< Luka 12 >
1 Nthawi yomweyo, anthu miyandamiyanda atasonkhana, ndi kumapondanapondana, Yesu anayamba kuyankhula poyamba kwa ophunzira ake, nati, “Chenjereni ndi yisiti wa Afarisi, amene ndi chinyengo.
Wakati owo amabungano nabhatangene elfu elfu hata bhakhanyanaga, ahandile abhabhole asambe leziwa bhakwe nantele, “Hwilindi ne chachu eya Mafarisayo ambayo unafiki.”
2 Palibe chinthu chophimbika chimene sichidzawululika, kapena chobisika chimene sichidzadziwika.
Lelo nalimo izu lyalifisishe lyasalyaibhonaha wala lyalifisilye lyaselyayi julihana. Eshi gagonti gamuyanjile hunkisi gabhahwovwehwe pawelele.
3 Chimene mwanena mu mdima chidzamveka dzuwa likuwala, ndipo zimene mwanongʼona mʼkhutu mʼchipinda chamʼkati, zidzayankhulidwa pa denga la nyumba.
Na gamuyanjile mmakutu mwa bhantu katika mpanda ezya mhati gayitu mbele wa pamwanya eye golu.
4 “Ine ndikuwuzani, abwenzi anga, musachite mantha ndi amene amapha thupi chifukwa akatero sangachitenso kanthu.
Nane ambabhola amwa rafiki bhane, mgaje bhaogapa ebho bhabhagoga oele afwanaje baada eyeso sebhanowezo abhombe zaidi.
5 Koma Ine ndidzakuonetsani amene muyenera kumuopa: Wopani Iye, amene pambuyo pakupha thupi, ali ndi mphamvu yakukuponyani ku gehena. Inde, Ine ndikuwuzani, muopeni Iye. (Geenna )
Lelo embabhasunda owahumwogope. Mwogopaji ola ambaye nkashele wagoga omntu anakwezo huponye hujehanamu. Antele embabhola mwogapaji oyo. (Geenna )
6 Kodi atimba asanu samagulidwa ndi ndalama ziwiri? Ngakhale zili chomwecho palibe imodzi ya izo imene imayiwalika ndi Mulungu.
Nkashe mshomolo gasanu segakatiwa husenti zibhele? Wala sebhahwewehwa hata om hwitagalila elya Ngolobhe.
7 Ndithudi, tsitsi lonse la mʼmutu mwanu ndi lowerengedwa. Musachite mantha; inu ndi oposa kwambiri mpheta zambiri.
Lelo hata lisisi eya mwi atwa genyu zibhaziwe zyonti, mganje ahwa gape esho. Nafu amwe ashile amashomolo gaminji.
8 “Ine ndikukuwuza kuti, aliyense amene avomereza Ine pamaso pa anthu, Mwana wa Munthu adzamuvomerezanso pamaso pa angelo a Mulungu.
Nane embabhola, nkashele yayineteha hwitagalile elya bhantu, omwana owa Adamu wapa ayihumweteha hwitagalila elya malaika owa Ngolobhe.
9 Koma iye amene andikana Ine pamaso pa anthu adzakanidwanso pamaso pa angelo a Mulungu.
Wape wahana hwitagalila elya bhantu, oyo ayikhanwa hwitagalila elya malaika owa Ngolobhe.
10 Ndipo aliyense amene ayankhulira Mwana wa Munthu mawu oyipa adzakhululukidwa, koma iye wochitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa.
Na shila mntu yayiyanga enongwa juu ya omwana wa Adamu, ayisajilwa, nkashele yayihuliga opepo uzelu sagayisajilwa.
11 “Akadzakutengerani ku masunagoge pamaso pa oweruza ndi a maulamuliro, musadere nkhawa mmene mudzadzitchinjirizire nokha kapena chimene mudzayankhule,
Nabhayibhatwala amwe hwitagalila elye mabhanza, na hwaliwali na hwaongozi, msazugumile asebhe enongwa zyenyu shamwayigalula au ayanje,
12 pakuti Mzimu Woyera nthawi imeneyo adzakuphunzitsani zoyenera kunena.”
afwanaje opepo ozeru ayibhasambelezya, esaa zyezyo zyazihwaziwa aziyanje.”
