< Oweruza 1 >

1 Atamwalira Yoswa Aisraeli anafunsa Yehova kuti, “Ndani mwa ife ayambe nkhondo yomenyana ndi Akanaani?”
Tukun misa lal Joshua, mwet Israel elos siyuk sin LEUM GOD, “Su inmasrlon sruf inge ac tufah fahsr meet in mweun lain mwet Canaan?”
2 Yehova anayankha kuti, “Fuko la Yuda ndilo liyambe kupita. Ndawapatsa dzikolo mʼmanja mwawo.”
Ac LEUM GOD El topuk, “Sruf lal Judah pa ac fahsr meet. Nga ac sang tuh in elos pa nununku acn we.”
3 Choncho Ayuda anawuza abale awo a fuko la Simeoni kuti, “Bwerani tipitire limodzi mʼdziko limene tapatsidwa kuti tikamenyane ndi Akanaani. Ifenso tidzapita nanu mʼdziko limene anakugawirani.” Ndipo Asimeoni anapita nawo.
Mwet in sruf lal Judah elos fahk nu sin mwet in sruf lal Simeon, “Fahsru wi kut som nu in acn se ituku nu sesr, kut tukeni mweuni mwet Canaan, na kut fah wi kowos pac nu ke acn se itukot nu suwos.” Na sruf lal Simeon
4 Choncho Ayuda ananyamuka, ndipo Yehova anapereka Akanaani ndi Aperezi mʼmanja mwawo. Ndipo anapha anthu 10,000 ku Bezeki.
ac sruf lal Judah elos tukeni som mweun. LEUM GOD El sang kutangla nu selos fin mwet Canaan ac mwet Periz, ac oayapa elos kutangla singoul tausin mwet in acn Bezek.
5 Ku Bezekiko anakumana ndi ankhondo a mfumu Adoni-Bezeki ndipo anamenyana nawo, ndipo Ayudawo anagonjetsa Akanaani ndi Aperezi.
Elos konalak Adonibezek ingo ac mweunel.
6 Adoni-Bezekiyo anathawa, koma anamuthamangira ndi kumupeza, namugwira. Atamugwira anamudula zala zake zazikulu za ku manja ndi miyendo.
El kaingla, tusruktu elos ukwal nwe sruokilya ac pakela kuf lulap ke paol ac ke nial ah kewa.
7 Tsono Adoni-Bezeki anati, “Mafumu 70 omwe anadulidwa zala zazikulu za ku manja ndi miyendo yawo ankatola nyenyeswa pansi pa tebulo langa. Mulungu tsopano wandibwezera zomwe ndinawachita.” Kenaka anapita naye ku Yerusalemu ndipo anafera komweko.
Ac Adonibezek el fahk, “Tokosra itngoul su kufla kuf lulap ke paolos ac nialos, elos tuh eis kutkut in mongo ye tepu luk. Na pa inge God El furokma nu sik ma nga tuh oru nu selos.” Ac elos usalla nu Jerusalem ac el misa we.
8 Pambuyo pake Ayuda anakathira nkhondo mzinda wa Yerusalemu ndipo anawulanda. Anapha anthu ambiri ndi kutentha mzinda wonse.
Mwet in sruf lal Judah elos mweuni acn Jerusalem ac sruokya. Elos uniya mwet we, ac esukak siti sac.
9 Kenaka Ayuda anapita kukamenyana ndi Akanaani omwe amakhala ku dziko la ku mapiri, dziko la Negevi kummwera ndiponso mu zigwa.
Tukun ma inge elos som mweuni mwet Canaan su muta fineol uh ac pe eol uh ac acn mwesis nu eir.
10 Anakalimbananso ndi Akanaani amene ankakhala ku Hebroni (mzinda womwe kale unkatchedwa Kiriyati-Araba). Kumeneko anagonjetsa Sesai, Ahimani ndi Talimai.
Elos fahsryak lain mwet Canaan su muta in siti se pangpang Hebron, su mwet meet ah pangon Kiriath Arba. Elos kutangla ota tolu inge: Sheshai, Ahiman, ac Talmai.
11 Kuchokera kumeneko, iwo anakathira nkhondo anthu amene ankakhala ku Debri (mzindawu poyamba unkatchedwa Kiriati Seferi).
Tukun ma inge, mwet in sruf lal Judah elos som ac mweuni siti Debir, su pangpang Kiriath Sepher in pacl sac.
12 Tsono Kalebe anati, “Munthu amene angathire nkhondo mzinda wa Kiriati Seferi ndi kuwulanda, ndidzamupatsa mwana wanga Akisa kuti akhale mkazi wake.”
Sie sin mwet ingan, su pangpang Caleb, el fahk, “Nga ac elsalang Achsah, acn se nutik, tuh elan payuk nu sin mukul se ma ac sruokya siti Kiriath Sepher.”
13 Otanieli mwana wa Kenazi, mngʼono wake wa Kalebe, ndiye anawulanda. Choncho Kalebe anamupatsa mwana wake Akisa kuti akhale mkazi wake.
