< Levitiko 5 >
1 “‘Ngati munthu anayitanidwa ku bwalo kuti akachitire umboni pa zimene anaziona kapena kuzimva koma iye nʼkukana kuchitira umboni, munthu ameneyo wachimwa ndipo ayenera kulangidwa.
Hinglu pakhat te tholh tih thaephoeinah ol a yaak. Te vaengah amah te laipai la a om dongah a hmuh tih a ming. Tedae a puen pawt atah anih kathaesainah te phuei saeh.
2 “‘Munthu akakhudza chinthu chilichonse chodetsedwa, monga nyama yakufa ya mʼthengo, kapena chiweto chakufa kapenanso chokwawa chakufa, ngakhale iyeyo wachikhudza mosadziwa, wasanduka wodetsedwa ndipo wachimwa.
Hinglu pakhat loh rhalawt hno khaw, rhalawt mulhing rhok mai khaw cuem pawh rhamsa rhok mai khaw, rhalawt rhulcai rhok khat khat mai khaw buengrhuet a ben vaengah tah rhalawt la boe mai ni.
3 “‘Munthu akakhudza choyipitsa munthu cha mtundu uliwonse, ndipo pochikhudzapo ndi kuyipitsidwa nacho mosadziwa, munthuyo adzakhala wopalamula akangodziwa chimene wachitacho.
Hlang kah a tihnai dongkah khaw, a tihnai boeih dongah khaw a ben mai atah te nen te poeih uh coeng. Te te a phah akhaw a ming akhaw anih boe saeh.
4 “‘Munthu akalumbira mofulumira kapena mosasamala kuti adzachita chinthu, choyipa kapena chabwino, ngakhale kuti wachita izi mosadziwa kuti nʼkulakwa, pamene wazindira kulakwa kwake, iye adzakhalabe wopalamula akangodziwa chimene wachitacho.
Hinglu pakhat loh a cungkuem dongah thaehuet ham neh voelphoeng ham a hmuilai neh khungrhap la a toemngam mai ni. Hlang he olhlo neh a khungrhap coeng dongah te te a phah a khaw a ming akhaw te pakhat dongah anih boe saeh.
5 “‘Pamene munthu wazindikira kuti wachimwa motere, awulule tchimo limene wachitalo.
Tedae he rhoek khuikah khat nen khaw a boe mai akhaw te kah a tholh te. loh phoe saeh.
6 Pambuyo pake, munthuyo abwere kwa Yehova ndi mwana wankhosa wamkazi kapena mbuzi kuti ikhale chopereka chopepesera tchimo ndipo wansembe achite mwambo wopepesera tchimo lomwe wachitalo. Tsono wansembe achite mwambo wopepesera tchimo la munthuyo.
Te vaengah a tholhnah neh a tholh bangla BOEIPA taengah a hmaithennah khuen saeh. Boirhaem la boiva khuikah tu a la mai khaw, maae la ca mai khaw om saeh. Te daengah ni a tholhnah dongah khosoih loh anih ham a dawth pa eh.
7 “‘Ngati munthuyo alibe mwana wankhosa, abweretse njiwa ziwiri kapena nkhunda ziwiri kwa Yehova ngati chopereka chopepesera tchimo lake. Imodzi ikhale nsembe yopepesera tchimo, ndipo inayo ikhale nsembe yopsereza.
Tedae boiva kangna khaw a kut loh a na pawt atah a tholh bangla a hmaithennah te vahu phiknit mai khaw, vahui ca phiknit mai khaw, pakhat te boirhaem la, pakhat te hmueihhlutnah la BOEIPA taengah khuen saeh.
8 Tsono abwere nazo kwa wansembe, ndipo wansembeyo ayambe wapereka mbalame imodzi ngati yopepesera tchimo. Apotole khosi koma osayidula mutu,
Te phoeiah khosoih taengla khuen saeh lamtah boirhaem ham te nawn lamhma saeh. A lu te a rhawn lamloh paimaelh pah saeh lamtah boe boel saeh.
9 kenaka awaze magazi a chopereka chopepesera tchimocho mʼmbali mwa guwa. Magazi ena onse awathire pa tsinde la guwa. Imeneyi ndi nsembe yopepesera tchimo.
Te phoeiah boirhaem thii te hmueihtuk pangbueng dongah haeh saeh lamtah thii aka coih te boirhaem hmueihtuk kah khoengim taengah ci saeh.
10 Pambuyo pake wansembe apereke mbalame inayo kuti ikhale chopereka chopsereza potsata mwambo wake. Wansembe atatha kupereka nsembe yopepesera tchimo limene munthu uja wachita, wochimwayo adzakhululukidwa.
