< Levitiko 2 >

1 “‘Munthu wina aliyense akabwera ndi nsembe ya chakudya kwa Yehova, chopereka chake chizikhala ufa wosalala. Ufawo ausakanize ndi mafuta ndi lubani,
Mago'mo'ma Ra Anumzamofonte'ma witi ofa'ma hunaku'ma erino esuno'a kaneno eri osi huteno, erino eno. Anampina masavena taginenteno frenkinsensi nehaza mnanentake'zana erinteno,
2 ndipo apite nawo kwa ansembe, ana a Aaroni. Atapeko modzazitsa dzanja ufa wosalala uja kuti ukhale wachikumbutso pamodzi ndi mafuta ndi lubani ndipo atenthe zonsezi pa guwa lansembe kuti zilandiridwe ndi Yehova mʼmalo mwa chopereka chonse. Iyi ndi nsembe yotentha pa moto ndiponso fungo lokomera Yehova.
erino Aroni mofavreramima pristi eri'zama e'neriza vahete vino. Ana masavene frenkinsensinema eri haviama hu'nea witifintira mago aza huno, kresramana vu itare ome kresigeno Ra Anumzamo'a mana'a nentahino musena hugahie.
3 Zotsala za nsembe ya chakudyazo ndi za Aaroni pamodzi ndi ana ake. Chimenechi ndi chigawo chopatulika kwambiri chifukwa chatapidwa pa chopereka chotentha pa moto cha Yehova.
Hagi mago'ama mesia witia Aronine mofavre'amokizmi su'a megahie. Anama Ra Anumzamofonte'ma kre sramana vunente'za atresazama'amo'a ruotagetfaza hu'ne.
4 “‘Ukabweretsa nsembe ya chakudya chophika mu uvuni, ikhale ya buledi wa ufa wosalala wopanda yisiti koma wosakaniza ndi mafuta, kapena timitanda ta buledi topyapyala, topanda yisiti koma topaka mafuta.
Avenifima kre'nesaza bretima ofama hunaku'ma erita esazana, zisti onte breti masaventeti eri havia huno kre'ne'nia kekio, hagege bisketire masave fre'ne'nia erita eho.
5 Ngati nsembe yako yachakudya ndi yophika pa chitsulo chamoto, ikhale ya buledi wa ufa wosalala wopanda yisiti koma wosakaniza ndi mafuta.
Kuta fraimpenifima kre'ne'nia witireti'ma ofama hunaku'ma hanutma, kaneosi'ma hu'nesia flaua'ene olivi masavenena erihavia nehuta, anampina zistia onteho.
6 Umuduledule bulediyo ndi kumupaka mafuta; imeneyo ndi nsembe yachakudya.
Hagi ana bretia goli osi osi huteta, anampina masave taginteho. E'i witi ofa hugahaze.
7 Ngati nsembe yako yachakudya ndi yophikidwa pa chiwaya, ikhale ya buledi wa ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta.
Kresramana vu witi ofama kre hagage hu kavofima kresazana, kaneosi osi'ma hu'nesia flauateti masavene eri havia huteta kregahaze.
8 Munthu azibwera ndi nsembe za chakudya zimene wapanga ndi zinthu zimenezi. Atachipereka kwa wansembe, iyeyu adzipita nacho ku guwa.
Hagi ama ana zantetima witi ofama kreta erita Ra Anumzamofonte'ma esuta, pristi vahe ome aminkeno, erino kresramna vu itarera vino.
9 Wansembeyo atengeko gawo lina la nsembeyo kukhala ufa wachikumbutso kuti ilandiridwe ndi Yehova mʼmalo mwa nsembe yonse ndipo ayitenthe pa moto monga nsembe yopsereza ya fungo lokomera Yehova.
Ana bretifintira pristi vahe'mo'za huvame hu'za mago zamaza hu'za eri'za kre manavu itare tevefi kresageno, Ra Anumzamo'a mana'a nentahino musena hugahie.
10 Zotsala za nsembe ya chakudyayo zikhale za Aaroni ndi ana ake. Chimenechi ndi chigawo chopatulika kwambiri chifukwa chatapidwa pa chopereka chotentha pa moto cha Yehova.
Hagi anama Ra Anumzamofonte'ma tevefima kresramana vunente'za atresaza bretimo'a, ruotgetfa hu'neankino Aronine mofavre'amokizmi su'a megahie.
11 “‘Nsembe ya chakudya chilichonse imene ubweretsa kwa Yehova ikhale yopanda yisiti, pakuti suyenera kupereka kwa Yehova nsembe yotentha pa moto imene ili ndi yisiti kapena uchi.
Kresramana vu witima ofama erita vanazana, zistia onteho, na'ankure zistima antege tumerima antege'ma hu'nesia witiretira tevefina kreta Ra Anumzamofona ofa huontegahaze.
12 Ziwirizi ungathe kubwera nazo kwa Yehova ngati chopereka cha zokolola zoyambirira. Koma usazitenthe pa guwa kuti zikhale fungo lokomera Yehova.
Hozafinti'ma e'sema ne'zama nenama hania ofama hanutma, zistine tumerinena amne tamagra erita Ra Anumzamofonte egahazanagi, e'i ana ofa kremnavu itarera Ra Anumzamo muse hanie huta onkregahaze.
13 Zopereka zako zonse zachakudya uzithire mchere. Usayiwale kuthira mchere pa chopereka chako popeza mcherewo ukusonyeza pangano pakati pa iwe ndi Mulungu wako. Tsono uzinthira mchere pa chopereka chako chilichonse.
Miko ofama hanaza witifina hagea antenageno, e'i ana zamo'a Anumzamo'enema huhagerafi huvempa ke'ma hu'naza kemofo huramagesa nehanigetma, tamagera okanigahazanki maka ofama hanaza witifina hagea atintegahaze.
14 “‘Mukamapereka kwa Yehova chopereka cha chakudya choyamba kucha, choperekacho chikhale cha chipatso chatsopano chokazinga pa moto ndi chopunthapuntha.
Ana nehuta ese'ma nena hania witi raga Ra Anumzamofonte'ma ofa huku'ma erita esutma, refuzafupeta eritma ege' tevefi kre hagage hutma erita egahaze.
15 Uchithire mafuta ndi lubani pakuti ndi chopereka cha chakudya.
Ana ne'zampina olivi masavene, mnanentake'za insensi antegahazankino, e'i witi ofa hugahaze.
16 Tsono wansembe atenthe gawo la chopereka chopunthapuntha chija kuti chikhala ufa wachikumbutso ndi cha mafuta pamodzi ndi lubani yense kuti Yehova alandire mʼmalo mwa zopereka zonse. Ichi ndi chopereka chotentha pa moto cha Yehova.
Ana Witima kne'za masavene mnanentake'za insensinema eri haviama hunte'nazafinti osi'a eri'za, Pristi vahe'mo'za knare manavu ofa Anumzamofontega huntegahaze.

< Levitiko 2 >