< Levitiko 10 >
1 Ana a Aaroni, Nadabu ndi Abihu, aliyense anatenga chofukizira lubani chake nayikamo makala a moto ndi kuthiramo lubani. Iwo anapereka pamaso pa Yehova moto wachilendo, moto umene Yehova sanawalamule.
Harun'un oğulları Nadav'la Avihu buhurdanlarını alıp içlerine ateş, ateşin üstüne de buhur koydular. RAB'bin buyruklarına aykırı bir ateş sundular.
2 Choncho moto unatuluka pamaso pa Yehova ndi kuwapsereza, ndipo anafa pamaso pa Yehova.
RAB bir ateş gönderdi. Ateş onları yakıp yok etti. RAB'bin huzurunda öldüler.
3 Pamenepo Mose anawuza Aaroni kuti, “Pajatu Yehova ananena kuti, “‘Kwa iwo amene amandiyandikira ndidzaonetsa ulemerero wanga; pamaso pa anthu onse ndidzalemekezedwa.’” Aaroni anakhala chete wosayankhula.
Musa Harun'a şöyle dedi: “RAB demişti ki, ‘Bana hizmet edenler kutsallığıma saygı duyacak Ve halkın tümü beni yüceltecek.’” Harun hiçbir şey söylemedi.
4 Mose anayitana Misaeli ndi Elizafani, ana a Uzieli, abambo angʼono a Aaroni, ndipo anawawuza kuti, “Bwerani kuno mudzachotse abale anuwa pa malo wopatulika ndi kuwatulutsira kunja kwa msasa.”
Musa Harun'un amcası Uzziel'in oğullarını, Mişael'le Elsafan'ı çağırdı, “Gelin, kardeşlerinizi kutsal yerin önünden kaldırıp ordugahın dışına çıkarın” dedi.
5 Choncho anabwera atavala minjiro yawo ndipo anawatenga ndi kuwatulutsa kunja kwa msasawo monga momwe Mose analamulira.
Geldiler ve Musa'nın buyurduğu gibi cesetleri üzerlerindeki mintanlarıyla ordugahın dışına çıkardılar.
6 Ndipo Mose anawuza Aaroni ndi ana ake Eliezara ndi Itamara kuti, “Musalileke tsitsi lanu nyankhalala ndipo musangʼambe zovala zanu kuti mungafe, ndi mkwiyo wa Yehova ungagwere anthu onsewa. Koma abale anu okha, kutanthauza fuko lonse la Israeli ndiwo ayenera kulira omwalira aja amene Yehova wawapsereza ndi moto.
Sonra Musa Harun'la oğulları Elazar'la İtamar'a, “Saçlarınızı dağıtmayın, giysilerinizi yırtmayın” dedi, “Yoksa ölürsünüz ve RAB bütün topluluğa öfkelenir. Ama kardeşleriniz, bütün İsrail halkı RAB'bin ateşle yok ettiği bu insanlar için yas tutsun.
7 Musatuluke kunja kwa tenti ya msonkhano, mungafe, chifukwa munadzozedwa ndi mafuta a Yehova kukhala ansembe.” Choncho iwo anachita monga Mose ananenera.
Buluşma Çadırı'nın giriş bölümünden ayrılmayın, yoksa ölürsünüz. Çünkü RAB'bin mesh yağıyla kutsandınız.” Harun'la oğulları Musa'nın dediğine uydular.
8 Pambuyo pake Yehova anayankhula ndi Aaroni nati,
RAB Harun'a şöyle dedi:
9 “Iwe ndi ana ako musamamwe vinyo kapena chakumwa chilichonse choledzeretsa pamene mukulowa mu tenti ya msonkhano kuti mungafe. Ili ndi lamulo lamuyaya pa mibado yanu yonse.
“Sen ve oğulların Buluşma Çadırı'na şarap ya da herhangi bir içki içip girmeyin, yoksa ölürsünüz. Kuşaklar boyunca bir kural olsun bu.
10 Muzisiyanitsa pakati pa zinthu zopatulika ndi zinthu wamba, pakati pa zinthu zodetsedwa ndi zinthu zoyeretsedwa,
Kutsalla bayağı olanı, kirliyle temizi birbirinden ayırt etmelisiniz.
11 ndipo muyenera kuphunzitsa Aisraeli onse malamulo amene Yehova wakupatsani kudzera mwa Mose.”
