< Oweruza 20 >

1 Ndipo Aisraeli onse kuyambira ku dziko la Dani mpaka ku Beeriseba ndiponso ku dziko la Giliyadi ananyamuka ngati munthu mmodzi nakasonkhana pamaso pa Yehova ku Mizipa.
and to come out: come all son: descendant/people Israel and to gather [the] congregation like/as man one to/for from Dan and till Beersheba Beersheba and land: country/planet [the] Gilead to(wards) LORD [the] Mizpah
2 Atsogoleri a anthu onse ndi a mafuko onse Aisraeli anali nawo pa msonkhano wa anthu a Mulungu. Onse pamodzi analipo asilikali oyenda pansi 400,000 atanyamula malupanga.
and to stand corner all [the] people all tribe Israel in/on/with assembly people [the] God four hundred thousand man on foot to draw sword
3 Anthu a fuko la Benjamini anali atamva kuti Aisraeli apita ku Mizipa. Tsono Aisraeli anati, “Tiwuzeni, zinthu zoyipa izi zinachitika bwanji.”
and to hear: hear son: descendant/people Benjamin for to ascend: rise son: descendant/people Israel [the] Mizpah and to say son: descendant/people Israel to speak: speak how? to be [the] distress: evil [the] this
4 Choncho Mlevi uja, mwamuna wa mkazi wophedwa uja anayankha nati, “Ine ndinapita ku Gibeya mʼdziko la Benjamini pamodzi ndi mzikazi wanga kuti tikagone kumeneko.
and to answer [the] man [the] Levi man: husband [the] woman [the] to murder and to say [the] Gibeah [to] which to/for Benjamin to come (in): come I and concubine my to/for to lodge
5 Usiku anthu a ku Gibeya anandiwukira, nazinga nyumba munali ine. Ankafuna kundipha ndipo anagona ndi mzikazi wanga momukakamiza mpaka anafa.
and to arise: rise upon me master [the] Gibeah and to turn: surround upon me [obj] [the] house: home night [obj] me to resemble to/for to kill and [obj] concubine my to afflict and to die
6 Ine ndinatenga mzikazi wangayo ndi kumudula nthulinthuli ndikuzitumiza kwa fuko lililonse la Aisraeli. Anthu amenewa, zedi achita chinthu chonyansa kwambiri mʼdziko lino la Israeli.
and to grasp in/on/with concubine my and to cut her and to send: depart her in/on/with all land: country inheritance Israel for to make: do wickedness and folly in/on/with Israel
7 Ndi zimenezotu inu Aisraeli nonse; yankhulaponi mawu ndi kupereka maganizo anu.”
behold all your son: descendant/people Israel to give to/for you word and counsel here
8 Anthu onse anayimirira ngati munthu mmodzi nanena kuti, “Palibe mmodzi wa ife amene apite ku nyumba kwake. Palibe amene abwerere ku nyumba kwake.
and to arise: rise all [the] people like/as man one to/for to say not to go: went man: anyone to/for tent his and not to turn aside: depart man: anyone to/for house: home his
9 Koma tsopano chimene ife tichite ndi dziko la Gibeya ndi ichi: Tidzapita kukamenyana nawo potsatira zimene maere anene.
and now this [the] word: thing which to make: do to/for Gibeah upon her in/on/with allotted
10 Mʼmafuko onse a Aisraeli tidzasankha anthu khumi pa anthu 100 aliwonse: ndiye kuti anthu 100 pa anthu 1,000 aliwonse kapena anthu 1,000 pa anthu 10,000 aliwonse. Anthu amenewa adzasonkhanitsa zakudya za ankhondo, ndipo ankhondowo adzapita kukalipsira anthu a ku Geba mʼdziko la Benjamini chifukwa chochita chinthu chonyansa chotere mʼdziko la Israeli.”
and to take: take ten human to/for hundred to/for all tribe Israel and hundred to/for thousand and thousand to/for myriad to/for to take: bring provision to/for people: soldiers to/for to make: do to/for to come (in): come them to/for Gibeah Benjamin like/as all [the] folly which to make: do in/on/with Israel
11 Choncho anthu a ku Israeli anasonkhana pamodzi nagwirizana chimodzi, kukalimbana ndi mzindawo.
and to gather all man Israel to(wards) [the] city like/as man one companion
12 Mafuko a Israeli anatumiza anthu kwa fuko lonse la Benjamini kukafunsa kuti, “Kodi zoyipa zachitika pakati panuzi ndi zotani?
and to send: depart tribe Israel human in/on/with all tribe Benjamin to/for to say what? [the] distress: evil [the] this which to be in/on/with you
13 Tsono tikuti mutipatse anthu achabechabe a ku Gibeya kuti tiwaphe kuti tichotse chinthu choyipachi mʼdziko la Israeli.” Koma fuko la Benjamini silinafune kumvera zimene ananena Aisraeli anzawo.
