< Luka 12 >
1 Nthawi yomweyo, anthu miyandamiyanda atasonkhana, ndi kumapondanapondana, Yesu anayamba kuyankhula poyamba kwa ophunzira ake, nati, “Chenjereni ndi yisiti wa Afarisi, amene ndi chinyengo.
Ya yogu ke ku niwulgu den taani ki pundi a tuda, ke bi niba ji ŋmaadi bi lieba, ke o cili ki dá maadi leni o ŋɔdkaaba, “Fangi mani i yuli leni farisienba nɔbli, bani yaaba n pia mi muyima.
2 Palibe chinthu chophimbika chimene sichidzawululika, kapena chobisika chimene sichidzadziwika.
Ama bonlibá ki ye ki duagi, ki kan dɔgdi, bonli ki ye ki wuo, ke bi kan bandi.
3 Chimene mwanena mu mdima chidzamveka dzuwa likuwala, ndipo zimene mwanongʼona mʼkhutu mʼchipinda chamʼkati, zidzayankhulidwa pa denga la nyumba.
Lanwani i, yin maadi yaali li biigli nni, bi ba gbadi li mi yenyenma nni, ke yin sɔbi ki maadi yaali li dieli nni, ke a gana luo, bi ba kpaandi la li dieli binbinli po.
4 “Ine ndikuwuzani, abwenzi anga, musachite mantha ndi amene amapha thupi chifukwa akatero sangachitenso kanthu.
N dɔnlinba, n yedi yi, da jie mani yaaba n ba kpa ti gbannandi, ki ji kan fidi ki tieni libá kuli ki pugni.
5 Koma Ine ndidzakuonetsani amene muyenera kumuopa: Wopani Iye, amene pambuyo pakupha thupi, ali ndi mphamvu yakukuponyani ku gehena. Inde, Ine ndikuwuzani, muopeni Iye. (Geenna )
Ama, n ba tuodi ki waani yi yin ba ya jie yua. Yin jie yua kpa, ki go pia ya paalu n ba lu ŋa ku mubuogu nni. Nn, n maadi yi, jie mani o. (Geenna )
6 Kodi atimba asanu samagulidwa ndi ndalama ziwiri? Ngakhale zili chomwecho palibe imodzi ya izo imene imayiwalika ndi Mulungu.
bi ki kuadi nuanmu mu mu ka kuumu lie e? Leni lani kuli, U Tienu nunga nni, bi kan sundi mu siiga nni bá yenga po.
7 Ndithudi, tsitsi lonse la mʼmutu mwanu ndi lowerengedwa. Musachite mantha; inu ndi oposa kwambiri mpheta zambiri.
Ama yinba wani, bá i yudi, bi cɔdi ki bani ti dugli. Da jie mani pu, i pia muyuli ki cie ya nuankuli n yabi.
8 “Ine ndikukuwuza kuti, aliyense amene avomereza Ine pamaso pa anthu, Mwana wa Munthu adzamuvomerezanso pamaso pa angelo a Mulungu.
N yedi yi, ya nilo kuli n tuo ke o bani nni, bi niba siiga, o 'Ja Bijua' mo ba tuo ke n bani o U Tienu malekinba kani.
9 Koma iye amene andikana Ine pamaso pa anthu adzakanidwanso pamaso pa angelo a Mulungu.
Ama yua nia bi niba siiga ke waa tie n yua, bi ba sundi o po U Tienu malekinba kani.
10 Ndipo aliyense amene ayankhulira Mwana wa Munthu mawu oyipa adzakhululukidwa, koma iye wochitira mwano Mzimu Woyera sadzakhululukidwa.
Yua n maadi mabiadma o 'Ja Bijua' po, ba baa sugli, ama yua n maadi ki sugi U Tienu Foŋanma, o kan baa sugli.
11 “Akadzakutengerani ku masunagoge pamaso pa oweruza ndi a maulamuliro, musadere nkhawa mmene mudzadzitchinjirizire nokha kapena chimene mudzayankhule,
Bi ya dia yi, ki caa leni yi ti jaandiedi nni, ti buudi danba kani leni yikodanba kani ti buudi po, yin da yagi i yama leni yin ba maadi yaala ki fie i yuli, bii yin ba yedi yaala.
