< Levitiko 7 >

1 “‘Malamulo a nsembe yopepesera kupalamula imene ndi nsembe yopatulika kwambiri ndi awa:
Te dongah hmaithennah olkhueng he a cim khuikah a cim koek la om.
2 Nsembe yopepesera machimo iziphedwa pamalo pomwe amaphera nsembe yopsereza ndipo awaze magazi ake mbali zonse za guwa.
Hmueihhlutnah a ngawn uh hmuen ah hmaithennah te ngawn uh saeh lamtah a thii te hmueihtuk kaepvai ah haeh saeh.
3 Tsono apereke mafuta ake onse: mchira wamafuta ndi mafuta amene amakuta matumbo.
Te vaengah a kawl dongkah a tha boeih neh a kotak aka dah maehtha te nawn saeh.
4 Aperekenso impsyo ziwiri, mafuta ake pamodzi ndi mafuta onse amene ali chamʼchiwuno, ndiponso mafuta onse amene aphimba chiwindi.
A kuel rhoi neh a uen kaep dongkah maehtha khaw, a thin dongkah a thinhnun te khaw a kuel neh rhen hluep saeh.
5 Wansembe azitenthe pa guwa kuti zikhale nsembe yotentha pa moto, yoperekedwa kwa Yehova. Imeneyi ndi nsembe yopepesera tchimo lopalamula.
Te phoeiah hmaithennah te BOEIPA taengkah hmueihtuk sokah hmaihlutnah dongah khosoih loh phum saeh.
6 Munthu wamwamuna aliyense wa mʼbanja la wansembe angathe kudyako nsembeyo koma adyere ku malo opatulika. Imeneyi ndi nsembe yopatulika kwambiri.
Hmueihlutnah maeh te khosoih tongpa boeih loh hmuen cim ah ca uh saeh lamtah a cim khuikah a cim koek la ca saeh.
7 “‘Nsembe yopepesera tchimo lopalamula ndi yofanana ndi nsembe yoperekedwa chifukwa cha tchimo. Ndipo nsembe ziwiri zonsezi zili ndi lamulo limodzi lokha. Wansembe amene wachita mwambo wa nsembe yopepesera machimo a kupalamula atenge nyamayo ngati yake.
Boirhaem khaw hmaithennah khaw a olkhueng pakhat la a om dongah dawth ham koi te khosoih hut la om.
8 Wansembe wopereka nsembe yopsereza ya munthu wina aliyense, atenge chikopa cha nsembe yopserezayo kuti chikhale chake.
Te dongah khosoih loh hlang khat khat kah hmueihhlutnah te a nawn pah vaengah a nawn hmueihhlutnah kah a pho khaw khosoih amah hut la om saeh.
9 Chopereka chilichonse cha chakudya chophika mu uvuni kapena chokazinga mu mʼphika kapena mu chiwaya ndi cha wansembe amene wapereka nsembezo.
Tapkhuel dongkah a thong khocang boeih, thi-am dongkah neh thiphael dongkah a saii boeih khaw khocang aka nawn khosoih amah hut la om saeh.
10 Ndipo chopereka china chilichonse cha chakudya chosakaniza ndi mafuta kapena chowuma, chikhale cha ana onse a Aaroni ndipo anawo achigawane mofanana.
Situi neh a thoek khaw, a kaksap akhaw khocang boeih tah Aaron koca rhoek boeih neh amih boeinaphung ham rhip om saeh.
11 “‘Malamulo a nsembe ya chiyanjano imene munthu angathe kupereka kwa Yehova ndi awa:
Tedae tahae kah he tah BOEIPA taengah rhoepnah hmueih a nawn vaengkah olkhueng ni.
12 “‘Ngati munthuyo apereka chifukwa cha kuthokoza, apereke nsembeyo pamodzi ndi makeke wopanda yisiti, osakaniza ndi mafuta; timitanda ta buledi wopanda yisiti, topyapyala, topaka mafuta, ndiponso makeke a ufa wosalala wophikidwa bwino, wosakaniza ndi mafuta.
Uemonah ham a nawn atah uemonah hmueih la situi neh a thoek vaidamding vaidam laep khaw, situi neh a koelh vaidamding kah vaidam rhawm khaw, situi neh a thoek tih a kae vaidam laep khaw nawn saeh.
13 Pamodzi ndi nsembe yachiyanjano yothokozerayo abwerenso ndi makeke opangidwa ndi yisiti ngati chopereka chake.
Te vaengkah tolrhu buhham vaidam laep te uemonah, rhoepnah hmueih neh nawnnah la nawn saeh.
14 Munthuyo atenge mtanda umodzi pa mtanda wa buledi wa mtundu uliwonse kuti ukhale nsembe yopereka kwa Yehova. Tsono mtanda umenewo ndi wake wa wansembe amene awaze magazi a nsembe yachiyanjano.
