< Oweruza 4 >
1 Ehudi atamwalira, Aisraeli anachitanso zinthu zoyipira Yehova.
Ehud a due hnukkhu hoi Isarelnaw ni Cathut hmalah hno kahawihoeh bout a sak awh.
2 Choncho Yehova anawapereka mʼmanja mwa Yabini, mfumu ya ku Kanaani, imene inkalamulira ku Hazori. Mkulu wa ankhondo ake anali Sisera, amene ankakhala ku Haroseti-Hagoyimu.
BAWIPA ni Kanaan ram Hazor kho dawk siangpahrang lah kaawm e Jabin koe a yo awh. A ransabawi teh Harosheth-hagoyim kaawm e Sisera doeh.
3 Aisraeli analira kwa Yehova kuti awathandize, chifukwa Sisera anali ndi magaleta achitsulo 900 ndipo anazunza Aisraeli mwankhanza kwa zaka makumi awiri.
Hahoi teh, Isarelnaw ni Bawipa koe kabawpnae a hei awh teh a kaw awh. Bangkongtetpawiteh, Jabin ni sumrangleng 900 touh a tawn. Isarelnaw teh kum 20 touh thung puenghoi a rektap awh.
4 Debora, mneneri wamkazi, mkazi wake wa Rapidoti ndiye ankatsogolera Israeli nthawi imeneyo.
Hatnae tueng dawkvah Lappidoth tami profet napui Deborah teh, Isarelnaw hah a uk.
5 Iye ankakhala pansi pa mtengo wa mgwalangwa wa Debora, pakati pa Rama ndi Beteli mʼdziko la ku mapiri la Efereimu, ndipo Aisraeli ankapita kwa iye kuti akaweruze milandu yawo.
Ephraim mon dawk e hmuen, Ramah hoi Bethel rahak kaawm koe Deborah teh samtue rahim vah a tahung teh, haw hoiyah Isarelnaw lawk ouk a ceng.
6 Debora uja anatuma munthu kuti akayitane Baraki mwana wa Abinoamu wa ku Kedesi mʼdziko la Nafutali ndipo anati kwa iye, “Yehova Mulungu wa Israeli akukulamula iwe kuti, ‘Pita kasonkhanitse anthu ku phiri la Tabori. Ubwere nawo anthu 10,000 a fuko la Nafutali ndi a fuko la Zebuloni.
Tami a patoun teh, Abinoam capa Barak hah Naphtali ram Kedesh kho hoi a kaw teh, nang ni, Naphtali miphun, Zebulun miphun dawk e tami 10, 000 touh Tabor mon koe pâkhueng awh.
7 Ine ndidzakokera Sisera mkulu wa ankhondo a Yabini pamodzi ndi magaleta ake ndi asilikali ake kwa inu ku mtsinje wa Kisoni ndipo ndidzamupereka mʼmanja mwanu.’”
Jabin ransabawi kalenpounge Sisera teh a marangnaw, a kaw e naw khuehoi nang na dawn hanelah, Kishion tui teng vah ka hrawi vaiteh, ahni teh na kut dawk na poe han telah, Isarelnaw e BAWIPA Cathut ni lawk na thui atipouh.
8 Baraki anamuyankha kuti, “Mukapita nane limodzi ine ndipita. Koma ngati sitipitira limodzi, inenso sindipita.”
Hahoi Barak ni ahnimouh koe, na cetkhai pawiteh ka cei van han, na cet hoehpawiteh ka cet van mahoeh atipouh.
9 Debora anati, “Chabwino, ine ndipita nawe limodzi. Koma mudziwe kuti inu simudzalandirapo ulemu pa zimene mwachitazi popeza Yehova wapereka Sisera mʼmanja mwa munthu wamkazi.” Choncho Debora ananyamuka kupita ku Kedesi pamodzi ndi Baraki.
Hahoi ahnimouh ni, na ceikhai roeroe han. Hatei na ceinae lamthung ni nama teh minhmai kahawi na hmawt mahoeh. Bangkongtetpawiteh, BAWIPA ni Sisera teh napui buet touh e kut dawk a yo han telah ati. Hathnukkhu, a thaw teh, Barak hoi Kedesh kholah a cei.
10 Baraki anayitana mafuko a Zebuloni ndi Nafutali kuti abwere ku Kedesi. Anthu 10,000 anamutsatira, ndipo Debora anapita naye pamodzi.
Barak ni Zebulun hoi Naphtali hah Kedesh vah a kaw teh, tami 10, 000 touh a cei teh Deborah hai a kâbang van.
11 Nthawi imeneyo nʼkuti Mkeni wina dzina lake Heberi atalekana ndi Akeni anzake, zidzukulu za Hobabu, mlamu wa Mose, nakamanga tenti yake pafupi ndi mtengo wa thundu ku Zananimu pafupi ndi Kedesi.
Ken miphun Heber teh, Mosi e a masei napui Hobab e catoun, Ken miphunnaw hoi a kampek awh teh Kedesh teng, Zaanannim kaawm e kathen kung koe, rim a sak teh ao awh.
12 Pamene Sisera anamva kuti Baraki mwana wa Abinoamu wapita ku phiri la Tabori,
Abinoam capa Barak teh, Tabor mon dawk a luen tie Sisera koe a dei pouh toteh,
13 anasonkhanitsa magaleta ake achitsulo 900 ndi anthu onse amene anali naye ndipo anachoka ku Haroseti-Hagoyimu kupita ku mtsinje wa Kisoni.
