< Luka 11 >

1 Tsiku lina Yesu amapemphera pamalo ena. Atamaliza, mmodzi wa ophunzira ake anati kwa Iye, “Ambuye tiphunzitseni kupemphera, monga momwe Yohane anaphunzitsira ophunzira ake.”
and to be in/on/among the/this/who to exist it/s/he in/on/among place one to pray as/when to cease to say one the/this/who disciple it/s/he to/with it/s/he lord: God to teach me to pray as/just as and John to teach the/this/who disciple it/s/he
2 Yesu anawawuza kuti, “Pamene mukupemphera muzinena kuti: “‘Atate, dzina lanu lilemekezedwe, ufumu wanu ubwere.
to say then it/s/he when(-ever) to pray to say father (me the/this/who in/on/among the/this/who heaven *K*) to sanctify the/this/who name you to come/go the/this/who kingdom you (to be *KO*) (the/this/who will/desire you as/when in/on/among heaven and upon/to/against the/this/who earth: planet *K*)
3 Mutipatse chakudya chathu chalero,
the/this/who bread me the/this/who daily to give me the/this/who according to day
4 mutikhululukire machimo athu, monga ifenso timakhululukira aliyense amene watilakwira. Ndipo musalole kuti tigwe mʼmayesero.’”
and to release: forgive me the/this/who sin me and for it/s/he to release: forgive all to owe me and not to bring in me toward temptation/testing: temptation (but to rescue me away from the/this/who evil/bad *K*)
5 Kenaka anawawuza kuti, “Tiyerekeze: Mmodzi mwa inu atakhala ndi bwenzi lake, ndipo iye nʼkupita ku nyumba yake pakati pa usiku, nakanena kuti, ‘Mnzanga, bwereke malofu atatu abuledi,
and to say to/with it/s/he which? out from you to have/be friendly/friend and to travel to/with it/s/he midnight and to say it/s/he friendly/friend to lend me Three bread
6 chifukwa ndalandira bwenzi langa amene ali pa ulendo ndipo ine ndilibe choti ndimupatse.’
since friendly/friend me to come out from road to/with me and no to have/be which to set before it/s/he
7 “Ndipo yerekezani kuti amene ali mʼnyumbamo ndi kuyankha kuti, ‘Usandivutitse ine, ndatseka kale chitseko, ndipo ine ndi ana anga tagona. Ine sindingadzukenso kuti ndidzakupatse.’
and that inwardly to answer to say not me labor to furnish occasion already the/this/who door to shut and the/this/who child me with/after I/we toward the/this/who bed to be no be able to arise to give you
8 Ine ndikukuwuzani kuti adzadzuka ndi kumupatsa bulediyo, osati chifukwa ndi bwenzi lake, koma chifukwa cha liwuma la munthu wopemphayo, ndipo kudzamupatsa zonse zimene akuzifuna.
to say you if: even though and no to give it/s/he to arise through/because of the/this/who to exist friendly/friend it/s/he through/because of indeed the/this/who shamelessnes it/s/he to arise to give it/s/he (just as/how much *NK(o)*) to need
9 “Choncho Ine ndikunena kwa inu kuti: Pemphani ndipo adzakupatsani. Funafunani ndipo mudzapeza. Gogodani ndipo adzakutsekulirani.
I/we and you to say to ask and to give you to seek and to find/meet to knock and to open you
10 Pakuti aliyense amene amapempha amalandira. Munthu amene amafunafuna amapeza. Iye amene amagogoda amamutsekulira.
all for the/this/who to ask to take and the/this/who to seek to find/meet and the/this/who to knock to open
11 “Ndani mwa inu abambo, kodi mwana wanu atapempha nsomba, mʼmalo mwake mungamupatse njoka?
