< Yoswa 21 >

1 Tsono atsogoleri a mabanja a fuko la Levi anabwera kwa wansembe Eliezara, Yoswa mwana wa Nuni, ndi kwa atsogoleri a mabanja a mafuko onse a Aisraeli,
Kwasekusondela inhloko zaboyise bamaLevi kuEleyazare umpristi lakuJoshuwa indodana kaNuni lakuzo inhloko zaboyise bezizwe zabantwana bakoIsrayeli,
2 ku Silo mʼdziko la Kanaani ndipo anati, “Yehova analamula kudzera mwa Mose kuti atipatse mizinda kuti tikhalemo, pamodzi ndi malo odyetseramo ziweto zathu.”
bakhuluma kubo eShilo elizweni leKhanani, besithi: INkosi yalaya ngesandla sikaMozisi ukusinika imizi yokuhlala, lamadlelo ayo ezifuyo zethu.
3 Choncho, Aisraeli anapereka kwa fuko la Levi mizinda iyi pamodzi ndi malo owetera ziweto zawo kuchokera ku madera awo, monga Yehova analamulira:
Ngakho abantwana bakoIsrayeli banika amaLevi okwelifa labo ngokomlayo weNkosi, limizi lamadlelo ayo.
4 Maere oyamba anagwera mabanja a Kohati, Alevi amene anali zidzukulu za wansembe Aaroni anapatsidwa mizinda 13 kuchokera ku mafuko a Yuda, Simeoni ndi Benjamini.
Kwasekuvela inkatho yensendo zamaKohathi. Abantwana bakoAroni umpristi, abavela kumaLevi, ngenkatho esizweni sakoJuda lesizweni sakoSimeyoni lesizweni sakoBhenjamini, basebesiba lemizi elitshumi lantathu.
5 Ndipo mabanja otsala a Kohati anapatsidwa mizinda khumi kuchokera ku mafuko a Efereimu, Dani ndi theka la fuko la Manase.
Labaseleyo kubantwana bakaKohathi, ngenkatho ensendweni zesizwe sakoEfrayimi lesizweni sakoDani lengxenyeni eyodwa kwezimbili yesizwe sakoManase, baba lemizi elitshumi.
6 Zidzukulu za Geresoni zinapatsidwa mizinda 13 kuchokera ku mabanja a mafuko a Isakara, Aseri, Nafutali ndi theka la fuko la Manase ku Basani.
Labantwana bakoGerishoni, ngenkatho ensendweni zesizwe sakoIsakari lesizweni sakoAsheri lesizweni sakoNafithali lengxenyeni eyodwa kwezimbili yesizwe sakoManase eBashani, baba lemizi elitshumi lantathu.
7 Mabanja a Merari anapatsidwa mizinda khumi ndi iwiri kuchokera ku mafuko a Rubeni, Gadi ndi Zebuloni.
Abantwana bakoMerari ngokwensendo zabo, esizweni sakoRubeni lesizweni sakoGadi lesizweni sakoZebuluni, baba lemizi elitshumi lambili.
8 Choncho Aisraeli anapereka kwa fuko la Levi mizindayi pamodzi ndi malo odyetserako ziweto pogwiritsa ntchito maere, monga Yehova analamula kudzera mwa Mose.
Labantwana bakoIsrayeli banika amaLevi le imizi lamadlelo ayo ngenkatho, njengokulaya kweNkosi ngesandla sikaMozisi.
9 Awa ndi mayina a mizinda ya mafuko a Yuda ndi Simeoni imene inaperekedwa kwa zidzukulu za Aaroni,
Basebenika esizweni sabantwana bakoJuda lesizweni sabantwana bakoSimeyoni le imizi, eqanjwa ngebizo,
10 ku banja la Kohati amene anali Alevi. Paja maere oyamba anagwera mabanja a Kohati kuti alandira mizinda.
eyayingeyabantwana bakoAroni, bevela kunsendo zamaKohathi ebantwaneni bakoLevi, ngoba baba lenkatho yokuqala.
11 Anapatsidwa mzinda wa Kiriati Ariba. (Paja Ariba ndiye kholo la Anaaki). Dzina lina la mzindawu ndi Hebroni, ndipo unali mʼdziko la mapiri la Yuda. Pamodzi ndi mzindawu anapatsidwanso mabusa ake onse ozungulira.
Basebebanika iKiriyathi-Arba, uyise kaAnoki, okuyiHebroni, ezintabeni zakoJuda lamadlelo inhlangothi zayo zonke.
12 Komabe minda ndi midzi yozungulira mizindayi inali itaperekedwa kale kwa Kalebe, mwana wa Yefune kuti ikhale cholowa chake.
Kodwa insimu yomuzi lemizana yawo bakunika uKalebi indodana kaJefune ukuba ngeyakhe.
