< Levitiko 22 >

1 Yehova anawuza Mose kuti,
BOEIPA loh Moses te a voek tih,
2 “Uza Aaroni ndi ana ake kuti azilemekeza zinthu zopatulika zimene Aisraeli azipereka kwa Ine, kuti asayipitse dzina langa loyera. Ine ndine Yehova.
“Aaron neh anih koca rhoek taengah thui pah. Israel ca kah buhcim te hai pa uh saeh. Te daengah ni kai ham a ciim uh vanbangla ka ming cim he a poeih uh pawt eh. Kai tah BOEIPA ni.
3 “Uwawuze kuti ngati wina aliyense mwa zidzukulu zawo mʼmibado yonse imene ikubwera adzayandikira zinthu zopatulika zimene ana a Israeli apereka kwa Yehova, ali wodetsedwa, ameneyo achotsedwe pamaso pa Yehova. Ine ndine Yehova.
Na cadilcahma ham khaw thui pah. Israel ca rhoek tah BOEIPA ham a ciim uh coeng dongah buhcim te na tii na ngan khat khat khui lamkah hlang khat khat long ni a pum dongkah a ti a hnai neh a nawn atah tekah hlanghing te ka mikhmuh lamkah khoe uh saeh. Kai tah BOEIPA ni.
4 “Munthu aliyense mwa zidzukulu za Aaroni amene ali ndi khate kapena amatulutsa zoyipa mʼthupi mwake, asadye zinthu zopatulika mpaka atayeretsedwa. Wansembe angakhale wodetsedwa atakhudzana ndi chinthu chimene chadetsedwa ndi chinthu chakufa kapena kukhudza munthu amene wataya umuna,
Aaron tiingan khuikah hlang khat khat te pahuk tih a hnai atah a caihcil hlanhil buhcim te ca boel saeh. Te phoeiah rhalawt hinglu khat khat aka ben neh yangtui aka coe hlang khaw,
5 kapena kukhudza chilichonse chokwawa chomwe chimadetsa munthu, kapena kukhudza munthu amene angamudetse, kapenanso kukhudza kanthu kena kalikonse kodetsedwa.
Rhulcai khat khat te a ben tih amah aka poeih uh hlang te khaw, A ti a hnai khat khat dongah amah aka poeih uh hlang te khaw,
6 Tsono ngati wansembe angakhudze chilichonse mwa zimenezi ndiye kuti adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo. Asadye chopereka chilichonse chopatulika mpaka atasamba thupi lake lonse.
te te aka ben hinglu te khaw kholaeh duela poeih uh. Te dongah a pum te tui neh a silh pawt atah buhcim te ca boel saeh.
7 Munthuyo adzakhala woyeretsedwa pamene dzuwa lalowa, ndipo angathe kudya chopereka chopatulikacho popeza ndi chakudya chake.
Tedae khomik a tlak phoeiah atah koep caihcil bitni. Te vaengah buhcim dongkah amah buh te koep ca saeh.
8 Wansembe sayenera kudya chinthu chofa chokha kapena chojiwa ndi chirombo kuopa kuti angadzidetse ndi chakudyacho. Ine ndine Yehova.
Maehrhok neh saha sa a caak nen te poeih uh boel saeh. Kai tah BOEIPA ni.
9 “‘Choncho ansembe azisunga malamulo angawa kuti asapezeke wolakwa ndi kufa chifukwa chopeputsa malamulowa. Ine ndine Yehova, amene ndimawayeretsa.
Ka kueknah te a ngaithuen uh daengah ni tholh loh a poeih tih aka duek ham long khaw amah tholh te a phueih pawt eh. Kai tah amih aka ciim BOEIPA ni.
10 “‘Aliyense amene si wabanja la wansembe, kaya ndi mlendo wa wansembe, kapena wantchito wake, asadye chopereka chopatulika.
Kholong hlang khat khat long khaw buhcim te ca boel saeh. Khosoih kah impah neh kutloh long khaw buhcim te ca boel saeh.
11 Koma kapolo amene wagulidwa ndi ndalama kapena kubadwira mʼbanja la wansembe angathe kudya chakudya cha wansembeyo.
Tedae khosoih loh a tangka, hnopai neh a lai hlanghing long tah ca mai saeh. Amah im kah cahlah long khaw anih kah buh te ca saeh.
