< Maliro 2 >
1 Haa, Ambuye waphimba mwana wamkazi wa Ziyoni ndi mtambo wa mkwiyo wake! Iye wataya pansi ulemerero wa Israeli kuchoka kumwamba. Pa tsiku la mkwiyo wake Iye sanakumbukirenso popondapo mapazi ake.
Bawipa ni Zion canu dawkvah, a lungkhueknae tâmai hoi muen a ramuk toe. Isarel miphun e a minhawinae teh kalvan hoi talai dawk a tâkhawng toe. Ama e a lungkhueknae hnin nah, amae khok toungnae hai a pahnim toe.
2 Ambuye anawononga midzi yonse ya Yakobo mopanda chifundo; mu mkwiyo wake anagwetsa malinga a mwana wamkazi wa Yuda. Anagwetsa pansi mochititsa manyazi maufumu ndi akalonga ake.
Bawipa ni pahren laipalah Jakop onae hmuen pueng a raphoe pouh. Ama e a lungkhueknae hoi Judah canu e rapanimnaw hah talai totouh a sin teh, a uknaeram hoi a bawinaw hai he a raphoe pouh.
3 Atakwiya kwambiri, Ambuye anathyola nyanga iliyonse ya Israeli. Anabweza dzanja lake lamanja pamene mdani anamuyandikira. Ambuye anatentha fuko la Yakobo ngati moto wonyeketsa umene umawononga zinthu zonse zomwe zili pafupi.
A lungkhueknae hmai a kak teh, Isarel miphunnaw e ki pueng hah a tâtueng pouh. A taran hmalah aranglae a kut a la pouh. A tengpam e hmaipalai ka thaw e patetlah Jakop canaw teh a kamtawi toe.
4 Wakokera uta wake pa ife ngati ndife adani; wayimiritsa dzanja lake pa ife ngati ndife adani, ndipo anapha onse amene tinkawayangʼana monyadira. Ukali wake ukuyaka ngati moto pa tenti ya mwana wamkazi wa Ziyoni.
Taran patetlah a kangdue teh aranglae kut hoi licung hah a sawn. Zion canu lukkareiim dawk, a meikahawi e naw pueng hah be a thei teh, hmai patetlah lungkhueknae a rabawksin.
5 Ambuye ali ngati mdani; wawonongeratu Israeli; wawonongeratu nyumba zake zonse zaufumu ndipo wawononga malinga ake. Iye wachulukitsa kubuma ndi kulira kwa mwana wamkazi wa Yuda.
Bawipa ni a taran teh, Isarel miphun hai thoseh, imkahawinaw hai thoseh a payawp toe. Rapanimnaw hai he a raphoe toe. Judah canunaw e khuikanae hoi cingounae hoe a pung sak.
6 Wagwetsa malo ake okhalamo ngati khumbi la mʼmunda; wawononga malo ake a msonkhano. Yehova wayiwalitsa Ziyoni maphwando ake oyikika ndi masabata ake. Mokwiya kwambiri, Iye ananyoza mfumu ndi wansembe.
Lukkareiim hah takha patetlah koung a raphoe pouh. A sungren sak e pawi hah a raphoe pouh. Zion khopui dawk pawi a sak e hoi Sabbath hnin hah Bawipa ni a pahnim sak. A lungkhuek lawi siangpahrang hoi vaihma hah a hnoun pouh.
7 Ambuye wakana guwa lake la nsembe ndipo wasiya malo ake opatulika. Iye wapereka makoma a nyumba zake zaufumu kwa mdani wake; adaniwo anafuwula mʼnyumba ya Yehova ngati kuti ndi pa tsiku la chikondwerero.
Bawipa ni amae thuengnae khoungroe hah a pahnawt toe. Ama e hmuen kathoung hah a panuet toe. Siangpahrang im kalupnae hah taran kut dawk a poe toe. Ahnimanaw teh pawitonae hnin patetlah Bawipa e im dawk a hramki awh.
8 Yehova anatsimikiza kugwetsa makoma a mwana wamkazi wa Ziyoni. Anawayesa ndi chingwe ndipo sanafune kuleka kuwagwetsa. Analiritsa malinga ndi makoma; onse anawonongeka pamodzi.