13 Choncho zidzukulu za Aaroni wansembe, zinapatsidwa Hebroni (mzinda wopulumukirako amene wapha munthu), Libina,
Ngakho banika abantwana bakoAroni umpristi umuzi wokuphephela wombulali, iHebroni, lamadlelo ayo, leLibhina lamadlelo ayo,
14 Yatiri, Esitemowa,
leJatiri lamadlelo ayo, leEshithemowa lamadlelo ayo,
15 Holoni, Debri,
leHoloni lamadlelo ayo, leDebiri lamadlelo ayo,
16 Aini, Yuta, ndi Beti-Semesi pamodzi ndi mabusa odyetseramo ziweto ozungulira mizindayi. Yonse pamodzi inali mizinda isanu ndi inayi yochokera ku mafuko awiriwa.
leAyini lamadlelo ayo, leJuta lamadlelo ayo, leBeti-Shemeshi lamadlelo ayo; imizi eyisificamunwemunye kulezizizwe ezimbili.
17 Fuko la Benjamini linapereka Gibiyoni, Geba,
Lesizweni sakoBhenjamini: IGibeyoni lamadlelo ayo, iGeba lamadlelo ayo,
18 Anatoti ndi Alimoni, pamodzi ndi mabusa odyetsera ziweto ozungulira mizindayi. Yonse pamodzi inali mizinda inayi.
iAnathothi lamadlelo ayo, leAlimoni lamadlelo ayo: Imizi emine.
19 Choncho mizinda 13 pamodzi ndi malo odyetsera ziweto anapatsidwa kwa ansembe, zidzukulu za Aaroni.
Yonke imizi yabantwana bakoAroni, abapristi, yayilemizi elitshumi lantathu lamadlelo ayo.
20 Mabanja ena otsalira a Kohati a fuko la Levi anapatsidwa mizinda iyi kuchokera ku fuko la Efereimu:
Lensendo zabantwana bakoKohathi, amaLevi, asalayo ebantwaneni bakoKohathi, baba lemizi yenkatho yabo esizweni sakoEfrayimi.
21 Mizinda ya Sekemu ndi Gezeri ndiye inali mizinda wopulumukirako munthu aliyense wopha mnzake mwangozi. Mizindayi inali ku mapiri a Efereimu.
Basebebanika umuzi wokuphephela umbulali, iShekema lamadlelo ayo entabeni yakoEfrayimi, leGezeri lamadlelo ayo,
22 Analandiranso mizinda ya Gezeri, Kibuzaimu, Beti-Horoni pamodzi ndi malo odyetsera ziweto ozungulira mizindayi. Yonse pamodzi inali mizinda inayi.
leKibizayimi lamadlelo ayo, leBhethi-Horoni lamadlelo ayo: Imizi emine.
23 Fuko la Dani linapereka mizinda ya Eliteke, Gibetoni,
Lesizweni sakoDani iEliteke lamadlelo ayo, iGibethoni lamadlelo ayo,
24 Ayaloni, Gati-Rimoni pamodzi ndi mabusa odyetsera ziweto ozungulira mizindayi. Yonse pamodzi inali mizinda inayi.
iAjaloni lamadlelo ayo, iGathi-Rimoni lamadlelo ayo: Imizi emine.
25 Kuchokera ku theka la fuko la Manase analandira Taanaki ndi Gati-Rimoni pamodzi ndi malo awo owetera ziweto, mizinda iwiri.
Lengxenyeni eyodwa kwezimbili yesizwe sakoManase, iThahanakhi lamadlelo ayo, leGathi-Rimoni lamadlelo ayo: Imizi emibili.
26 Mizinda khumi yonseyi pamodzi ndi malo odyetsera ziweto, zinapatsidwa ku mabanja ena onse a Akohati.
Yonke imizi yensendo zabantwana bakoKohathi abaseleyo yayilitshumi lamadlelo ayo.
27 Mabanja a Ageresoni a fuko la Levi anapatsidwa mizinda iwiri kuchokera ku theka la Manase wa kummawa, Golani ku Basani (mzinda wopulumukirako amene wapha munthu mwangozi) ndi Beesitera, pamodzi ndi malo awo odyetserako ziweto.
Lakubantwana bakoGerishoni, bensendo zamaLevi, kungxenye yesizwe sakoManase, iGolani eBashani, umuzi wokuphephela umbulali, lamadlelo ayo, leBheyeshithera lamadlelo ayo: Imizi emibili.
28 Fuko la Isakara linapereka mizinda ya Kisoni, Daberati,
Lesizweni sakoIsakari, iKishiyoni lamadlelo ayo, iDaberathi lamadlelo ayo,
29 Yarimuti ndi Eni Ganimu, pamodzi ndi malo awo odyetsera ziweto. Yonse pamodzi inali mizinda inayi.
iJarimuthi lamadlelo ayo, iEni-Ganimi lamadlelo ayo: Imizi emine.