12 Mwana wamkazi wa wansembe amene wakwatiwa ndi munthu amene si wansembe, asadyeko nsembe zopatulikazo.
Khosoih canu khaw kholong hlang taengla a om coeng atah khocang neh buhcim te ca boel saeh.
13 Koma mwana wamkazi wa wansembe amene ali wamasiye kapena wosudzulidwa, ndipo alibe mwana, komanso anabwerera ku nyumba ya abambo ake monga pa nthawi ya utsikana wake, angathe kudya chakudya cha abambo ake. Mlendo asadye chakudya chopatulika.
Tedae khosoih canu nuhmai la om mai tih tiingan om mueh la a hlak uh atah a napa im la mael saeh lamtah a napa kah buh te a camoe vaengkah bangla ca saeh. Tedae kholong boeih long tah ca boel saeh.
14 “‘Ngati munthu wina aliyense adya chopereka chopatulika mosadziwa, munthuyo amubwezere wansembe chinthu chopatulikacho ndipo awonjezerepo limodzi la magawo asanu a chinthucho.
Hlang loh buhcim te tohtamaeh la a caak atah panga neh thap pah saeh lamtah buhcim te khosoih taengah pae saeh.
15 Choncho ansembe asayipitse zopereka zopatulika za Aisraeli zimene apereka kwa Yehova
Te dongah BOEIPA taengah Israel ca rhoek kah a tloeng buhcim te poeih uh boel saeh.
16 ndipo asachimwitse ndi kupalamulitsa Aisraeli powalola kudya zakudya zawo zopatulika. Ine ndine Yehova amene ndimawayeretsa.’”
Amih te BOEIPA kamah loh ka ciim coeng dongah amih kah buhcim aka ca tah amamih kathaesainah lai te amamih loh phuei saeh,” a ti nah.
17 Yehova anawuza Mose kuti,
Te phoeiah BOEIPA loh Moses te a voek tih,
18 “Yankhula ndi Aaroni, ana ake pamodzi ndi Aisraeli onse, ndipo uwawuze kuti, ‘Ngati wina aliyense wa inu, Mwisraeli kapena mlendo amene akukhala mu Israeli abwera ndi mphatso ya nsembe yopsereza kwa Yehova, kupereka chimene analumbira kapena kuti ikhale nsembe yaufulu,
“Aaron neh anih koca rhoek khaw Israel ca rhoek boeih te khaw voek lamtah thui pah. Israel imkhui kah hlang boeih khaw, Israel taengkah yinlai long khaw, a olcaeng cungkuem dongah amah kah nawnnah a nawn ham khaw, a kothoh cungkuem ham akhaw,
19 ndiye kuti abwere ndi ngʼombe yayimuna, nkhosa yayimuna kapena mbuzi yayimuna. Izi zikhale zopanda chilema kuti zilandiridwe.
nangmih taengah kolonah ham saelhung khuikah khaw, tu khuikah khaw mae khuikah khaw, a tal a cuemthuek te tah hmueihhlutnah ham BOEIPA taengah nawn uh saeh.
20 Musapereke nyama iliyonse yokhala ndi chilema chifukwa sidzalandiridwa mʼmalo mwanu.
A pum dongah khat khat te a lolh a maih atah khuen boeh. Nang ham kolonah khaw om hae mahpawh.
21 Pamene wina aliyense abweretsa ngʼombe kapena nkhosa kuti ikhale nsembe yachiyanjano kwa Yehova, kukwaniritsa zimene analumbira kapena kuti ikhale nsembe yaufulu, nyamayo iyenera kukhala yangwiro ndi yopanda chilema kuti ilandiridwe.
Hlang loh olcaeng soep sak ham BOEIPA taengah rhoepnah hmueih a nawn atah kothoh bangla kolonah ham saelhung khaw boiva khaw a cuemthuek la om saeh. A pum dongah a lolh a maih khat khat khaw om boel saeh.
22 Musapereke kwa Yehova nyama zakhungu, zovulala kapena zolumala, kapena nyama zimene zikutulutsa mafinya mʼthupi mwake, kapena zimene zili ndi nthenda yonyerenyetsa, kapena zimene zili ndi mphere. Nyama zotere musaziyike pa guwa kuti zikhale nsembe yopsereza kwa Yehova.