13 Munthu wina mʼgulu la anthu anati kwa Iye, “Aphunzitsi, muwuzeni mʼbale wanga andigawireko chuma chamasiye.”
Omntu omo katika mabungano wabhola, “Sambelezi bhole oholo wane angabhile vulithi wetu.”
14 Yesu anayankha kuti, “Munthu iwe, ndani anandiyika Ine kukhala woweruza kapena wogawa chuma pakati panu?”
Wabhola, womntu awe, wenu yambeshele ane aje endi watazanye au wagabhanya juu yenyu?
15 Kenaka Iye anawawuza kuti, “Chenjerani! Khalani tcheru ndi makhalidwe onse adyera; moyo wa munthu sukhala chifukwa cha kuchuluka kwa zimene ali nazo.”
Wabhabhola enyaji, hwilindaji no wimi afwanaje owomi wamntu sauhuvintu evinji evya mntu vyu unavyo.”
16 Ndipo Iye anawawuza fanizo ili, “Munda wa munthu wina wachuma unabereka kwambiri.
Wabhabhola eshilale wayanga ogonda ogwa mntu omo otajili lyali lipepe tee,
17 Iye anaganiza kuti, ‘Ndichite chiyani? Ndilibe malo osungiramo mbewu zanga.’
wanda asebhe humwoyo gwakwe, wayanga, embombo wele, afwanaje sendi nupabheshe eshanga eshe viyabho vyane?
18 “Ndipo Iye anati, ichi ndi chimene ndidzachite: Ndidzaphwasula nkhokwe zanga zonse ndi kumanga zokulirapo, ndipo ndidzasungira mʼmenemo mbewu ndi katundu.
Wayanga embabhombe eshi, embabozolanye evyanga vyane, ezenje eshamwabho eshi gosi tee, nomwo embabheshe evyelewa vyane vyonti nevintu vyane.
19 Ndipo ndidzawuza moyo wanga kuti, ‘Uli nazo zinthu zabwino zambiri zimene zikhalepo zaka zambiri, usapupulume; idya, imwa ndi kukondwera.’”
Nantele, nayihwibhozya, awe womwoyo gwane olinevintu evinza vinji vyo hwibheye mbuto humaha gaminji. Toyo eshi, alye, omwele, osongwe.”
20 “Koma Mulungu anati kwa iye, ‘Iwe wopusa! Usiku womwe uno moyo wako udzachotsedwa kwa iwe, ndipo ndi ndani amene adzatenge zimene iwe wadzikonzera?’
Lelo Ongolobhe wabhozya, olilema awe, osiku ou owasanyono bhahwanza owomi waho, nevintu vyohwibhesheye vibhabhe vyananu?
21 “Umu ndi mmene zidzakhalire ndi aliyense amene amadziwunjikira chuma, koma si wachuma pamaso pa Mulungu.”
Shesho shali omntu yahwibheye omwoyo gwakwe mbuto, asahwitajilisye hwa Ngolobhe.
22 Kenaka Yesu anati kwa ophunzira ake, “Choncho Ine ndikuwuzani kuti musadere nkhawa za moyo wanu, zimene mudzadya; kapena za thupi lanu, zimene mudzavala.
Wabhabhola asambelezwa bhakwe, afwatana nesho embabhozya mgaje ahwihangayishile amayisha genyu mbhalya yenu wala amabele genyu mbhakwate yenu.
23 Moyo uposa chakudya, ndi thupi liposa chovala.
Afwanaje amayisha gazaidieyeshu lya nobele zaidi yemenda.
24 Taonani makwangwala: iwo safesa kapena kukolola, alibe nyumba zosungamo zinthu kapena nkhokwe; komabe, Mulungu amawadyetsa. Koposa kotani inu amene ndi ofunikira kuposa mbalame.