which? then (out from *no*) you the/this/who father to ask the/this/who son (bread not stone to give/deliver it/s/he *KO*) (if *K(o)*) fish and (not *ko*) for fish snake it/s/he to give/deliver
12 Kapena atapempha dzira, kodi mungamupatse chinkhanira?
or and (if *K*) (to ask *NK(O)*) an egg (not *ko*) to give/deliver it/s/he scorpion
13 Tsono ngati inu, anthu oyipa, mumadziwa kupereka mphatso zabwino kwa ana anu, koposa kotani Atate anu akumwamba, angalephere bwanji kupereka Mzimu Woyera kwa amene awapempha!”
if therefore/then you evil/bad be already to know gift good to give the/this/who child you how much/many? more the/this/who father the/this/who out from heaven to give spirit/breath: spirit holy the/this/who to ask it/s/he
14 Yesu amatulutsa chiwanda chimene chinali chosayankhula. Chiwandacho chitatuluka, munthu wosayankhulayo anayankhula, ndipo gulu la anthu linadabwa.
and to be to expel demon and it/s/he to be deaf/mute to be then the/this/who demon to go out to speak the/this/who deaf/mute and to marvel the/this/who crowd
15 Koma ena mwa iwo anati, “Iye akutulutsa ziwanda ndi mphamvu ya Belezebabu mfumu ya ziwanda.”
one then out from it/s/he to say in/on/among Beelzebul (the/this/who *no*) ruler the/this/who demon to expel the/this/who demon
16 Ena anamuyesa pomufunsa chizindikiro chochokera kumwamba.
other then to test/tempt: test sign out from heaven to seek from/with/beside it/s/he
17 Yesu anadziwa maganizo awo ndipo anawawuza kuti, “Ufumu uliwonse wogawikana udzawonongeka, ndipo nyumba yogawikana idzapasuka.
it/s/he then to know it/s/he the/this/who thought to say it/s/he all kingdom upon/to/against themself to divide to lay waste and house: household upon/to/against house: household to collapse
18 Ngati Satana adziwukira yekha, ufumu wake ungalimbe bwanji? Ine ndikunena izi chifukwa inu mukuti Ine ndimatulutsa ziwanda ndi mphamvu ya Belezebabu.
if then and the/this/who Satan upon/to/against themself to divide how! to stand the/this/who kingdom it/s/he that/since: since to say in/on/among Beelzebul to expel me the/this/who demon
19 Tsopano ngati Ine ndimatulutsa ziwanda ndi mphamvu ya Belezebabu, nanga ophunzira anu amazitulutsa ndi mphamvu ya ndani? Choncho, iwowo ndiye adzakhala oweruza anu.
if then I/we in/on/among Beelzebul to expel the/this/who demon the/this/who son you in/on/among which? to expel through/because of this/he/she/it it/s/he you judge to be
20 Koma ngati ndimatulutsa ziwanda ndi mphamvu ya Mulungu, ndiye kuti ufumu wa Mulungu wafika pakati panu.
if then in/on/among finger God (I/we *no*) to expel the/this/who demon therefore to precede/arrive upon/to/against you the/this/who kingdom the/this/who God
21 “Munthu wamphamvu, amene ali ndi zida, akamalondera nyumba yake, katundu wake amatetezedwa.
when(-ever) the/this/who strong to arm fully to keep/guard: guard the/this/who themself palace/courtyard in/on/among peace to be the/this/who be already it/s/he
22 Koma pakabwera wina wamphamvu zoposa namugonjetsa, amalanda zida zimene munthuyo amazidalirazo ndi kugawa katundu wake.
when/as soon as then (the/this/who *k*) strong it/s/he to arrive/invade to conquer it/s/he the/this/who complete armor it/s/he to take up upon/to/against which to persuade and the/this/who plunder it/s/he to distribute
23 “Munthu amene sali mbali yanga ndi wotsutsana nane. Ndipo wosandithandiza kusonkhanitsa, ameneyo ndi womwaza.
