< Luka 12 >
1 Nthawi yomweyo, anthu miyandamiyanda atasonkhana, ndi kumapondanapondana, Yesu anayamba kuyankhula poyamba kwa ophunzira ake, nati, “Chenjereni ndi yisiti wa Afarisi, amene ndi chinyengo.
Maelufu ga wantu pawaliwoniti pamuhera, ata waweriti wankulitimbanga, Yesu kawagambiriti huti wafundwa wakuwi, “Mliloleri weri na simika ya Mafalisayu, nana mana ufyangu.
2 Palibe chinthu chophimbika chimene sichidzawululika, kapena chobisika chimene sichidzadziwika.
Kila shintu shawashigubikiti hashiweri paweru na kila bada hayimaniki.
3 Chimene mwanena mu mdima chidzamveka dzuwa likuwala, ndipo zimene mwanongʼona mʼkhutu mʼchipinda chamʼkati, zidzayankhulidwa pa denga la nyumba.
Su vyoseri vyamtakuliti muluwindu havipikaniki paluwala, ata vilii vyamulipwepwera shipindi pamtatiti milyangu havibwerwi panani pa numba.
4 “Ine ndikuwuzani, abwenzi anga, musachite mantha ndi amene amapha thupi chifukwa akatero sangachitenso kanthu.
“Nukugambirani waganja wangu, namuwatira woseri yawalaga nshimba kumbiti wasinda kutenda shintu shimonga nentu.
5 Koma Ine ndidzakuonetsani amene muyenera kumuopa: Wopani Iye, amene pambuyo pakupha thupi, ali ndi mphamvu yakukuponyani ku gehena. Inde, Ine ndikuwuzani, muopeni Iye. (Geenna )
Hanuwalanguziyani gwa kumtira, mumtiri Mlungu, ayu pakawalaga kala kana uwezu wa kumwasira muntu mumotu gwa Jehanamu. Munjimiri, ayu ndo yumu gwa kumtira! (Geenna )
6 Kodi atimba asanu samagulidwa ndi ndalama ziwiri? Ngakhale zili chomwecho palibe imodzi ya izo imene imayiwalika ndi Mulungu.
“Iwera ndiri washomolu wamuhanu wawawuza kwa senti ndikandika mbili? Kumbiti Mlungu hapeni kamuwaluwi shomolu ata yumu.
7 Ndithudi, tsitsi lonse la mʼmutu mwanu ndi lowerengedwa. Musachite mantha; inu ndi oposa kwambiri mpheta zambiri.
Ata vilii zya mumtuwi mwenu waziwalangiti kala. Su namtira, mwenga wa mana nentu kuliku washomolu wavuwa!
8 “Ine ndikukuwuza kuti, aliyense amene avomereza Ine pamaso pa anthu, Mwana wa Munthu adzamuvomerezanso pamaso pa angelo a Mulungu.
“Nankuwagambira nakaka, kila muntu yakatakula kulongolu kwa wantu kulonga ndo gwaneni, Mwana gwa Muntu hakatakuli kulongolu kwa wantumintumi wa kumpindi wa Mlungu kuwera muntu ayu ndo gwakuwi.
9 Koma iye amene andikana Ine pamaso pa anthu adzakanidwanso pamaso pa angelo a Mulungu.
Kumbiti woseri yawanema kulongolu kwa wantu, Mwana gwa muntu viraa hakawalemi kulongolu kwa wantumintumi wa kumpindi wa Mlungu.
10 Ndipo aliyense amene ayankhulira Mwana wa Munthu mawu oyipa adzakhululukidwa, koma iye wochitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa.
“Na yoseri Yakamtakulira visoweru vidoda mwana gwa Muntu hakalekiziwi, kumbiti yoseri yakamwigilanga Rohu Mnanagala hapeni kalekeziwi.
11 “Akadzakutengerani ku masunagoge pamaso pa oweruza ndi a maulamuliro, musadere nkhawa mmene mudzadzitchinjirizire nokha kapena chimene mudzayankhule,
“Pawawabata na kuwajega munumba za Mlungu, ama kwa wakulu na wakolamlima, namulihola hola ntambu yakutakula ama ntambu ya kujiteteya.
12 pakuti Mzimu Woyera nthawi imeneyo adzakuphunzitsani zoyenera kunena.”