Bhasebhaji enkogolo eyaje sebhato tuwala sebhayabhila, seline shanga wa eshitala, no Ngolobhe abhalisya, mrinafu amwe shila enyonyi!
25 Ndi ndani wa inu akhoza kuwonjeza ora pa moyo wake chifukwa cha kudandaula?
Yonanu hwilimwe yabhajiye ahwi ngayisye nawezye ahwiyonjezye otali wakwe hata okhono gumo?
26 Popeza simungathe kuchita kanthu kakangʼono aka, nʼchifukwa chiyani mumadandaula ndi zinazi?
Eshi nkashele semwezizye hata lizu lyalili lidodo, yenu mhwiyazya kwajili yegamwabho?
27 “Taonani mmene maluwa amakulira. Iwo sagwira ntchito kapena kusoka zovala. Koma Ine ndikuwuzani kuti, ngakhale Solomoni muulemelero wake wonse sanavalepo ngati limodzi la awa.
Gasebhelaji amawowa ejinsi shamela segahuhambo embombo wala segabhilinga, neane embubhola yaje hata Osulemani katika efahali yakwe yonti saga kwatiziwe shinza kama neshe eyego,
28 Ngati umu ndi mmene Mulungu amavekera udzu wakuthengo, umene lero ulipo ndipo mawa uponyedwa pa moto, nanga Iye adzakuvekani inu motani. Haa! Inu achikhulupiriro chochepa!
Eshi nkebhe Ongolobhe akwatizya eshi amasole agamwipali, gagali sanyo no na sandabho gatagwa papepe. Je sagayibhabhombela amwe? Enyi amwe mwemli imani endodo!
29 Ndipo musayike mtima wanu pa zimene mudzadye kapena kumwa; musade nazo nkhawa.
Amwe msahwanza shamwayilya wala shamwaimwele wala mgaje abhombe nowoga.
30 Pakuti anthu akunja amathamanga kufunafuna zinthu zotere, ndipo Atate amadziwa kuti mumazifuna zimenezi.
Afwanaje egogonti ebhamnsi omu. Lelo o yise wenyu amenye aje mganza ego.
31 Koma funafunani ufumu wake, ndipo mudzapatsidwa zonsezi.
Eshi anzaji omwene owa NGOLOBHE, nego mwayonjezewa,
32 “Musachite mantha, inu kagulu kankhosa, pakuti zinakondweretsa Atate anu kuti akupatseni ufumu.
Mganje hwogope, amwe mwikundi idodo, afanaje oYise wenyu alolile shinza abhapele ula oumwene.
33 Gulitsani zonse zimene muli nazo, ndipo ndalama zake mupereke kwa osauka. Dzipezereni zikwama zandalama zimene sizidzatha, ndi kudzikundikira chuma chomwe sichidzatha kumwamba, kumene mbala sizingafikeko, ndipo dzimbiri silingawononge.
Kazi vyamlinavyo mfumye sadaka, hwibheshalaji amafuko yasagalala—embuto yasepogoha, humwanya pasaga afiha omwibha wala no ndo sana nkaya.
34 Popeza kumene kuli chuma chanu, mtima wanunso udzakhala komweko.”
Afanaje embuto yenyu, pehweli pagayibha gahweli na moyo genyu.
35 “Khalani okonzekeratu ndipo nyale zanu ziziyaka,
Amasana genyu gabhe gapinyilya nehozyo, zyenyu zibhe zihwaha,
36 ngati anthu oyembekezera kubwera kwa mbuye wawo kuchokera kuphwando la ukwati, kuti pamene afika ndi kugogoda akhoza nthawi yomweyo kumutsekulira chitseko.
Namwe bhanji neshe abhantu bhabhahugolezya OGOSI wabho naiwela afume huweji, ili na hwenza na khome ehodi bhamwigulile.
37 Zidzakhala bwino kwa antchitowo amene mbuye wawo pobwera adzawapeze akudikira. Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti adzakonzekera kuwatumikira, adzakhala nawo pa tebulo ndipo adzabwera ndi kuwatumikira.
