< Yoswa 19 >

1 Maere achiwiri anagwera mabanja a fuko la Simeoni. Dziko lawo linali mʼkati mwenimweni mwa dziko la Yuda.
Sedan föll den andre lotten Simeons barnas slägtes, efter deras ätter; och deras arfvedel var ibland Juda barnas arfvedel.
2 Dzikolo linaphatikiza zigawo izi: Beeriseba (ndi Seba), Molada,
Och kom på deras arfvedel BerSeba, Seba, Molada,
3 Hazari-Suwali, Bala, Ezemu,
HazarSual, Bala, Azem,
4 Elitoladi, Betuli, Horima,
Eltolad, Bethul, Horma,
5 Zikilagi, Beti-Marikaboti, Hazari-Susa,
Ziklag, BethMarkaboth, HazarSusa,
6 Beti-Lebaoti ndi Saruheni. Yonse pamodzi inali mizinda 13 ndi midzi yawo.
BethLebaoth, Saruhen. Det äro tretton städer, och deras byar.
7 Panalinso mizinda inayi iyi: Aini, Rimoni, Eteri ndi Asani pamodzi ndi midzi yawo.
Ain, Rimmon, Ether, Asan. Det äro fyra städer och deras byar.
8 Dzikolo linaphatikizanso midzi yonse yozungulira mizinda imeneyi mpaka ku Baalati-Beeri, ndiye kuti Rama wa kummwera. Ili ndi dziko limene mabanja a fuko la Simeoni analandira kukhala lawo.
Dertill alla byar, som ligga omkring dessa städerna, allt intill BaalathBer, Ramath söderut. Detta är Simeons barnas arfvedel i deras ätter.
9 Cholowa cha fuko la Simeoni chinatengedwa kuchokera ku gawo la Yuda chifukwa fuko la Yuda linali lalikulu kwambiri. Izi zinachititsa fuko la Simeoni kukhala mʼkati mwenimweni mwa dziko la Yuda.
Ty Simeons barnas arfvedel är ibland Juda barnas snöre; efter Juda barnom var deras arfvedel för stor; derföre fingo Simeons barn del ibland deras arfvedel.
10 Maere achitatu anagwera mabanja a fuko la Zebuloni: Malire a dziko lawo anafika mpaka ku Saridi.
Tredje lotten föll på Sebulons barn efter deras ätter; och deras arfvedels gränsa var allt intill Sarid;
11 Malirewo anakwera kupita cha kumadzulo ku Marala nakafika ku Dabeseti ndi ku mtsinje wa kummawa kwa Yokineamu.
Och går uppåt vesterut till Marala, och stöter inpå Dabbaseth, och stöter inpå bäcken, som löper framom Jokneam;
12 Kuchokera ku mbali ina ya Saridi malire anakhota kupita kummawa ku malire a Kisiloti-Tabori mpaka ku Daberati nakwera mpaka ku Yafiya.
Och vänder sig ifrå Sarid österut, allt intill den gränsan CislothThabor; och går ut till Dabberath, och räcker upp till Japhia;
13 Kuchokera kumeneko anabzola kulowa cha kummawa mpaka ku Gati-Heferi ndi ku Eti Kazini ndi kumaloza ku Neya njira ya ku Rimoni.
Och löper dädan österåt igenom GittaHepher, IttaKazin, och kommer ut till Rimmon, Hammethoar, Hannea;
14 Mbali ya kumpoto malirewo analoza ku Hanatoni ndipo anakathera ku chigwa cha Ifita Eli.
Och böjer sig omkring ifrå nordan inåt Nathon; och utgången är i den dalen JiphtaEl;
15 Anaphatikizapo Katati, Nahalala, Simironi, Idala ndi Betelehemu. Mizinda yonse inakwana khumi ndi iwiri pamodzi ndi midzi yake.
Kattath, Nahalal, Simron, Jideala och BethLehem. Det äro tolf städer, och deras byar.
16 Mizinda imeneyi pamodzi ndi midzi yake ndi imene mabanja a fuko la Zebuloni analandira.
Detta är nu Sebulons barnas arfvedel till deras ätter; och detta är deras städer och byar.
