< Levitiko 4 >

1 Yehova anayankhula ndi Mose kuti,
Hina Gode da Mousesema e da Isala: ili dunuma amane alofele sia: ma: ne sia: i,
2 “Awuze Aisraeli kuti, ‘Munthu akachimwa mosadziwa ndi kuchita chilichonse chimene Yehova walamula kuti asachite, azichita izi:
“Nowa da Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i hame dawa: beba: le giadofai galea, e da amane hamoma: mu,
3 “‘Ngati wansembe wodzozedwa achimwa, ndi kuchimwitsa anthu onse, iyeyu ayenera kupereka mwana wangʼombe wamphongo wopanda chilema chifukwa cha tchimo limene wachitalo. Imeneyi ndi nsembe ya Yehova yopepesera tchimo lake.
Gobele salasu Ouligisu dunu da giadofabeba: le, fofada: su da Isala: ili dunu huluane ilima doaga: sea, e da bulamagau mano gawali (noga: idafa, ledo hamedei) ea giadofabeba: le dabe ima: ne, Hina Godema gobele salimu.
4 Wansembeyo abwere nayo ngʼombeyo pa khomo la tenti ya msonkhano pamaso pa Yehova. Asanjike dzanja lake pamutu pa ngʼombeyo ndipo ayiphe pamaso pa Yehova.
E da bulamagau gawali amo Abula Diasu holeiga oule asili, ea dialuma da: iya ea lobo ligisili, Hina Gode ba: ma: ne amo bulamagau medole legemu.
5 Kenaka wansembe wodzozedwa atengeko magazi a ngʼombeyo ndi kulowa nawo mu tenti ya msonkhano.
Amasea, gobele salasu hina dunu da bulamagau ea maga: me mogili lale, Abula Diasua golili gaguli masunu.
6 Iye aviyike chala chake mʼmagazi, ndipo awawaze kasanu ndi kawiri pamaso pa Yehova, patsogolo pa katani yotchinga malo wopatulika.
E da ea lobo sogo maga: mega gele, amo maga: me hadigi Abula (amo da Abula Diasu afafaia) ea midadi fesuale agoane foga: gagala: mu.
7 Kenaka wansembe apake magaziwo pa nyanga za guwa lofukizira lubani limene lili pamaso pa Yehova mu tenti ya msonkhano. Magazi ena otsalawo awathire pa tsinde pa guwa lansembe zopsereza, limene lili pa khomo la tenti ya msonkhano.
Amasea, e da maga: me eno amo hono da gabusiga: manoma oloda ea hegomaiga gala amoga foga: gagala: mu. E da maga: me eno diala amo oloda (Abula Diasu holeiga diala amola amoga ilia da gobele salasu liligi gobesisa) amo ea baiga sogadigimu.
8 Pambuyo pake achotse mafuta onse a ngʼombe yayimuna yopepesera machimoyo: mafuta okuta zamʼkati kapena mafuta onse amʼkatimo.
9 Achotsenso ndi kubwera ndi impsyo zonse ziwiri pamodzi ndi mafuta onse ndiponso mafuta onse amene aphimba chiwindi ndi impsyo
E da amo bulamagau ea sefe, sefe da iga dedebosa (oso sefe), fogome ganumui amola ilia sefe amola habe ea la: idi noga: iwane, amo lale,
10 monga momwe amachotsera mafuta a ngʼombe yoperekedwa kuti ikhale chopereka chachiyanjano. Tsono wansembe atenthe zimenezi pa guwa lansembe zopsereza.
oloda (amoga ilia da gobele salasu liligi gobesisa) amo da: iya gobesimu. E da Hahawane Gilisili Olofole Iasu ohe ea sefe gobesisu amo defele gobesimu.
11 Koma chikopa cha ngʼombe yayimunayo ndi mnofu wake wonse, pamodzi ndi mutu ndi miyendo, zamʼkati ndi matumbo,
Be amo bulamagau ea gadofo, ea hu huluane, ea emo amola ea iga huluane,
12 kapena kuti ngʼombe yonse yotsalayo apite nayo kunja kwa msasa ku malo woyeretsedwa, kumene amatayako phulusa ndi kuyitentha pa nkhuni, pa phulusapo.
e da abula diasu gilisisu amoga gadili gaguli asili, ledo hamedei sogebi (amoga ilia da nasubu duduli fasisu) amogai nema: ne gobesimu.
13 “‘Ngati gulu lonse la Aisraeli lichimwa mosadziwa, nachita chomwe ndi choletsedwa ndi Yehova, ngakhale kuti gulu lonselo silikudziwa kuti lachimwa, anthuwo ndi olakwa ndithu.
