< Oweruza 19 >

1 Pa nthawi imeneyo ku Israeli kunalibe mfumu. Mlevi wina ankakhala kutali ku dziko lamapiri la Efereimu. Iyeyu anatenga mzikazi wa ku Betelehemu, mʼdziko la Yuda.
В ония дни, когато нямаше цар в Израиля, имаше един левитин, който живееше на отвъдната страна на Ефремовата хълмиста земя, и който се беше взел наложница от Витлеем Юдов.
2 Tsiku lina mzikazi uja anakwiyira mwamuna wake ndipo anamuchokera kupita kwa abambo ake ku Betelehemu mʼdziko la Yuda. Anakakhala kumeneko miyezi inayi.
Но наложницата му блудствува против него, и отиде си от него в бащината си къща във Витлеем Юдов, гдето остана около четири месеца.
3 Mwamuna wake anamulondola kuti akayankhule naye mofatsa kumupempha kuti abwerere. Iye anali ndi antchito ake ndi abulu ake awiri. Anafika ku nyumba kwa mkazi uja ndipo iye anamulowetsa mʼnyumba ya abambo ake. Abambo aja atamuona mnyamata uja anamulandira mwachimwemwe.
И мъжът й стана та отиде подир нея, за да й говори любезно и да я върне, като водеше със себе си слугата си и два осела. И тя го въведе в бащината си къща; и когато го видя бащата на младата, посрещна го с радост.
4 Mpongozi wake, yemwe anali abambo a mtsikanayo, anamupempha kuti aswere. Choncho anakhalako masiku atatu. Ankadya, kumwa ndi kugona komweko.
И тъстът му, бащата на младата го задържа, та преседя с него три дена; и ядоха и пиха и пренощуваха там.
5 Tsiku lachinayi anadzuka mʼmamawa kukonzekera kuti azipita kwawo, koma abambo ake a mtsikanayo anawuza mkamwini wawo uja kuti, “Yambani mwadya chakudya, ndipo kenaka mutha kupita.”
На четвъртия ден, като станаха рано, той се дигна да си иде; но бащата на младата рече на зетя си: Подкрепи сърцето си с малко хляб и после ще си отидеш.
6 Choncho onse awiri anakhala pansi ndi kudya ndi kumwa pamodzi. Atadya, abambo a mtsikanayo anati, “Chonde mugonenso konkuno musangalale.”
И така, седнаха та ядоха и пиха двамата заедно; после бащата на младата рече на мъжа: Склони, моля, да пренощуваш, и нека се развесели сърцето ти.
7 Ndipo pamene mwamunayo anakonzeka kuti azipita, apongozi ake anamuwumirizanso kuti asapite. Choncho anagona komweko usiku umenewo.
Обаче, човекът се дигна да си иде; но понеже тъстът му настояваше пред него, той пак пренощува там.
8 Mmawa wa tsiku lachisanu, atadzuka kuti azipita abambo ake a mtsikanayo anamuwuza kuti, “Yambani mwadya chakudya ndipo mutandale mpaka madzulo.” Choncho awiriwo anadya pamodzi.
А на петия ден стана рано да си иде; но бащата на младата рече: Подкрепи, моля, сърцето си. И остана догдето превали денят, като ядоха двамата.
9 Pambuyo pake munthu uja pamodzi ndi mzikazi wake ndiponso mtumiki anakonzeka kuti azipita. Koma abambo a mtsikana uja anatinso kwa iye, “Onani tsopano kukuda. Gonani konkuno pakuti tsiku latha kale. Gonani ndipo musangalale. Mawa mudzuka mʼmamawa ndi kumapita kwanu.”
Сетне, когато човекът стана да си отиде - той и наложницата му и слугата му, рече тъстът му, бащата на младата: Ето, сега денят преваля към вечер; пренощувайте, моля. Ето, денят е на свършване; пренощувайте тук и нека се развесели сърцето ти; а утре тръгнете рано на път, за да отидеш у дома си.
10 Koma munthuyo sanafune kugonanso tsiku limenelo. Choncho ananyamuka kumapita, ndipo anakafika ku malo oyangʼanana ndi Yebusi (ndiye kuti Yerusalemu). Iyeyo anali atatenga abulu ake awiri okhala ndi zokhalira zake, ndipo mzikazi wake uja anali naye limodzi.