Toziya Rohu Mnanagala shipindi shiraa shilii hakawafundi ntambu yakutakula.”
13 Munthu wina mʼgulu la anthu anati kwa Iye, “Aphunzitsi, muwuzeni mʼbale wanga andigawireko chuma chamasiye.”
Muntu yumu mulipinga lya wantu kamgambiriti Yesu, “Mfunda, gumgambiri mlongu gwangu tugawani uhala yakatulekeleriti tati gwetu.”
14 Yesu anayankha kuti, “Munthu iwe, ndani anandiyika Ine kukhala woweruza kapena wogawa chuma pakati panu?”
Yesu kamwankula, “Ganja gwangu, gaa yakantyeka neni weri mtoza gwenu?”
15 Kenaka Iye anawawuza kuti, “Chenjerani! Khalani tcheru ndi makhalidwe onse adyera; moyo wa munthu sukhala chifukwa cha kuchuluka kwa zimene ali nazo.”
Su kawagambira woseri, “Muweri masu na muliloli weri na ntambu zoseri za matamata, toziya makaliru ganakaka ga muntu galitumbira ndiri vintu vivuwa vyakawera navi.”
16 Ndipo Iye anawawuza fanizo ili, “Munda wa munthu wina wachuma unabereka kwambiri.
Yesu kawagambira mfanu agu, “Kuweriti na mlunda yumu yakaweriti na lirambu lyakuwi lyalileriti viboga nentu.
17 Iye anaganiza kuti, ‘Ndichite chiyani? Ndilibe malo osungiramo mbewu zanga.’
Kanjiti kulihola mumoyu mwakuwi pakalonga, ‘Nahera pahala pa kutula viboga vyangu vyoseri. Su hantendi hashi?’
18 “Ndipo Iye anati, ichi ndi chimene ndidzachite: Ndidzaphwasula nkhokwe zanga zonse ndi kumanga zokulirapo, ndipo ndidzasungira mʼmenemo mbewu ndi katundu.
Kaligambiriti mweni, ‘Hantendi hangu, hambomoli hanja zyangu zoseri na kunyawa nkulu nentu, su hantuli viboga vyangu na lunda zyangu zimonga.
19 Ndipo ndidzawuza moyo wanga kuti, ‘Uli nazo zinthu zabwino zambiri zimene zikhalepo zaka zambiri, usapupulume; idya, imwa ndi kukondwera.’”
Shakapanu hanuligambiri mweni, Muntu yakana bahati! Gwana vintu vivuwa viherepa vya kuliya vinja ivuwa. Guvibojoli, vinu su gulii, gulandi na gulinemiziyi gumweni!’
20 “Koma Mulungu anati kwa iye, ‘Iwe wopusa! Usiku womwe uno moyo wako udzachotsedwa kwa iwe, ndipo ndi ndani amene adzatenge zimene iwe wadzikonzera?’
Kumbiti Mlungu kamgambira, ‘mzyigizyigi gwenga! Leru pashiru rohu yaku hayitolwi. Vinu gaa hakatoli vintu vyoseri vyaguvituliti kwajili yaku gumweni?’”
21 “Umu ndi mmene zidzakhalire ndi aliyense amene amadziwunjikira chuma, koma si wachuma pamaso pa Mulungu.”
Na Yesu kamaliriti pakatakula, “Ayi ndo ntambu hayiweri kwa muntu ulii yakalitulira ulunda kwajili yakuwi mweni kumbiti hapeni kaweri mlunda kwa Mlungu.”
22 Kenaka Yesu anati kwa ophunzira ake, “Choncho Ine ndikuwuzani kuti musadere nkhawa za moyo wanu, zimene mudzadya; kapena za thupi lanu, zimene mudzavala.
Yesu kawagambira wafundwa, “Nankuwagambira mleki kulihola hola makaliru genu ama nguwu zya kuvala.
23 Moyo uposa chakudya, ndi thupi liposa chovala.
Ukomu wa mana nentu kuliku shiboga na nshimba yana mana nentu kuliku nguwu.
24 Taonani makwangwala: iwo safesa kapena kukolola, alibe nyumba zosungamo zinthu kapena nkhokwe; komabe, Mulungu amawadyetsa. Koposa kotani inu amene ndi ofunikira kuposa mbalame.