Be Isala: ili fi dunu huluane da hame dawa: beba: le Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i afae giadofasea,
14 Akazindikira tchimo limene achita, gulu lonse lipereke mwana wangʼombe wamphongo kuti akhale chopereka chopepesera tchimo ndipo abwere naye pa khomo la tenti ya msonkhano.
ilia wadela: i hou hamoi ilia dawa: sea, ilia huluane da bulamagau mano gawali ilia Wadela: i Hou Gogolema: ne Olofoma: ne Iasu ima: ne, Hina Gode Ea Abula Diasu amoga oule masunu.
15 Akuluakulu a anthuwo asanjike manja awo pa mutu pa ngʼombe pamaso pa Yehova, ndipo ayiphe pomwepo pamaso pa Yehova.
Isala: ili fi ilia ouligisu dunu da bulamagau ea dialuma da: iya ilia lobo ligisili, amogawi medole legemu.
16 Tsono wansembe wodzozedwa atengeko magazi a ngʼombeyo ndi kulowa nawo mu tenti ya msonkhano.
Gobele Salasu hina dunu da bulamagau ea maga: me mogili lale, Abula Diasu ganodini gaguli misunu.
17 Aviyike chala chake mʼmagaziwo ndi kuwawaza pamaso pa Yehova kasanu ndi kawiri patsogolo pa nsalu yotchinga.
E da ea lobo sogo maga: me ganodini gele, hadigi Abula ea midadi fesuale agoane foga: gagala: mu.
18 Pambuyo pake iye apake magaziwo pa nyanga za guwa limene lili pamaso pa Yehova mu tenti ya msonkhano. Magazi ena otsalawo awathire pa tsinde pa guwa lansembe zopsereza limene lili pa khomo la tenti ya msonkhano.
Amasea, e da maga: me eno amo hono da gabusiga: manoma oloda ea hegomaiga gala, amoga foga: gagala: mu. E da maga: me eno diala amo oloda (Abula Diasu holeiga diala amola amoga ilia da gobele salasu liligi gobesisa) amo ea baiga sogadigimu.
19 Kenaka achotse mafuta onse a ngʼombeyo ndi kuwatentha pa guwa,
Amasea, e da sefe huluane lale, oloda da: iya gobesimu.
20 ndipo achite ndi ngʼombe yayimunayi monga anachitira ndi ngʼombe yayimuna yopepesera machimo. Potero, wansembe adzapereka nsembe yopepesera anthu, ndipo machimo awo adzakhululukidwa.
E da Wadela: i Hou Gogolema: ne Olofoma: ne Iasu ima: ne gobele salasu defele, amo bulamagau gobele salimu. Amasea, Isala: ili fi dunu ilia wadela: i hou da gogolema: ne olofoi dagoi ba: mu.
21 Kenaka atulutse ngʼombeyo kunja kwa msasa ndi kuyitentha monga anatenthera ngʼombe yoyamba ija. Imeneyi ndiyo nsembe yopepesera machimo a gulu lonse.
Amasea, e da hi Wadela: i Hou Gogolema: ne Olofoma: ne Iasu ima: ne, bulamagau amo abula diasu gilisisu gadili gaguli asili gobesisa, amo defele e amo bulamagau gobesimu. Amo gobele salasu da Isala: ili fi dunu huluane ilia wadela: i hou dodofema: ne hamosa.
22 “‘Ngati mtsogoleri achimwa mosadziwa nachita zimene ndi zoletsedwa ndi Yehova Mulungu wake, ndiye kuti wapalamula.
Be fi ouligisu dunu da hame hanaiba: le amola hame dawa: beba: le, Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i afae giadofasea,
23 Ndipo ngati wauzidwa za tchimo limene wachita, iye abwere ndi mbuzi yayimuna yopanda chilema kuti ikhale chopereka chake.
dunu eno da e da giadofai ema olelesea, e da goudi gawali ida: iwane ledo hamedei, gaguli misa: ne sia: ma.
24 Asanjike dzanja lake pa mutu wa mbuziyo ndi kuyiphera pamalo pamene amaphera zopereka zopsereza pamaso pa Yehova. Ichi ndi chopereka chopepesera tchimo.
E da amo goudi ea dialuma da: iya ea lobo ligisili, oloda ea gagoe (north) la: idi, (amoga ohe gobele salasu hamoma: ne ilia medole legebe) amoga medole legemu. Amo gobele salasu iasu da ouligisu dunu ea wadela: i hou fadegale fasima: ne hamosa.
25 Pambuyo pake wansembe atengeko magazi a chopereka chopepesera tchimocho ndi chala chake, ndipo awapake pa nyanga za guwa lansembe zopsereza. Athire magazi otsalawo pa tsinde la guwalo.
Gobele salasu dunu da ea lobo sogo maga: me ganodini gele, hono amo oloda hegomaiga gala amoga legelu amola maga: me eno diala amo oloda ea baiga sogadigimu.