Othniel, wen natul Kenaz su tamulel fusr wial Caleb, el kutangla acn Debir, na Caleb el eisalang Achsah tuh elan mutan kial.
14 Tsiku lina atafika Akisayo, Otanieli anamuwumiriza mkazi wakeyo kuti apemphe munda kwa Kalebe abambo ake. Pamene Akisa anatsika pa bulu wake, Kalebe anamufunsa kuti, “Kodi ukufuna ndikuchitire chiyani?”
In len in marut laltal ah, Othniel el kwafe sel Achsah elan siyuk sin papa tumal ah ke sie ipin acn. Na ke Achsah el fani liki donkey natul, Caleb el siyuk sel lah oasr ma el lungse.
15 Iye anayankha kuti, “Mundikomere mtima. Popeza mwandipatsa ku Negevi, kumalo kumene kulibe madzi, mundipatsenso akasupe amadzi.” Choncho Kalebe anamupatsa akasupe a kumtunda ndi a kumunsi.
Na Achsah el fahk, “Nga lungse kutu luf in kof. Acn ma kom ase luk meet ah acn na pao.” Na Caleb el sang lal unon in kof su oan lucng ac ten in acn Gulloth.
16 Tsono zidzukulu za Hobabu, Mkeni uja, mpongozi wa Mose, zinachoka ku Yeriko mzinda wa migwalangwa pamodzi ndi anthu a fuko la Yuda mpaka ku chipululu chimene chili kummwera kwa Aradi ndi kukakhala ndi Aamaleki.
Mwet Ken, su sou lun papa tumun mutan kial Moses, elos wi mwet Judah som liki acn Jericho, siti in sak palm, nu yen mwesis nu eir, su oan sisken acn Arad in Judah. Ingo elos oakwuki muta inmasrlon mwet Amalek.
17 Kenaka anthu a fuko la Yuda anapita pamodzi ndi abale awo a fuko la Simeoni ndi kukagonjetsa Akanaani amene amakhala ku Zefati, ndipo mzindawo anawuwononga kwambiri. Choncho mzindawo anawutcha Horima.
Mwet Judah elos wi mwet Simeon som mweuni mwet Canaan su muta in siti Zephath. Elos selngawiya siti sac, ac kunausla, ac sang inen acn sac Hormah.
18 Anthu a fuko la Yuda analandanso mzinda wa Gaza ndi dziko lonse lozungulira, mzinda wa Asikeloni pamodzi ndi dziko lake lonse lozungulira, ndi mzinda wa Ekroni pamodzi ndi dziko lonse lozungulira.
Mwet Judah elos sruokya acn Gaza ac Ashkelon ac Ekron wi acn nukewa ma oan raunela acn inge.
19 Yehova anathandiza anthu a fuko la Yuda. Iwo analanda dziko la kumapiri, koma sanathe kuwachotsa anthu ku zigwa, chifukwa anali ndi magaleta azitsulo.
LEUM GOD El kasrelos mwet Judah, ac elos sruokya acn fineol uh, tusruktu elos koflana lusak mwet ma muta acn tupasrpasr, mweyen oasr chariot osra natulos.
20 Monga analonjezera Mose, Kalebe anapatsidwa Hebroni. Kalebe anapirikitsa mafuko atatu a Anaki mu mzindamo.
In oana ma Moses el tuh sapkin ah, acn Hebron tuh itukyang lal Caleb su tuh lusak sou tolu natul Anak ah.
21 Koma fuko la Benjamini linalephera kuwachotsa Ayebusi, amene amakhala mu Yerusalemu. Choncho Ayebusiwo akukhalabe ndi fuko la Benjamini mu Yerusalemu mpaka lero.
Tusruktu mwet in sruf lal Benjamin elos tuh tiana lusak mwet Jebus ma muta Jerusalem, oru mwet Jebus inge srakna muta inmasrlon sruf lal Benjamin nwe misenge.
22 A banja la Yosefe nawonso anathira nkhondo mzinda wa Beteli, ndipo Yehova anali nawo.
Sruf lal Ephraim ac sruf lal Manasseh elos som ac lain acn Bethel, ac LEUM GOD El welulos.
23 Anatumiza anthu kuti akazonde Beteli. Mzindawo kale unkatchedwa Luzi.
Elos supwala mwet kalngeyuk nu Bethel (inen siti sacn meet pa Luz).
24 Anthu okazondawo anaona munthu akutuluka mu mzindamo ndipo anamuwuza kuti, “Tisonyeze njira yolowera mu mzindamu, ndipo ife tidzakuchitira chifundo.”
Ac ke mwet kalngeyuk inge liye sie mwet illa liki siti uh, elos fahk nu sel, “Fahkma nu sesr lah kut ac utyak fuka nu in siti uh, na kut ac kulang nu sum.”
25 Choncho iye anawaonetsa njirayo, ndipo iwo anapha anthu onse mu mzindamo ndi lupanga koma munthu uja pamodzi ndi banja lake sanawaphe.