Но човекът не склони да пренощува, а като стана, тръгна и дойде срещу Евус (който е Ерусалим), като водеше със себе си два оседлани осела; и наложницата му беше с него.
11 Akuyandikira ku Yebusi nʼkuti kutada ndithu. Tsono mtumiki uja anawuza mbuye wake kuti, “Tiyeni, tipatukire ku mzinda wa Ayebusiwa ndipo tigone.”
Когато се приближиха до Евус, денят беше много преминал; и слугата рече на господаря си: Дойди, моля, нека се отбием в тоя град на евусите, за да пренощуваме в него.
12 Mbuye wake anamuyankha kuti, “Ayi, tisapatukire ku mzinda wa alendo, anthu amene sali Aisraeli. Koma tipitirire mpaka ku Gibeya.”
Но господарят му рече: Няма да се отбием в град на чужденци, гдето не се намират от израилтяните, но ще заминем за Гавая.
13 Tsono anamuwuza mtumiki wake uja kuti, “Tiye tipite ku amodzi a malo awa, ku Gibeya kapena ku Rama ndipo tikagone kumeneko.”
Рече още на слугата си: Дойди, нека се приближим до едно от тия места, и ще пренощуваме в Гавая или в Рама.
14 Choncho nayenda ulendo wawo, ndipo dzuwa linawalowera akuyandikira ku Gibeya mʼdziko la Benjamini.
И тъй, те заминаха та вървяха; а зайде им слънцето близо при Гавая, която принадлежи на Вениамина.
15 Ndipo anapatukira kumeneko kuti alowe mu mzinda wa Gibeya kukagona usiku umenewo. Anakalowa mu mzindamo ndi kukakhala pabwalo popeza panalibe munthu amene anawalandira ku nyumba kwake kuti akagone.
И там се отбиха, за да влязат да пренощуват в Гавая; и когато влезе, седна край градската улица, защото никой не ги прибираше в къщата си, за да пренощуват.
16 Pambuyo pake anangoona munthu wina wokalamba akuchokera ku ntchito ya ku munda kwake madzulo. Iyeyu anali wa ku dziko la mapiri ku Efereimu, koma ankakhala ku Gibeya. Koma anthu a kumeneko anali a fuko la Benjamini.
И, ето, един старец идеше вечерта от работата си на полето, и тоя човек беше от хълмистата земя на Ефрема и пришелствуваше в Гавая, а местните човеци бяха вениаминци.
17 Munthu wokalamba uja anakweza maso ndipo anaona munthu wa paulendo uja atakhala pabwalo la mzindawo, ndipo anamufunsa kuti, “Kodi mukupita kuti? Nanga mukuchokera kuti?”
И като подигна очи и видя пътника на градската улица, старецът му каза: Къде отиваш? и от где идеш?
18 Iye anayankha kuti, “Tikuchokera ku Betelehemu ku dziko la Yuda ndipo tikupita kutali ku dziko lamapiri la Efereimu kumene ndimakhala. Ndinapita ku Betelehemu mʼdziko la Yuda ndipo tsopano ndikubwerera kwathu. Koma palibe aliyense amene wanditengera ku nyumba yake.
А той му рече: Ние заминаваме от Витлеем Юдов към отвъдната страна на хълмистата земя на Ефрема, отдето съм аз. Ходих до Витлеем Юдов, и сега отивам за Господния дом; а никой не ме прибра в къщата си.
19 Tili ndi udzu ndi chakudya cha abulu athu. Tilinso ndi buledi ndi vinyo wokwanira ifeyo: ine, mdzakazi wanuyu, ndi mtumiki amene ali nafeyu. Palibe chimene tikusowa.”
А пък ние си имаме плява и храна за ослите си, също и хляб и вино за мене и за слугинята ти и за момчето, което е със слугите ти; нямаме нужда от нищо.
20 Munthu wokalambayo anati, “Mtendere ukhale nanu. Ine ndikuthandizani pa zosowa zanu zonse, koma musagone pabwalo usiku uno.”
И старецът рече: Бъди спокоен; обаче, всичките ти нужди нека понеса аз; само да не пренощуваш на улицата.