Nafu asontezewa bhala, ambao OGOSI wabho nayenza ayibhaga bhagonezezye. Eteshi embabhola abhahwipinye nabhakaribizye pa shalye, ayenza nabhavwe.
38 Zidzakhala bwino kwa antchitowo amene mbuye wawo adzawapeze ali okonzeka, ngakhale iye atabwera pa ora lachiwiri kapena lachitatu usiku.
Nankayenze olyondizanyo olwa bhele, au nkayenza olwandiznyo olwatatu nabhaje eshi, nafu ontezewa ebho.
39 Koma zindikirani izi: Ngati mwini nyumba akanadziwa ora limene mbala ibwera, sakanalola kuti nyumba yake ithyoledwe.
Lelo mmanye, izu eli, aje omwane sho nyumba agamenye esaa ya bhahwenze omwibha, handa agone zyezye, wala handa sagaleshele enyumba yakwe ebozolwe.
40 Inunso muyenera kukhala okonzeka, chifukwa Mwana wa Munthu adzabwera pa ora limene simukumuyembekezera Iye.”
Namwe hwibhehaji tayari afwanaje esaa yasagammenye shesho sha hwenza omwana wa Adamu.
41 Petro anafunsa kuti, “Kodi mukunena fanizoli kwa ife, kapena kwa aliyense?”
OPetro wabhola, “GOSI, eshilale esho otibholele tele wene, au abhantu bhonti antele?
42 Ambuye anayankha kuti, “Kodi tsono woyangʼanira wokhulupirika ndi wanzeru ndani? Kodi ndi amene mbuye wake wamuyika kukhala oyangʼanira antchito ake kuti aziwapatsa ndalama yachakudya pa nthawi yake yoyenera?
OGOSI wayanga, “Wenu eshi yali mtunzaji mwinza yali nebusara ambaye ogosi wakuwe abhahubheshe bhombambombo wakwe wonti, abhapele abhantu eposho huwakati wakwe?
43 Zidzamukhalira bwino wantchito amene mbuye wake adzamupeza akuchita zimene pamene iye abwera.
Nafu osontezi ola, ambaye gosi wakwe nahwenza awahumwaje abhomba esho.
44 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti adzamuyika kukhala woyangʼanira katundu wake yense.
Lyoli embabhola abhahubheshe juu yevintu vyakwe vyonti.
45 Koma tiyerekeze kuti wantchitoyo aziganiza mu mtima mwake kuti, ‘Bwana wanga akuchedwa kwambiri kubwera,’ ndipo kenaka ndi kuyamba kumenya antchito aamuna ndi aakazi ndi kudya, kumwa ndi kuledzera.
Lelo osontelezewa ola nkayanje humwoyo gwakwe, “OGOSI wane wakhala ahwenze wanda; abhakhome aholo bhakwe, alume na bhashe, alya na mwele na kholwe,
46 Mbuye wake adzabwera tsiku limene iye sakumuyembekezera ndi ora limene iye sakudziwa. Iye adzamulanga ndi kumusiya kumalo kumene kuli osakhulupirira.
Ogosi wakwe otumwa oyo ayenza isiku lyasategemeye nesaa yasayimenye, abhahudumranye evipande vibhele nahubheshe ifungu lyakwe pandwemo na bhasaga bhalino lyeteho'
47 “Wantchito amene amadziwa chifuniro cha mbuye wake koma wosakonzeka kapena wosachita chimene mbuye wake akufuna adzakwapulidwa zikwapu zambiri.
No tumwa, ola yagamenye omapenzi ga gosi wakwe, sahwibhe tayari wala agabhombe amapenzi gakwe, ayikhomwa tee.
48 Koma wantchito amene sadziwa koma nʼkuchita zinthu zoyenera chilango, adzakwapulidwa zikwapu zochepa. Aliyense amene anapatsidwa zambiri, adzayenera kubwezanso zambiri; ndipo amene anamusungitsa zambiri, adzamulamula kuti abweze zambirinso.”