and now to give: give [obj] [the] human son: type of Belial which in/on/with Gibeah and to die them and to burn: purge distress: evil from Israel and not (be willing son: descendant/people *Q(K)*) Benjamin to/for to hear: hear in/on/with voice brother: compatriot their son: descendant/people Israel
14 Mʼmalo mwake, Abenjaminiwo anatuluka mʼmizinda yawo ku Gibeya kukamenyana ndi Aisraeli.
and to gather son: descendant/people Benjamin from [the] city [the] Gibeah [to] to/for to come out: come to/for battle with son: descendant/people Israel
15 Tsiku limenelo Abenjamini anasonkhanitsa kuchokera ku mizinda yawo ankhondo 26,000 amalupanga awo, osawerengera anthu ena 700 a ku Gibeya amene anasankhidwa.
and to reckon: list son: descendant/people Benjamin in/on/with day [the] he/she/it from [the] city twenty and six thousand man to draw sword to/for alone: besides from to dwell [the] Gibeah to reckon: list seven hundred man to choose
16 Mwa onsewa panali ankhondo 70 amanzere amene aliyense anali wodziwa kulasa ngakhale tsitsi limodzi ndi mwala osaphonya.
from all [the] people: soldiers [the] this seven hundred man to choose lefthanded hand right his all this to sling in/on/with stone to(wards) [the] hair and not to sin
17 Aisraeli, kupatula fuko la Benjamini, anasonkhanitsa anthu 400,000 a malupanga, onse odziwa bwino nkhondo.
and man Israel to reckon: list to/for alone: besides from Benjamin four hundred thousand man to draw sword all this man battle
18 Ndipo Aisraeli ananyamuka kupita ku Beteli kukafunsira kwa Mulungu. Iwo anati, “Ndani mwa ife amene angayambe kukamenyana ndi fuko la Benjamini?” Yehova anayankha kuti, “Fuko la Yuda ndilo liyambe.”
and to arise: rise and to ascend: rise Bethel Bethel and to ask in/on/with God and to say son: descendant/people Israel who? to ascend: rise to/for us in/on/with beginning to/for battle with son: descendant/people Benjamin and to say LORD Judah in/on/with beginning
19 Mmawa mwake Israeli ananyamuka nakamanga msasa moyangʼanana ndi Gibeya.
and to arise: rise son: descendant/people Israel in/on/with morning and to camp upon [the] Gibeah
20 Aisraeli anapita kukachita nkhondo ndi fuko la Benjamini ndipo anandandalika ankhondo awo moyangʼanana ndi Gibeya.
and to come out: come man Israel to/for battle with Benjamin and to arrange with them man Israel battle to(wards) [the] Gibeah
21 A fuko la Benjamini anatuluka ku Gibeya ndipo tsiku limenelo anapha Aisraeli 22,000 ku nkhondoko.
and to come out: come son: descendant/people Benjamin from [the] Gibeah and to ruin in/on/with Israel in/on/with day [the] he/she/it two and twenty thousand man land: soil [to]
22 Koma ankhondo a Israeli analimbikitsananso mtima ndipo anasonkhanitsanso kachiwiri ankhondo awo pa malo pamene anawandandalika poyamba paja.
and to strengthen: strengthen [the] people: soldiers man Israel and to add: again to/for to arrange battle in/on/with place which to arrange there in/on/with day [the] first
23 Aisraeli anapita kukalira pamaso pa Yehova mpaka madzulo. Iwo anafunsa Yehova kuti, “Kodi tipitenso kukamenyana ndi a fuko la Benjamini abale athu?” Yehova anayankha kuti, “Pitani mukalimbane nawo.”
and to ascend: rise son: descendant/people Israel and to weep to/for face: before LORD till [the] evening and to ask in/on/with LORD to/for to say to add: again to/for to approach: approach to/for battle with son: descendant/people Benjamin brother: compatriot my and to say LORD to ascend: rise to(wards) him
24 Ndipo Aisraeli anayandikiranso pafupi ndi fuko la Benjamini tsiku lachiwiri lake kuti amenyane nawo.
and to present: come son: descendant/people Israel to(wards) son: descendant/people Benjamin in/on/with day [the] second
25 Pa tsiku lachiwiri lomwelo Abenjamini anatulukanso mu mzinda wa Gibeya ndipo anaphanso ankhondo 18,000. Onse amene anawaphawo anali odziwa kugwiritsa ntchito bwino malupanga.