12 pakuti Mzimu Woyera nthawi imeneyo adzakuphunzitsani zoyenera kunena.”
Kelima lanyognu liga, U Tienu Foŋanma ba tundi yin ba yedi yaala.
13 Munthu wina mʼgulu la anthu anati kwa Iye, “Aphunzitsi, muwuzeni mʼbale wanga andigawireko chuma chamasiye.”
Ke niyendo yedi o ku niwulgu siiga “Canbaa, maadi n kpelo wan bɔgdi ti báa ń sieni ti ya faali, ki teni nni.
14 Yesu anayankha kuti, “Munthu iwe, ndani anandiyika Ine kukhala woweruza kapena wogawa chuma pakati panu?”
Jesu ń yedi o, “O ja, ŋma n kaani nni ke min ya tie i buudidaano bii i ke min tua i kɔnpaadilo li faali bɔgdima po?
15 Kenaka Iye anawawuza kuti, “Chenjerani! Khalani tcheru ndi makhalidwe onse adyera; moyo wa munthu sukhala chifukwa cha kuchuluka kwa zimene ali nazo.”
Ki yedi ba, “Fangi mani yibá lini mi ŋalmanbuacianma, kelima nilo miali ki ŋua o ŋalmani yabmu ka.
16 Ndipo Iye anawawuza fanizo ili, “Munda wa munthu wina wachuma unabereka kwambiri.
Lani ke Jesu pua ba ya kpanjama ne, “Piado bá den koni ki baa boncianla,
17 Iye anaganiza kuti, ‘Ndichite chiyani? Ndilibe malo osungiramo mbewu zanga.’
ke o kali, ki jagi, ki yedi o pali nni, “N ji ba tieni ledi i, kelima mii ji pia kaanu ki ba bili n kpaandi ne kuli?
18 “Ndipo Iye anati, ichi ndi chimene ndidzachite: Ndidzaphwasula nkhokwe zanga zonse ndi kumanga zokulirapo, ndipo ndidzasungira mʼmenemo mbewu ndi katundu.
ki yedi, “Min ba tieni maama n ne. N ba mumudi n bunbuana, ki guani ki ma yia n tiani, ki bili lien nni n bondikaali leni n bonpiakaali kuli.
19 Ndipo ndidzawuza moyo wanga kuti, ‘Uli nazo zinthu zabwino zambiri zimene zikhalepo zaka zambiri, usapupulume; idya, imwa ndi kukondwera.’”
Lani, n ji ba pagi n yuli “Mini, min bili ya piama kandi, ki ba tuoni nni ya bina n yabi. Ya kaa, ki fuo, ki di, ki ñu, ki mangdi a pali.
20 “Koma Mulungu anati kwa iye, ‘Iwe wopusa! Usiku womwe uno moyo wako udzachotsedwa kwa iwe, ndipo ndi ndani amene adzatenge zimene iwe wadzikonzera?’
Ama, ke U Tienu yedi o “O yanluodaano ne, dinne ñiagu liga i, ke n ba ñani a naano, ki ŋa a. ŋan bili yaali kuli ba tua ŋma ya yaali i?
21 “Umu ndi mmene zidzakhalire ndi aliyense amene amadziwunjikira chuma, koma si wachuma pamaso pa Mulungu.”
Li tie nani yua n taagi mi piama o yuli po, ki nan ki pia pu U Tienu kani.”
22 Kenaka Yesu anati kwa ophunzira ake, “Choncho Ine ndikuwuzani kuti musadere nkhawa za moyo wanu, zimene mudzadya; kapena za thupi lanu, zimene mudzavala.
Jesu yedi o ŋɔdkaaba, “lanwani i, yin da buali i miali po, yin ba di yaali bii, i gbanu po, li bonlakaali po
23 Moyo uposa chakudya, ndi thupi liposa chovala.
Kelima, li miali gie ti jiedi, ke u gbanu mo cie ti tialakaadi.
24 Taonani makwangwala: iwo safesa kapena kukolola, alibe nyumba zosungamo zinthu kapena nkhokwe; komabe, Mulungu amawadyetsa. Koposa kotani inu amene ndi ofunikira kuposa mbalame.
Diidi mani a bonyugda, baa buu, baa yendi, baa pia bilkaanu, baa pia bɔnbuana, ama U Tienu nan dingi a. yinba, i pia mayuli ki cie ti bonyugditi!
