< Maliro 1 >

1 Haa! Mzinda uja wasiyidwa wokhawokha, umene kale unali wodzaza ndi anthu! Kale unali wotchuka pakati pa mitundu ya anthu! Tsopano wasanduka ngati mkazi wamasiye. Kale unali mfumukazi ya onse pa dziko lapansi, tsopano wasanduka kapolo.
Pakomuta! Fuka mukela lun Jerusalem, su sie pacl ah sessesla ke mwet. Sie pacl ah akfulatyeyuk el sin faclu nufon, a inge el supwar oana sie katinmas. Meet el arulana fulat, a inge el putatyang nu in moul in mwet kohs.
2 Ukulira mowawidwa mtima usiku wonse, misozi ili pa masaya pake. Mwa abwenzi ake onse, palibe ndi mmodzi yemwe womutonthoza. Abwenzi ake onse amuchitira chiwembu; onse akhala adani ake.
El tung ke fong nufon, ac sroninmutal sorori ke likintupal. Inmasrlon mwet kawuk lal meet ah nufon, tiana sie lula in akwoyal. Mwet asruoki nu sel meet ah sisella, ac inge elos nukewa lainul.
3 Yuda watengedwa ku ukapolo, kukazunzika ndi kukagwira ntchito yolemetsa. Iye akukhala pakati pa anthu a mitundu ina; ndipo alibe malo opumulira. Onse omuthamangitsa iye amupitirira, ndipo alibe kwina kothawira.
Mwet Judah elos mwet kohs ke sripen lillilyak elos liki acn selos. Elos muta in facl saya, ac wangin acn elos in pangon acn selos sifacna. Mwet lokoalok lalos raunelosla, ac wangin innek in kaingla lalos.
4 Misewu yopita ku Ziyoni ikulira, chifukwa palibe ndi mmodzi yemwe akubwera ku maphwando ake. Zipata zake zonse zili pululu, ansembe akubuwula. Anamwali ake akulira, ndipo ali mʼmasautso woopsa.
Wanginla mwet tuku nu ke Tempul in pacl inge in tuh alu ke len mutal. Tulik mutan su tuh alullul we elos muta in keok, ac mwet tol elos sasao na. Mutunpot in siti uh oalallana, ac acn Zion oan in ongoiya lulap.
5 Adani ake asanduka mabwana ake; odana naye akupeza bwino. Yehova wamubweretsera mavuto chifukwa cha machimo ake ambiri. Ana ake atengedwa ukapolo pamaso pa mdani.
Mwet lokoalok lal elos kutangulla, ac el oan ye ku lalos. LEUM GOD El oru elan keok ke sripen ma koluk puspis lal. Tulik natul uh sruoh ac utukla lukel.
6 Ulemerero wonse wa mwana wamkazi wa Ziyoni wachokeratu. Akalonga ake ali ngati mbawala zosowa msipu; alibe mphamvu zothawira owathamangitsa.
Wolana lun Jerusalem wanginla, Mwet kol lalos elos oana deer ma munasla ke masrinsral, Su apkuran in wanginla ku la ke elos kaingkin mwet ma ukwalos uh.
7 Pa masiku a masautso ndi kuzunzika kwake, Yerusalemu amakumbukira chuma chonse chimene mʼmasiku amakedzana chinali chake. Anthu ake atagwidwa ndi adani ake, panalibe aliyense womuthandiza. Adani ake ankamuyangʼana ndi kumuseka chifukwa cha kuwonongeka kwake.
Ke Jerusalem el musalla ac mukaimtalla in pacl inge, el esamak ma nukewa ma wo nu sel meet ah. Ke el putatyang nu inpoun mwet lokoalok lal, wangin sie acn ku in kasrel mweuni mwet lokoalok lal. Mwet kutangulla uh isrunul ke el ikori.
8 Yerusalemu wachimwa kwambiri ndipo potero wakhala wodetsedwa. Onse amene ankamulemekeza pano akumunyoza, chifukwa aona umaliseche wake. Iye mwini akubuwula ndipo akubisa nkhope yake.
Wanginla sunakinyal; el koflufolla, ac sununteiyuk el. El sao ac wikin mutal ke mwekin. Jerusalem el aktaekyal sifacna ke ma koluk lulap lal.
9 Uve wake umaonekera pa zovala zake; iye sanaganizire za tsogolo lake. Nʼchifukwa chake kugwa kwake kunali kwakukulu; ndipo analibe womutonthoza. “Inu Yehova, taonani masautso anga, pakuti mdani wapambana.”
Ma fohkfok lal arulana mohtotla, tusruktu wanginna nunkeyen ma ac sikyak uh sel. Ikori lal ah arulana koluk, ac wangin sie mwet ku in akwoyal. Mwet lokoalok lal elos kutangla, ac el wowoyak nu sin LEUM GOD ac siyuk ke pakoten lal.
10 Adani amulanda chuma chake chonse; iye anaona mitundu ya anthu achikunja ikulowa mʼmalo ake opatulika, amene Inu Mulungu munawaletsa kulowa mu msonkhano wanu.
Mwet lokoalok lal elos pisrala ma saok lal nukewa. El sifacna liye ke elos utyak nu in Tempul, Yen LEUM GOD El tia lela mwet pegan in utyak nu we.
11 Anthu ake onse akubuwula pamene akufunafuna chakudya; asinthanitsa chuma chawo ndi chakudya kuti akhale ndi moyo. “Inu Yehova, taonani ndipo ganizirani, chifukwa ine ndanyozeka.”