Tedae a pabae te tah laitloeknah vanbangla hmueihhlutnah saii saeh. Te vaengah, a tholhnah neh a tholh dongah khosoih. loh anih ham dawth pah saeh lamtah anih te khodawkngai saeh.
11 “‘Koma ngati munthuyo alibe njiwa ziwiri kapena nkhunda ziwiri, abweretse ufa wosalala wokwanira kilogalamu imodzi kuti ukhale chopereka chopepesera tchimo limene wachita. Asathiremo mafuta kapena lubani chifukwa ndi chopereka chopepesera tchimo.
Tedae vahu phiknit mai khaw, vahui ca phiknit mai khaw a kut loh a na pawt oeh atah, a tholh bangla a boirhaem ham nawnnah te vaidam cangnoek parha khuen saeh. Te tah boirhaem la a om dongah a soah situi bueih boel saeh lamtah hmueihtui khaw tloeng thil boel saeh.
12 Abweretse ufawo kwa wansembe ndipo wansembeyo atapeko dzanja limodzi kuti ukhale ufa wachikumbutso ndi kuwutentha pa guwa pamodzi ndi chopereka chopsereza kwa Yehova. Imeneyi ndi nsembe yopepesera tchimo.
Te vaengah khosoih taengla khuen saeh lamtah kamhoeinah te khosoih loh a kut dongah a bae mawk la paco saeh. Te phoeiah boirhaem te BOEIPA hmueihtuk kah hmaihlutnah soah phum saeh.
13 Umu ndi mmene wansembe adzachitire mwambo wopepesera machimo ena aliwonse amene munthu wachita, ndipo munthuyo adzakhululukidwa. Zopereka zonse zotsala zidzakhala za wansembeyo monga momwe amachitira ndi chopereka chachakudya.’”
Te daengah ni te khuikah pakhat nen khaw a tholh vanbangla a tholhnah dongah khosoih loh anih ham a dawth pah vetih anih te khodawk a ngai eh. Tedae khosaa bangla khosoih hamla om saeh.
14 Yehova anawuza Mose kuti,
BOEIPA. loh Moses a voek tih,
15 “Munthu akachita zinthu mosakhulupirika, nachimwa mosadziwa posapereka zinthu zopatulika zofunika kwa Yehova, munthuyo apereke kwa Yehova nsembe yopepesera machimo ake. Nsembeyo ikhale nkhosa yayimuna yopanda chilema ndipo mtengo wake ukhale wokwana masekeli oyenera a siliva pakawerengedwe ka ku Nyumba ya Mulungu. Imeneyi ndi nsembe yopepesera kupalamula.
“Hinglu pakhat loh tholh tih BOEIPA taengah boekoeknah la boe a koek mai ni. Te vaengah hnokhueh neh kut khoom kawng dongah a imben taengah a basa atah, huencannah neh a imben te a hnaemtaek atah,
16 Munthuyo ayenera kubweza zinthu zopatulika zimene sanaperekezo. Awonjezepo chimodzi mwa zigawo zisanu zilizonse ndi kuzipereka zonsezo kwa wansembe amene adzachita mwambo wopepesera machimo a munthuyo, popereka nkhosa yayimuna ija ngati nsembe yopepesera ndipo wochimwayo adzakhululukidwa.
Hmuencim dongah lai a hmuh te a sah phoeiah panga neh thap saeh lamtah khosoih taengla thak saeh. Te daengah ni khosoih loh anih kah hmaithennah ham te tutal neh a dawth pah vetih anih te khodawk a ngai eh.
17 “Ngati munthu wachimwa mosadziwa pochita chilichonse chimene Yehova salola, munthuyo ndi wopalamula ndithu, ndipo ayenera kulangidwa.
Hinglu pakhat loh BOEIPA olpaek khat khat khuikah saii pawt koi te pakhat khaw a saii tholh coeng dae a boe te khaw a ming pawt atah amah kathaesainah te phuei van saeh.
18 Abwere kwa wansembe ndi chopereka chopepesera kupalamula kwake. Chopereka chikhale nkhosa yayimuna yopanda chilema ndipo mtengo wake ukhale woyenera nsembe yopepesera kupalamula kumene anachimwa mosadziwako, ndipo munthuyo adzakhululukidwa.
Te vaengah a phu aka ting boiva khuikah tutal a cuemthuek te khosoih taengah hmaithennah la khuen saeh. Te daengah ni anih. loh ming pawt tih tohtamaeh la a taengphael te khosoih loh anih ham a dawth pah vetih anih te khodawk a ngai eh.
19 Imeneyi ndi nsembe yopepesera kupalamula popeza munthuyo wapezeka wolakwa pamaso pa Yehova.”
He tah a boe, a boe vaengah BOEIPA taengkah a saii hmaithennah ni,” a ti nah.