< Levitiko 16 >

1 Atafa ana awiri a Aaroni amene anaphedwa atapita pamaso pa Yehova mosayenera, Yehova anayankhula ndi Mose.
Dan toh kitoh louva Pathen angsunga thilto anabol lhon jal'a, thina chang teni Aaron chapate ni thinung in Pakai, Pathen in Mose henga hiti hin aseipeh in,
2 Yehova anawuza Mose kuti, “Uza mchimwene wako Aaroni kuti asamalowe ku Malo Wopatulika, kuseri kwa katani, pamaso pa chivundikiro cha Bokosi la Chipangano nthawi iliyonse imene akufuna kuopa kuti angadzafe, pakuti Ine ndimaoneka mu mtambo umene uli pamwamba pa chivundikiro cha Bokosi la Chipangano.
Pakai, Pathen in Mose henga hiti hin asei tan, “Na sopipa Aaron jah a seipeh tan pondal kidalna muntheng lailung, thingkong chunga um ngailut hepi touna maiya ama cham in alut nom phat chan in hung lut lou ding, hichu ahilouleh thi jeng thei ahi; ajeh chu hichea ngailut hepi touna chunga khu keima meiloma kilahji kahi.”
3 “Aaroni azilowa Malo Wopatulika Kwambiri motere: azitenga mwana wangʼombe wamwamuna kuti akhale nsembe yopepesera machimo ndi nkhosa yayimuna kuti ikhale nsembe yopsereza.
Aaron vang hiche munthenga hi lut theia, chonset thilto dinga bongchal gol khat leh kelngoi chal khat jaonaa ahin kai ding,
4 Azivala mwinjiro wopatulika wa nsalu yosalala, azivalanso kabudula wa mʼkati wa nsalu yosalala, azimanga lamba wa nsalu yosalala, ndipo avalenso nduwira ya nsalu yosalala kumutu. Zimenezi ndi nsalu zopatulika ndipo atasamba thupi lonse azivala zimenezi.
Chule tupet ponnema kikhui sangkhol chol len chu aki ah ding, tupet ponnem a kikhui toka chol jong akichen a, chule tupet ponnem a kikhui chalchep konggah chu akong akigah a, tupet'a kikhong delkop jong akop ding, hichengse hi von lah a atheng ahin, hijeh chun thempu pan jong hiche von hochu akivon theina din atahsa pumpi tuiya kisil thengsel ding ahi.
5 Kuchokera pa gulu la Aisraeli, Aaroni azitenga mbuzi zazimuna ziwiri kuti zikhale nsembe yopepesera machimo ndi nkhosa yayimuna kuti ikhale nsembe yopsereza.
Chule Israel chate khoppi apat chu kelchal nou nitah, pumgo thiltoa to dinga kelchal khat ma akimat ding ahi.
6 “Aaroni apereke ngʼombe yayimuna kuti ikhale yopepesera machimo a iye mwini kuti achite mwambo wopepesera machimo ake pamodzi ndi a banja lake.
Aaron in jong atumbeh a ama dinga bongchal khat atodoh ding, hitia chu amading leh ainsung mite dinga kithoidamna anei masat ding ahi.
7 Kenaka atenge mbuzi ziwiri zija ndipo aziyimike pamaso pa Yehova pa khomo la tenti ya msonkhano.
Chule Aaron in jong kelchal teni chu akai ding, kikhop khomna ponbuh kotbul Pathen ansunga chu adinsah a,
8 Aaroni ndiye achite maere pa mbuzi ziwirizo kuti imodzi ikhale ya Yehova, ndipo inayo ikhale ya Azazele.
Chule Aaron in jong kelchal teni dia phun asan ding, hiche aphunsan lah a khat chu, Pakai ding chule aphunsan khat vang chu Azazel chang ding ahi.