Mikdael khaw, aka paep khaw, vitvawt khaw, aka hnai khaw, phaikawk khaw, vinhna khaw BOEIPA taengah nawn boel saeh. BOEIPA taengkah hmueihtuk dongah hmaihlutnah ham khaw te khuikah te tloeng boeh.
23 Koma mungathe kupereka ngʼombe yayimuna kapena nkhosa imene ili ndi chiwalo chachitali kapena chachifupi kukhala nsembe yaufulu. Koma simungayipereke ngati nsembe yoperekera zimene munalumbirira chifukwa sidzalandiridwa.
Tedae kothoh ham tah vaito mai khaw tu mai khaw sahoei neh vitvawt lamkhaw na nawn suidae olcaeng ham tah doe mahpawh.
24 Nyama iliyonse imene mavalo ake ndi onyuka kapena ophwanyika, ongʼambika kapena oduka, musamayipereke kwa Yehova mʼdziko lanu.
Te dongah a neet tangtae, a phop tangtae, vitvawt, aka moeng tangtae te BOEIPA taengah nawn uh boeh. Na khohmuen ah khaw saii uh boeh.
25 Ndipo musalandire nyama zotere kuchokera kwa mlendo ndi kuzipereka kukhala zakudya za Mulungu wanu. Zimenezi sizidzalandiridwa mʼmalo mwanu chifukwa zili ndi chilema ndipo ndi zolumala.’”
Kholong ca kut lamkah te khaw na Pathen kah buh la nawn boeh. Amih sokah a lolh a maih khat khat loh amih rhoek te a poeih thai dongah nangmih ham a kolo mahpawh,” a ti nah.
26 Yehova anawuza Mose kuti,
Te phoeiah BOEIPA loh Moses te a voek tih,
27 “Pamene mwana wangʼombe, mwana wankhosa kapena mwana wambuzi wabadwa, akhale ndi make kwa masiku asanu ndi awiri. Kuyambira tsiku lachisanu ndi chitatu mpaka mʼtsogolo mwake, angathe kulandiridwa kuti akhale nsembe yopsereza ya kwa Yehova.
“Vaito khaw, tu khaw, maae khaw, a thang atah a manu taengah hnin rhih om dae saeh. Tedae a hnin rhet lamkah tah BOEIPA taengah nawnnah hmaihlutnah la thuem pawn ni.
28 Musaphe ngʼombe kapena nkhosa pamodzi ndi mwana wake tsiku limodzi. Muyidye pa tsiku lomwelo; musasiyeko ina mpaka mmawa. Ine ndine Yehova.
Tedae vaito khaw, tu khaw, a ca neh khohnin pakhat dongah hmaih ngawn boeh.
29 “Pamene mupereka nsembe yoyamika kwa Yehova, muyipereke mwakufuna kwanu mu njira yoti ilandiridwe mʼmalo mwanu.
BOEIPA taengah uemonah hmueih na nawn uh vaengah namamih taengah kolonah la nawn uh.
30 Muyidye pa tsiku lomwelo, wosasiyako ina mpaka mmawa. Ine ndine Yehova.
Khohnin pakhat dongah hlawp ca uh lamtah mincang duela paih uh boeh. Kai tah BOEIPA ni.
31 “Choncho sungani malamulo anga ndi kuwatsatira. Ine ndine Yehova.
Te dongah ka olpaek tuem uh lamtah vai uh. Kai tah BOEIPA ni.
32 Musanyoze dzina langa loyera. Koma lilemekezedwe pakati pa Aisraeli. Ine ndine Yehova amene ndimakuyeretsani
Israel ca rhoek taeng ah ka ciim vanbangla ka ming cim te poeih uh boeh. Kai tah nangmih aka ciim BOEIPA ni.
33 ndipo ndine amene ndinakutulutsani mu Igupto kuti ndikhale Mulungu wanu. Ine ndine Yehova.”
Nangmih kah Pathen la om ham ni nangmih te Egypt kho lamkah kan doek. Kai tah BOEIPA ni,” a ti nah.

< Levitiko 22 >