Mloli wampongu, wayala ndiri ama wabenanga ndiri, kayi wahera ata luhanja lwa kutulila viboga, kumbiti Mlungu kawapanana shiboga! Mwenga muwera na mana nentu kuliku wampongu!
25 Ndi ndani wa inu akhoza kuwonjeza ora pa moyo wake chifukwa cha kudandaula?
Kwana muntu yoseri pakati penu yakaweza kwongera mweni makaliru gakuwi ata kwa saa yimu?
26 Popeza simungathe kuchita kanthu kakangʼono aka, nʼchifukwa chiyani mumadandaula ndi zinazi?
Handa pamuweza ndiri ata kutenda shintu shididini, iwera hashi mulihola hola vintu vimonga?
27 “Taonani mmene maluwa amakulira. Iwo sagwira ntchito kapena kusoka zovala. Koma Ine ndikuwuzani kuti, ngakhale Solomoni muulemelero wake wonse sanavalepo ngati limodzi la awa.
Muloli mawuwa ga kuntundu ntambu yagakula, gatenda ndiri lihengu ama galinyawa ndiri geni. Kumbiti nukugambirani kuwera Mfalumi Selemani pamuhera na ulunda wakuwi woseri kapatiti ndiri kuvalisiwa gambira mawuwa aga.
28 Ngati umu ndi mmene Mulungu amavekera udzu wakuthengo, umene lero ulipo ndipo mawa uponyedwa pa moto, nanga Iye adzakuvekani inu motani. Haa! Inu achikhulupiriro chochepa!
Payiwera Mlungu kaluvalusiya luhamba lya kuisi, lweni leru luwera na shirawu walwasila pamotu, ashi ndiri hakawatenderi nentu mwenga? Mwenga yamuwera na njimiru ndidini!
29 Ndipo musayike mtima wanu pa zimene mudzadye kapena kumwa; musade nazo nkhawa.
“Su namuligaziya kwa kusaluka shintu sha kuliya ama shintu sha kulanda.
30 Pakuti anthu akunja amathamanga kufunafuna zinthu zotere, ndipo Atate amadziwa kuti mumazifuna zimenezi.
Toziya wantu yawamumana ndiri Mlungu pasipanu wavisakula nentu vintu vyoseri avi. Tati gwenu kavimana mfira vintu avi.
31 Koma funafunani ufumu wake, ndipo mudzapatsidwa zonsezi.
Kumbiti msakuli huti Ufalumi wa Mlungu na hakawapanani vintu avi.
32 “Musachite mantha, inu kagulu kankhosa, pakuti zinakondweretsa Atate anu kuti akupatseni ufumu.
“Mwenga shipinga shididini namtira, toziya Tati gwenu kafira kuwapanana Ufalumi.
33 Gulitsani zonse zimene muli nazo, ndipo ndalama zake mupereke kwa osauka. Dzipezereni zikwama zandalama zimene sizidzatha, ndi kudzikundikira chuma chomwe sichidzatha kumwamba, kumene mbala sizingafikeko, ndipo dzimbiri silingawononge.
Muwuzi vyoseri vyamuwera navi na muwapanani mpiya wahushu. Mulinyawili mihaku yayidegeka ndiri na mtuli ulunda wenu kumpindi kwa Mlungu, kweni aku hapeni ipungulwi toziya kwahera mpoka yakaweza kwiwa, ama wameyi yawaweza kuhalibisiya.
34 Popeza kumene kuli chuma chanu, mtima wanunso udzakhala komweko.”
Ulunda waku pawuwera, ndo na moyu gwaku haguweri.
35 “Khalani okonzekeratu ndipo nyale zanu ziziyaka,
“Muweri kala kwa kila shintu shashiza na muviwashi vikoloboyi vyenu,
36 ngati anthu oyembekezera kubwera kwa mbuye wawo kuchokera kuphwando la ukwati, kuti pamene afika ndi kugogoda akhoza nthawi yomweyo kumutsekulira chitseko.
gambira wantumintumi yawamuhepera mtuwa gwawu yakiza kulawa mumsambu gwa ndowa. Pakawera kankwiza na kutenda hodi, su hawamvugulili mlyangu kamukamu.
37 Zidzakhala bwino kwa antchitowo amene mbuye wawo pobwera adzawapeze akudikira. Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti adzakonzekera kuwatumikira, adzakhala nawo pa tebulo ndipo adzabwera ndi kuwatumikira.