9 Aaroni abwere ndi mbuzi imene maere aonetsa kuti ndi ya Yehova, ndipo apereke kuti ikhale nsembe yopereka chifukwa cha tchimo.
Chule Aaron in jong Pakaiya dia phun, achunga phunchan chuhna kelcha chu akai ding, chonset thiltoa atodoh ding ahi.
10 Koma mbuzi imene maere aonetsa kuti ndi yosenza machimo, apereke ya moyo pamaso pa Yehova, kuti achite mwambo wopepesera machimo pa mbuziyo poyitumiza ku chipululu kuti ikhale ya Azazele.
Hitobanga chu Azazel chan ding phun pha, achunga phunchan chuhna kelcha chu kithoidamna dinga ahing laiya todoh ding, hichu Azazel chan dinga gamlah a ahinga lha mang ding ahi.
11 “Aaroni apereke ngʼombe yayimuna kuti ikhale nsembe yopepesera machimo ake. Ndiye achite mwambo wopepesera machimo a iye mwini wake pamodzi ndi banja lake. Pambuyo pake aphe ngʼombe yopepesera machimo ake aja.
Aaron in jong amatah chonset thilto dinga bongchal chu atodoh ding, hiche bongchal chu ama chonset thilto dinga akitha ding ahi.
12 Kenaka iye atenge chofukizira chodzaza ndi makala a moto ochokera pa guwa lansembe pamaso pa Yehova. Atengenso lubani wonunkhira ndi woperapera wokwanira manja awiri, ndipo alowe naye kuseri kwa katani.
Chule Aaron in jong Pakai angsung maicham phunga pat, meiam kong khat dim hichu gimnamtui lhutna ding, chule hoitah a kisemsa gimnamtui khut dimni aham doh a, hichu pondal kikhai kal lama chu apohlut ding ahi.
13 Athire lubani pa moto pamaso pa Yehova kuti utsi wa lubaniyo uphimbe chivundikiro chimene chili pamwamba pa Bokosi la Chipangano, kuti Aaroniyo asafe.
Hitia chu Pakai angsunga meikong lah a gimnamtui chu alelhah ding, chule hettohsahna dinga kido ngailut hepi touna chu, gimnamtui kilhutna meikhu chun atom sohhel ding ahi, hichu ahilouleh thinan alhun thei ahi.
14 Ndipo atenge magazi ena a ngʼombeyo, awawaze ndi chala chake pa chivundikiro cha kummawa; kenaka awaze magaziwo ndi chala chake kasanu ndi kawiri patsogolo pa chivundikirocho.
Chule bongchal thisan chu themkhat alah ding, akhut jung akona ngailut hepi touna mailah a chu athe lhah ding, ngailut hepi touna mailah a chu akhut jung akona sagi veijen athe khum ding ahi.
15 “Kenaka Aaroni aphe mbuzi ya nsembe yopepesera machimo a anthu, ndipo magazi ake alowe nawo kuseri kwa katani ndi kuchita chimodzimodzi monga anachitira ndi magazi a ngʼombe aja: Aaroni awaze magaziwo pa chivundikiro chija ndi patsogolo pa chivundikirocho.
Hiche jouteng chule mipi dinga chonset thilto kelcha chu atha ding, athisan vang chu pondal sunglama achoilut a, hiche kelcha thisan chu bongchal thisan kibolna bang bang achu abol ding, ngailut hepi touna chungvum chule ngailut hepi touna maiya chu athin khum ding ahi.
16 Pamenepo ndiye kuti wansembeyo wachita mwambo wopepesera ku Malo Wopatulika chifukwa cha kudetsedwa ndi kuwukira kwa Aisraeli pa machimo ena aliwonse amene achita. Achite chimodzimodzi ndi tenti ya msonkhano imenenso ili yodetsedwa chifukwa cha machimo awo.
Hitobang achu Israel chate aboh a aumna jouseu leh chonset a aumnauva kona muntheng pen chu asuhtheng ding, hitobang akona hi ngahmun lailung chu atheng loua umji ahitan, suh thengna abolji ding ahi.