BAWIPA ni Zion canu e rapan hah raphoe hane a noe e patetlah raphoe hanelah a kut hno hoeh. Bangnuenae rui a payang teh, athung lae rapan hoi alawilae rapan hah khuikanae lah reirei a coung sak.
9 Zipata za Yerusalemu zalowa pansi; wathyola ndi kuwononga mipiringidzo yake. Mfumu ndi akalonga ake agwidwa ukapolo pakati pa mitundu ya anthu, palibenso lamulo, ndipo aneneri ake sakupeza masomphenya kuchokera kwa Yehova.
A tungdumnae longkhanaw teh talai thung lah a bo toe. Longkha tarennae sumtaboungnaw teh, koung kâkhoe toe. Siangpahrang hoi bawinaw teh Jentelnaw rahak ao awh teh, kâlawk awm hoeh. Profetnaw hai Bawipa koehoi vision hmawt awh hoeh toe.
10 Akuluakulu a mwana wamkazi wa Ziyoni akhala chete pansi; awaza fumbi pa mitu yawo ndipo avala ziguduli. Anamwali a Yerusalemu aweramitsa mitu yawo pansi.
Zion canu e kacuenaw teh, vaiphu a lû dawk a kâphuen awh te, buri a kâkhu teh, tanglakacuem teh amamae a lû hah talai dawk a saling awh.
11 Maso anga atopa ndi kulira, ndazunzika mʼmoyo mwanga, mtima wanga wadzaza ndi chisoni chifukwa anthu anga akuwonongeka, chifukwa ana ndi makanda akukomoka mʼmisewu ya mu mzinda.
Camoca hoi sanu ka net naw ni khopui thung lamnaw dawk sut a kamlei awh teh, ka miphun tanglanaw a rawk dawkvah, ka mitphi a bo teh, ka lungthin teh runae a kâhmo.
12 Anawo akufunsa amayi awo kuti, “Kodi tirigu ndi vinyo zili kuti?” pamene akukomoka ngati anthu olasidwa mʼmisewu ya mʼmizinda, pamene miyoyo yawo ikufowoka mʼmanja mwa amayi awo.
Ahnimanaw teh, a hmâ ka cat e patetlah khopui thung lamnaw dawk sut a kamlei awh teh, a manunaw e lungtabue dawk amamae a hringnae hah a awi awh teh, a manunaw koe satun hoi misurtuinaw hah nâmaw ao telah a pacei awh.
13 Ndinganene chiyani za iwe? Ndingakufanizire ndi chiyani, iwe mwana wamkazi wa Yerusalemu? Kodi ndingakufanizire ndi yani kuti ndikutonthoze, iwe namwali wa Ziyoni? Chilonda chako ndi chozama ngati nyanja, kodi ndani angakuchiritse?
Oe Jerusalem canu nang teh, kai ni bangtelamaw na bangnue han. Bangmaw na panue sak han. Bangtelamaw na o ka ti han. Oe Zion canu tanglakacuem, nang na lungroum thai nahanlah kai ni bangtelamaw lung na pahawi han. Nang e na rawknae teh tuipui patetlah a kaw dawkvah, apinimaw nang teh na dam sak thai han.
14 Masomphenya a aneneri ako anali abodza ndi achabechabe. Iwo sanakupulumutse kuti usapite ku ukapolo poyika poyera mphulupulu zako. Mauthenga amene anakupatsa anali achabechabe ndi osocheretsa.
Nange profetnaw teh, dumyennae hoi payonnae vision hah nang hanelah a hmu awh teh, na onae dawk bout o sak hanelah, nange yonnae pâpho laipalah, huenghai onae pathunae hnonaw hoi nangmouh na dum awh teh, a pathang awh toe.
15 Onse oyenda mʼnjira yako akukuwombera mʼmanja; akugwedeza mitu yawo ndi kukunyodola iwe mwana wamkazi wa Yerusalemu: “Kodi mzinda uja ndi uwu umene unkatchedwa wokongola kotheratu, chimwemwe cha dziko lonse lapansi?”
Lam dawk ka cet kaawmnaw pueng ni, kut na tabawng sin awh teh, na kayasak awh. A lû a kahek awh teh, talai van pueng dawk e kanawm poung e teh, hete khopui maw telah Jerusalem canu hah ati awh.
