< Oweruza 17 >

1 Munthu wina dzina lake Mika wochokera ku dziko la mapiri la Efereimu anawuza amayi ake kuti
Byl pak muž nějaký s hory Efraim, jehož jméno bylo Mícha.
2 “Ndinamva inu mukutemberera munthu amene anaba ndalama zanu zasiliva 1,100. Ndalamazo zili ndi ine, ndinatenga ndine.” Pamenepo amayi akewo anati, “Yehova akudalitse mwana wanga!”
Kterýž řekl matce své: Ten tisíc a sto stříbrných, kteříž vzati byli tobě, pro něž jsi zlořečila a mluvilas přede mnou, hle, stříbro to u mne jest, já jsem je vzal. I řekla matka jeho: Požehnaný jsi, synu můj, od Hospodina.
3 Choncho Mika anabweza ndalama 1,100 za siliva kwa amayi ake, ndipo amayi akewo anati, “Ine ndapatulira Yehova ndalama za silivazi kuti mwana wanga aseme fano ndi kulikuta ndi siliva. Ndiye tsopano ndikubwezera ndalamazo.”
Navrátil tedy ten tisíc a sto stříbrných matce své. I řekla matka jeho: Jižť jsem zajisté posvětila stříbro to Hospodinu z ruky své, a tobě synu svému, aby udělán byl obraz rytý a slitý. Protož nyní dám je tobě.
4 Tsono Mika atabweza ndalama zija kwa amayi ake, iwo anatengapo ndalama za siliva 200 namupatsa mmisiri wosula siliva. Iye anakonza fano, nasungunula siliva uja ndi kulikutira fano lija. Ndipo Mika anayika fanolo mʼnyumba mwake.
On pak navrátil to stříbro matce své, z něhož vzala matka jeho dvě stě stříbrných, a dala zlatníku. I udělal z nich obraz rytý a slitý, kterýž byl v domě Míchově.
5 Mikayu anali ndi kachisi, ndipo anapanga efodi ndi mafano otchedwa terafimu. Anapatula mwana wake mmodzi kuti akhale wansembe.
Měl pak ten Mícha chrám bohů, i udělal efod a terafim, a naplnil ruce jednoho z synů svých, aby mu byl knězem.
6 Masiku amenewo kunalibe mfumu ku Israeli. Aliyense amachita zomwe zinamukomera.
Toho času nebylo krále v Izraeli; jeden každý, což se mu za dobré vidělo, to činil.
7 Ku Betelehemu mʼdziko la Yuda kunali mnyamata wina amene anali wa fuko la Levi.
Byl pak mládenec z Betléma Judova, totiž z čeledi Judovy, kterýž, jsa Levíta, byl tam pohostinu.
8 Iyeyu anachoka mu mzinda wa Betelehemu uja ku Yuda kukafuna malo ena okhala. Akuyenda, anafika ku dziko la mapiri la Efereimu ku nyumba ya Mika.
Odšel tedy člověk ten z města Betléma Judova, aby byl pohostinu, kdež by se mu koli nahodilo. I přišel na horu Efraim, až k domu Míchovu, jda cestou svou.
9 Tsono Mika anamufunsa kuti, “Mukuchokera kuti?” Ndipo iye anayakha kuti, “Ndine Mlevi wochokera ku Betelehemu mʼdziko la Yuda. Ndikufunafuna malo okhala.”
Jemuž řekl Mícha: Odkud jdeš? Odpověděl mu: Já jsem Levíta, z Betléma Judova beru se, abych byl pohostinu, kdež by mi se koli nahodilo.
10 Tsono Mika anati kwa iye, “Khalani ndi ine. Mukhale ngati mlangizi wanga ndi wansembe, ndipo ine ndizikupatsani ndalama za siliva khumi pa chaka komanso zovala ndi zakudya.”
I řekl jemu Mícha: Zůstaň u mne, a buď mi za otce a za kněze, a buduť dávati deset stříbrných na každý rok, a dvoje roucho i stravu tvou. I šel Levíta.
11 Choncho Mleviyo anavomera kuti azikhala naye, ndipo mnyamatayo anakhala ngati mmodzi mwa ana ake aamuna.
Líbilo se pak Levítovi zůstati u muže toho, a byl u něho mládenec ten, jako jeden z synů jeho.
12 Pambuyo pake Mika anapatula Mleviyo ndipo mnyamatayu anakhala wansembe. Tsono ankakhala mʼnyumba ya Mika.
I posvětil Mícha rukou Levíty, a byl mu mládenec ten za kněze; i bydlil v domě jeho.
13 Ndipo Mika anati, “Tsopano ndadziwa kuti Yehova adzandikomera mtima chifukwa Mleviyu ndiye wakhala wansembe wanga.”
Řekl pak Mícha: Nyníť vím, že mi dobře učiní Hospodin, proto že mám toho Levítu za kněze.

< Oweruza 17 >