nu bûm zoi sikin, sâk inla nêk roh, ningbei riemin om roh tipe ki tih” a tia.
20 “Koma Mulungu anati kwa iye, ‘Iwe wopusa! Usiku womwe uno moyo wako udzachotsedwa kwa iwe, ndipo ndi ndani amene adzatenge zimene iwe wadzikonzera?’
Ania, Pathien'n a kôma, “Amo, avien jân reng ni ringna aboi rang kêng ani zoi, hi neinun ni isuo ngei hih tuta rang tak mini?” a tipea.
21 “Umu ndi mmene zidzakhalire ndi aliyense amene amadziwunjikira chuma, koma si wachuma pamaso pa Mulungu.”
Hanchu Jisua'n, “Pathien tieng nei loia, eini ta rang vaia rochon a bûm chu ha anga han nîng a tih” a tia.
22 Kenaka Yesu anati kwa ophunzira ake, “Choncho Ine ndikuwuzani kuti musadere nkhawa za moyo wanu, zimene mudzadya; kapena za thupi lanu, zimene mudzavala.
Jisua'n a ruoisingei kôma, masikin nangni ki ti, nin taksa sâk nêk rang, nin sil nin bom rang nin kâng mindoi no roi.
23 Moyo uposa chakudya, ndi thupi liposa chovala.
Sâk nêk rang nêkin ringna alut uol, silbom rang nêkin takpum alut uol.
24 Taonani makwangwala: iwo safesa kapena kukolola, alibe nyumba zosungamo zinthu kapena nkhokwe; komabe, Mulungu amawadyetsa. Koposa kotani inu amene ndi ofunikira kuposa mbalame.
Invatengei en ta u, chimu khom tu mak ngei, bu khom ât mak ngei, sasier khom nei mak ngei, hankhoma Pathien'n a vâia, vangei nêkin nin lut uol ok.
25 Ndi ndani wa inu akhoza kuwonjeza ora pa moyo wake chifukwa cha kudandaula?
Tumo a kângdoi sika a ringna a min sôt thei uola?
26 Popeza simungathe kuchita kanthu kakangʼono aka, nʼchifukwa chiyani mumadandaula ndi zinazi?
Ma ngeite luo nin tho thei loiin, imo neinun dang vângte nin kâng nin mindoi?
27 “Taonani mmene maluwa amakulira. Iwo sagwira ntchito kapena kusoka zovala. Koma Ine ndikuwuzani kuti, ngakhale Solomoni muulemelero wake wonse sanavalepo ngati limodzi la awa.
Ram pârngei en ta u, sin khom tho mak ngei, puon khom không mak ngei. Ania nangni ki ril, ma dôra anei, rêng Solomon luo han hi pârte hih phâk mak.
28 Ngati umu ndi mmene Mulungu amavekera udzu wakuthengo, umene lero ulipo ndipo mawa uponyedwa pa moto, nanga Iye adzakuvekani inu motani. Haa! Inu achikhulupiriro chochepa!
Pathien kêng loisûl puon minsil, sûl aviena oma nangtûka lungthua hâl rip rang. Nangni vâng chu, nangni minsil no ni mo? Nin taksônna achîn bah na!
29 Ndipo musayike mtima wanu pa zimene mudzadye kapena kumwa; musade nazo nkhawa.
Masikin nin sâk nin nêk rang mindonin nin kângmindoi no roi.
30 Pakuti anthu akunja amathamanga kufunafuna zinthu zotere, ndipo Atate amadziwa kuti mumazifuna zimenezi.
Jentailngeiin ma ang roi chu an mindon ngâi. Nin Pa'n nin inâng chu a riet let.
31 Koma funafunani ufumu wake, ndipo mudzapatsidwa zonsezi.
Manêkin a Rêngram mindon bak ungla hanchu ha neinunngei ha chu nangni pêng a tih.
32 “Musachite mantha, inu kagulu kankhosa, pakuti zinakondweretsa Atate anu kuti akupatseni ufumu.
“Chi no roi, lôm achînte ngei, nin Pa'n a Rêngram nangni pêk rang a nuom.
33 Gulitsani zonse zimene muli nazo, ndipo ndalama zake mupereke kwa osauka. Dzipezereni zikwama zandalama zimene sizidzatha, ndi kudzikundikira chuma chomwe sichidzatha kumwamba, kumene mbala sizingafikeko, ndipo dzimbiri silingawononge.