RAB'bin Musa aracılığıyla İsrail halkına bildirdiği bütün kuralları onlara öğretmelisiniz.”
12 Mose anawuza Aaroni ndi ana ake otsalawo, Eliezara ndi Itamara kuti, “Tengani zopereka zachakudya zopanda yisiti zimene zatsala pa nsembe zopsereza za kwa Yehova ndipo muzidye pafupi ndi guwa pakuti ndi zopatulika kwambiri.
Musa Harun'a ve sağ kalan oğulları Elazar'la İtamar'a şöyle dedi: “RAB için yakılan sunulardan artan tahıl sunusunu alın, mayasız ekmek yapıp sunağın yanında yiyin. Çünkü çok kutsaldır.
13 Muzidye pa malo wopatulika chifukwa zimenezi ndi gawo lako ndi la ana ako pa zopereka zopsereza kwa Yehova. Izitu ndi zimene Yehova anandilamulira.
Onu kutsal bir yerde yemelisiniz. Çünkü RAB için yakılan sunulardan senin ve oğullarının payıdır bu. Bana böyle buyruk verildi.
14 Koma iwe pamodzi ndi ana ako aamuna ndi aakazi muzidya chidale chimene chinaweyulidwa ndi ntchafu zimene zinaperekedwa nsembe. Muzidye pamalo woyeretsedwa. Zimenezi zaperekedwa kwa iwe ndi ana ako monga gawo lanu pa zopereka zachiyanjano zimene apereka Aisraeli.
Sallamalık döşle bağış olarak sunulan budu ise oğulların ve kızlarınla birlikte temiz bir yerde yemelisin. Çünkü bunlar İsrail halkının sunduğu esenlik kurbanlarından senin ve çocuklarının payı olarak ayrıldı. Bağış olarak sunulan butla sallamalık döşü, yakılacak sunu yağlarıyla birlikte getirip RAB'bin önünde sallamalık sunu olarak sunacaklar. RAB'bin buyruğu uyarınca bunlar sonsuza dek senin ve çocuklarının payı olacak.”
15 Ntchafu imene inaperekedwayo ndi chidale chomwe chinaweyulidwacho abwere nazo pamodzi ndi nsembe ya mafuta ya Yehova yotentha pa moto, ndipo uziweyule kuti zikhale zopereka zoweyula pamaso pa Yehova. Zimenezi zizikhala zako ndi ana ako nthawi zonse monga walamulira Yehova.”
16 Pambuyo pake Mose anafunafuna mbuzi ya nsembe yopepesera machimo koma anapeza kuti anayitentha kale. Apa Mose anakalipira Eliezara ndi Itamara, ana a Aaroni otsala aja nati,
Musa günah sunusu olarak sunulacak tekeyi soruşturdu, yakılmış olduğunu öğrenince, Harun'un sağ kalan oğulları Elazar'la İtamar'a çok öfkelendi, “Neden günah sunusunu kutsal bir yerde yemediniz?” diye sordu, “O çok kutsaldır. Topluluğun suçunu üstlenmesi ve günahlarını bağışlatmanız için RAB onu size vermişti.
17 “Chifukwa chiyani simunadyere pamalo wopatulika nsembe yopepesera machimo ija? Kodi imene ija siyopatulika? Kodi Yehova sanapereke nyamayo kwa inu kuti muchotse machimo a mpingo wonse powachitira mwambo wa nsembe yopepesera machimo pamaso pa Yehova?
18 Pakuti magazi ake sanalowe nawo ku Malo Wopatulika, mukanadya nyama ya mbuziyo pa malo wopatulikawo monga Yehova analamulira.”
Tekenin kanı kutsal çadıra getirilmemiş. Buyurduğum gibi tekeyi kesinlikle kutsal yerde yemeniz gerekirdi.”
19 Aaroni anamuyankha Mose kuti, “Lero anthu apereka nsembe yawo yopepesera machimo ndiponso nsembe yawo yopsereza pamaso pa Yehova komabe zinthu zoterezi zandichitikira. Kodi Yehova akanakondwa ndikanadya nsembe yopepesera machimo lero?”
Harun, “Halk bugün RAB'be günah sunusu ve yakmalık sunu sundu” diye yanıtladı, “Benim başıma ise bunlar geldi. Günah sunusunu bugün yemiş olsaydım, RAB bundan hoşnut olur muydu?”
20 Pamene Mose anamva zimenezi, anakhutira.
Musa yanıtı uygun buldu.