Mbaka kwa walii wantumintumi, mtuwa gwawu pakiza hakawawoni wankali masu! Nukugambirani nakaka, hakavuli nguwu yakuwi, nakuwagambira walivagi pasi na kuwatendera.
38 Zidzakhala bwino kwa antchitowo amene mbuye wawo adzawapeze ali okonzeka, ngakhale iye atabwera pa ora lachiwiri kapena lachitatu usiku.
Hawaweri na manemu ga ntambu gaa handa pakawawona wankali masu, ata pakiza pashiru ama pamandawira!
39 Koma zindikirani izi: Ngati mwini nyumba akanadziwa ora limene mbala ibwera, sakanalola kuti nyumba yake ithyoledwe.
Muvimani nakaka kuwera handa mweni kana numba pakavimaniti shipindi shakwiza mpoka, hapeni kamleki mpoka kubomolanga numba yakuwi.
40 Inunso muyenera kukhala okonzeka, chifukwa Mwana wa Munthu adzabwera pa ora limene simukumuyembekezera Iye.”
Na mwenga viraa, muweri kala, toziya Mwana gwa Muntu hakizi shipindi shamumana ndiri.”
41 Petro anafunsa kuti, “Kodi mukunena fanizoli kwa ife, kapena kwa aliyense?”
Peteru kamgambira, “Mtuwa, mfanu agu ndo kwajili ya twenga, ama kwajili ya kila muntu?”
42 Ambuye anayankha kuti, “Kodi tsono woyangʼanira wokhulupirika ndi wanzeru ndani? Kodi ndi amene mbuye wake wamuyika kukhala oyangʼanira antchito ake kuti aziwapatsa ndalama yachakudya pa nthawi yake yoyenera?
Mtuwa kawankula, “Ndo gaa yakawera ntumintumi kaaminika na yakana mahala? Ndo ulii mtuwa gwakuwi yakamtula kaweri mlolera gwa numba na kuwapanana wantumintumi wamonga wa mtuwa gwakuwi kwa shipindi shifaa.
43 Zidzamukhalira bwino wantchito amene mbuye wake adzamupeza akuchita zimene pamene iye abwera.
Mbaka yakuwi ntumintumi ulii, mtuwa gwakuwi pakawuya hakamwoni pakatenda hangu.
44 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti adzamuyika kukhala woyangʼanira katundu wake yense.
Nakaka nukugambirani, mtuwa hakampanani ukulu gwa vintu vyakuwi vyoseri.
45 Koma tiyerekeze kuti wantchitoyo aziganiza mu mtima mwake kuti, ‘Bwana wanga akuchedwa kwambiri kubwera,’ ndipo kenaka ndi kuyamba kumenya antchito aamuna ndi aakazi ndi kudya, kumwa ndi kuledzera.
Kumbiti handa ntumintumi pakalitakulila mweni mumoyu, kuwera mtuwa gwakuwi kakawa shipindi shivuwa nentu kwiza, su kanja kuwakomanga wantumintumi wamonga, woseri wapalu pamuhera na wadala, su kalanda na kuliya shiboga pamuhera na kulanda ujimbi,
46 Mbuye wake adzabwera tsiku limene iye sakumuyembekezera ndi ora limene iye sakudziwa. Iye adzamulanga ndi kumusiya kumalo kumene kuli osakhulupirira.
shakapanu mtuwa gwakuwi ntumintumi ulii hakizi lishaka na shipindi shakashimana ndiri. Mtuwa hakamdumuli vipandi vipandi na kumwasira kunja na kumtula mushipinga shimuhera na yawajimira ndiri.
47 “Wantchito amene amadziwa chifuniro cha mbuye wake koma wosakonzeka kapena wosachita chimene mbuye wake akufuna adzakwapulidwa zikwapu zambiri.
“Ntumintumi yakavimana shakafira mtuwa gwakuwi kutenda, kumbiti kawera ndiri kala kutenda, hawamkomi nentu.
48 Koma wantchito amene sadziwa koma nʼkuchita zinthu zoyenera chilango, adzakwapulidwa zikwapu zochepa. Aliyense amene anapatsidwa zambiri, adzayenera kubwezanso zambiri; ndipo amene anamusungitsa zambiri, adzamulamula kuti abweze zambirinso.”