25 Ndi ndani wa inu akhoza kuwonjeza ora pa moyo wake chifukwa cha kudandaula?
I siiga, ŋma ba fidi ki fagni o miali bá a dana waamu?
26 Popeza simungathe kuchita kanthu kakangʼono aka, nʼchifukwa chiyani mumadandaula ndi zinazi?
I ya ya bani ke i kan fidi ki tieni yaali n waa ki cie ne, be ya po i ke i maali yaali n sieni kuli po o?
27 “Taonani mmene maluwa amakulira. Iwo sagwira ntchito kapena kusoka zovala. Koma Ine ndikuwuzani kuti, ngakhale Solomoni muulemelero wake wonse sanavalepo ngati limodzi la awa.
Diidi mani ti puudi ń tie maama, tii tuuni, tii pia gaalu mo, ama bá o badciamo Salomɔn leni o kpiagdi, waa pundi bi siiga bá yengu ń bobi maama.
28 Ngati umu ndi mmene Mulungu amavekera udzu wakuthengo, umene lero ulipo ndipo mawa uponyedwa pa moto, nanga Iye adzakuvekani inu motani. Haa! Inu achikhulupiriro chochepa!
U Tienu ya bobindi u kuanu nni muadi yeni, tini yaadi ye dinne ke bi ba faa ki taa ti, ki kuuni u fanu nni, ki cuoni umu, li ki pia tama ke o ba bobni yi mo, oo yinba yaaba ya dudugdi n ki pia fuoma!
29 Ndipo musayike mtima wanu pa zimene mudzadye kapena kumwa; musade nazo nkhawa.
Da buali mani yin ba di yaali leni yin ba ñu yaali po, ki go da yagni i yama.
30 Pakuti anthu akunja amathamanga kufunafuna zinthu zotere, ndipo Atate amadziwa kuti mumazifuna zimenezi.
Kelima ŋanduna dogi kuli lingi lanya bona i, ke i Báa moko bani ke i bua li bona.
31 Koma funafunani ufumu wake, ndipo mudzapatsidwa zonsezi.
Ama yin lingi mani o diema, i ba baa lanya bona ki pugni
32 “Musachite mantha, inu kagulu kankhosa, pakuti zinakondweretsa Atate anu kuti akupatseni ufumu.
Da jie mani ba waamu, kelima i Báa pali mani ke wan puni yi o diema.
33 Gulitsani zonse zimene muli nazo, ndipo ndalama zake mupereke kwa osauka. Dzipezereni zikwama zandalama zimene sizidzatha, ndi kudzikundikira chuma chomwe sichidzatha kumwamba, kumene mbala sizingafikeko, ndipo dzimbiri silingawononge.
Kuadi mani i piama, ki puni a luoda li ligi. ŋali mani i po ya ligbɔgli n kan cadi, ŋaljanli nni ya ŋalmani yaali n ki pia gbenma.
34 Popeza kumene kuli chuma chanu, mtima wanunso udzakhala komweko.”
Kelima a ŋalmani ń ye naani, a pali mo ye lankani i.
35 “Khalani okonzekeratu ndipo nyale zanu ziziyaka,
N̄agni mani i liadfagda u gbanñagdu, i fidsanmu ń ya tundi ki co;
36 ngati anthu oyembekezera kubwera kwa mbuye wawo kuchokera kuphwando la ukwati, kuti pamene afika ndi kugogoda akhoza nthawi yomweyo kumutsekulira chitseko.
Yin ya tie nani ya niba n guu bi canbáa ń ba ña mi pocaajaama po, ki kpeni yeni, o ya pua li ganli ya yognu, ban kagni ki luodi o po.
37 Zidzakhala bwino kwa antchitowo amene mbuye wawo pobwera adzawapeze akudikira. Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti adzakonzekera kuwatumikira, adzakhala nawo pa tebulo ndipo adzabwera ndi kuwatumikira.
Ya tuonsɔnba, ke bi canbáa ba pundi ki sua ke bi dá nua, bani baa mi yedŋanma n yeni. I mɔmɔni, n maadi yi, o ba ñagni o gaaligu u gbanñagdu, ki cedi ban kali u jedikaanu, wan tieni ba mi jiema ban je.