the/this/who not to be with/after I/we according to I/we to be and the/this/who not to assemble with/after I/we to scatter
24 “Mzimu woyipa ukatuluka mwa munthu, umakayendayenda ku malo owuma, kufunafuna malo opumulirako ndipo suwapeza. Kenaka umati, ‘Ndibwerera ku nyumba kwanga kumene ndachokera.’
when(-ever) the/this/who unclean spirit/breath: spirit to go out away from the/this/who a human to pass through through/because of waterless place to seek rest and not to find/meet (then *NO*) to say to return toward the/this/who house: home me whence to go out
25 Ukafika umapeza mʼnyumba mosesedwa bwino ndi mokonza.
and to come/go to find/meet (be devoted/empty *O*) to sweep and to arrange
26 Pamenepo umakatenga mizimu ina isanu ndi iwiri yoyipa kwambiri kuposa iwowo ndipo imakalowa ndi kukhala mʼmenemo. Ndipo makhalidwe otsiriza a munthuyo amakhala oyipa kuposa oyamba aja.”
then to travel and to take other spirit/breath: spirit evil/bad themself seven and (to enter *NK(o)*) to dwell there and to be the/this/who last/least the/this/who a human that worse than the/this/who first
27 Pamene Yesu ankanena zonsezi, mayi wina mʼgulu la anthuwo anafuwula nati, “Ndi wodala amayi amene anakubalani ndi kukulerani!”
to be then in/on/among the/this/who to say it/s/he this/he/she/it to lift up one voice/sound: voice woman out from the/this/who crowd to say it/s/he blessed the/this/who belly/womb/stomach the/this/who to carry you and breast which to suckle
28 Koma Yesu anayankha kuti, “Odala ndi amene amamva mawu a Mulungu ndi kuwasunga.”
it/s/he then to say rather blessed the/this/who to hear the/this/who word the/this/who God and to keep/guard: observe (it/s/he *k*)
29 Pamene gulu la anthu limachuluka, Yesu anati, “Uno ndi mʼbado oyipa. Umafuna kuona chizindikiro chodabwitsa. Koma sadzachiona kupatula chizindikiro chija cha Yona.
the/this/who then crowd to collect/crowd be first to say the/this/who generation this/he/she/it (generation *no*) evil/bad to be sign (to seek *N(k)O*) and sign no to give it/s/he if: not not the/this/who sign Jonah (the/this/who prophet *K*)
30 Monga Yona uja anali chizindikiro kwa anthu ku Ninive, momwemonso Mwana wa Munthu adzakhala chizindikiro kwa anthu a mʼbado uno.
as/just as for to be (the/this/who *o*) Jonah the/this/who Ninevite sign thus(-ly) to be and the/this/who son the/this/who a human the/this/who generation this/he/she/it
31 Mfumu yayikazi yakummwera idzayimirira tsiku lachiweruzo pamodzi ndi anthu a mʼbado uno ndipo idzawatsutsa, chifukwa iyo inachokera kumapeto a dziko lapansi kudzamva nzeru za Solomoni. Ndipo tsopano pano pali wina woposa Solomoni.
queen (Queen of) the South to arise in/on/among the/this/who judgment with/after the/this/who man the/this/who generation this/he/she/it and to condemn it/s/he that/since: since to come/go out from the/this/who end the/this/who earth: planet to hear the/this/who wisdom Solomon and look! greater Solomon here
32 Anthu a ku Ninive adzayimirira tsiku lachiweruzo pamodzi ndi mʼbado uno ndipo adzawutsutsa, pakuti anatembenuka mtima ndi ulaliki wa Yona. Ndipo tsopano pano pali wina woposa Yona.
man (Ninevite *N(k)O*) to arise in/on/among the/this/who judgment with/after the/this/who generation this/he/she/it and to condemn it/s/he that/since: since to repent toward the/this/who preaching Jonah and look! greater Jonah here
33 “Palibe amene amayatsa nyale ndi kuyiika pa malo poti sionekera, kapena pansi pa mtsuko. Mʼmalo mwake amayika pa choyikapo chake, kuti iwo amene akulowamo aone kuwunika.
