< Levitiko 17 >
1 Yehova anawuza Mose kuti,
Pakaiyin, Mose henga hiti hin aseipeh in,
2 “Uza Aaroni ndi ana ake, pamodzi ndi Aisraeli onse kuti, ‘Chimene Yehova walamula ndi ichi:
Aaron le achapte chule Israel chate jouse henga aseipeh ding in, bannei chan dan hochu athupeh in ahi.
3 Mwisraeli aliyense amene apha ngʼombe, mwana wankhosa kapena mbuzi mu msasa kapena kunja kwa msasa,
Israel telah a koi hijong leh, Pakai, Pathen chenna ponbuh kot phung tailouva; Pakai adia kilhaina bong, kelngoi chule kelcha that pen pen in danthu apalkeh ahi.
4 mʼmalo mobwera nayo pa khomo la tenti ya msonkhano pamaso pa Yehova ndi kuyipereka kuti ikhale nsembe ya Yehova, ameneyo wapalamula mlandu wa magazi, wakhetsa magazi ndipo ayenera kuchotsedwa pakati pa anthu anzake.
Ama chun thisan asotah jeh a, Pathen miteh lah a kona kisimtha lou ding ahi.
5 Izi zili choncho kuti Aisraeli azibwera ndi nyama zawo za nsembe zimene akanaphera ku malo kwina kulikonse. Aisraeli azibwera nazo nyamazo kwa Yehova, kwa wansembe wokhala pa khomo la tenti ya msonkhano ndipo aziphere pomwepo kuti zikhale nsembe za chiyanjano.
Hiche thupeh in adeisah pen chu, gammang tollah a kithat gancha jouse chu, Pakai angsunga ahin kailut diuva thupeh ahi. Kotbul lama thempupa henga ahinkai lut diu, kiloikhomna thilto dia kithat ding ahi.
6 Wansembe awaze magazi ake pa guwa la Yehova limene lili pa khomo la tenti ya msonkhano ndipo atenthe mafuta ake kuti atulutse fungo lokomera Yehova.
Thisan chu thempu pan ki khop khomna ponbuh kot phung maicham kimvel jousea athe thang ding, Pakaiya dia sathao hochu gimnamtuiya agovam ding ahi.
7 Motero asadzapherenso nsembe fano la mbuzi limene amachita nalo zadama. Limeneli ndi lamulo la muyaya kwa iwo ndi mibado ya mʼtsogolo.’”
Israel chaten Pathen ajoulhep nauva kelcha limsemthu, doihou dinga gammang lah a gancha atha kitlou diu ahi. Hiche dan thupeh hi Israelten akhang akhanga ajui diu ahi.
8 “Uwawuze kuti, ‘Mwisraeli aliyense kapena mlendo amene amakhala pakati pawo akapereka nsembe yopsereza kapena nsembe ina iliyonse
Israel mite hihen amaho lah a cheng gamchom mi hijong leh pumgo thilto ahi.
9 popanda kubwera nayo pa khomo la tenti ya msonkhano kudzayipereka pamaso pa Yehova, munthu ameneyo achotsedwe pakati pa anthu anzake.’”
Kikhop khomna ponbuh kotphung tailouva Pathen adia kilhaina sem jouse, Pathen mite holah a kona kisim thalou ding ahi.
10 “Mwisraeli aliyense kapena mlendo aliyense wokhala pakati panu amene adya magazi, ndidzamufulatira ndipo ndidzamuchotsa pakati pa anthu anzake.
Israel hihen gamchom mi hijong leh, thisan lhoh lha theng louva sa toh neh tha aum le, hichu Pakai, Pathen toh kidou ahin, amite lah akona simtha lou ding ahi.
11 Pakuti moyo wa cholengedwa chilichonse uli mʼmagazi, ndipo ndawupereka kwa inu kuti muzichitira mwambo wopepesera machimo a moyo wanu pa guwa. Pajatu magazi ndiwo amachotsa machimo chifukwa moyo uli mʼmenemo.
Ganhing jouse hinna hi thisan akon ahi, hiche jeh achu Pakaiyin mi jouse chonset suhmang ahitheina dinga, hichu maicham phunga asun lhah dinga thupeh ahi.
12 Choncho ndikuwawuza Aisraeli kuti, ‘Pasapezeke aliyense wa inu wodya magazi, ngakhale mlendo wokhala pakati panu.’”
Hijeh chun Pakaiyin Israel chate le alah uva cheng gamchom miho jaonaa, sa chu thisan jaonaa neh lou dia athupeh ahi.
13 “Mwisraeli aliyense kapena mlendo aliyense wokhala pakati panu amene amasaka ndi kupha nyama zakuthengo kapena mbalame zimene amadya, ataye magazi ake pansi ndi kuwakwirira ndi dothi,
Israel mi hihen, gamchom mi alah uva cheng hi jong leh, gamlah a saham vacha ham, houtoh kitoh a atheng, hiche ho that pen pen chu thisanso ahitan, hichu leiset avuh khu ding ahi.
14 chifukwa moyo wa cholengedwa chilichonse uli mʼmagazi ake. Nʼchifukwa chake ndinawawuza Aisraeli kuti, ‘Musamadye magazi a cholengedwa chilichonse, chifukwa moyo wa cholengedwa chilichonse uli mʼmagazi. Aliyense wodya magaziwo ayenera kuchotsedwa pakati pa anthu anzake.
Ganhing hinna kiti hi thisan ahin, hibanga chu sa kiti phot Israel chaten thisan jaonaa nehlou dia Pakai thupeh ahi, koi hileh anetha chu amite lah a kona pampeiya um ding ahi.
15 “‘Munthu aliyense, kaya ndi mbadwa kapena mlendo, amene amadya chilichonse chofa chokha, kapena chojiwa ndi zirombo, achape zovala zake ndi kusamba, komabe adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo. Kenaka adzakhala woyeretsedwa.
Israel mi hihen gamchom mi hijong leh, gan thikam ahilouleh, sa hang ham in atha nekha aum le avon jouse akisop theng ding, ama jong kisil lha ding, nilhum keiya atheng louva um ding ahi.
16 Koma ngati sachapa zovala zake ndi kusamba, adzasenzabe machimo ake.’”
Hichu abol tah louva ahileh, themmo chang ding ahi.