Nin neinun murdi zuor ungla, inrieng ngei pêk roi. Sumkok chettheiloia thun ungla, invâna achiem thei khâiloina ranga, inrungeiin an murûk thei khâiloina, rengên a siet thei khâiloina ranga ninta rangin rochon bûm roi.
34 Popeza kumene kuli chuma chanu, mtima wanunso udzakhala komweko.”
No rochonngei omna kipa nu mulungrîl khom om tit a tih.
35 “Khalani okonzekeratu ndipo nyale zanu ziziyaka,
“Nin puon insilin, nin kong khitin, nin châti mochokin, tiklâi khomin intûng chienin om roi,
36 ngati anthu oyembekezera kubwera kwa mbuye wawo kuchokera kuphwando la ukwati, kuti pamene afika ndi kugogoda akhoza nthawi yomweyo kumutsekulira chitseko.
tîrlâm, an pu innei ruolhoi renga juong rang lei ngâk chien anghan. A juongleh, inkhâr a tôka mo-ong kelen rangin.
37 Zidzakhala bwino kwa antchitowo amene mbuye wawo pobwera adzawapeze akudikira. Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti adzakonzekera kuwatumikira, adzakhala nawo pa tebulo ndipo adzabwera ndi kuwatumikira.
Tîrlâm, an pu juonga intûng chiena om ai juong mu chu mi satvur anni. Nang ki ril, a kong khit a ta, insung a ta, ngâk a tih.
38 Zidzakhala bwino kwa antchitowo amene mbuye wawo adzawapeze ali okonzeka, ngakhale iye atabwera pa ora lachiwiri kapena lachitatu usiku.
Jânchima mo, arkhuona mo, a juonga intûng chiena ai mu ngei chu mi satvur anni.
39 Koma zindikirani izi: Ngati mwini nyumba akanadziwa ora limene mbala ibwera, sakanalola kuti nyumba yake ithyoledwe.
Mahih riettit roi, in pumapa'n inru hong rang riet senla chu a in minset no nih.
40 Inunso muyenera kukhala okonzeka, chifukwa Mwana wa Munthu adzabwera pa ora limene simukumuyembekezera Iye.”
Masikin nangni khom intûng chienin om roi, nin tûng loi lâitakin Miriem Nâipasal juong a tih,” a tia.
41 Petro anafunsa kuti, “Kodi mukunena fanizoli kwa ife, kapena kwa aliyense?”
Peter'n, “Pumapa, hi chongmintêk hih keini rang vai mo ni ti, mi murdi rang mo?” a tia.
42 Ambuye anayankha kuti, “Kodi tsono woyangʼanira wokhulupirika ndi wanzeru ndani? Kodi ndi amene mbuye wake wamuyika kukhala oyangʼanira antchito ake kuti aziwapatsa ndalama yachakudya pa nthawi yake yoyenera?
Pumapa'n a thuona, “tîrlâm iem om avâr tak, a pûn a insûng a cherêla, tîrlâm dang ngei azora kipa, an sâk a sem pe ranga uliena ai be chu tumo nini?
43 Zidzamukhalira bwino wantchito amene mbuye wake adzamupeza akuchita zimene pamene iye abwera.
a pu a honga, ha anga lei tho tîrlâm ai mu chu mi satvur ani.
44 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti adzamuyika kukhala woyangʼanira katundu wake yense.
Adiktakin nangni ki ril, ha tîrlâm tak hah a pun neinun enkolpun sin a tih.
45 Koma tiyerekeze kuti wantchitoyo aziganiza mu mtima mwake kuti, ‘Bwana wanga akuchedwa kwambiri kubwera,’ ndipo kenaka ndi kuyamba kumenya antchito aamuna ndi aakazi ndi kudya, kumwa ndi kuledzera.
Hannisenla ha tîrlâm han a mulungin, ku pu la juong vak no nih, tiin a tîrlâmpa ngei, a tîrlâmnu ngei jêm senla, sâkin nêkin lênrûi senla,
46 Mbuye wake adzabwera tsiku limene iye sakumuyembekezera ndi ora limene iye sakudziwa. Iye adzamulanga ndi kumusiya kumalo kumene kuli osakhulupirira.
Ha tîrlâm hah ân ningloi, ân tûngloi kârin, a pu juong a ta, tuk nôinek a ta, a iemloi ngei rangtum minchang a tih.
47 “Wantchito amene amadziwa chifuniro cha mbuye wake koma wosakonzeka kapena wosachita chimene mbuye wake akufuna adzakwapulidwa zikwapu zambiri.