Kumbiti ntumintumi yakavimana ndiri shilii shakafira mtuwa gwakuwi, na viraa katenda shilii shimtenda wamkomi, hawamkomi padidika. Yawampananiti vivuwa hawamdayi vivuwa, kumbiti yawampananiti vivuwa nentu hawamdayi vintu vivuwa nentu.
49 “Ine ndabwera kudzayatsa moto pa dziko lapansi, ndipo ndikanakonda ukanayaka kale.
“Niza kukoziya motu pasipanu, hera hangu meguweri gwakiti kala!
50 Koma Ine ndiyenera kubatizidwa, ndipo ndikusautsika mu mtima mpaka utachitika!
Nana ubatizu weni nfiruwa nuwanki na ntabika nentu mpaka ukamiliki.
51 Kodi mukuganiza kuti Ine ndinabwera kudzabweretsa mtendere pa dziko lapansi? Ayi, Ine ndikukuwuzani kuti, ndinabweretsa kugawikana.
Mulihola niza kujega ponga pasipanu? Ndala, kumbiti niza kupalanganyiya.
52 Kuyambira tsopano mpaka mʼtsogolo mʼbanja limodzi mudzakhala anthu asanu ndipo adzawukirana wina ndi mnzake, atatu kuwukira awiri, ndipo awiri kuwukira atatu.
Kwanjira vinu na kwendeleya kaya ya wantu wamuhanu hawapalanganyiki na wantu watatu hawalisingani kwa wantu wawili na wantu wawili hawalisingani kwa wantu watatu.
53 Anthu adzawukirana. Abambo kudzawukira mwana wawo wamwamuna, mwana wawoyo adzawukira abambo ake. Amayi adzawukira mwana wawo wamkazi, mwana wawoyo adzawukira amayi ake. Amayi adzawukira mpongozi wawo wamkazi, mpongoziyo adzawukira amayiwo.”
Watati hawalisingani na wana wawu na wana hawalisingani na watati na wamawu hawawalemi wahinga wawu na wahinga hawawalemi wamawu na wanahonga hawawalemi wamika mwana na wamika mwana hawawalemi wanahonga wawu.”
54 Iye anati kwa gulu la anthu, “Pamene mukuona mtambo ukukwera kummawa, nthawi yomweyo inu mumati, ‘kugwa mvula,’ ndipo imagwadi.
Yesu viraa kawagambiriti wantu, “Pamuwona liwundi lilawira kushana, mala mlonga hakatowi na nakaka vula itowa.
55 Ndipo pamene mphepo yakummwera ikuwomba, inu mumati ‘kutentha’ ndipo kumaterodi.
Pamuwona lihemuhemu lya kusika lyankuvuma, mlonga hakuweri na mshenji na nakaka iwera.
56 Achiphamaso inu! Inu mumadziwa kutanthauzira maonekedwe a dziko lapansi ndi thambo. Zikutheka bwanji kuti simukudziwa kumasulira kwa nthawi ino?
Mwawafyangu mwenga! Muvimana kutunga lishaka ntambu yaliwera kwa kulola isi na liyera, kumbiti kwa ntambu gaa muvimana ndiri mana ya shipindi ashi?”
57 “Bwanji simukuzindikira nokha zoyenera kuchita?
“Ntambu gaa msinda kuamuwa maweni kutenda shitwatira shiheri?
58 Pamene mukupita kwa woweruza ndi amene munalakwirana naye, yesetsani kwambiri kuti muyanjane naye mʼnjiramo, chifukwa mukapanda kutero akhoza kukutengerani ku bwalo la milandu ndipo woweruzayo adzakuperekani kwa woyangʼanira ndende, ndipo woyangʼanira ndendeyo adzakuponyani mʼndende.
Handa mstaki gwaku kankukujega pashizyungu, iherepa nentu mulikoli mawoku pamuwera mwankali munjira. Pamutenda ndiri hangu, nakakujega kwa mtoza mweni hakakujegi kwa wamanjagila na womberi hawakutuli mushibetubetu.
59 Ine ndikuwuzani kuti, simudzatulukamo mpaka mutalipira ndalama zonse.”
Nakaka nukugambira hapeni gulawi mulii mpaka gulipi ata ligwala lya kumalalira.”