Sisera ni marang a tawn e naw hoi, a tawn e sumrangleng 900 touh hoi Harosheth-hagoyim hoi Kishion palang totouh a taminaw a pâkhueng.
14 Debora anawuza Baraki kuti, “Dzukani! Paja ndi lero limene Yehova wapereka Sisera mʼmanja mwako. Kodi Yehova sanakhale akukutsogolerani?” Choncho Baraki anatsika phiri la Tabori, anthu 10,000 akumutsata.
Deborah ni Barak teh, thaw haw, Sisera teh BAWIPA ni na kut dawk poenae hnin a pha toe. BAWIPA teh na hmalah yo a cei toe vaiyaw telah atipouh. Barak ni Tabor mon dawk hoi a hnukkâbang tami 10, 000 touh hoi a cathuk sin.
15 Yehova anasokoneza Sisera ndi magaleta ake pamodzi ndi ankhondo ake onse. Baraki ndi anthu ake anawapirikitsa ndipo Sisera anatsika pa galeta yake nayamba kuthawa pansi.
Hahoi, BAWIPA ni Sisera hoi a marangnaw hoi a ransanaw pueng teh, Barak hmalah koung a thei pouh. Sisera ma teh, amae rangleng dawk hoi a kum teh, a khok hoi a yawng.
16 Baraki analondola magaletawo pamodzi ndi ankhondo onse mpaka ku Haroseti-Hagoyimu, ndipo ankhondo onse a Sisera anaphedwa ndi lupanga. Palibe munthu ndi mmodzi yemwe anatsala.
Hahoi Barak ni rangleng hoi ransanaw hoi Harosheth-hagoyim kho totouh a pâlei teh, Sisera ransanaw pueng teh tahloi hoi he a thei awh. Buet touh boehai hlout a hoeh.
17 Komabe Sisera anathawa pansi mpaka anakafika ku tenti ya Yaeli mkazi wa Heberi Mkeni uja, chifukwa panali mtendere pakati pa Yabini mfumu ya Hazori ndi banja la Heberi, Mkeni uja.
Hateiteh, Sisera teh a khok hoi Ken tami Hiber e yu Jael e rim dawk a yawng. Bangkongtetpawiteh, Hazor siangpahrang Jabin hoi Ken tami Haber rim imthungkhunaw hoi a kâhuiko awh.
18 Yaeli anatuluka kukachingamira Sisera ndipo anati, “Bwerani mbuye wanga, lowani momwemo musaope.” Choncho analowa mʼtenti muja, ndipo anamufunditsa chofunda.
Jael ni Sisera kâhmo hanlah a tâco teh, bawipa kâen leih, kai koe kâenh, taket hanh atipouh. A rim thung a kâen sak teh, hni hai a khu.
19 Anati, “Ndili ndi ludzu, chonde patseniko madzi pangʼono akumwa, ndili ndi ludzu.” Mkaziyo anatsekula thumba la chikopa mmene munali mkaka, namupatsa kuti amwe, ndipo anamufunditsanso.
Hahoi ahni ni, pahren lahoi tui nei hane na poe haw, tui kahran poung atipouh. Hateh, napui ni, maito sanu bom a paawng teh a nei sak hnukkhu hni bout a khu.
20 Kenaka anawuza mkaziyo kuti, “Muyime pa khomo la tentili, ndipo munthu wina akabwera kudzakufunsani kuti, ‘Kodi kwafika munthu wina kuno?’ Inu muyankha kuti, ‘Ayi.’”
Hahoi ahni ni, tho koe kangdout nateh tami buetbuet touh ni tongpa hah ao maw telah na pacei pawiteh, awm hoeh telah tet pouh lah a, atipouh.
21 Koma Yaeli mkazi wa Heberi, anatenga chikhomo cha tenti ndi hamara ndi kupita mwakachetechete kwa Sisera uja. Tsono Sisera ali mtulo chifukwa chotopa, mkazi uja anamukhomera chikhomo chija mʼmutu mwake. Chinatulukira kwinaku mpaka kulowa mʼnthaka, ndipo anafa pomwepo.
Hatei, Haber e a yu Jael ni rim a hetnae cawt hoi cakkin a la teh, ngawt a tawn dawk a i lahun nah, arulahoi duem a cei sin teh, a hnâlakheng dawk pawk a het pouh teh, talai dawk moncawm a um, hateh a due.
22 Baraki atafika akulondola Sisera, Yaeli anatuluka kukamuchingamira namuwuza kuti, “Lowani mudzaone munthu amene mukumufunafuna.” Tsono atalowa anangoona Sisera ali thapsa pansi wakufa ndi chikhomo chili mʼmutu mwake.
Khenhaw! Barak ni Sisera a pâlei navah, Jael ni kâhmo hanlah a tâco sin teh, tho leih, na tawng e tami teh na patue han atipouh teh, Barak rim thung a kâen navah, Sisera teh a hnâlakheng dawk cawt hoi pawk kâpâcue lah ao e hah a hmu.
23 “Choncho pa tsiku limenelo Mulungu anagonjetsa Yabini mfumu ya Akanaani, pamaso pa Aisraeli.
Hat hnin vah, BAWIPA ni Kanaan siangpahrang Jabin teh, Isarelnaw hmalah a sung sak.
24 Ndipo Aisraeli anapanikizabe Yabini, mfumu ya Akanaani, mpaka kumuwonongeratu.
Isarelnaw teh a tha hoehoe ao awh teh, a hnukteng vah Kanaan siangpahrang Jabin hah a raphoe awh.