< Yoswa 20 >
1 Pambuyo pake Yehova anati kwa Yoswa:
Hahoi BAWIPA Cathut ni Joshua hah a kaw teh,
2 “Uza Aisraeli kuti apatule mizinda yopulumukiramo, monga ine ndinakulangizira kudzera mwa Mose,
nang ni Isarel miphunnaw,
3 kuti aliyense amene wapha munthu mosazindikira osati mwadala azithawirako. Motero adzatetezedwa kwa wolipsira.
tami thei hanelah pouknae awm laipalah, ka tet payon e tami ni, a yawng nahane khonaw hah kârawi awh. Kut pathungnae koehoi hlout nahane kho lah ao han.
4 Ngati munthu wathawira ku umodzi mwa mizinda imeneyi, akafike pa malo oweruzira milandu amene ali pa chipata cha mzindawo ndipo akafotokoze mlandu wake pamaso pa akuluakulu a mzindawo. Kenaka iwo adzamulola kulowa mu mzinda wawo ndi kumupatsa malo woti akhale nawo.
Hote kho buetbuet touh dawk ka yawng e tami teh, kho e longkha koe kangdue vaiteh, hote kho dawk kacuenaw koe amae kong hah a thaisak vaiteh, ahnimouh ni kho thung a kaw vaiteh, amamouh koe hmuen a poe han.
5 Ngati munthu wolipsirayo amutsatira komweko atsogoleriwo asapereke munthu wakuphayo chifukwa anapha Mwisraeli mnzakeyo mosazindikira, osati mwachiwembu.
Kut ka pathung hane tami ni pâlei pawiteh, ahnie kut dawk poe mahoeh. Bangkongtetpawiteh, ahni ni amae a hui hah kâtarannae awm laipalah a thei payon toe.
6 Munthu wakuphayo adzakhalabe mu mzindawo mpaka atayimbidwa mlandu pamaso pa gulu lonse, ndiponso mpaka atamwalira mkulu wa ansembe amene akutumikira pa nthawiyo. Pamenepo munthuyo atha kubwereranso ku mudzi kwawo kumene anachoka mothawa kuja.”
Ahni teh tamimaya hmalah a kangdue teh, lawkcengnae a khang hoehnahlan, hatnae tueng nah vaihma kacue a due hoehnahlan, hote kho dawk ao han. Hathnukkhu hoi a yawng takhai e kho, ama a onae im koe bout ban vaiteh o thainae kâ ao han.
7 Choncho iwo anapatula Kedesi mʼdera la Galileya ku mapiri a Nafutali, Sekemu ku mapiri a Efereimu, ndi Kiriati Ariba (ndiye Hebroni) ku mapiri a Yuda.
Ahnimouh ni Galilee ram, Naphtali mon dawk Kedesh vah, Ephraim mon dawk Shekhem kho, Judah mon dawk Hebron kho tie Kiriath-Arba khonaw hai thoseh,
8 Kummawa kwa Yorodani, mʼmapiri a chipululu a kummawa kwa Yeriko, anapatula Bezeri pakati pa dera la fuko la Rubeni. Anapatulanso Ramoti ku Giliyadi mʼdera la fuko la Gadi, ndiponso Golani ku Basani mʼdera la fuko la Manase.
Jordan palang namran, Jeriko kho, Kanîtholah Reuben ram, Kahrawngum dawk e Bezer kho, Gad ram, Gilead ram dawk Ramoth kho, Manasseh ram, Bashan ram dawk Golan khonaw hah a rawi awh.
9 Imeneyi ndiyo inali mizinda yopulumukiramo ya Aisraeli onse ngakhalenso mlendo wokhala pakati pawo. Munthu aliyense wopha mnzake mwangozi ankathawira ku mizinda imeneyi. Munthu wolipsira sankaloledwa kuti aphe munthu wothawayo ngati mlandu wake sunazengedwe pamaso pa gulu lonse.
Hete khonaw teh, Isarel miphun dawk hai thoseh, ahnimouh koe kaawm e Jentelnaw hai thoseh, pouk laipalah tami thet payon pawiteh, ka thet e tami ni kut pathungnae dawk hoi a hlout vaiteh, tamimaya hmalah a pha hoehnahlan a yawng vaiteh, ao thai nahanelah rawi e khonaw lah ao.