none (then *k*) lamp to touch toward (cellar *N(K)O*) to place nor by/under: under the/this/who bucket but upon/to/against the/this/who lampstand in order that/to the/this/who to enter the/this/who (light *N(k)O*) to see
34 Diso lanu ndi nyale ya thupi lanu. Pamene maso anu ali bwino, thupi lanu lonse limadzaza ndi kuwunika. Koma ngati ali oyipa, thupi lanunso ndi lodzaza ndi mdima.
the/this/who lamp the/this/who body to be the/this/who eye (you *no*) when(-ever) (therefore/then *K*) the/this/who eye you sound to be and all the/this/who body you bright to be when/as soon as then evil/bad to be and the/this/who body you dark
35 Onetsetsani tsono, kuti kuwunika kuli mwa inu si mdima.
to watch out therefore/then not the/this/who light the/this/who in/on/among you darkness to be
36 Choncho, ngati thupi lanu lonse ndi lodzaza ndi kuwunika, ndiye kuti palibe dera lina lili mdima, lonselo lidzakhala kuwunika, monga momwe kuwunika kwa nyale kumakuwalirani.”
if therefore/then the/this/who body you all bright not to have/be part one dark to be bright all as/when when(-ever) the/this/who lamp the/this/who lightning to illuminate you
37 Yesu atamaliza kuyankhula, Mfarisi wina anamuyitana kuti akadye naye. Tsono Yesu analowa mʼnyumba ndi kukhala podyera.
in/on/among then the/this/who to speak (to ask *N(k)O*) it/s/he Pharisee (one *k*) that to eat early meal from/with/beside it/s/he to enter then to recline
38 Mfarisiyo anadabwa atazindikira kuti Yesu anayamba kudya wosatsata mwambo wawo wakasambidwe ka mʼmanja.
the/this/who then Pharisee to perceive: see to marvel that/since: that no first to baptize before the/this/who early meal
39 Kenaka Ambuye anamuwuza kuti, “Inu Afarisi mumatsuka kunja kwa chikho ndi mbale, koma mʼkati mwanu ndi modzaza ndi kudzikonda ndi zoyipa.
to say then the/this/who lord: God to/with it/s/he now you the/this/who Pharisee the/this/who outside the/this/who cup and the/this/who platter to clean the/this/who then inwardly you be full plunder and evil
40 Anthu opusa inu! Kodi amene anapanga zamʼkati sanapangenso zakunja?
foolish no the/this/who to do/make: do the/this/who outside and the/this/who inwardly to do/make: do
41 Koma popereka kwa osauka, perekani chimene chili mʼkati ndipo chilichonse chidzakhala choyera.
but/however the/this/who be in to give charity and look! all clean you to be
42 “Tsoka kwa inu Afarisi, chifukwa mumapereka kwa Mulungu chakhumi cha timbewu tonunkhira, ndi timbewu tokometsera chakudya ndi mbewu zina zonse za mʼmunda, koma mumakana chilungamo ndi chikondi cha Mulungu. Mumayenera kuchita zomalizirazi osalekanso kuchita zoyambazi.
but woe! you the/this/who Pharisee that/since: since to tithe the/this/who mint and the/this/who rue and all plant and to pass by the/this/who judgment and the/this/who love the/this/who God this/he/she/it (then *NO*) be necessary to do/make: do and that not (be present *N(k)O*)
43 “Tsoka kwa inu Afarisi, chifukwa mumakonda mipando yofunika kwambiri mʼmasunagoge ndi malonje mʼmalo a pa msika.
woe! you the/this/who Pharisee that/since: since to love the/this/who seat of honor in/on/among the/this/who synagogue and the/this/who salutation in/on/among the/this/who marketplace
44 “Tsoka kwa inu Afarisi, chifukwa muli ngati manda osawaka, amene anthu amangoyendapo, osawadziwa.”
