< Oweruza 17 >

1 Munthu wina dzina lake Mika wochokera ku dziko la mapiri la Efereimu anawuza amayi ake kuti
Kwakukhona-ke umuntu wentabeni yakoEfrayimi, obizo lakhe lalinguMika.
2 “Ndinamva inu mukutemberera munthu amene anaba ndalama zanu zasiliva 1,100. Ndalamazo zili ndi ine, ndinatenga ndine.” Pamenepo amayi akewo anati, “Yehova akudalitse mwana wanga!”
Wasesithi kunina: Izinhlamvu zesiliva eziyinkulungwane lekhulu ezathathwa kuwe, owaqalekisa ngazo, njalo wakhuluma endlebeni zami, khangela, leyomali ikimi, mina ngayithatha. Unina wasesithi: Kawubusiswe eNkosini, ndodana yami.
3 Choncho Mika anabweza ndalama 1,100 za siliva kwa amayi ake, ndipo amayi akewo anati, “Ine ndapatulira Yehova ndalama za silivazi kuti mwana wanga aseme fano ndi kulikuta ndi siliva. Ndiye tsopano ndikubwezera ndalamazo.”
Wathi esezibuyisele kunina izinhlamvu eziyinkulungwane lekhulu zesiliva, unina wathi: Ngasengisehlukanisile lokusehlukanisela iNkosi isiliva sami sivela esandleni sami sibe ngesendodana yami, ukuze ngenze isithombe esibaziweyo lesithombe esibunjwe ngokuncibilikisa. Khathesi-ke ngizasibuyisela kuwe.
4 Tsono Mika atabweza ndalama zija kwa amayi ake, iwo anatengapo ndalama za siliva 200 namupatsa mmisiri wosula siliva. Iye anakonza fano, nasungunula siliva uja ndi kulikutira fano lija. Ndipo Mika anayika fanolo mʼnyumba mwake.
Kodwa wayibuyisela imali kunina. Unina wasethatha izinhlamvu zesiliva ezingamakhulu amabili, wazinika umkhandi, owenza ngazo isithombe esibaziweyo lesithombe esibunjwe ngokuncibilikisa; zasezisiba sendlini kaMika.
5 Mikayu anali ndi kachisi, ndipo anapanga efodi ndi mafano otchedwa terafimu. Anapatula mwana wake mmodzi kuti akhale wansembe.
Njalo lowomuntu uMika wayelendlu yabonkulunkulu, wenza i-efodi lamatherafi, wehlukanisa omunye wamadodana akhe, ukuze abe ngumpristi wakhe.
6 Masiku amenewo kunalibe mfumu ku Israeli. Aliyense amachita zomwe zinamukomera.
Ngalezonsuku kwakungelankosi koIsrayeli; wonke umuntu wayesenza okwakulungile emehlweni akhe.
7 Ku Betelehemu mʼdziko la Yuda kunali mnyamata wina amene anali wa fuko la Levi.
Njalo kwakukhona ijaha leBhethelehema-Juda, elosendo lukaJuda, elalingumLevi, njalo lahlala njengowezizwe khona.
8 Iyeyu anachoka mu mzinda wa Betelehemu uja ku Yuda kukafuna malo ena okhala. Akuyenda, anafika ku dziko la mapiri la Efereimu ku nyumba ya Mika.
Lowomuntu wasesuka emzini, eBhethelehema-Juda, ukuyahlala njengowezizwe lapho ayengathola khona indawo. Wafika entabeni yakoEfrayimi, endlini kaMika, ehamba ngendlela yakhe.
9 Tsono Mika anamufunsa kuti, “Mukuchokera kuti?” Ndipo iye anayakha kuti, “Ndine Mlevi wochokera ku Betelehemu mʼdziko la Yuda. Ndikufunafuna malo okhala.”
UMika wasesithi kuye: Uvela ngaphi? Wasesithi kuye: NgingumLevi weBhethelehema-Juda, ngiya ukuyahlala njengowezizwe lapho engingathola khona indawo.
10 Tsono Mika anati kwa iye, “Khalani ndi ine. Mukhale ngati mlangizi wanga ndi wansembe, ndipo ine ndizikupatsani ndalama za siliva khumi pa chaka komanso zovala ndi zakudya.”
UMika wasesithi kuye: Hlala lami, ube kimi ngubaba lompristi, mina ngizakunika izinhlamvu zesiliva ezilitshumi ngomnyaka, lezigqoko zokugqoka, lokudla kwakho. UmLevi wasengena.
11 Choncho Mleviyo anavomera kuti azikhala naye, ndipo mnyamatayo anakhala ngati mmodzi mwa ana ake aamuna.
UmLevi wavuma ukuhlala lalowomuntu; njalo ijaha laba kuye njengomunye wamadodana akhe.
12 Pambuyo pake Mika anapatula Mleviyo ndipo mnyamatayu anakhala wansembe. Tsono ankakhala mʼnyumba ya Mika.
UMika wamehlukanisa umLevi, ijaha laselisiba ngumpristi wakhe, laba sendlini kaMika.
13 Ndipo Mika anati, “Tsopano ndadziwa kuti Yehova adzandikomera mtima chifukwa Mleviyu ndiye wakhala wansembe wanga.”
UMika wasesithi: Khathesi ngiyazi ukuthi iNkosi izangenzela okuhle, ngoba ngilomLevi ongumpristi.

< Oweruza 17 >