17 Maere achinayi anagwera mabanja a fuko la Isakara.
Fjerde lotten föll på Isaschars barn efter deras ätter.
18 Dziko lawo linaphatikiza zigawo izi: Yezireeli, Kesuloti, Sunemu,
Och deras gränsa var Jisreel, Chesulloth, Sunem,
19 Hafaraimu, Sioni, Anaharati,
Hapharaim, Sion, Anaharath,
20 Rabiti, Kisoni, Ebezi,
Rabbith, Kisjon, Abez.
21 Remeti, Eni Ganimu, Eni Hada ndi Beti-Pazezi.
Remeth, EnGannim, EnHadda, BethPazzez;
22 Malirewa anakafikanso ku Tabori, Sahazuma ndi Beti-Semesi ndipo anakathera ku Yorodani. Mizinda yonse inalipo 16 ndi midzi yake.
Och stöter inpå Thabor, Sahazima, BethSemes, och utgången deraf var inuppå Jordan; sexton städer, och deras byar.
23 Mizinda imeneyi pamodzi ndi midzi yake ndiyo inali cholowa cha mabanja a fuko la Isakara.
Detta är nu Isaschars barnas slägters arfvedel till deras ätter, städer och byar.
24 Maere achisanu anagwera mabanja a fuko la Aseri.
Femte lotten föll på Assers barnas slägte i deras ätter.
25 Gawo lawo linaphatikiza Helikati, Hali, Beteni, Akisafu,
Och deras gränsa var Helkath, Hali, BetenAchsaph,
26 Alameleki, Amadi ndi Misali. Kumadzulo malire anafika ku Karimeli ndi Sihori Libinati.
Alammelech, Amead, Miseal; och stöter inpå Carmel vid hafvet, och till SihorLibnath;
27 Kenaka anakhotera kummawa kulowera ku Beti-Dagoni nafika ku dziko la Zebuloni ndi ku chigwa cha Ifita Eli, ndipo anapita kumpoto ku Beti-Emeki ndi Neieli. Anapitirirabe kumpoto mpaka kukafika ku Kabuli,
Och vänder sig österut till BethDagon, och stöter inpå Sebulon, och till den dalen JiphthahEl norrut, BethEmek, Negiel, och kommer ut vid Cabul på venstra sidone;
28 Ebroni, Rehobu, Hamoni, ndi Kana, mpaka ku Sidoni Wamkulu.
Ebron, Rehob, Hammon, Kana, allt intill det stora Zidon;
29 Kenaka malirewo anakhotera ku Rama ndi kupita ku mzinda wotetezedwa wa ku Turo. Kuchokera pamenepo malirewo anakhota kupita ku Hosa nakatulukira ku Nyanja, mʼchigawo cha Akizibu,
Och vänder sig inåt Rama, allt intill den fasta staden Zor; och vänder sig åt Hosa, och går ut vid hafvet efter snöret åt Achsib;
30 Uma, Afeki ndi Rehobu. Mizinda yonse inalipo 22 pamodzi ndi midzi yake.
Umma, Aphek, Rehob; två och tjugu städer, och deras byar.
31 Mizinda yonseyi pamodzi ndi midzi yake ndiyo inali cholowa cha mabanja a fuko la Aseri.
Detta är nu Assers barnas slägters arfvedel till deras ätter, städer och byar.
32 Maere achisanu ndi chimodzi anagwera mabanja a fuko la Nafutali.
Sjette lotten föll på Naphthali barn i deras ätter.
33 Malire awo anayambira ku Helefu mpaka ku mtengo wa thundu wa ku Zaananimu, ndipo anapitirira nʼkukafika ku Adami Nekebu, Yabineeli mpaka ku Lakumi ndi kukathera ku Yorodani.
Och deras gränsa var ifrå Heleph, Allon, igenom Zaanannim, Adami, Nekeb, JabneEl, allt intill Lakum, och går ut inpå Jordan;
34 Tsono malirewo anakhotera kumadzulo kupita ku Azinoti-Tabori. Kuchoka kumeneko anapita ku Hukoki, modutsa Zebuloni cha kummwera, Aseri cha kumadzulo ndi mtsinje wa Yorodani cha kummawa.
