< Oweruza 15 >

1 Patapita nthawi, mu nyengo yodula tirigu, Samsoni anatenga kamwana kambuzi ndipo anapita kukacheza kwa mkazi wake. Iye anati, “Ndikufuna kukalowa ku chipinda cha mkazi wanga.” Koma abambo a mkaziyo anamuletsa kutero.
Kalpasan iti sumagmamano nga al-aldaw, kabayatan ti tiempo a panaga-ani iti trigo, nangala ni Samson iti urbon a kalding, ket napan sumarungkar iti asawana. Kinunana iti bagina, “Sumrekakto iti siled ti asawak”. Ngem saan isuna a palubosan ti ama iti asawana a sumrek.
2 Abambo a mkaziyo anati, “Ine ndimaganiza kuti umamuda kwambiri nʼchifukwa chake ndinamupereka kwa mnzako. Kodi mngʼono wake uja sindiye wokongola kupambana iye? Ingotengani ameneyo mʼmalo mwake.”
Kinuna ti ama iti asawana, “Ti pagarupek ket pudno a kinaguram ti asawam, isu nga intedko isuna iti gayyemmo. Napinpintas ti ub-ubing a kabsatna ngem isuna, saan kadi? Alaem ketdi isuna a kasukatna.”
3 Samsoni anawawuza kuti, “Pano sindikhala wochimwa ndikawachita choyipa chachikulu Afilistiwa.”
Kinuna ni Samson kadakuada, “Ita a kanito awan basolko no maipapan kadagiti Filisteo inton dangrak ida.”
4 Choncho Samsoni anapita nakagwira nkhandwe 300 nazimangirira michira ziwiriziwiri ndipo pa fundo iliyonse ya michirayo anamangirira nsakali.
Napan nagtiliw ni Samson iti tallo-gasut nga atap nga aso ket pinagrinneppetna dagiti ipus ti tunggal pares. Ket nangala isuna kadagiti pagsilawan ken inreppetna dagitoy iti nagtengngaan ti tunggal agpares nga ipus.
5 Anayatsa nsakalizo kenaka ndi kuzitayira nkhandwe zija mʼminda ya tirigu ya Afilisti, ndipo zinatentha milu ya tirigu, ndi wosadula yemwe pamodzi ndi mitengo ya mpesa ndi ya olivi.
Idi naseggedannan dagiti pagsilawan imbulosna dagiti atap nga aso kadagiti saan pay a naani a trigo dagiti Filisteo, ket pinuoran dagitoy dagiti nakapenpen a trigo ken dagiti saan pay naani a trigo idiay talon, agraman dagiti kaubasan ken dagiti kaoliboan.
6 Tsono Afilisti anayamba kufunsana kuti, “Ndani wachita izi?” Ena anati, “Ndi Samsoni mkamwini wa munthu wa ku Timna uja chifukwa Mtimunayo anatenga mkazi wake ndi kumupereka kwa mnzake.” Choncho Afilisti anapita kukatentha mtsikanayo pamodzi ndi abambo ake.
Nagsaludsod dagiti Filisteo, “Siasino ti nangaramid iti daytoy?” Naibaga kadakuada, “Ni Samson, a manugang ti Timniteo, ti nangaramid iti daytoy, gapu ta innala ti Timniteo ti asawa ni Samson ket intedna daytoy iti gayyemna.” Ket napan pinuoran dagiti Filisteo ti babai ken ti amana.
7 Samsoni anawawuza kuti, “Ngati mumachita zangati zimenezi, ndiye ine sindileka mpaka nditakulipsirani.”
Kinuna ni Samson kadakuada, “No daytoy iti aramidenyo, agibalesakto kadakayo, ket kalpasan a maaramid dayta, agsardengakto.”
8 Choncho Samsoni anamenyana nawo koopsa ndipo anapha ambiri a iwo. Kenaka anakalowa mʼphanga la Etamu, nakhala momwemo.
Ket pinutedputedna ida a pinidaso, iti patong ken luppoda, pinatay na ida iti nakaro a panangpapatay. Kalpasanna simmalog isuna ket nagnaed iti maysa a rukib idiay rangkis ti Etam.
9 Pambuyo pake Afilisti anakamanga misasa ya nkhondo mʼdziko la Yuda, ndi kuthira nkhondo mʼdera la Lehi.
Ket simmang-at dagiti Filisteo ket nagsaganada a manggubat iti Juda ket impuestoda ti armadada idiay Lehi.
10 Anthu a fuko la Yuda anafunsa kuti, “Nʼchifukwa chiyani mwabwera kudzamenyana nafe?” Iwo anayankha kuti, “Tabwera kudzamanga Samsoni ndi kuti timuchite zofanana ndi zimene anatichita.”
Kinuna dagiti lallaki ti Juda, “Apay a simmang-atkayo a mangraut kadakami?” Kinunada, “Rumautkami tapno matiliwmi ni Samson, tapno maaramidmi kenkuana ti inaramidna kadakami.”