16 Adani ako onse akutsekulira pakamwa ndi kukunyoza; iwo akunyogodola ndi kukukuta mano awo, ndipo akuti, “Tamumeza. Tsiku ili ndi lomwe timayembekezera; tili ndi moyo kuti tilione.”
Na tarannaw pueng ni nang koe lah pahni a ang awh teh, a hâ cakkarue teh, maimanaw hah na payawp toe. Hete hnin teh maimouh ni ring e hnin doeh, maimouh ni hmu awh toe ati awh.
17 Yehova wachita chimene anakonzeratu; wakwaniritsa mawu ake, amene anatsimikiza kale lomwe. Wakuwononga mopanda chifundo, walola mdani kuti akondwere chifukwa cha kugwa kwako, wakweza mphamvu za adani ako.
BAWIPA ni a noe tangcoung e hno hah a sak toe. Ayan hoi ka ti han ati e a lawk hah a kuep sak toe. Pahrennae awm laipalah, a raphoe toe. Taran teh nang dawkvah, a lunghawi sak teh taran e a ki teh a ouphlawp toe.
18 Mitima ya anthu ikufuwulira Ambuye. Iwe khoma la mwana wamkazi wa Ziyoni, misozi yako itsike ngati mtsinje usana ndi usiku; usadzipatse wekha mpumulo, maso ako asaleke kukhetsa misozi.
Ahnimouh teh a lungthin thung hoi Bawipa koe a hramki awh. Oe Zion canu e rapan, nange mitphi teh, palang tui ka lawng e patetlah karum khodai pout laipalah lawng naseh. Nama hai kâhat hanh. Na mit hai kâhat sak hanh.
19 Dzuka, fuwula usiku, pamene alonda ayamba kulondera; khuthula mtima wako ngati madzi pamaso pa Ambuye. Kweza manja ako kwa Iye chifukwa cha miyoyo ya ana ako, amene akukomoka ndi njala mʼmisewu yonse ya mu mzinda.
Karumsaning hai thaw nateh, hram haw. Bawipa e a hmalah, na lungthin teh, tui patetlah rabawk haw. Lam tangkuem vah a vawn ka hlam niteh, sut ka yan e camonaw a lungngai kuep thai nahanelah, na kut hah ahnimouh koe lah dâw haw.
20 Inu Yehova, onani, ndipo ganizirani: kodi ndani amene mwamuchitirapo zinthu ngati izi? Kodi amayi adye ana awo, amene amawasamalira? Kodi ansembe ndi aneneri awaphere mʼmalo opatulika a Ambuye?
Oe BAWIPA, apimaw hettelah ka tet e hah, khen nateh pouk haw. Napuinaw ni ama ni a cun e camonaw hah a ca han namaw. Vaihmanaw hoi profetnaw teh BAWIPA e a thoungnae hmuen dawkvah, thei awh han na maw.
21 Anyamata ndi okalamba aligone pamodzi pa fumbi la mʼmisewu ya mu mzinda; anyamata anga ndi anamwali anga aphedwa ndi lupanga. Inu Yehova mwawapha pa tsiku la mkwiyo wanu; mwawapha mopanda chifundo.
Camo hoi matawngnaw teh talai dawk a kamlei awh toe. Kaie tami, thoundoun tanglakacuemnaw hai tahloi hoi koung a kamlei toe. Na lungkhueknae hnin dawk ahnimouh teh pahren laipalah na thei teh koung na raphoe toe.
22 Ngati momwe mumayitanira pa tsiku la phwando, chimodzimodzinso mwandiyitanira zoopsa mbali zonse. Pa tsiku limene Yehova wakwiya palibe amene angathawe ndi kukhala ndi moyo; mdani wanga wawononga onse amene ndinkawasamala ndi kuwalera.
Pawi hnin dawk coun e patetlah tengpam pueng vah kai ni ka taki e hno hah na coun toe. BAWIPA lungkhueknae hnin dawk ka hlout ni teh kahring e tami ni buet touh hai awm hoeh. Ka kawkhik e camonaw patenghai ka tarannaw ni koung a raphoe toe.