Tîrlâm a pu nuomlam riet chaka intûng loia, sin nuomloi chu na takin jêmpol nîng a tih.
48 Koma wantchito amene sadziwa koma nʼkuchita zinthu zoyenera chilango, adzakwapulidwa zikwapu zochepa. Aliyense amene anapatsidwa zambiri, adzayenera kubwezanso zambiri; ndipo amene anamusungitsa zambiri, adzamulamula kuti abweze zambirinso.”
Hannirese, riet loi sika, tôkmol sâkna rak tho minchâi chu jâmin jêm nîng a tih. Tutu atam an pêk kôma atam zong an ta, atam uol an ipêk kôma chu atam uol rok an tih.
49 “Ine ndabwera kudzayatsa moto pa dziko lapansi, ndipo ndikanakonda ukanayaka kale.
“Pilchung mei leh hâl ranga juong kini, atûn khom kâng kelen tarse ku nuom.
50 Koma Ine ndiyenera kubatizidwa, ndipo ndikusautsika mu mtima mpaka utachitika!
Baptisma ka chang ranga om hih, ânzoi mâka chu ki ning ânîp bah!
51 Kodi mukuganiza kuti Ine ndinabwera kudzabweretsa mtendere pa dziko lapansi? Ayi, Ine ndikukuwuzani kuti, ndinabweretsa kugawikana.
Rammuola inngeina min lêng ranga juongin mo mi nin tûng? Inngêina min lêng ranga juong ni mu unga, insenna min lêng ranga juong kêng kini.
52 Kuyambira tsopano mpaka mʼtsogolo mʼbanja limodzi mudzakhala anthu asanu ndipo adzawukirana wina ndi mnzake, atatu kuwukira awiri, ndipo awiri kuwukira atatu.
Atûn renga insûngkuo inkhata mi rangnga insen an ta, inthum ngeiin inik ngei doi an ta, inik ngeiin inthum ngei doi an tih.
53 Anthu adzawukirana. Abambo kudzawukira mwana wawo wamwamuna, mwana wawoyo adzawukira abambo ake. Amayi adzawukira mwana wawo wamkazi, mwana wawoyo adzawukira amayi ake. Amayi adzawukira mpongozi wawo wamkazi, mpongoziyo adzawukira amayiwo.”
Pa ngeiin an nâingei, nâingeiin an pangei, nungeiin an nâinupangngei, nâinupangngeiin an nungei, tarpingeiin an moingei, moingeiin an tarpingei doi an tih,” a tia.
54 Iye anati kwa gulu la anthu, “Pamene mukuona mtambo ukukwera kummawa, nthawi yomweyo inu mumati, ‘kugwa mvula,’ ndipo imagwadi.
Jisua'n mipui ngei kôma khom, “Nitâk tieng sûm a jînga anîn chu ruo a juong rang kêng nin tia, juong khom a juong ngâi.
55 Ndipo pamene mphepo yakummwera ikuwomba, inu mumati ‘kutentha’ ndipo kumaterodi.
Hanchu thînthi a hong sêma anîn chu alum rang kêng nin tia, alum khom alum ngâi.
56 Achiphamaso inu! Inu mumadziwa kutanthauzira maonekedwe a dziko lapansi ndi thambo. Zikutheka bwanji kuti simukudziwa kumasulira kwa nthawi ino?
Asarotholngei o! phil le invân nin ena, khuo om rang tie nin riet theia, ania, atûnlâi zora om tie ithomo nin riet thei loi?” a tia.
57 “Bwanji simukuzindikira nokha zoyenera kuchita?
“Ithomo nin theiin neinun dik sin rang nin mindon loi?
58 Pamene mukupita kwa woweruza ndi amene munalakwirana naye, yesetsani kwambiri kuti muyanjane naye mʼnjiramo, chifukwa mukapanda kutero akhoza kukutengerani ku bwalo la milandu ndipo woweruzayo adzakuperekani kwa woyangʼanira ndende, ndipo woyangʼanira ndendeyo adzakuponyani mʼndende.
Mîn roijêkmuna nang an kai rangin chu, ha mi lehhan roijêkmun tung mân inngêina sinpui roh, aninôn chu, roijêkpu makunga nang kai a ta, intâng ina nang khum an tih.
59 Ine ndikuwuzani kuti, simudzatulukamo mpaka mutalipira ndalama zonse.”
Nang ki ril, poisa apêkte luo ne pêk let mâka chu mahan om ni tih,” a tia.

< Luka 12 >