No ola yasagamenye wape abhombile gagahwanziwa akhomwe, akhomwa hashe. Na shila yapewewe evinji, hwamwahale oyo bhanza wanze vivinji, wape wabhesheye amana evintu evinji hwamwahale oyo wabhanza ahwanze zaidi.
49 “Ine ndabwera kudzayatsa moto pa dziko lapansi, ndipo ndikanakonda ukanayaka kale.
Enenzere aponye omwoto pansi, na nkashile gwandue ahwanshe lyenu lyehwanza zaidi,
50 Koma Ine ndiyenera kubatizidwa, ndipo ndikusautsika mu mtima mpaka utachitika!
Lelo endi no wonzwe wauhwanziwa ahwoziwe, nene endi namalabha neshe eyenu ili gatimizwe!
51 Kodi mukuganiza kuti Ine ndinabwera kudzabweretsa mtendere pa dziko lapansi? Ayi, Ine ndikukuwuzani kuti, ndinabweretsa kugawikana.
Eshi! mwadhani eyaje enenzele alete eamani? Pansi, embabhola, la seshashesho eshi Mafarakano.
52 Kuyambira tsopano mpaka mʼtsogolo mʼbanja limodzi mudzakhala anthu asanu ndipo adzawukirana wina ndi mnzake, atatu kuwukira awiri, ndipo awiri kuwukira atatu.
Afwanaje afume eshi enyumba emo bhayibha abhantu bhasanu bhavisenye, bhantu hwabhabhele, bhabhele hwa bhantu.
53 Anthu adzawukirana. Abambo kudzawukira mwana wawo wamwamuna, mwana wawoyo adzawukira abambo ake. Amayi adzawukira mwana wawo wamkazi, mwana wawoyo adzawukira amayi ake. Amayi adzawukira mpongozi wawo wamkazi, mpongoziyo adzawukira amayiwo.”
Bhayivisanya, oYise no mwana no mwana no Yise wakwe, onyino no lendu wakwe, khoyi wakwe, okhamwana no khamwana wa mntu.
54 Iye anati kwa gulu la anthu, “Pamene mukuona mtambo ukukwera kummawa, nthawi yomweyo inu mumati, ‘kugwa mvula,’ ndipo imagwadi.
Wabhabhola amabungano nantele, “Shila namlola ibhengo nkalifumile oupanda wa magharibi tiyanga, evula ehwenza, ibha shesho,
55 Ndipo pamene mphepo yakummwera ikuwomba, inu mumati ‘kutentha’ ndipo kumaterodi.
Na shila nevugula hukuskazini, liyanga, hubhabhe nilyoto, na shashi hweli.
56 Achiphamaso inu! Inu mumadziwa kutanthauzira maonekedwe a dziko lapansi ndi thambo. Zikutheka bwanji kuti simukudziwa kumasulira kwa nthawi ino?
Amwe mwanafiki, mmenye atambule amaso agensine mwanya, shiliwele eshi abhe semumenye atambule amajira ega?
57 “Bwanji simukuzindikira nokha zoyenera kuchita?
Na mbona amwe mwemwe hunafsi zyenu semu hwamla gagali gelyoli?
58 Pamene mukupita kwa woweruza ndi amene munalakwirana naye, yesetsani kwambiri kuti muyanjane naye mʼnjiramo, chifukwa mukapanda kutero akhoza kukutengerani ku bwalo la milandu ndipo woweruzayo adzakuperekani kwa woyangʼanira ndende, ndipo woyangʼanira ndendeyo adzakuponyani mʼndende.
Eshi namulongozenye no mshitaki waho abhale hwa lonzi, epo pidala bhomba ebidii akondane nawo, asabhe agaburuzya mpaka hwitagalila elya lonzi, ola olonzi wakhata mmakhono gakwe, hwamwenesho yagalipizya nola owalipizye asije agafunga mwijela.
59 Ine ndikuwuzani kuti, simudzatulukamo mpaka mutalipira ndalama zonse.”
Ehubhola, sofuma omwo nkahashe hata omale asombe esenti eya mwisho.