Och vänder sig vesterut åt Asnoth Thabor; och kommer dädan ut och till Hukkob, och stöter inpå Sebulon söderut, och till Assur vesterut, och till Juda invid Jordan österut;
35 Mizinda yotetezedwa inali Zidimi, Zeri, Hamati, Rakati, Kinereti,
Och hafver fasta städer, Ziddim, Zer, Hammath, Rakkath, Chinnareth,
36 Adama, Rama, Hazori,
Adama, Rama, Hazor,
37 Kedesi, Ederi, Eni Hazori,
Kedes, Edrei, EnHazor,
38 Yironi, Migidali Eli, Horemu, Beti-Anati ndi Beti-Semesi. Yonse pamodzi inalipo mizinda 19 ndi midzi yake.
Jireon, MigdalEl, Horem, BethAnath, BethSames; nitton städer, och deras byar.
39 Mizinda yonseyi pamodzi ndi midzi yawo ndiyo inali cholowa cha mabanja a fuko la Nafutali.
Detta är nu Naphthali barnas slägters arfvedel till deras ätter, städer och byar.
40 Maere achisanu ndi chiwiri anagwera mabanja a fuko la Dani.
Sjunde lotten föll på Dans barnas slägte i deras ätter.
41 Gawo lawo linaphatikiza mizinda iyi: Zora, Esitaoli, Iri Semesi,
Och gränsan af deras arfvedel var: Zorga, Esthaol, IrSames,
42 Saalabini, Ayaloni, Itira,
Saalabbin, Ajalon, Jithla,
43 Eloni, Timna, Ekroni,
Elon, Timnatha, Ekron,
44 Eliteke, Gibetoni, Baalati,
Eltheke, Gibbethon, Baalath,
45 Yehudi, Beni Beraki, Gati-Rimoni,
Jehud, Benebarak, GathRimmon,
46 Me-Yarikoni ndi Rakoni, pamodzi ndi dera loyangʼanana ndi Yopa.
MeJarkon, Rakkon med den gränsona vid Japho:
47 Anthu a fuko la Dani atalandidwa dziko lawo, anapita kukathira nkhondo Lesemu. Iwo anapha anthu ake onse, nawulandiratu mzindawo, kuwusandutsa wawo ndi kumakhalamo. Tsono anatcha mzindawo dzina loti Dani popeza ndilo linali dzina la kholo lawo.
Och der går Dans barnas gränsa ut. Och Dans barn drogo upp, och stridde emot Lesem och vunno det, och slogo det med svärdsegg; och togo det in, och bodde deruti, och kallade det Dan, efter deras faders namn.
48 Mizinda yonseyi pamodzi ndi midzi yake ndiyo inali cholowa cha mabanja a fuko la Dani.
Detta är nu Dans barnas slägtes arfvedel i deras ätter, städer och byar.
49 Atatha kugawana zigawo zosiyanasiyana za dzikolo, Aisraeli anamupatsa Yoswa mwana wa Nuni chigawo chake.
Och då de hade lyktat utskifta landet med dess gränsor, gåfvo Israels barn Josua, Nuns son, en arfvedel ibland sig;
50 Potsata zimene Yehova anawalamula, anamupatsa mzinda wa Timnati-Sera umene anawupempha. Mzindawu unali mʼdziko lamapiri la Efereimu. Iye anawumanga mzindawu ndi kukhazikikako.
Och gåfvo honom efter Herrans befallning den stad, som han begärade, som var ThimnathSerah uppå Ephraims berg; den staden byggde han, och bodde deruti.
51 Wansembe Eliezara, Yoswa ndi atsogoleri a mabanja onse a Israeli anagawa dziko lija zigawozigawo pogwiritsa ntchito maere pamaso pa Yehova. Izi zinachitika ku Silo pa khomo la tenti ya msonkhano. Choncho anamaliza kugawa dzikolo.
Desse äro nu de arfvedelar, som Eleazar Presten, och Josua, Nuns son, och de öfverste af fäderna ibland slägterna, genom lott utskifte Israels barnom i Silo för Herranom, inför dörrene af vittnesbördsens tabernakel; och lyktade så landsens utskiftning.

< Yoswa 19 >