< Yoswa 7 >
1 Koma Aisraeli anachita zachinyengo ndi lamulo lija loti asatenge kalikonse koyenera kuwonongedwa. Akani mwana wa Karimi, mwana wa Zabidi, mwana wa Zera, wa fuko la Yuda anatengako zinthu zina. Choncho Yehova anakwiyira Israeli kwambiri.
Fe nandilatse amo raha navikeo o ana’ Israeleo; amy te nandrambe raha navike t’i Akane, ana’i Karmý, ana’ i Zabdý, ana’i Zerake, fifokoa’ Iehodà; vaho nisolebatse amo ana’ Israeleo ty haviñera’ Iehovà.
2 Tsono Yoswa anatuma anthu kuchokera ku Yeriko kukazonda ku mzinda wa Ai umene uli pafupi ndi mzinda wa Beti-Aveni kummawa kwa Beteli, ndipo anawawuza kuti, “Pitani mukazonde chigawochi.” Anthuwo anapitadi kukazonda Ai.
Nañirake ondaty boake Ieriko mb’amy Ày marine i Bete-avene, atiñana’ i Betele mb’eo t’Iehosoa, le hoe ty nanoe’e: Akia, tampono i taney. Aa le nionjoñe mb’eo ondatio nanampoñe i Ày.
3 Atabwera kwa Yoswa, anamuwuza kuti, “Sikofunika kuti apite anthu onse kukathira nkhondo mzinda wa Ai. Mutumizeko anthu 2,000 kapena 3,000 kuti akatenge mzindawo. Musawatume anthu onse kumeneko popeza kuli anthu ochepa.”
Ie nibalike mb’amy Iehosoa mb’eo le nitalily ty hoe: Ko ampionjoneñe mb’eo iaby ondatio; fe añiraho ondaty telo arivo ndra ro’ arivo hionjoñe mb’eo handafa i Ày; ko votsora’o hifanehake mb’eo i maro iabiy, amy t’ie tsy ampeampe.
4 Choncho kunapita anthu 3,000. Koma iwo anathamangitsidwa ndi anthu a ku Ai.
Va’e lahilahy telo-arivo amy màroy ty nionjomb’eo; f’ie nitriban-day añatrefa’ ondati’ i Àio,
5 Anthu a ku Ai anathamangitsa Aisraeli kuchokera pa chipata cha mzindawo mpaka ku ngwenya ndipo anapha anthu 36. Iwowa anawapha pamene ankatsika phiri. Choncho mitima ya anthu inasweka ndipo analibenso mphamvu.
naho nañohofa’ ondati’ i Àio loza t’indaty telopolo eneñ’ amby; le hinorida’e boak’amy lalam-beiy pake Sebarime añe, naho linafa’ iareo amy fizotsoañey mb’ eo vaho nalorè aman’ arofo ondatio, nitranake hoe rano.
6 Tsono Yoswa anangʼamba zovala zake nagwada nʼkuweramitsa mutu wake pansi patsogolo pa Bokosi la Yehova. Akuluakulu a Israeli nawonso anadzigwetsa pansi ndipo anakhala pomwepo mpaka madzulo atadziwaza fumbi kumutu kwawo.
Rinia’ Iehosoa i saro’ey naho nibabok’ an-tane an-dahara’e añatrefa’ i vatam-pañina’ Iehovày ampara’ te haleñe, ie naho o androanavi’ Israeleo songa nampibobò deboke añambone’e.
7 Ndipo Yoswa anati, “Kalanga ine, Ambuye Wamphamvuzonse chifukwa chiyani munatiwolotsa Yorodani? Kodi mumalinga zotipereka mʼmanja mwa Aamori kuti atiwononge chotere? Kukanakhala kwabwino ife tikanakhala tsidya linalo la Yorodani!
Le hoe t’Iehosoa: Hoke! ry Rañandria Iehovà, aa vaho akore ty nampitsaha’o Iardeney ondaty retoañe hanesea’o am-pità’ o nte-Amoreo, hampihomaha’o anay? Hamake t’ie nilesa naho nitobok’ alafe’ Iardeney añe!
8 Tsono Ambuye, ine ndinene chiyani, pakuti tsopano Israeli anathamangitsidwa ndi adani ake?
O Rañandria, ino ty ho asako, kanao niambohoa’ Israele o rafelahi’eo!
9 Akanaani ndi anthu ena a dziko lino adzamva zimenezi ndipo adzatizinga ndi kutiwonongeratu. Nanga inu mudzatani ndi dzina lanu lamphamvulo?”