17 Mu tenti ya msonkhano musakhale munthu ndi mmodzi yemwe nthawi imene Aaroni akupita kukachita mwambo wopepesera ku Malo Wopatulika mpaka atatulukako. Musakhale munthu mu tenti ya msonkhano mpaka atachita mwambo wopepesera machimo a iye mwini wake, banja lake ndi gulu lonse la Aisraeli.
Muntheng pen suhthengna dia Aaron asung lhah a ahung potdoh kit kahsea, kikhop khomna ponbuh sunga koima umthei lou ding ahi. Amavang ama le ainsung mite chule miho dinga thensona anei ding,
18 “Kenaka, Aaroniyo akatuluka apite ku guwa limene lili pamaso pa Yehova ndi kulichitira mwambo wolipepesera. Atengeko magazi a ngʼombe yayimuna ndiponso magazi a mbuzi ndi kuwapaka pa nyanga zonse za guwa lansembe.
Chule maicham phunga pumgo thilto abola suh thengna anei ding, hichea chu bongchal thisan phabep le kelcha thisan phabep alah a, maicham ninga selki hose chu anunat ding ahi.
19 Magazi ena awawaze pa guwalo ndi chala chake kasanu ndi kawiri kuliyeretsa ndi kulipatula kuchotsa zodetsa za Aisraeli.
Hiche thisan chu akhut junga akhoi ding, chuteng maicham chung vum lah achu athin khum ding ahi. Hitia hi Israelte chonset jal'a maicham asema athenso ding ahi.
20 “Aaroni akatsiriza mwambo wopepesera Malo Wopatulika, tenti ya msonkhano ndi guwa, azibwera ndi mbuzi yamoyo kudzayipereka nsembe.
Chule Aaron in jong muntheng pen jouse le Pakai Pathen chenna ponbuh suhthengna chule maicham sutheng naho achai kimsoh teng leh, phun phatna dia kelcha chu akatdoh ding ahi.
21 Aaroni asanjike manja ake pa mutu wa mbuziyo ndipo awulule pa mbuziyo zoyipa zonse ndi zowukira zonse za Aisraeli, kutanthauza machimo awo onse. Machimowo awayike pa mutu wa mbuziyo. Kenaka munthu amene anasankhidwa athamangitsire mbuziyo ku chipululu.
Chuteng Aaron in akhut teni kelcha chunga chu angap ding, chonset thil ho ahin, gitlouna jouse, Israel chaten doumah aboldoh jouseu aphondoh ding, kelcha chunga buhlhah peh banga abola, chuteng son umtah mikhat chun gammang lah a dellut ding ahi.
22 Mbuziyo isenze machimo awo onse ndi kupita nawo kutali ndipo munthuyo aleke mbuziyo kuti ipite ku chipululuko.
Hiche kelcha chun achonsetna ho jouseu chu, chenna loubeh gammang lah khat a apohmang ding ahi.
23 “Pambuyo pake Aaroni alowe mu tenti ya msonkhano ndi kuvula zovala zosalala zija zimene anavala polowa ku Malo Wopatulika ndi kuzisiya komweko.
Chujouteng muntheng sung alut masanga, thempu vona kivon chengse chu kikhop khomna ponbuh lut a Aaron in aga puilut ding, hiche muna chu ahin dalhah diu ahi.
24 Asambe thupi lonse ku Malo Wopatulika ndi kuvala zovala zake za nthawi zonse. Kenaka atuluke ndi kukapereka nsembe yopsereza ya iye mwini, ndiponso nsembe yopsereza yoperekera anthu. Akatero ndiye kuti wachita mwambo wopepesera machimo a iye mwini wake ndi a anthu.
Chule muntheng khat a kisil lha ding, akivona ngai banga kivona hichea chu amatah chonsetna le mipi chonset thensona dinga, pumgo thilto chu anei ding ahi.