38 Zidzakhala bwino kwa antchitowo amene mbuye wawo adzawapeze ali okonzeka, ngakhale iye atabwera pa ora lachiwiri kapena lachitatu usiku.
Canbàa ya pundi yɔgsiigu bii siŋaafaani, ki sua ke bi cegni ki guu o, lan ya tuonsɔnba baa mi yedŋanma n yeni.
39 Koma zindikirani izi: Ngati mwini nyumba akanadziwa ora limene mbala ibwera, sakanalola kuti nyumba yake ithyoledwe.
Ama, min ba pugni yaali n ne, yin ya bani ke o diedaano ya bi bani ya yognu ke o suuro ba kua o deni ki suu o, o bi kan ŋa ban kua o deni ki su o,
40 Inunso muyenera kukhala okonzeka, chifukwa Mwana wa Munthu adzabwera pa ora limene simukumuyembekezera Iye.”
Yin egni iba, ki ya guu kelimaa i ki baniO Ja bijua n ́ ba guaniya yognu.
41 Petro anafunsa kuti, “Kodi mukunena fanizoli kwa ife, kapena kwa aliyense?”
Pieri ń buali: «O Diedo, a pua lan ya kpanjama tinba baba ya po bii, li tie yuakuli ya po i?»
42 Ambuye anayankha kuti, “Kodi tsono woyangʼanira wokhulupirika ndi wanzeru ndani? Kodi ndi amene mbuye wake wamuyika kukhala oyangʼanira antchito ake kuti aziwapatsa ndalama yachakudya pa nthawi yake yoyenera?
O Diedo ń yedi: «O laa tuonsɔnlo i, ke o canbáa ba guuni ke wan ya diidi o tuonsɔnlieba tuona, ki puuni ba bi daali jiema lan buali ya yognu,
43 Zidzamukhalira bwino wantchito amene mbuye wake adzamupeza akuchita zimene pamene iye abwera.
o canbáa ya kpeni ki sua ke o tuuni lan buali maama, lanya tuonsɔnlo baa mi yedŋanma n yeni.
44 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti adzamuyika kukhala woyangʼanira katundu wake yense.
I mɔmɔni n maadi yi, canbáa ba taa o piama kuli ki piani lanya tonsɔnlo.
45 Koma tiyerekeze kuti wantchitoyo aziganiza mu mtima mwake kuti, ‘Bwana wanga akuchedwa kwambiri kubwera,’ ndipo kenaka ndi kuyamba kumenya antchito aamuna ndi aakazi ndi kudya, kumwa ndi kuledzera.
Ama li tuonsɔnlo ya maadi o pali nni: «N canbáa kpenma dá ba fagdi», ki ji cili ki pua o tuonsɔnlieba, bi jaba yeni bi puoba kuli, ki go cili ki di ki go ñu wan bua maama, ke mi daama ga o.
46 Mbuye wake adzabwera tsiku limene iye sakumuyembekezera ndi ora limene iye sakudziwa. Iye adzamulanga ndi kumusiya kumalo kumene kuli osakhulupirira.
O ya tie yeni, o canbáa ba ti ludi ki kpeni wan ki guu o ya yognu, ki cedi ban pua ki duoli o kaani kuli, ki beli ki ñani o, ki kuani o bi tuonsɔbiadba danba siiga nni.
47 “Wantchito amene amadziwa chifuniro cha mbuye wake koma wosakonzeka kapena wosachita chimene mbuye wake akufuna adzakwapulidwa zikwapu zambiri.
Nani li tuosɔnlo ń den bani o canbáa ń bili o ya tuonli yeni i, ki nan ki sɔni lan buali maama yeni i, o canbáa ba cedi ban pua o ya lanbana n yabi.
48 Koma wantchito amene sadziwa koma nʼkuchita zinthu zoyenera chilango, adzakwapulidwa zikwapu zochepa. Aliyense amene anapatsidwa zambiri, adzayenera kubwezanso zambiri; ndipo amene anamusungitsa zambiri, adzamulamula kuti abweze zambirinso.”