Te vaengkah BOEIPA taengla a nawn, nawnnah boeih khui lamkah pakhat te tah rhoepnah thii aka haeh khosoih kah khocang la om saeh.
15 Nyama ya nsembe yachiyanjano yothokozera idyedwe pa tsiku lomwe nsembeyo yaperekedwa ndipo isatsaleko mpaka mmawa.
Rhoepnah dongkah uemonah hmueih saa te tah amah nawnnah hnin ah ca saeh lamtah mincang duela paih boel saeh.
16 “‘Koma ngati nsembe yakeyo apereka chifukwa cha lumbiro kapena mwaufulu, nsembeyo adye tsiku lomwe yaperekedwalo. Koma yotsala angathe kuyidya mmawa mwake.
Tedae olcaeng neh kothoh nawnnah hmueih tah a nawn khohnin vaengah hmueih te ca saeh lamtah a caknoi te a vuen ah ca saeh.
17 Ngati nyama ina ya nsembe yatsalabe mpaka tsiku lachitatu, imeneyo itenthedwe pa moto.
Hmueih saa khui lamkah a coih te a thum hnin ah hmai neh hoeh saeh.
18 Ngati munthu adya nyama yachiyanjano pa tsiku lachitatu, nsembeyo sidzalandiridwa. Amene wayipereka nsembeyo Mulungu sadzamulandira ndipo nsembeyo idzakhala yonyansa pamaso pa Mulungu, yosamupindulira kanthu woperekayo.
Amah kah rhoepnah hmueih saa te a thum hnin dongah a caak la a caak atah anih kah a nawn te doe pah mahpawh. Anih te a nawt a na pawt atah dikyik dikyak la om ni. Te te aka ca hinglu tah amah kathaesainah te amah loh phuei saeh.
19 “‘Nyama imene yakhudza chilichonse chodetsedwa, munthu asayidye, koma itenthedwe pa moto. Aliyense amene ali woyeretsedwa angathe kudya nyama inayo.
Rhalawt hno boeih dongah a ben maeh te ca boel saeh lamtah hmai neh hoeh saeh. Tedae aka caih maeh saa boeih tah ca saeh.
20 Koma ngati munthu wina amene ndi wosayeretsedwa adya nyama ya nsembe yachiyanjano imene ndi ya Yehova, ameneyo achotsedwe pakati pa anthu a mtundu wake.
Hinglu pakhat loh BOEIPA taengkah rhoepnah hmueih saa a caak vaengah amah te amah dongah a ti a hnai a om atah tekah hinglu te a pilnam khui lamloh hnawt saeh.
21 Ndipo ngati munthu wina akhudza chinthu chodetsedwa, kaya chonyansa cha munthu kapena cha nyama, kapenanso chonyansa china chilichonse, ndipo kenaka nʼkudya nyama ya nsembe yachiyanjano imene ndi ya Yehova, munthu ameneyo achotsedwe pakati anthu a mtundu wake.’”
Hinglu te rhalawt cungkuem dongah, hlang kah a tihnai dongah khaw, rhalawt rhamsa dongah khaw, konawhnah boeih dongah a rhalawt te a ben atah. BOEIPA taengkah rhoepnah hmueih saa te a caak atah tekah hinglu te pilnam lamloh hnawt saeh.
22 Yehova anayankhula ndi Mose kuti,
BOEIPA loh Moses te a voek tih,
23 “Awuze Aisraeli kuti, ‘Musadye mafuta a ngʼombe, nkhosa kapenanso mbuzi.
“Israel ca rhoek te voek lamtah thui pah. Vaito, tu, maae kah a tha boeih ca uh boeh.
24 Mafuta a nyama yofa yokha, kapena mafuta a nyama yophedwa ndi zirombo akhoza kuwagwiritsa ntchito iliyonse, koma inu musadye mafuta amenewo.
Te dongah maehrhok tha neh saha tha tah bibi khat khat dongah hnonah mai cakhaw ca rhoe ca uh boeh.
25 Pakuti munthu wakudya mafuta a nyama yoperekedwa kwa Yehova ngati nsembe yotentha pa moto, ayenera kuchotsedwa pakati pa anthu a mtundu wake.
Khat khat long ni BOEIPA taengkah hmaihlutnah ham a nawn rhamsa tha te a caak atah, aka ca hinglu te pilnam lamloh hnawt saeh.
26 Ndipo kulikonse kumene mukakhale musakadye magazi a mbalame iliyonse kapena magazi a nyama iliyonse.
Na tolrhum boeih ah vaa lamkah khaw, rhamsa lamkah khaw thii boeih te ca uh boeh.