25 Mafuta a nyama yopepesera machimo awatenthe pa guwa lansembe.
Chule chonset thoidam nadia sathao jouse chu, maicham phunga agovam ding ahi.
26 “Tsono munthu amene anaperekeza mbuzi yosenza machimo ija achape zovala zake ndi kusamba. Pambuyo pake alowe ku msasa.
Chule gammang lah a kelcha delmang pachu, ngahmun ahung lhun kah a avon jouse akisop lhah ding, ama jeng jong kisil lha ding ahi.
27 Ngʼombe ndi mbuzi zoperekera nsembe yopepesera machimo zimene magazi ake anabwera nawo kuti achitire mwambo wopepesera Malo Wopatulika, azitulutsire kunja kwa msasa. Koma zikopa zake, nyama yake ndi matumbo ake azitenthe.
Chonset thoidamna dia kithat bongchal le kelcha teni thisan jong chonset abeina thei ding in, muntheng pena kikoisa chu ngahmun polama govam ding, avun leh asa chule agil jaonaa aboncha govam ding ahi.
28 Munthu amene azitenthe achape zovala zake ndi kusamba. Pambuyo pake alowe mu msasa.
Hitia chu agouvam penpen in ngahmun asung lhah kah a, aponsil jouse asop lhah ding, chuteng ngahmun lai achu sunglha bep ding ahi.
29 “Ili likhale lamulo lanu lamuyaya: Mwezi wachisanu ndi chiwiri, pa tsiku la khumi la mwezi, mugonje pamaso pa Yehova. Musamagwire ntchito iliyonse, kaya ndinu mbadwa kapena mlendo amene akukhala pakati panu,
Chule hiche dan hi akhang akhanga na jui diu, lha sagi, nisom alhin nikho teng Israel chate chule alah uva cheng gamchom mihon an angol diu, na atoh louhel diu ahi.
30 chifukwa tsiku limeneli kudzachitika mwambo wopepesera machimo anu, kukuyeretsani kuti mukhale oyeretsedwa ku machimo anu pamaso pa Yehova.
Hou thulam dola thenna anei na ding un, hiche nikhoa chu achonset nau thoidamna nei ding ahi.
31 Limeneli ndi tsiku lanu la Sabata lopumula, ndipo muzigonja pamaso pa Yehova. Limeneli ndi lamulo lanu la muyaya.
Hiche nikho hi nikho theng ahin, an ngol ding natoh jong bol louva umding ahi. Hitia chu dan jouse hi akhang akhanga chepi ding ahi.
32 Wansembe amene wadzozedwa ndi kupatulidwa kuti akhale wansembe kulowa mʼmalo mwa abambo ake ndiye azichita mwambo wopepesera machimo atavala zovala zake zosalala ndi zopatulika.
Thempupa khela dantoh kitoh a thensona changsa, thempu chungnung in suh thengna kin anei ding, thempu vona kivon ding,
33 Adzachite mwambo wopepesera machimo Malo Wopatulika, tenti ya msonkhano ndi guwa lansembe. Adzachitenso mwambo wopepesera anzake ndi gulu lonse la anthu.
Pakai chenna ponbuh chule muntheng chungnung, maicham phung chule thempu ho jouse le mipi ho chu suhthengna abolpeh ding ahi.
34 “Ili likhale lamulo lanu lamuyaya. Mwambo wopepesera machimo uzichitika kamodzi pa chaka chifukwa cha machimo a anthu onse.” Ndipo Mose anachita monga momwe Yehova analamulira.
Hitia chu dan hichengse hi akhang akhanga jui ding ahi. Israel chate achonset nauva kona suhthengna thei dia, hiche kithoidamna hi kumseh a khatvei bol ding, hichu Pakai, Pathen thupeh bang in Mose’n jong aboltan ahi.

< Levitiko 16 >