Ie mahajanjiñe izay o nte-Kanàneo naho o hene mpimoneñe an-tane atoio, le hiariseho anay, vaho hapitso’ iareo an-tane atoy ty tahina’ay, le hatao’o akore i Tahina’o jabahinakey?
10 Koma Yehova anati kwa Yoswa, “Imirira! Chifukwa chiyani wagwada pansi chotere?
Le hoe t’Iehovà am’ Iehosoa: Miongaha, ino ty ibaboha’o an-dahara’o?
11 Aisraeli achimwa. Iwo aphwanya pangano limene ndinawalamula kuti asunge. Anatengako zinthu zina zofunika kuwonongedwa. Choncho anabako, ananena bodza ndi kuyika zinthu zakubazo pamodzi ndi katundu wawo.
Toe nanao hakeo t’Israele; nililare’ iareo i fañinako nandiliako am’iareoy; nangalake amo raha navikeo; naho nampikametse naho nañetake vaho napoke amo harao’eo.
12 Nʼchifukwa chake Aisraeli sangathe kulimbana ndi adani awo. Iwo anathawa pamaso pa adani awo chifukwa ndiwo oyenera kuwonongedwa. Ine sindikhalanso ndi inu pokhapokha mutawononga chilichonse choyenera kuwonongedwa pakati panu.
Aa le tsy nahafitroatse añatrefan-drafelahi’e o ana’ Israeleo; niambohoa’ iareo o rafelahi’eo amy t’ie ninjare fokom-patse; tsy hindre ama’ areo iraho naho tsy mongore’ areo hey o nozoñeñe ama’ areoo.
13 “Nyamuka, ukawawuze anthu kuti, ‘Mudzipatule nokha kukonzekera kuonana nane mawa; pakuti Yehova Mulungu wa Israeli akuti choyenera kuwonongedwa chija chili pakati panu, inu Aisraeli. Simungathe kulimbana ndi adani anu mpaka mutachichotsa.’
Miongaha, ampiavaho ondatio, ano ty hoe: Miefera ho ami’ty maray; fa hoe ty tsara’ Iehovà Andrianañahare’ Israele: Aman’ onjitse ty añivo’o ao, ry Israele; tsy mahafijohañe añatrefa’ o rafelahi’oo irehe ampara’ te akareñe ama’ areo hey i natokañey.
14 “Mawa mmamawa adzabwere pamaso pa Yehova fuko limodzilimodzi. Fuko limene Yehova adzaliloze lidzabwere patsogolo mbumba imodziimodzi. Tsono mbumba imene Yehova adzayiloze idzabwere patsogolo banja limodzilimodzi. Banja limene Yehova adzaliloze lidzabwere patsogolo munthu mmodzimmodzi.
Aa ie maraindray, miheova mb’eo am-pifokoañe; vaho ze fifokoa rambese’ Iehovà ro hañarine an-kasavereña’e; le ty hasavereñañe edrè’ Iehovà ro hañarine mb’eo ki-anjomba’e; le ty anjomba edrè’ Iehovà ro hitotoke ki’ ondaty.
15 Iye amene adzagwidwe ndi zinthu zoyenera kuwonongedwazo adzawotchedwa ndi moto, pamodzi ndi banja lake lonse ndi zinthu zake zonse. Iyeyutu wachita chinthu chonyansa pakati pa Aisraeli ndi kuphwanya pangano limene anthu anga anachita ndi Ine!”
Ie amy zay, ho forototoeñe añ’afo ao ty nandrambe o raha navikeo rekets’ o fanaña’e iabio; amy te nililare’e ty fañina’ Iehovà, vaho nanao hatsivokarañe e Israele ao.
16 Mmawa mwake Yoswa anabweretsa Israeli fuko limodzilimodzi ndipo fuko la Yuda linalozedwa.
Aa le nañaleñàleñe amy maraiñey t’Iehosoa vaho nampitotohe’e t’Israele am-pifokoa’e le nivoa ty fifokoa’ Iehoda.
17 Anabweretsa poyera mbumba zonse za fuko la Yuda, ndipo mbumba ya Zera inagwidwa. Kenaka anatulutsa poyera mabanja onse a mbumba ya Zera ndipo banja la Zabidi linagwidwa.
Nampitotohe’e ty fifokoa’ Iehoda, le voa ty hasavereña’ i Zerake; nampitotohe’e ty hasavereña’ i Zerake, lahilahy an-dahilahy le voa ty Zabdý.
18 Potsiriza anatulutsa anthu onse a banja la Zabidi ndipo Akani anagwidwa. Iyeyu anali mwana wa Karimi, mwana wa Zabidi, mwana wa Zera wa fuko la Yuda.