27 Ngati munthu aliyense adya magazi achotsedwe pakati pa anthu a mtundu wake.’”
Hinglu khat khat loh thii khat khat ni a caak atah tekah hinglu te pilnam lamloh hnawt saeh,” a ti nah.
28 Yehova anayankhula ndi Mose kuti,
BOEIPA loh Moses te a voek tih,
29 “Awuze Aisraeli kuti, Aliyense amene apereka nsembe yachiyanjano kwa Yehova, abwere ndi gawo la nsembeyo kwa Yehova.
“Israel ca rhoek te voek lamtah thui pah. BOEIPA taengah rhoepnah hmueih aka khuen long tah rhoepnah hmueih khui lamkah a nawnnah te BOEIPA taengla pawk puei saeh.
30 Atenge ndi manja ake zigawo za chopereka zoyenera kuzitentha pa moto ngati chopereka kwa Yehova. Abweretse mafuta, pamodzi ndi chidale chomwe, ndipo chidalecho achiweyule kuti chikhale chopereka choweyula kwa Yehova.
BOEIPA taengkah hmaihlutnah ham te a kut loh a khuen vaengah a tha neh a rhang te khuen saeh. A rhang te BOEIPA mikhmuh ah thueng hmueih la thueng saeh.
31 Wansembe atenthe mafutawo pa guwa koma chidalecho chikhale cha Aaroni ndi ana ake.
Maehtha te khosoih loh hmueihtuk soah phum saeh. Tedae a rhang te Aaron ham neh anih koca rhoek hamla om saeh.
32 Mumupatse wansembe ntchafu ya kumanja ya nsembe yanu yachiyanjano kuti ikhale chopereka chanu kwa iye.
Te dongah nangmih kah rhoepnah hmueih khui lamkah bantang benkah a laeng te tah khosoih taengah khosaa la pae uh.
33 Mwana wa Aaroni amene amapereka magazi ndi mafuta a nsembe yachiyanjano, adzitenga ntchafu ya kumanja kukhala gawo lake.
Aaron koca rhoek khui lamkah rhoepnah thii neh maehtha aka nawn ham maehvae la bantang laeng te om saeh.
34 Choncho pa zopereka zachiyanjano za Aisraeli, Ine ndatengapo chidale chomwe amaweyula ndi ntchafu zimene amapereka nsembe ndipo ndazipereka kwa wansembe Aaroni ndi ana ake. Izi ndizo gawo lawo nthawi zonse pa zopereka za Aisraeli.”
Rhoepnah hmueih khuiah thueng hmueih kah a rhang neh a laeng he Israel ca rhoek taeng lamkah khosa la ka loh tih Israel ca rhoek taengkah kumhal maehvae la khosoih Aaron neh anih koca rhoek taengah ka paek coeng.
35 Zimenezi ndi chigawo cha Aaroni ndi ana ake chotapidwa pa zopereka kwa Yehova zoti zitenthedwe pa moto zimene zinaperekedwa pa tsiku limene anapatulidwa kuti akhale ansembe otumikira Yehova.
He tah BOEIPA taengah khosoih la a nuen hnin vaengah BOEIPA hmaihlutnah khui lamkah Aaron kah maeham neh anih koca rhoek kah maeham ni,” a ti nah.
36 Yehova ndiye analamulira kuti pa zopereka za Aisraeli azitapapo zimenezi ndi kuwapatsa ansembe ngati gawo lawo. Yehovayo analamula zimenezi pa tsiku limene ansembewo anapatulidwa ndipo anachikhazikitsa ngati lamulo la nthawi zonse.
Anih a koelh hnin van vaengah Israel ca rhoek loh khosoih rhoek taengah paek ham koi te tah cadilcahma due kumhal khosing la khueh ham BOEIPA loh a uen coeng.
37 Awa ndi malamulo a nsembe izi: nsembe yopsereza, nsembe yachakudya, nsembe yopepesera machimo, nsembe yopepesera kupalamula, nsembe ya mwambo wodzoza ndi nsembe yachiyanjano.
Hekah olkhueng dongkah hmueihhlutnah ham, khosaa ham khaw, boirhaem ham khaw, hmaithennah ham khaw, saboi ham khaw, rhoepnah hmueih ham khaw,
38 Malamulo amenewa Yehova anapereka kwa Mose pa Phiri la Sinai pa tsiku limene Yehova analamulira Aisraeli kuti abwere ndi zopereka za kwa Yehova, ku chipululu cha Sinai kuja.
BOEIPA loh Sinai tlang ah Moses a uen vanbangla amah a uen khohnin vaengah Israel ca rhoek amamih kah nawnnah te Sinai khosoek kah BOEIPA taengah a nawn uh.

< Levitiko 7 >