woe! you (scribe and Pharisee hypocrite *K*) that/since: since to be as/when the/this/who grave the/this/who unclear and the/this/who a human the/this/who to walk above no to know
45 Mmodzi mwa akatswiri a Malamulo anamuyankha Iye nati, “Aphunzitsi, pamene mukunena zinthu izi, mukutinyoza ifenso?”
to answer then one the/this/who lawyer to say it/s/he teacher this/he/she/it to say and me to mistreat
46 Yesu anayankha kuti, “Tsoka kwa inunso akatswiri a Malamulo chifukwa mumawalemetsa anthu ndi mtolo umene iwo sangathe kunyamula, ndipo inu eni ake simutenga chala chanu kuti muwathandize.
the/this/who then to say and you the/this/who lawyer woe! that/since: since to burden the/this/who a human burden ponderous and it/s/he one the/this/who finger you no to touch the/this/who burden
47 “Tsoka kwa inu, chifukwa mumawaka manda a aneneri, komatu ndi makolo anu amene anawapha.
woe! you that/since: since to build the/this/who grave the/this/who prophet the/this/who then father you to kill it/s/he
48 Tsono potero mumachitira umboni za zimene makolo anu anachita. Anapha aneneri, ndipo inu mumawaka manda awo.
therefore (witness *N(k)O*) (to be *no*) and to agree to the/this/who work the/this/who father you that/since: since it/s/he on the other hand to kill it/s/he you then to build (it/s/he *K*) (the/this/who *k*) (grave *K*)
49 Chifukwa cha ichi, Mulungu mu nzeru zake anati, ‘Ine ndidzawatumizira aneneri ndi atumwi, ena mwa iwo adzawapha ndipo ena adzawazunza.’
through/because of this/he/she/it and the/this/who wisdom the/this/who God to say to send toward it/s/he prophet and apostle and out from it/s/he to kill and (to pursue *N(k)O*)
50 Choncho mʼbado uwu udzasenza magazi a aneneri onse amene anakhetsedwa kuyambira pachiyambi cha dziko,
in order that/to to seek out the/this/who blood all the/this/who prophet the/this/who (to pour out *N(k)O*) away from beginning world away from the/this/who generation this/he/she/it
51 kuyambira magazi a Abele kufikira magazi a Zakariya amene anaphedwa pakati pa guwa lansembe ndi malo opatulika. Inde, Ine ndikuwuzani inu, mʼbado uno udzasenza zonsezi.
away from (the/this/who *k*) blood Abel until (the/this/who *k*) blood Zechariah the/this/who to destroy between/meanwhile the/this/who altar and the/this/who house: household yes to say you to seek out away from the/this/who generation this/he/she/it
52 “Tsoka kwa inu akatswiri a Malamulo, chifukwa mwachotsa kiyi wachidziwitso inu eni akenu musanalowemo, ndipo mwatsekerezanso iwo amene amalowa.”
woe! you the/this/who lawyer that/since: since to take up the/this/who key the/this/who knowledge it/s/he no to enter and the/this/who to enter to prevent
53 Pamene Yesu anachokamo, Afarisi ndi aphunzitsi a Malamulo anayamba kumamutsutsa koopsa ndi kumupanikiza ndi mafunso,
(and from there *no*) (to go out *N(k)O*) (then *k*) it/s/he (this/he/she/it to/with it/s/he *k*) be first the/this/who scribe and the/this/who Pharisee terribly to oppose and to interrogate it/s/he about greater
54 pofuna kumukola muchina chilichonse chimene Iye angayankhule.
to ambush it/s/he (and *K*) (to seek *KO*) to hunt/catch one out from the/this/who mouth it/s/he (in order that/to to accuse it/s/he *KO*)

< Luka 11 >