21 Choncho anapita nawo ku nyumba yake, ndipo anawapatsa abulu ake chakudya. Alendo aja anasamba mapazi awo, nalandira chakudya ndi chakumwa.
И така, той го въведе в къщата си, и даде зоб на ослите; а те си умиха нозете и ядоха и пиха.
22 Pamene ankadya mosangalala, anangoona anthu ena achabechabe a mu mzindawo azungulira nyumba ija nʼkumamenya chitseko. Tsono anawuza mwini nyumbayo, munthu wokalamba uja kuti, “Mutulutse munthu amene wabwera mʼnyumba yakoyu kuti tigone naye.”
Като веселяха сърцата си, ето, едни градски мъже, развратници, обиколиха къщата, блъскаха на вратата, и говориха на стареца домакин, казвайки: Изведи човека, който влезе в къщата ти, за да го познаем.
23 Koma mwini nyumba uja anatuluka ku bwalo nawawuza kuti, “Ayi, abale anga musachite zoyipa zotere. Popeza munthu uyu walowa mʼnyumba mwanga muno, musachite chinthu chonyansa chotere.
А човекът, то ест, домакинът, излезе при тях та им каза: Не, братя мои! моля, недейте прави това зло; тъй като тоя човек е мой гост, недейте струва това безумие.
24 Onani, pano pali mwana wanga wamkazi wosadziwa mwamuna pamodzi ndi mzikazi wa mlendoyu. Ndikutulutsirani amenewa tsopano ndipo atengeni ndi kuchita nawo chomwe chikukomerani. Koma musachite chinthu chonyansa ndi munthuyu.”
Ето дъщеря ми, девица, и неговата наложница; тях ще изведа вън сега; опозорете ги, и сторете им каквото ви е угодно; но на тоя човек да не сторите едно такова безумно дело.
25 Koma anthuwo sanafune kumumvera. Choncho mlendo uja anagwira mzikazi wake namutulutsa kuja kumene kunali iwo. Tsono iwowo anagona naye ndi kuchita naye zonyansa usiku wonse mpaka mmawa. Mʼbandakucha anamulola kuti apite.
Но мъжете не искаха да го послушат; за това, човекът взе наложницата му та им я изведе вън; и те я познаха и обезчестяваха я цялата нощ дори до утринта, а като се зазори пуснаха я.
26 Ndipo mmawa kukucha mzikazi uja anabwerera nakagwa pansi pa khomo pa nyumba imene mwamuna wake anali, ndipo anakhala pomwepo mpaka kunayera.
И тъй призори жената дойде и падна при вратата на къщата на човека, гдето беше господарят й, и там лежа до съмване.
27 Mwamuna wake anadzuka mʼmamawa, natsekula chitseko cha nyumba kuti atuluke ndi kumapita. Koma anangoona mzikazi wake uja ali thapsa pa khomo la nyumbayo, manja ake ali pa khonde.
И на утринта господарят й стана та отвори вратата на къщата и излезе, за да си отиде по пътя, и ето наложницата му паднала при врата на къщата, и ръцете й на прага.
28 Iye anati kwa mkaziyo, “Dzuka tizipita.” Koma sanayankhe kanthu. Kenaka anamukweza pa bulu wake ndipo ananyamuka kumapita kwawo.
И рече й: Стани да си отидем. Но нямаше отговор. Тогава човекът я дигна на осела, и стана та отиде на мястото си.
29 Atafika ku nyumba yake, anatenga mpeni, nagwira mzikazi wake uja ndi kuduladula thupi lake nthuli khumi ndi ziwiri. Kenaka anazitumiza ku zigawo zonse za Israeli.
И като дойде в дома си, взе нож, хвана наложницата си, и я разсече член по член на дванадесет части, и прати ги във всичките предели на Израиля.
30 Aliyense amene anaona zimenezi ankanena kuti, “Zoterezi sizinaonekepo kuyambira pamene Aisraeli anatuluka mʼdziko la Igupto mpaka lero lino. Ganizirani bwino chinthu chimenechi ndipo tiwuzeni zoyenera kuchita!”
И всички, които видяха това, думаха: Не е ставало, нито се е виждало такова нещо от деня, когато израилтяните излязоха из Египетската земя, до днес; размислете, прочее, затова, съветвайте се, и изказвайте се.

< Oweruza 19 >