< Oweruza 12 >
1 Gulu la nkhondo la fuko la Efereimu linayitanidwa ndipo anawolokera ku Zafoni nakafunsa Yefita kuti, “Nʼchifukwa chiyani unawoloka kukachita nkhondo ndi Aamoni osatiyitana kuti tipite nawe? Ife tikutenthera mʼnyumba mwakomu.”
A KOAKOA mai la na kanaka o ka Eperaima, a hele ae la i ka aoao akau, i aku la ia Iepeta, No ke aha la oe i hele aku e kaua aku i na mamo a Amona, aole kii mai ia makou e hele pu me oe? E puhi ana makou i kou hale i ke ahi maluna ou.
2 Yefita anayankha kuti, “Ine ndi anthu anga tinakangana kwambiri ndi Aamoni. Ndinakuyitanani koma inu simunandipulumutse mʼmanja mwawo.
I mai la o Iepeta ia lakou, He kanaka hakaka nui loa au me na mamo a Amona, a o ko'u poe kanaka kekahi; a i ko'u hea ana aku ia oukou, aole oukou i hoopakele mai ia'u, mai ko lakou lima mai.
3 Nditaona kuti simundithandiza, ndinayika moyo wanga pa chiswe ndipo ndinawoloka kukachita nkhondo ndi a Aamoni. Yehova anandithandiza ndipo ndinawagonjetsa. Nanga nʼchifukwa chiyani mwabwera kwa ine lero kuti muchite nane nkhondo?”
A ike aku la au, aole oukou i hoopakele mai ia'u, alaila waiho iho la au i ko'u ola ma kuu lima, a hele ku e aku la i na mamo a Amona. Haawi mai no o Iehova ia lakou iloko o kuu lima. No ke aha la hoi oukou i hele mai ai ia'u i keia la e kaua mai ia'u?
4 Choncho Yefita anasonkhanitsa anthu a ku Giliyadi ndi kuchita nkhondo ndi Aefereimu. Ndipo Agiliyadi anagonjetsa Aefereimu chifukwa Aefereimuwo amati, “Inu a Giliyadi ndinu othawa kuchokera ku Efereimu ndi pakati pa Amanase.”
Alaila hoakoakoa mai la o Iepeta i na kanaka o Gileada, a kaua pu iho la me ka Eperaima. Luku aku la na kanaka o Gileada i ka Eperaima, no ka mea, olelo lakou, O oukou, o ko Gileada, he poe aea oukou no Eperaima, e noho ana mawaena o ka Eperaima, a me ka Manase.
5 Choncho Agiliyadi analanda Aefereimu madooko a mtsinje wa Yorodani. Munthu aliyense wothawa ku Efereimu amati akanena kuti, “Ndiloleni ndiwoloke,” Agaliyadi ankafunsa kuti, “Kodi ndiwe mu Efurati?” Ngati iye ayankha kuti, “Ayi”
Lilo iho la na ahua o Ioredane i ka Gileada, mamua o ka Eperaima. A ina i hele mai kekahi o ka Eperaima, i pakele, a olelo mai, E hele paha wau i kela aoao; alaila ninau ae la na kanaka o Gileada ia ia, No ka Eperaima oe? A ina olelo mai oia, Aole;
6 Ndiye amamuwuza kuti, “Nena kuti ‘Shiboleti.’” Tsono munthuyo akanena kuti Siboleti popeza samatha kutchula bwino mawuwa, ankamugwira ndi kumupha pomwepo pa madooko a mtsinje wa Yorodani. Nthawi imeneyo anaphedwa Aefereimu 42,000.
Alaila, olelo mai lakou ia ia, E i iho oe, Sehiboleta. I mai la kela, Siboleta; no ka mea, aole hiki ia ia ke olelo pololei pela. Alaila hoopaa lakou ia ia, a pepehi no ma na ahua o Ioredane. Ia manawa haule na kanaka o Eperaima, he kanahakumamalua tausani.
7 Yefita anatsogolera Israeli zaka zisanu ndi chimodzi. Kenaka Yefita wa ku Giliyadi anamwalira, ndipo anayikidwa mu mzinda wake ku Giliyadi.
Hooponopono o Iepeta i ka Iseraela, i eono makahiki. Alaila, make o Iepeta no Gileada, a kanuia oia ma kekahi o na kulanakauhale o Gileada.
8 Atamwalira Yefita, Ibizani wa ku Betelehemu anatsogolera Israeli.
A mahope iho ona, na Ibezana o Betelehema i hooponopono i ka Iseraela.
9 Iye anali ndi ana aamuna makumi atatu ndi ana aakazi makumi atatu. Anakwatitsa ana ake akaziwo kwa anthu a fuko lina, ndipo ana ake aamuna aja anawabweretsera atsikana makumi atatu kuti awakwatire amenenso anali a fuko lina. Ibizani anatsogolera Israeli kwa zaka zisanu ndi ziwiri.
He kanakolu ana keikikane, a he kanakolu kaikamahine. Hoouna aku la ia ia lakou i kahi e, a lawe mai i kanakolu kaikamahine, mai kahi e, na kana poe keikikane. Nana i hooponopono i ka Iseraela, i ehiku makahiki.
10 Kenaka Ibizani anamwalira, ndipo anayikidwa mu Betelehemu.
Alaila make o Ibezana, a kanuia ma Betelehema.
11 Iye atamwalira, Eloni wa fuko la Zebuloni anakhala mtsogoleri wa Aisraeli, ndipo anatsogolera Aisraeli kwa zaka khumi.
A mahope iho ona, hooponopono o Elona, no ka Zebuluna i ka Iseraela. Hooponopono ia i ka Iseraela, he umi makahiki.
12 Kenaka Eloni anamwalira ndipo anayikidwa ku Ayaloni mʼdziko la Zebuloni.
A make iho la o Elona, no ka Zebuluna, a kauia iho la ia ma Aialona, ma ka aina o Zebuluna.
13 Iye atamwalira, Abidoni mwana wa Hilelo wochokera ku Piratoni, anatsogolera Israeli.
A mahope iho ona, na Abedona, ke keiki a Hilela, no ka Piratona, i hooponopono i ka Iseraela.
14 Iye anali ndi ana aamuna makumi anayi ndi zidzukulu makumi atatu, amene ankakwera pa abulu 70. Iye anatsogolera Israeli kwa zaka zisanu ndi zitatu.
He kanaha kana poe keikikane, a he kanakolu moopuna kane, a holo lakou maluna o na hoki keiki, he kanahiku. Nana i hooponopono i ka Iseraela, i ewalu makahiki.
15 Ndipo Abidoni mwana wa Hilelo Mpiratoni uja anamwalira, nayikidwa ku Piratoni, mʼdziko la Efereimu, dziko lamapiri la Aamaleki.
Make iho la o Abedona, ke keiki a Hilela no Piratona, a kanuia iho la ia ma Piratona, ka aina o Eperaima ma ka mauna o ka Ameleka.