and to come out: come Benjamin to/for to encounter: toward them from [the] Gibeah in/on/with day [the] second and to ruin in/on/with son: descendant/people Israel still eight ten thousand man land: soil [to] all these to draw sword
26 Tsono Aisraeli onse, gulu lonse la ankhondo, anapita ku Beteli kukalira pamaso pa Yehova. Anakhala pansi nasala zakudya tsiku lonse mpaka madzulo. Anapereka nsembe zopsereza ndi nsembe zachiyanjano pamaso pa Yehova.
and to ascend: rise all son: descendant/people Israel and all [the] people: soldiers and to come (in): come Bethel Bethel and to weep and to dwell there to/for face: before LORD and to fast in/on/with day [the] he/she/it till [the] evening and to ascend: offer up burnt offering and peace offering to/for face: before LORD
27 Bokosi la Chipangano cha Yehova linali kumeneko.
and to ask son: descendant/people Israel in/on/with LORD and there ark covenant [the] God in/on/with day [the] they(masc.)
28 Finehasi mwana wa Eliezara mwana wa Aaroni ndiye ankatumikira nthawi imeneyo. Tsono Aisraeli anafunsa Yehova kuti, “Kodi tipitenso kukachita nkhondo ndi mʼbale athu Abenjamini, kapena ayi?” Yehova anayankha kuti, “Pitaninso chifukwa mawa ndidzawapereka mʼmanja mwanu.”
and Phinehas son: child Eleazar son: child Aaron to stand: appoint to/for face: before his in/on/with day [the] they(masc.) to/for to say to add: again still to/for to come out: come to/for battle with son: descendant/people Benjamin brother: compatriot my if to cease and to say LORD to ascend: rise for tomorrow to give: give him in/on/with hand: power your
29 Choncho Aisraeli anayika anthu obisalira mozungulira Gibeya.
and to set: make Israel to ambush to(wards) [the] Gibeah around
30 Tsiku lachitatu anapita kukamenyana ndi Benjamini ndipo anayika ankhondo mʼmalo mwawo kuti amenyane ndi Gibeya monga anachitira poyamba.
and to ascend: rise son: descendant/people Israel to(wards) son: descendant/people Benjamin in/on/with day [the] third and to arrange to(wards) [the] Gibeah like/as beat in/on/with beat
31 Abenjamini anatuluka kukamenyana nawo anthuwo ndipo anapita kutali ndi mzindawo. Iwo anayamba kupha Aisraeli monga poyamba paja, kotero kuti anapha anthu pafupifupi makumi atatu. Mitembo ya ena inali mu misewu yayikulu yopita ku Beteli ndi ku Gibeya, ndipo ina inali kwina poyera.
and to come out: come son: descendant/people Benjamin to/for to encounter: toward [the] people: soldiers to tear from [the] city and to profane/begin: begin to/for to smite from [the] people: soldiers slain: killed like/as beat in/on/with beat in/on/with highway which one to ascend: rise Bethel Bethel and one Gibeah [to] in/on/with land: country like/as thirty man in/on/with Israel
32 Abenjamini ankanena kuti, “Tikuwagonjetsa monga poyamba.” Koma Aisraeli ankanena kuti, “Tiyeni tithawe kuti apite ku msewu chapatali ndi mzinda wawo.”
and to say son: descendant/people Benjamin to strike they(masc.) to/for face: before our like/as in/on/with first and son: descendant/people Israel to say to flee and to tear him from [the] city to(wards) [the] highway
33 Choncho Aisraeli onse anachoka mʼmalo mwawo ndi kukandanda ku Baala-Tamara, ndipo Aisraeli obisalira aja anatuluka mʼmalo awo kummawa kwa Geba.
and all man Israel to arise: rise from place his and to arrange in/on/with Baal-tamar Baal-tamar and to ambush Israel to burst/come out from place his from Maareh (Maareh)-geba
34 Aisraeli osankhidwa 10,000 ndiwo anabwera kudzalimbana ndi mzinda wa Gibeya. Nkhondoyo inafika poyipa kwambiri mwakuti Abenjamini samadziwa kuti zoopsa zili pafupi kuwagwera.
and to come (in): come from before to/for Gibeah ten thousand man to choose from all Israel and [the] battle to honor: heavy and they(masc.) not to know for to touch upon them [the] distress: harm
35 Tsono Yehova anagonjetsa Abenjamini pamaso pa Israeli motero kuti Aisraeli anapha ankhondo a Abenjamini 25,100 tsiku limenelo.
and to strike LORD [obj] Benjamin to/for face: before Israel and to ruin son: descendant/people Israel in/on/with Benjamin in/on/with day [the] he/she/it twenty and five thousand and hundred man all these to draw sword
36 Choncho Abenjamini anaona kuti agonjetsedwa. Paja Aisraeli anathawa fuko la Benjamini chifukwa ankadalira anthu amene anawayika kuti abisalire mzinda wa Gibeya.