Na mwet sac fahkang nu selos, na mwet Ephraim ac mwet Manasseh inge elos uniya mwet nukewa in siti sac sayen mwet se ma kasrelos ah ac sou lal ah.
26 Ndipo iye anapita ku dziko la Ahiti, kumene anamangako mzinda nawutcha dzina lake Luzi. Mpaka lero lino mzindawo dzina lake ndi lomwelo.
Tok mwet sac som nu in acn sin mwet Hit ac musaeak siti se we, ac pangon acn sac Luz. Srakna pangpang acn sac Luz nwe misenge.
27 Koma a fuko la Manase sanachotse nzika za mzinda wa Beti-Seani pamodzi ndi mʼmidzi yake yozungulira, kapena nzika za mzinda wa Taanaki ndi mʼmidzi yake yozungulira, kapenanso nzika za mzinda wa Dori ndi mʼmidzi yake yozungulira. Iwo sanapirikitse nzika za mzinda wa Ibuleamu ndi mʼmidzi yake yozungulira, kapena mzinda wa Megido ndi mʼmidzi yake yozungulira. Choncho Akanaani anapitirirabe kukhala mʼdzikomo.
Sruf lal Manasseh tuh tiana lusak mwet ma muta in siti Beth Shan, Taanach, Dor, Ibleam, Megiddo, ac acn ma oan apkuran nu in acn inge. Oru mwet Canaan elos mutana in facl sac.
28 Aisraeli atakhala amphamvu, anawagwiritsa Akanaaniwo ntchito yakalavulagaga, koma sanawapirikitse.
Ke mwet Israel elos kui, na elos sang orekma na upa nu sin mwet Canaan inge, tusruktu elos tiana luselosla.
29 Nawonso Aefereimu sanathamangitse Akanaani amene amakhala mu Gezeri, choncho Akanaaniwo ankakhalabe pakati pawo ku Gezeriko.
Sruf lal Ephraim elos tiana lusak mwet Canaan su muta in siti Gezer, oru mwet inge elos mutana inmasrlolos.
30 Azebuloni sanathamangitse Akanaani amene amakhala mu Kitironi kapena a ku Nahaloli. Iwo ankakhala pakati pawo ndipo ankawagwiritsa ntchito yakalavulagaga.
Sruf lal Zebulun tuh tiana lusak mwet muta in siti Kitron ac Nahalal, oru mwet Canaan inge elos srak pacna mutana inmasrlolos, tusruktu akkohsyeyuk elos in orekma nu sin mwet Zebulun.
31 A fuko la Aseri nawo sanathamangitse amene amakhala mu Ako, Sidoni, Ahilabu, Akizibu, Heliba, Afiki, ndi Rehobu.
Sruf lal Asher tuh tiana lusla mwet muta in siti Acco, Sidon, Ahlab, Achzib, Helbah, Aphek, ac Rehob.
32 Choncho anthu a fuko la Aseri anakhala pakati pa Akanaani amene ankakhala mʼdzikomo popeza sanawapirikitse.
Mwet ke sruf lal Asher elos tuh wi na mwet Canaan inge muta, ke sripen elos tiana luselosla.
33 Nalonso fuko la Nafutali silinathamangitse anthu amene ankakhala ku Beti Semesi kapena ku Beti Anati. Koma Anafutaliwo ankakhala pakati pa Akanaaniwo mʼdzikomo. Koma anthu amene ankakhala ku Beti Semesi ndi ku Beti Anati anawasandutsa kukhala ogwira ntchito yathangata.
Sruf lal Naphtali tiana lusla mwet ma muta in siti Beth Shemesh ac Bethanath. Mwet Naphtali inge wi na mwet Canaan inge muta, tusruktu elos akkohsyelos in orekma nu selos.
34 Aamori anapirikitsira anthu a fuko la Dani ku dziko la ku mapiri popeza sanawalole kuti atsikire ku chigwa.
Mwet Amor elos lusak mwet in sruf lal Dan nu fineol uh, ac tia lela elos in tuku nu yen tupasrpasr uh.
35 Aamori anatsimikiza mtima zokhalabe ku phiri la Hara-Heresi, ku Ayaloni, ndiponso ku Saalibimu. Koma a fuko la Yosefe anakula mphamvu ndipo anagwiritsa Aamoriwo ntchito yakalavulagaga.
Mwet Amor elos mutana in Aijalon, Shaalbim, ac Fineol Heres, tusruktu sruf lal Ephraim ac Manasseh elos leum faclos ac akkohsyelos in orekma nu selos.
36 Malire a Aamori anayambira ku chikweza cha Akirabimu nʼkulowera ku Sela napitirira kumapita chakumapiri ndithu.
Masrol ke acn Edom ac Ephraim mutawauk ke acn Sela fahsryak nu epang ac sasla ke Innek In Utyak Nu Akrabbim.

< Oweruza 1 >