< Levitiko 5 >

1 “‘Ngati munthu anayitanidwa ku bwalo kuti akachitire umboni pa zimene anaziona kapena kuzimva koma iye nʼkukana kuchitira umboni, munthu ameneyo wachimwa ndipo ayenera kulangidwa.
Un ja kas laban apgrēkotos, dzirdēdams kādu sazvērestību, par ko viņš ir liecinieks, ja viņš to dzirdējis, vai zina, un to nedara zināmu, tad tam būs nest savu noziegumu.
2 “‘Munthu akakhudza chinthu chilichonse chodetsedwa, monga nyama yakufa ya mʼthengo, kapena chiweto chakufa kapenanso chokwawa chakufa, ngakhale iyeyo wachikhudza mosadziwa, wasanduka wodetsedwa ndipo wachimwa.
Vai ja kas laban aizskartu kādu nešķīstu lietu, vai tā ir nešķīstu zvēru maita, vai nešķīstu lopu maita, vai nešķīstu tārpu maita, un viņš to nav zinājis, - tomēr viņš ir nešķīsts un noziedzies.
3 “‘Munthu akakhudza choyipitsa munthu cha mtundu uliwonse, ndipo pochikhudzapo ndi kuyipitsidwa nacho mosadziwa, munthuyo adzakhala wopalamula akangodziwa chimene wachitacho.
Vai ja viņš kāda cilvēka nešķīstumu aizskartu, kaut kādu nešķīstumu, ar ko viņš apgānījies, un viņš to nav zinājis, un viņam top zināms, - tad viņš ir noziedzies.
4 “‘Munthu akalumbira mofulumira kapena mosasamala kuti adzachita chinthu, choyipa kapena chabwino, ngakhale kuti wachita izi mosadziwa kuti nʼkulakwa, pamene wazindira kulakwa kwake, iye adzakhalabe wopalamula akangodziwa chimene wachitacho.
Vai ja kas laban neapdomīgām lūpām zvērē, ļaunu vai labu darīt, ko vien cilvēks neapdomīgi var zvērēt, un ja to nav zinājis un to atzīst, tad viņš vai nu tā vai tā ir noziedzies.
5 “‘Pamene munthu wazindikira kuti wachimwa motere, awulule tchimo limene wachitalo.
Kad nu notiek ka viņš vai šā vai tā noziedzies, tad tam būs izteikt, ar ko tas apgrēkojies,
6 Pambuyo pake, munthuyo abwere kwa Yehova ndi mwana wankhosa wamkazi kapena mbuzi kuti ikhale chopereka chopepesera tchimo ndipo wansembe achite mwambo wopepesera tchimo lomwe wachitalo. Tsono wansembe achite mwambo wopepesera tchimo la munthuyo.
Un atnest par noziedzības upuri Tam Kungam par tiem grēkiem, ko viņš darījis, mātīti no sīkiem lopiem, aitiņu, vai kaziņu, par grēku upuri; tad priesterim viņu būs salīdzināt par to grēku.
7 “‘Ngati munthuyo alibe mwana wankhosa, abweretse njiwa ziwiri kapena nkhunda ziwiri kwa Yehova ngati chopereka chopepesera tchimo lake. Imodzi ikhale nsembe yopepesera tchimo, ndipo inayo ikhale nsembe yopsereza.
Bet ja viņam nav pie rokas, cik par avi vajag, tad par to noziegumu, ko viņš darījis, būs atnest Tam Kungam divas ūbeles vai divus jaunus baložus, vienu par grēku upuri un otru par dedzināmo upuri.
8 Tsono abwere nazo kwa wansembe, ndipo wansembeyo ayambe wapereka mbalame imodzi ngati yopepesera tchimo. Apotole khosi koma osayidula mutu,
Un tos būs nest pie priestera; tam papriekš to būs upurēt, kas ir dots par grēku upuri, un viņa galvu pie pakauša būs nokniebt, bet nenolauzt.
9 kenaka awaze magazi a chopereka chopepesera tchimocho mʼmbali mwa guwa. Magazi ena onse awathire pa tsinde la guwa. Imeneyi ndi nsembe yopepesera tchimo.
Un no tā grēku upura asinīm būs slacīt uz altāra sienu, bet kas atliek no tām asinīm, to būs iztecināt uz altāra grīdu; tas ir grēku upuris.
10 Pambuyo pake wansembe apereke mbalame inayo kuti ikhale chopereka chopsereza potsata mwambo wake. Wansembe atatha kupereka nsembe yopepesera tchimo limene munthu uja wachita, wochimwayo adzakhululukidwa.
