< Levitiko 12 >

1 Yehova anayankhula ndi Mose kuti,
Hiti hin Pakaiyin, Mose henga thu aseipeh in,
2 “Awuze Aisraeli kuti, ‘Mkazi akakhala woyembekezera, nabala mwana wa mwamuna, mkaziyo adzakhala wodetsedwa kwa masiku asanu ndi awiri, ngati pa masiku ake akusamba.
Israel chate jouse jah a hiti hin seipeh in, Numei khat in nao avop a anavah lhah a nao chu pasal ahileh, hiche numeinu chu athi neipet banga, ni sagi sung aboh a um ding ahi.
3 Pa tsiku lachisanu ndi chitatu, mwanayo achite mdulidwe.
Hitobanga chu niget lhinni le, achapa chu chep kitan ding ahi.
4 Mkaziyo adikire masiku ena 33 kuti ayeretsedwe ku matenda ake. Asakhudze kanthu kalikonse koyera kapena kulowa mʼmalo wopatulika mpaka masiku a kuyeretsedwa kwake atatha.
Chujouteng hiche numeinu chu athisana kona thenso kinbolna dinga, nisom thumle nithum hitia chu um ding; hiche nikho kitipna nikho sunga chu hiche numeinu chun thiltheng khat jong atoh khah lou ding, houin munthenga jong lutlou ding ahi.
5 Ngati abala mwana wamkazi, adzakhala wodetsedwa kwa masabata awiri, monga zikhalira pa nthawi yake yosamba. Ndipo mkaziyo adikire masiku ena 66, kuti ayeretsedwe ku matenda akewo.
Hiche numei chun cha ahin a numei ahileh, athi neiphat bang banga hapta ni kah atheng loua um ding; chujouteng athisana kona thenso nadia nisom le nigup angai banga anga ding ahi.
6 “‘Masiku ake wodziyeretsa akatha, kaya ndi a mwana wamwamuna kapena a mwana wamkazi, abwere kwa wansembe ndi mwana wankhosa wa chaka chimodzi pa khomo la tenti ya msonkhano kuti ikhale nsembe yopsereza. Abwerenso ndi chiwunda cha nkhunda kapena njiwa kuti ikhale nsembe yopepesera machimo.
Chapa pen dol hihen lang chanu pen dola hijong leh, jechan ding numeinu kithensona nikho jat alhin teng, hiche numeinu chun kikhop khomna ponbuh kotbula chu, thempu henga pumgo maicham thilto dinga kum khat lhing kelngoi ahin kai ding, chule chonset maicham thilto dinga vapal nou ahin choi thading ahi.
7 Wansembeyo apereke zimenezi pamaso pa Yehova pochita mwambo wopepesera mkaziyo. Ndipo mkaziyo adzakhala woyeretsedwa ku msambo wake. “‘Amenewa ndiwo malamulo a mkazi amene wabala mwana wamwamuna kapena wamkazi.
Chuteng numei naosen neinu dia thempu pan kithoina dinga Pakai henga akatdoh peh ding, chule numei nu chu athisan lonna akona athenga umbep ding ahi. Hiche dan hi numei chanu le chapa hing thei jouse dinga dan ahi.
8 Ngati mkaziyo sangathe kupeza mwana wankhosa, abwere ndi njiwa ziwiri kapena mawunda ankhunda awiri: imodzi ikhale ya nsembe yopsereza ndipo inayo ikhale ya nsembe yopepesera machimo. Tsono wansembe achite mwambo wopepesera wa mkaziyo ndipo adzayeretsedwa.’”
Hiche numei chanei nuchun kelngoinou anei louva ahileh, vakhu nou ni pumgo maicham thiltoa anei ding, hiche lah a adang khat chu chonset maicham thiltoa ding, chuteng thempu pan amanu dinga kithoina asempeh a athenga um ding ahi.

< Levitiko 12 >