and to see: see son: descendant/people Benjamin for to strike and to give: give man Israel place to/for Benjamin for to trust to(wards) [the] to ambush which to set: make to(wards) [the] Gibeah
37 Tsono anthu amene anabisala aja anachita changu kuwuthira nkhondo mzinda wa Gibeyawo. Ndipo anapha anthu onse a mu mzindawo ndi lupanga.
and [the] to ambush to hasten and to strip to(wards) [the] Gibeah and to draw [the] to ambush and to smite [obj] all [the] city to/for lip: edge sword
38 Chizindikiro chimene Aisraeli anapangana ndi anthu obisalira aja chinali chakuti obisalira aja akangofukiza utsi wambiri ngati mtambo mu mzindamo,
and [the] meeting: signal appointed to be to/for man Israel with [the] to ambush to multiply to/for to ascend: rise them tribute [the] smoke from [the] city
39 ndiye kuti Aisraeli enawo abwerere ku nkhondo. Pa nthawiyo nʼkuti Abenjamini atayamba kale kumenya Aisraeliwo kwambiri ndi kupha pafupifupi anthu makumi atatu. Ndipo iwo ankanena kuti, “Ndithu tawapha monga poyamba paja.”
and to overturn man Israel in/on/with battle and Benjamin to profane/begin: begin to/for to smite slain: killed in/on/with man Israel like/as thirty man for to say surely to strike to strike he/she/it to/for face: before our like/as battle [the] first
40 Koma pamene utsi wa chizindikiro uja unayamba kukwera tolotolo mmwamba kuchoka mu mzindamo, Abenjamini anayangʼana mʼmbuyo ndipo anangoona utsi mu mzinda onse uli tolotolo kukwera mmwamba.
and [the] tribute to profane/begin: begin to/for to ascend: rise from [the] city pillar smoke and to turn Benjamin after him and behold to ascend: rise entire [the] city [the] heaven [to]
41 Kenaka Aisraeli anabwerera ndipo Abenjamini anachita mantha, chifukwa anaona kuti zoopsa zili pafupi kuwagwera.
and man Israel to overturn and to dismay man Benjamin for to see: see for to touch upon him [the] distress: harm
42 Choncho anathawa pamaso pa Aisraeli kudzera njira ya ku chipululu, koma nkhondo inawapeza. Ndipo anaphedwa kumeneko ndi Aisraeli amene anachokera mu mzindamo.
and to turn to/for face: before man Israel to(wards) way: direction [the] wilderness and [the] battle to cleave him and which from [the] city to ruin [obj] him in/on/with midst his
43 Anawazungulira Abenjaminiwo, nawathamangitsa ndi kuwagonjetseratu osawachitira chifundo mpaka ku dera la kummawa kwa Gibeya.
to surround [obj] Benjamin to pursue him Nohah to tread him till before [the] Gibeah from east sun
44 Abenjamini 18,000 olimba mtima anaphedwa.
and to fall: kill from Benjamin eight ten thousand man [obj] all these human strength
45 Koma ena anatembenuka nathawira ku chipululu ku thanthwe la Rimoni. Mwa iwowa Aisraeli anapha Abenjamini 5,000 mʼmisewu yayikulu. Anawapitikitsabe Abenjaminiwo mpaka kufika ku Gidomu ndi kuphanso ena 2,000.
and to turn and to flee [the] wilderness [to] to(wards) crag [the] (Rock of) Rimmon and to glean him in/on/with highway five thousand man and to cleave after him till Gidom and to smite from him thousand man
46 Pa tsiku limenelo Abenjamini olimba mtima okhala ndi malupanga okwana 25,000 anafa.
and to be all [the] to fall: kill from Benjamin twenty and five thousand man to draw sword in/on/with day [the] he/she/it [obj] all these human strength
47 Koma anthu 700 anabwerera ndi kuthawira ku chipululu ku thanthwe la Rimoni kumene anakhalako miyezi inayi.
and to turn and to flee [the] wilderness [to] to(wards) crag [the] (Rock of) Rimmon six hundred man and to dwell in/on/with crag (Rock of) Rimmon four month
48 Aisraeli anabwerera kukamenyana ndi Abenjamini otsala ndi kuwapha ndi lupanga kuphatikizapo ziweto ndi zonse anali nazo. Ndipo anayatsa moto mizinda yonse anayipeza.
and man Israel to return: turn back to(wards) son: descendant/people Benjamin and to smite them to/for lip: edge sword from city soundness till animal till all [the] to find also all [the] city [the] to find to send: burn in/on/with fire

< Oweruza 20 >