26 Wansembeyo atenthe mafuta onse pa guwapo monga amatenthera chopereka chachiyanjano. Pochita zimenezi, wansembe adzapereka nsembe yopepesera tchimo la munthuyo, ndipo adzakhululukidwa.
Amasea, e da Hahawane Gilisili Olofole Iasu ohe ilia sefe gobesibi defele, amo goudi ea sefe huluane oloda da: iya gobesimu. Gobele salasu dunu da amomane fi ouligisu dunu ea Wadela: i Hou Gogolema: ne Olofoma: ne Iasu ima: ne, gobele salasu hamomu. Amasea, ea wadela: i hou da gogolema: ne olofoi dagoi ba: mu.
27 “‘Ngati munthu wamba achimwa mosadziwa nachita zimene ndi zoletsedwa ndi Yehova, ndiye kuti wapalamula.
Be dunudafa da mae dawa: le, Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i afae giadofale, wadela: i hou hamosea,
28 Ndipo ngati wauzidwa za tchimo limene wachita, abweretse mbuzi yayikazi yopanda chilema kuti ikhale chopereka chopepesera tchimo.
dunu eno da ea giadofai amo ema olelesea, e da goudi aseme noga: idafa, ledo hamedei, amo Godema ima: ne gaguli misa: ne sia: ma.
29 Asanjike dzanja lake pamutu pa mbuziyo ndipo ayiphe pamalo pamene amaphera chopereka chopsereza.
E da amo goudi ea dialuma da: iya ea lobo ligisili, oloda ea gagoe (north) la: ididili (amoga ilia da gobele salasu ohe medole legesu) amoga medole legemu.
30 Ndipo wansembe atenge magazi ndi chala chake ndi kuwapaka pa nyanga za guwa lansembe zopsereza ndi kuthira magazi wotsalawo pa tsinde la guwalo.
Gobele salasu dunu da ea lobo sogo amo goudi ea maga: me ganodini gele, hono amo oloda ea hegomaiga dialebe amo foga: gagala: mu. Amola maga: me eno diala amo oloda ea baiga sogadigimu.
31 Kenaka iye achotse mafuta onse monga momwe anachotsera mafuta a chopereka chachiyanjano, ndipo awatenthe pa guwa kuti akhale fungo lokomera Yehova. Potero, wansembe adzapereka nsembe yopepesera tchimo la munthuyo ndipo adzakhululukidwa.
Amasea, e da goudi aseme ea sefe huluane bosolimu (ilia da ohe Hahawane Gilisili Olofole Iasu hamoma: ne medole legei sefe fadegasu defele). Amasea, e da amo sefe oloda da: iya gobesimu. Hina Gode da amo gobele salasu gabusiga: hahawane naba. Gobele salasu dunu da agoane hamosea, e da amo dunu ea wadela: i hou hamoi dabe iaha. Amola amo dunu da gogolema: ne olofosu ba: mu.
32 “‘Ngati munthu apereka mwana wankhosa ngati chopereka chopepesera tchimo lake, abwere ndi mwana wankhosa wamkazi wopanda chilema.
Dunu da Wadela: i Hou Gogolema: ne Olofoma: ne Iasu imunusa: , sibi gaguli masea, e da sibi aseme ida: iwane ledo hamedei gaguli misunu da defea.
33 Asanjike dzanja lake pa mutu wa mwana wankhosayo ndipo amuphe pamalo pamene amaphera chopereka chopsereza.
E da amo sibi ea dialuma da: iya ea lobo ligisili, oloda ea gagoe (north) la: ididili (amoga ilia da gobele salasu ohe medole lelegesu) amoga medole legemu.
34 Kenaka wansembe atengeko ndi chala chake magazi a mwana wankhosa uja ndi kuwapaka pa nyanga za guwa lansembe zopsereza. Magazi otsalawo athire pa tsinde la guwalo.
Gobele salasu dunu da ea lobo sogo amo sibi ea maga: me ganodini gele, hono amo oloda ea hegomaiga diala amoga legemu. Amola maga: me eno diala amo oloda ea baiga sogadigimu.
35 Iye achotse mafuta onse, monga amachotsera mafuta a mwana wankhosa wa chopereka chachiyanjano, ndipo wansembe awatenthe pa guwa pamodzi ndi zopereka zina zopsereza za Yehova. Potero, wansembe adzapereka nsembe yopepesera tchimo limene munthuyo anachita ndipo adzakhululukidwa.
Amasea, e da sibi aseme ea sefe huluane duga: le (ilia da sibi Hahawane Gilisili Olofole Iasu hamoma: ne medole legei ea sefe duga: su defele), amo sefe amola ha: i manu iasu Hina Godema i, amo gilisili gobesimu. Agoane hamobeba: le, gobele salasu dunu da amo dunu ea wadela: i hou hamoi ea dabe iaha. Amasea, amo dunu ea wadela: i hou da gogolema: ne olofoi dagoi ba: mu.

< Levitiko 4 >