< Levitiko 17 >

1 Yehova anawuza Mose kuti,
and to speak: speak LORD to(wards) Moses to/for to say
2 “Uza Aaroni ndi ana ake, pamodzi ndi Aisraeli onse kuti, ‘Chimene Yehova walamula ndi ichi:
to speak: speak to(wards) Aaron and to(wards) son: child his and to(wards) all son: descendant/people Israel and to say to(wards) them this [the] word: thing which to command LORD to/for to say
3 Mwisraeli aliyense amene apha ngʼombe, mwana wankhosa kapena mbuzi mu msasa kapena kunja kwa msasa,
man man from house: household Israel which to slaughter cattle or sheep or goat in/on/with camp or which to slaughter from outside to/for camp
4 mʼmalo mobwera nayo pa khomo la tenti ya msonkhano pamaso pa Yehova ndi kuyipereka kuti ikhale nsembe ya Yehova, ameneyo wapalamula mlandu wa magazi, wakhetsa magazi ndipo ayenera kuchotsedwa pakati pa anthu anzake.
and to(wards) entrance tent meeting not to come (in): bring him to/for to present: bring offering to/for LORD to/for face: before tabernacle LORD blood to devise: count to/for man [the] he/she/it blood to pour: kill and to cut: eliminate [the] man [the] he/she/it from entrails: among kinsman his
5 Izi zili choncho kuti Aisraeli azibwera ndi nyama zawo za nsembe zimene akanaphera ku malo kwina kulikonse. Aisraeli azibwera nazo nyamazo kwa Yehova, kwa wansembe wokhala pa khomo la tenti ya msonkhano ndipo aziphere pomwepo kuti zikhale nsembe za chiyanjano.
because which to come (in): bring son: descendant/people Israel [obj] sacrifice their which they(masc.) to sacrifice upon face: surface [the] land: country and to come (in): bring them to/for LORD to(wards) entrance tent meeting to(wards) [the] priest and to sacrifice sacrifice peace offering to/for LORD [obj] them
6 Wansembe awaze magazi ake pa guwa la Yehova limene lili pa khomo la tenti ya msonkhano ndipo atenthe mafuta ake kuti atulutse fungo lokomera Yehova.
and to scatter [the] priest [obj] [the] blood upon altar LORD entrance tent meeting and to offer: burn [the] fat to/for aroma soothing to/for LORD
7 Motero asadzapherenso nsembe fano la mbuzi limene amachita nalo zadama. Limeneli ndi lamulo la muyaya kwa iwo ndi mibado ya mʼtsogolo.’”
and not to sacrifice still [obj] sacrifice their to/for satyr which they(masc.) to fornicate after them statute forever: enduring to be this to/for them to/for generation their
8 “Uwawuze kuti, ‘Mwisraeli aliyense kapena mlendo amene amakhala pakati pawo akapereka nsembe yopsereza kapena nsembe ina iliyonse
and to(wards) them to say man man from house: household Israel and from [the] sojourner which to sojourn in/on/with midst their which to ascend: offer up burnt offering or sacrifice
9 popanda kubwera nayo pa khomo la tenti ya msonkhano kudzayipereka pamaso pa Yehova, munthu ameneyo achotsedwe pakati pa anthu anzake.’”
and to(wards) entrance tent meeting not to come (in): bring him to/for to make: offer [obj] him to/for LORD and to cut: eliminate [the] man [the] he/she/it from kinsman his
10 “Mwisraeli aliyense kapena mlendo aliyense wokhala pakati panu amene adya magazi, ndidzamufulatira ndipo ndidzamuchotsa pakati pa anthu anzake.
and man man from house: household Israel and from [the] sojourner [the] to sojourn in/on/with midst their which to eat all blood and to give: put face my in/on/with soul: person [the] to eat [obj] [the] blood and to cut: eliminate [obj] her from entrails: among kinsman her
11 Pakuti moyo wa cholengedwa chilichonse uli mʼmagazi, ndipo ndawupereka kwa inu kuti muzichitira mwambo wopepesera machimo a moyo wanu pa guwa. Pajatu magazi ndiwo amachotsa machimo chifukwa moyo uli mʼmenemo.
for soul: life [the] flesh in/on/with blood he/she/it and I to give: give him to/for you upon [the] altar to/for to atone upon soul your for [the] blood he/she/it in/on/with soul: life to atone
12 Choncho ndikuwawuza Aisraeli kuti, ‘Pasapezeke aliyense wa inu wodya magazi, ngakhale mlendo wokhala pakati panu.’”
upon so to say to/for son: descendant/people Israel all soul: person from you not to eat blood and [the] sojourner [the] to sojourn in/on/with midst your not to eat blood
13 “Mwisraeli aliyense kapena mlendo aliyense wokhala pakati panu amene amasaka ndi kupha nyama zakuthengo kapena mbalame zimene amadya, ataye magazi ake pansi ndi kuwakwirira ndi dothi,
and man man from son: descendant/people Israel and from [the] sojourner [the] to sojourn in/on/with midst their which to hunt wild game living thing or bird which to eat and to pour: pour [obj] blood his and to cover him in/on/with dust
14 chifukwa moyo wa cholengedwa chilichonse uli mʼmagazi ake. Nʼchifukwa chake ndinawawuza Aisraeli kuti, ‘Musamadye magazi a cholengedwa chilichonse, chifukwa moyo wa cholengedwa chilichonse uli mʼmagazi. Aliyense wodya magaziwo ayenera kuchotsedwa pakati pa anthu anzake.
for soul: life all flesh blood his in/on/with soul: life his he/she/it and to say to/for son: descendant/people Israel blood all flesh not to eat for soul: life all flesh blood his he/she/it all to eat him to cut: eliminate
15 “‘Munthu aliyense, kaya ndi mbadwa kapena mlendo, amene amadya chilichonse chofa chokha, kapena chojiwa ndi zirombo, achape zovala zake ndi kusamba, komabe adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo. Kenaka adzakhala woyeretsedwa.
and all soul: person which to eat carcass and torn animal in/on/with born and in/on/with sojourner and to wash garment his and to wash: wash in/on/with water and to defile till [the] evening and be pure
16 Koma ngati sachapa zovala zake ndi kusamba, adzasenzabe machimo ake.’”
and if not to wash and flesh his not to wash: wash and to lift: guilt iniquity: crime his

< Levitiko 17 >