Ama, ya tuonsɔnlo n ki tuodi ki bani, ki sɔni ya tuonli n buali ke lan dadi o tubli ii, bi ba pua o lanbana waaamu. Ban teni yua ke li yabi, bi ba buali o yaali n yabi. Ban piani yua yaali n cie, bi ba buali o yaali n cie.
49 “Ine ndabwera kudzayatsa moto pa dziko lapansi, ndipo ndikanakonda ukanayaka kale.
«N cua ki tinga po ke min sia mu i. N sugni ke li mu ji co i.
50 Koma Ine ndiyenera kubatizidwa, ndipo ndikusautsika mu mtima mpaka utachitika!
N pia mi ñinwulma, ke bi ba wuli nni. I ki bani min bua tonma maama, ke li kuli ń tieni ki tii.
51 Kodi mukuganiza kuti Ine ndinabwera kudzabweretsa mtendere pa dziko lapansi? Ayi, Ine ndikukuwuzani kuti, ndinabweretsa kugawikana.
I tama ke n cua ki tinga po yeni mi yanduanma yo oo? N n! I mɔmɔni, n maadi yi, n cua yeni mi paadma i.
52 Kuyambira tsopano mpaka mʼtsogolo mʼbanja limodzi mudzakhala anthu asanu ndipo adzawukirana wina ndi mnzake, atatu kuwukira awiri, ndipo awiri kuwukira atatu.
Kelimaa, lan cili mɔlane, dieyengu nni, niba mu ba paadi, niba lie ń kɔni yeni niba taa; niba taa mo ń kɔni yeni niba lie.
53 Anthu adzawukirana. Abambo kudzawukira mwana wawo wamwamuna, mwana wawoyo adzawukira abambo ake. Amayi adzawukira mwana wawo wamkazi, mwana wawoyo adzawukira amayi ake. Amayi adzawukira mpongozi wawo wamkazi, mpongoziyo adzawukira amayiwo.”
Bi ba paadi bibáa ń kɔni yeni o bijaba, a bila mo ń kɔni yeni bibáa. Binaá ba kɔni yeni o bisiaba, a bisala mo ń kɔni yeni binaá. Calnaá ba kɔni yeni o biyuaga, ki biyuaga ń kɔni yeni calnaá.»
54 Iye anati kwa gulu la anthu, “Pamene mukuona mtambo ukukwera kummawa, nthawi yomweyo inu mumati, ‘kugwa mvula,’ ndipo imagwadi.
Jesu go den maadi ku niwulgu yaali ne: «I ya la taayinbɔnu puoli, i yi maadi: “Ki taaga ba nii!” Lan go tieni yeni.
55 Ndipo pamene mphepo yakummwera ikuwomba, inu mumati ‘kutentha’ ndipo kumaterodi.
Mi faawaama ya fii nintuali, i yi maadi: “Ku wulgu ba tieni!” Lan go tua yeni.
56 Achiphamaso inu! Inu mumadziwa kutanthauzira maonekedwe a dziko lapansi ndi thambo. Zikutheka bwanji kuti simukudziwa kumasulira kwa nthawi ino?
Yinba i muyiidmu ne! I fidi ki diidi ki tinga maalma yeni tanpoli maalma, ki bandi a bona. Li nan tieni ledi i, ke yi ki fidi ki bandi U tienu n ́ bobindi yaali mɔlane?
57 “Bwanji simukuzindikira nokha zoyenera kuchita?
Li tieni ledi i, ke yi kan fidi ki tuodi ki cegni yaali n tiegi i po mɔlane?
58 Pamene mukupita kwa woweruza ndi amene munalakwirana naye, yesetsani kwambiri kuti muyanjane naye mʼnjiramo, chifukwa mukapanda kutero akhoza kukutengerani ku bwalo la milandu ndipo woweruzayo adzakuperekani kwa woyangʼanira ndende, ndipo woyangʼanira ndendeyo adzakuponyani mʼndende.
A ya caa ti buudi yeni a yibali, ŋan mɔndi ki mangi yeni o u sanu nni, wan da ti cedi ti buudi yudanba ń buu ki cuo a, ban mubni a bi paatieba nui nni, ban luoni a li kpaadidieli nni.
59 Ine ndikuwuzani kuti, simudzatulukamo mpaka mutalipira ndalama zonse.”
N maadi a, a kan ña li kpaadidieli nni, kaa pani a pana kuli ki gbeni.»