Mwet lal elos sasao ke sukyen ma elos in kang; Elos sang ma saok lalos ayaol mwe mongo in sruokya moul lalos. Ac siti uh wowoyak ac fahk, “Liyeyu, LEUM GOD. Liyeyu in keok luk.”
12 “Kodi zimenezi mukuziyesa zachabe, inu nonse mukudutsa? Yangʼanani ndipo muone. Kodi pali mavuto ofanana ndi amene andigwerawa, amene Ambuye anandibweretsera pa tsiku la ukali wake?
El pang nu selos nukewa su fufahsryesr yen el muta we, ac fahk, “Ngetma liyeyu! Wangin sie mwet nu pulakin waiok oana nga, Waiok su ma LEUM GOD El use nu fuk in pacl in kasrkusrak lal.
13 “Anatumiza moto kuchokera kumwamba, unalowa mpaka mʼmafupa anga. Anayala ukonde kuti ukole mapazi anga ndipo anandibweza. Anandisiya wopanda chilichonse, wolefuka tsiku lonse.
“El supwama e lucng me, sie e su firirrir in nga. El filiya sie kwasrip nu sik ac sisyuwi nu infohk uh. Na El sisyula ac likiyuwi in mutana in waiok luk.
14 “Wazindikira machimo anga onse ndipo ndi manja ake anawaluka pamodzi. Machimowa afika pakhosi panga, ndipo Ambuye wandithetsa mphamvu. Iye wandipereka kwa anthu amene sindingalimbane nawo.
“El tuni ma koluk luk nukewa ac kapsreni nu sie; El sripisrya ke kwawuk, ac nga munasla ke toasriya uh. Leum El eisyuyang nu sin mwet lokoalok luk, ac wangin ma nga ku in oru in lainulos.
15 “Ambuye wakana anthu anga onse amphamvu omwe ankakhala nane: wasonkhanitsa gulu lankhondo kuti lilimbane nane, kuti litekedze anyamata anga; mʼmalo ofinyira mphesa Ambuye wapondereza anamwali a Yuda.
“Leum El isrun mwet mweun fokoko luk nukewa; El supwama sie un mwet mweun in tuh kunausla mwet fusr luk. El itungya mwet luk oana grape ke nien fut wain.
16 “Chifukwa cha zimenezi ndikulira ndipo maso anga adzaza ndi misozi. Palibe aliyense pafupi woti anditonthoze, palibe aliyense wondilimbitsa mtima. Ana anga ali okhaokha chifukwa mdani watigonjetsa.
“Pa inge sripa se oru sroninmutuk kahkkakla uh. Wangin mwet ku in akwoyeyula; wangin mwet ku in akkeyeyu. Mwet lokoalok luk kutangyula; wangin kutena ma lula lun mwet luk.
17 “Ziyoni wakweza manja ake, koma palibe aliyense womutonthoza. Yehova walamula kuti abale ake a Yakobo akhale adani ake; Yerusalemu wasanduka chinthu chodetsedwa pakati pawo.
“Nga asroela pouk, tuh wangin mwet in kasreyu. LEUM GOD El pangon mwet lokoalok liki acn nukewa in lainyu. Elos oreyu oana sie ma na olafohkfok.
18 “Yehova ndi wolungama, koma ndine ndinawukira malamulo ake. Imvani inu anthu a mitundu yonse; onani masautso anga. Anyamata ndi anamwali anga agwidwa ukapolo.
“Tusruktu suwohs ma LEUM GOD El oru, mweyen nga tuh tia aksol. Porongeyu, kowos mwet yen nukewa; ngetma liyeyu in waiok luk. Mukul fusr ac mutan fusr luk elos utukla nu in sruoh.
19 “Ndinayitana abwenzi anga koma anandinyenga. Ansembe ndi akuluakulu anga anafa mu mzinda pamene ankafunafuna chakudya kuti akhale ndi moyo.
“Nga pang nu sin mwet ma asruoki nu sik, tuh elos srunga kasreyu. Mwet tol ac mwet kol elos misa fin inkanek in siti uh Ke elos sukok mongo in sruokya moul lalos sifacna.
20 “Inu Yehova, onani mmene ine ndavutikira! Ndikuzunzika mʼkati mwanga, ndipo mu mtima mwanga ndasautsidwa chifukwa ndakhala osamvera. Mʼmisewu anthu akuphedwa, ndipo ku mudzi kuli imfa yokhayokha.
“O LEUM GOD, ngetma liye keok lulap lun ngunik! Insiuk arulana musalla ke asroeyen ma koluk luk. Oasr akmas orek ke inkanek uh; finne in lohm uh oasr pac misa.
21 “Anthu amva kubuwula kwanga, koma palibe wonditonthoza. Adani anga onse amva masautso anga; iwo akusangalala pa zimene Inu mwachita. Lifikitseni tsiku limene munalonjeza lija kuti iwonso adzakhale ngati ine.
“Porongo sasao luk; wanginna mwet in akwoyeyu. Mwet lokoalok luk elos engan lah kom ase ongoiya nu sik. Tari supwama len se ma kom tuh wulema kac ah; oru mwet lokoalok luk in keok oapana nga.
22 “Lolani kuti ntchito zawo zoyipa zifike pamaso panu; muwalange ngati mmene mwandilangira ine chifukwa cha machimo anga onse. Ndikubuwula kwambiri ndipo mtima wanga walefuka.”
“Sang mwatalos ke ma koluk lalos nukewa. Kalyaelos oana ke kom tuh kalyeiyu ke ma koluk luk. Nga sasao in keok luk, ac insiuk musallana.”

< Maliro 1 >