Un to otru tam būs sataisīt par dedzināmo upuri, kā pienākas; tā priesterim to būs salīdzināt par viņa grēku, ko viņš darījis, - tad viņam taps piedots.
11 “‘Koma ngati munthuyo alibe njiwa ziwiri kapena nkhunda ziwiri, abweretse ufa wosalala wokwanira kilogalamu imodzi kuti ukhale chopereka chopepesera tchimo limene wachita. Asathiremo mafuta kapena lubani chifukwa ndi chopereka chopepesera tchimo.
Bet ja viņam tik daudz nav pie rokas, cik vajag par divām ūbelēm vai diviem jauniem baložiem, tad tam, kas grēkojis, par upuri būs atnest desmito daļu no vienas ēfas kviešu miltu par grēku upuri; tam nebūs eļļas uzliet, nedz vīraka uzlikt, jo tas ir grēku upuris.
12 Abweretse ufawo kwa wansembe ndipo wansembeyo atapeko dzanja limodzi kuti ukhale ufa wachikumbutso ndi kuwutentha pa guwa pamodzi ndi chopereka chopsereza kwa Yehova. Imeneyi ndi nsembe yopepesera tchimo.
To būs nest pie priestera, un priesterim no tā būs ņemt pilnu sauju par piemiņas tiesu, un to iededzināt uz altāra, par uguns upuri Tam Kungam; - tas ir grēku upuris.
13 Umu ndi mmene wansembe adzachitire mwambo wopepesera machimo ena aliwonse amene munthu wachita, ndipo munthuyo adzakhululukidwa. Zopereka zonse zotsala zidzakhala za wansembeyo monga momwe amachitira ndi chopereka chachakudya.’”
Un priesterim būs viņu salīdzināt par viņa grēku, ko viņš šā vai tā darījis, - tad viņam taps piedots; un tas pieder priesterim, tā kā ēdamais upuris.
14 Yehova anawuza Mose kuti,
Un Tas Kungs runāja uz Mozu un sacīja:
15 “Munthu akachita zinthu mosakhulupirika, nachimwa mosadziwa posapereka zinthu zopatulika zofunika kwa Yehova, munthuyo apereke kwa Yehova nsembe yopepesera machimo ake. Nsembeyo ikhale nkhosa yayimuna yopanda chilema ndipo mtengo wake ukhale wokwana masekeli oyenera a siliva pakawerengedwe ka ku Nyumba ya Mulungu. Imeneyi ndi nsembe yopepesera kupalamula.
Ja kas laban noziedzās un netīši apgrēkojās pie tā, kas Tam Kungam ir svētīts, tad tam par nozieguma upuri būs atnest Tam Kungam aunu, kas bez vainas, no ganāmā pulka, divu sudraba sēķeļu vērtībā pēc svētās vietas sēķeļa, par nozieguma upuri.
16 Munthuyo ayenera kubweza zinthu zopatulika zimene sanaperekezo. Awonjezepo chimodzi mwa zigawo zisanu zilizonse ndi kuzipereka zonsezo kwa wansembe amene adzachita mwambo wopepesera machimo a munthuyo, popereka nkhosa yayimuna ija ngati nsembe yopepesera ndipo wochimwayo adzakhululukidwa.
Un būs atdot, ko tas pret tām svētām lietām grēkojis, un piekto daļu būs pielikt pārāki un dot priesterim; tā priesterim viņu būs salīdzināt ar to nozieguma upura aunu, - tad viņam taps piedots.
17 “Ngati munthu wachimwa mosadziwa pochita chilichonse chimene Yehova salola, munthuyo ndi wopalamula ndithu, ndipo ayenera kulangidwa.
Un ja kas laban apgrēkotos, darīdams pret kaut kādu no Tā Kunga baušļiem, ko nebūs darīt, un to nav zinājis, tomēr viņš ir noziedzies un viņam būs nest savu noziegumu.
18 Abwere kwa wansembe ndi chopereka chopepesera kupalamula kwake. Chopereka chikhale nkhosa yayimuna yopanda chilema ndipo mtengo wake ukhale woyenera nsembe yopepesera kupalamula kumene anachimwa mosadziwako, ndipo munthuyo adzakhululukidwa.
Un tam būs nest no ganāmā pulka aunu, kas bez vainas, pie priestera par nozieguma upuri pēc tava sprieduma; un priesterim viņu būs salīdzināt par viņa netīšo apgrēkošanos, ko viņš darījis un pats nebija zinājis, - tad viņam taps piedots.
19 Imeneyi ndi nsembe yopepesera kupalamula popeza munthuyo wapezeka wolakwa pamaso pa Yehova.”
Tas ir nozieguma upuris, - viņš noziegdamies bija noziedzies pret To Kungu.

< Levitiko 5 >