Nampitotohe’e ki’ ondaty ki’ondaty i anjomba’ey le voa t’i Akane, ana’ i Karmi, ana’ i Zabdy, ana’ i Zerake, fifokoa’ Iehoda.
19 Ndipo Yoswa anati kwa Akani, “Mwana wanga pereka ulemerero kwa Yehova Mulungu wa Israeli ndipo umuyamike Iye. Ndiwuze zimene wachita, ndipo usandibisire.”
Aa le hoe t’Iehosoa amy Akane, O anako, ehe toloro engeñe t’Iehovà Andrianañahare’ Israele, vaho andriaño; atalilio ahy henaneo i nanoe’oy; le ko aetake.
20 Akani anayankha kuti, “Zoona! Ine ndachimwira Yehova Mulungu wa Israeli. Chimene ndachita ine ndi ichi:
Le hoe ty natoi’ i Akane am’ Iehosoa: Toe nandilatse am’ Iehovà Andrianañahare’ Israele iraho vaho zao naho zao ty nanoeko.
21 Ndinaona mwa zinthu zolanda ku nkhondo zija, mkanjo wokongola wa ku Babuloni, makilogalamu awiri a siliva ndiponso golide wolemera theka la kilogalamu. Zimenezi ndinazikhumba ndipo ndinazitenga. Ndazibisa mʼkati mwa tenti yanga, ndipo siliva ali pansi pake.”
Naho nitreako amo fikopahañeo ty sarimbo soa boake Sinare naho ty volafoty sekele roanjato, naho ty tseram-bolamena milanja sekele limampolo, le nihañeko, naho rinambeko; vaho ingo, mikafitse an-tane añivon-kibohoko ao, ambane ao i volafotiy.
22 Motero Yoswa anatuma anthu, ndipo anathamanga kupita ku tenti. Anthuwo anakapeza kuti zinthuzo zinabisidwadi mʼtenti yake, ndipo siliva analidi pansi pake.
Aa le nampañitrike irake t’Iehosoa, naho nilay mb’ amy kibohotsey iereo, le ingo t’ie nikafitse an-kiboho’e ao, vaho ambane’e ao i volafotiy.
23 Iwo anazichotsa zinthuzo mu tenti yake nabwera nazo kwa Yoswa ndi kwa Aisraeli onse ndipo anaziyika pamaso pa Yehova.
Rinambe’ iereo boak’ an-kibohotse ao izay le nendese’e mb’ amy Iehosoa, naho mb’amo hene ana’ Israeleo mb’eo vaho napo’ iereo añatrefa’ Iehovà.
24 Kenaka Yoswa pamodzi ndi Aisraeli onse anatenga Akani mwana wa Zera pamodzi ndi siliva, mkanjo, golide zimene anapezeka nazo zija. Anatenganso ana ake aamuna ndi aakazi, ngʼombe zake, abulu ndi nkhosa, tenti yake ndi zonse anali nazo, kupita nazo ku chigwa cha Akori.
Rinambe’ Iehosoa naho Israele iaby t’i Akane ana’ i Zerake naho i volafotiy, i sarimboy naho i tseram-bolamenay naho o ana-dahi’eo, o anak’ ampela’eo naho o añombe’eo naho o borìke’eo naho o añondri’eo naho i kiboho’ey naho ze ama’e iaby; le nampionjone’ iereo mb’ am-bavatane’ Akore mb’eo.
25 Yoswa anati “Chifukwa chiyani wabweretsa mavuto awa pa ife? Yehova ndiye abweretse mavuto pa iwe lero.” Kenaka Aisraeli onse anaponya miyala Akani, namupha. Anaponyanso miyala banja lake lonse, nʼkulipha. Pambuyo pake anatentha Akani uja, banja lake ndi zonse zimene anali nazo.
Le hoe t’Iehosoa: Ino ty nanolora’o sotry anay? Iehovà ty hanolo-sotry ama’o te anito. Aa le nametsaha’ Israele vato, naho namorototo iareo an’ afo vaho nametsa-bato ama’e.
26 Anawunjika mulu waukulu wa miyala pa Akani, imene ilipobe mpaka lero. Nʼchifukwa chake malowa amatchedwa chigwa cha Akori mpaka lero. Ndipo Yehova anachotsa mkwiyo wake.
Nampitoabora’ iareo votrim-bato jabajaba ty ambone’ iereo, ze mbe eo henaneo, le nitolik’ amy haviñera’ey t’Iehovà. Aa le natao Vavatane’ i Akore ty añara’ i toetsey, pake henane.