11 Ndipo anthu 3,000 a ku Yuda anapita ku phanga la Etamu, ndi kukamufunsa Samsoni kuti, “Kodi iwe sudziwa kuti ife amatilamulira ndi Afilisti? Tsono ndi chiyani chimene watichitachi?” Iye anayankha kuti, “Ine ndinachita zomwe iwo anandichita.”
Ket simmalog dagiti tallo ribu a lallaki ti Juda a napan iti rukib idiay rangkis ti Etam, ket kinunada kenni Samson, “Saanmo aya ammo a dagiti Filisteo ti mangiturturay kadatayo? Ania daytoy nga inaramidmo kadakami?” Kinuna ni Samson kadakuada, “Ti inaramidda kaniak, ket isu met ti inaramidko kadakuada.”
12 Iwo anati kwa iye, “Ife tabwera kuti tikumange ndi kukupereka kwa Afilisti.” Ndipo Samsoni anati, “Lonjezani mwa lumbiro kuti simundipha ndinu.”
“Kinunada kenni Samson, “Immaykami tapno reppetendaka, ket iyawatdaka iti turay dagiti Filisteo,” Kinuna ni Samson kadakuada, “Isapatayo kaniak a saan a dakayo a mismo ti mangpatay kaniak.”
13 Iwo anamuyankha kuti, “Ayi, ife sitikupha. Koma tingokumanga ndi kukupereka mʼmanja mwa Afilisti.” Choncho anamumanga ndi zingwe ziwiri zatsopano namutulutsa mʼphanga muja.
Kinunada kenkuana, “Saan, reppetendaka laeng ket iyawatdaka kadakuada. Ikarimi a saandaka a patayen.” Ket rineppetda isuna iti dua a baro a tali ket inruarda isuna manipud iti bato.
14 Samsoni anafika ku Lehi, ndipo Afilisti anamuchingamira akufuwula. Nthawi yomweyo Mzimu wa Yehova unatsika pa iye mwamphamvu ndipo zingwe zimene anamumanga nazo zinasanduka ngati thonje lopsa mʼmoto, zinachita ngati zasungunuka nʼkuchoka mʼmanja mwake.
Idi dimteng isuna idiay Lehi, nagpukkaw dagiti Filisteo idi sinabatda isuna. Ket immay kenkuana ti Espiritu ni Yahweh nga addaan pannakabalin. Nagbalin a kasla lino a napuoran dagiti tali iti takiagna, ket natnag dagitoy manipud kadagiti imana.
15 Anapeza chibwano cha bulu amene anali atangofa kumene. Anachitola ndi kuphera nacho anthu 1,000.
Nakasarak ni Samson iti sadiwa a tulang ti panga ti asno, pinidutna daytoy ket pinatayna ti sangaribu a lallaki babaen iti daytoy.
16 Ndipo Samsoni anati, “Ndi chibwano cha bulu, milu ndi milu ya anthu. Ndi chibwano cha bulu, ndapha anthu 1,000.”
Kinuna ni Samson, “Babaen iti tulang ti panga ti asno, nagabsuon iti rabaw dagiti gabsuon. Napapatayko ti sangaribu a lallaki babaen iti tulan ti panga ti asno.”
17 Atatsiriza kuyankhula, anataya chibwanocho, ndipo malowo anawatcha Ramati-Lehi.
Idi nalpas a nagsasao ni Samson, imbellengna ti tulang ti panga ti asno, ket naawagan ti lugar iti Ramat-Lehi.
18 Pambuyo pake anamva ludzu kwambiri ndipo anayitana Yehova mopempha kuti, “Inu mwapatsa mtumiki wanu chipulumutso chachikulu chotere. Kodi tsopano ndife ndi ludzu ndi kugwidwa ndi anthu osachita mdulidwewa?”
Mawaw unay ni Samson ket immawag kenni Yahweh ket kinuna, “Intedmo daytoy a dakkel a panagballigi iti adipenmo, ngem ita matayak gapu iti pannakawaw ket matnagakto kadagiti ima dagiti a saan a nakugit.”
19 Pamenepo Mulungu anangʼamba nthaka ku Lehi, ndipo madzi anatuluka mʼdzenjemo. Samsoni anamwa madziwo, ndipo mphamvu zake zinabwerera nakhalanso monga analili. Choncho chitsimecho chinatchedwa Eni-Hakore, ndipo chilipobe ku Lehiko mpaka lero.
Ket inungap ti Dios ti nalungog a lugar idiay Lehi, ket adda iti pimmusuak a danum. Idi nakainom isuna, nagsubli ti pigsana ket simmaranta isuna. Isu a napanaganan dayta a lugar iti En-Hakkore, ket adda pay daytoy idiay Lehi agingga ita nga aldaw.
20 Samsoni anatsogolera Israeli pa nthawi ya Afilisti kwa zaka makumi awiri.
Nagbalin nga ukom ni Samson ti Israel kadagiti al-aldaw dagiti Filisteo iti las-ud ti duapulo a tawen.

< Oweruza 15 >