30 Fuko la Aseri linapereka mizinda ya Misali, Abidoni,
Lesizweni sakoAsheri, iMishali lamadlelo ayo, iAbidoni lamadlelo ayo,
31 Helikati ndi Rehobu pamodzi ndi malo awo odyetsera ziweto. Yonse pamodzi inali mizinda inayi.
iHelkathi lamadlelo ayo, leRehobi lamadlelo ayo: Imizi emine.
32 Fuko la Nafutali linapereka mizinda ya Kedesi wa ku Galileya, mzinda umene unali wopulumukiramo munthu wopha mnzake mwangozi. Analandiranso mizinda ya Hamoti-Dori ndi Karitani. Kuphatikizira apa, analandira malo odyetsera ziweto a mizindayi. Yonse pamodzi inali mizinda inayi.
Lesizweni sakoNafithali, iKedeshi eGalili, umuzi wokuphephela umbulali, lamadlelo ayo, leHamothi-Dori lamadlelo ayo, leKaritani lamadlelo ayo: Imizi emithathu.
33 Mabanja onse a Ageresoni analandira mizinda 13 pamodzi ndi malo awo odyetsera a ziweto.
Yonke imizi yamaGerishoni ngokwensendo zawo yayiyimizi elitshumi lantathu lamadlelo ayo.
34 Mabanja a Merari amene anali otsala a fuko la Levi, anapatsidwa mizinda iyi kuchokera ku fuko la Zebuloni: Yokineamu, Karita,
Lensendo zabantwana bakoMerari, amaLevi aseleyo, zaba leJokineyamu esizweni sakoZebuluni lamadlelo ayo, leKarita lamadlelo ayo,
35 Dimuna ndi Nahalali, pamodzi ndi malo awo odyetsera ziweto. Yonse pamodzi inali mizinda inayi.
iDimina lamadlelo ayo, iNahalali lamadlelo ayo: Imizi emine.
36 Kuchokera ku fuko la Rubeni analandira Bezeri, Yahaza,
Lesizweni sakoRubeni, iBezeri lamadlelo ayo, leJahaza lamadlelo ayo,
37 Kedemoti ndi Mefaati, pamodzi ndi malo awo odyetsera ziweto. Yonse pamodzi inali mizinda inayi.
iKedemothi lamadlelo ayo, leMefahathi lamadlelo ayo: Imizi emine.
38 Kuchokera ku fuko la Gadi analandira mzinda wa Ramoti ku Giliyadi. Mzinda umene unali wopulumukiramo munthu wopha mnzake mwangozi.
Lesizweni sakoGadi, iRamothi eGileyadi, umuzi wokuphephela umbulali, lamadlelo ayo, leMahanayimi lamadlelo ayo,
39 Analandiranso mizinda ya Mahanaimu, Hesiboni, Yazeri pamodzi ndi malo odyetserako ziweto ozungulira mizinda yonseyi. Yonse pamodzi inali mizindayi anayi.
iHeshiboni lamadlelo ayo, iJazeri lamadlelo ayo: Imizi emine isiyonke.
40 Choncho mabanja onse a Merari, amene anali otsala a fuko la Levi analandira mizinda khumi ndi iwiri pogwiritsa ntchito maere.
Yonke imizi yayingeyabantwana bakoMerari, ngokwensendo zabo, abaseleyo ensendweni zamaLevi. Lenkatho yabo yayiyimizi elitshumi lambili.
41 Motero mizinda 48 ya mʼdziko limene Aisraeli analanda inapatsidwa kwa Alevi, kuphatikizapo malo ake odyetsera ziweto.
Yonke imizi yamaLevi phakathi kwelifa labantwana bakoIsrayeli yayiyimizi engamatshumi amane lesificaminwembili lamadlelo ayo.
42 Iliyonse mwa mizindayi inali ndi malo owetera ziweto oyizungulira.
Le imizi, lowo lalowo wawulamadlelo awo inhlangothi zawo zonke. Kwakunjalo kuleyo yonke imizi.
43 Motero Yehova anapereka kwa Israeli dziko limene analumbira kulipereka kwa makolo awo. Atalilandira anadzakhalamo.
INkosi yasinika uIsrayeli ilizwe lonke eyafunga ukubanika lona oyise; basebesidla ilifa lalo bahlala kulo.
44 Yehova anawapatsa mtendere mʼdziko lonse monga momwe analonjezera makolo awo. Palibe ndi mmodzi yemwe mwa adani awo amene anatha kuwagonjetsa chifukwa Yehova anapereka adani awo onse mʼmanja mwawo.
INkosi yasibanika ukuphumula inhlangothi zonke njengokufunga kwayo konke kuboyise. Kakumanga muntu phambi kwabo kuzo zonke izitha zabo. INkosi yazinikela izitha zonke zabo esandleni sabo.
45 Yehova anakwaniritsa zonse zimene analonjeza kwa Aisraeli.
Kakwehlulekanga lalutho lwayo yonke into enhle iNkosi eyayikhuluma kuyo indlu kaIsrayeli; konke kwenzeka.

< Yoswa 21 >