< Yoswa 19 >
1 Maere achiwiri anagwera mabanja a fuko la Simeoni. Dziko lawo linali mʼkati mwenimweni mwa dziko la Yuda.
U A puka mai ka lua o na hailona ana no Simeona, no ka ohana a ka poe mamo a Simeona mamuli o ko lakou mau ohua; a aia ko lakou ainahooili mawaena o ka ainahooili o ka poe mamo a Iuda.
2 Dzikolo linaphatikiza zigawo izi: Beeriseba (ndi Seba), Molada,
Aia iloko o ko lakou hooilina o Beeraseba, a me Seba, a me Molada,
3 Hazari-Suwali, Bala, Ezemu,
O Hazarasuala, a me Bala, a me Azema,
4 Elitoladi, Betuli, Horima,
O Eletolada, a me Betula, a me Horema,
5 Zikilagi, Beti-Marikaboti, Hazari-Susa,
O Zikelaga, a me Betemarekabota, a me Hazarasusa,
6 Beti-Lebaoti ndi Saruheni. Yonse pamodzi inali mizinda 13 ndi midzi yawo.
A me Betelebaota, a me Saruhena; he umikumamakolu mau kulanakauhale a me ko lakou mau kauhale:
7 Panalinso mizinda inayi iyi: Aini, Rimoni, Eteri ndi Asani pamodzi ndi midzi yawo.
O Aina, o Remona, a me Etera, a me Asana, eha kulanakauhale a me ko lakou mau kauhale:
8 Dzikolo linaphatikizanso midzi yonse yozungulira mizinda imeneyi mpaka ku Baalati-Beeri, ndiye kuti Rama wa kummwera. Ili ndi dziko limene mabanja a fuko la Simeoni analandira kukhala lawo.
O na kauhale a pau a puni i keia mau kulanakauhale a hiki i Baalatebeera, o Ramata ma ka hema. Oia ka hooilina o ka ohana o ka poe mamo a Simeona mamuli o ko lakou mau ohua.
9 Cholowa cha fuko la Simeoni chinatengedwa kuchokera ku gawo la Yuda chifukwa fuko la Yuda linali lalikulu kwambiri. Izi zinachititsa fuko la Simeoni kukhala mʼkati mwenimweni mwa dziko la Yuda.
Ma ka hooilina o ka poe mamo a Iuda ka hooilina o ka Simeona poe mamo; no ka mea, o ke kuleana o ka Iuda na nui loa aku ia no lakou; nolaila ua loaa ka uoho ana ka Simeona poe mamo mawaena o ko lakou.
10 Maere achitatu anagwera mabanja a fuko la Zebuloni: Malire a dziko lawo anafika mpaka ku Saridi.
Ua puka mai ke kolu o ka hailona ana no ka Zebuluna poe mamo mamuli o ko lakou mau ohua; a o ka mokuna o ko lakou ainahooili aia no ia i Sarida.
11 Malirewo anakwera kupita cha kumadzulo ku Marala nakafika ku Dabeseti ndi ku mtsinje wa kummawa kwa Yokineamu.
Ua moe ae ko lakou mokuna ma kai, a me Marala, ua pili ia i Dabaseta, a ua hiki ia i ka muliwai aia imua o Iokeneama.
12 Kuchokera ku mbali ina ya Saridi malire anakhota kupita kummawa ku malire a Kisiloti-Tabori mpaka ku Daberati nakwera mpaka ku Yafiya.
A ua huli ia mai Sarida ma ka hikina kahi i puka mai ai ka la, a hiki i ka mokuna o Kiselotabora, alaila moe ae la ia i Daberata, a pii iluna i Iapia.
13 Kuchokera kumeneko anabzola kulowa cha kummawa mpaka ku Gati-Heferi ndi ku Eti Kazini ndi kumaloza ku Neya njira ya ku Rimoni.
Alaila moe ae la ia ma ka hikina i Gitahepera a me Itakazina, a moe ae la ma Remonametoara a hiki i Nea.
14 Mbali ya kumpoto malirewo analoza ku Hanatoni ndipo anakathera ku chigwa cha Ifita Eli.
Ua poai ae la ka mokuna ma ka akau a hiki i Hanatona; a o kona welau aia ma ke awawa o Iipetaela.
15 Anaphatikizapo Katati, Nahalala, Simironi, Idala ndi Betelehemu. Mizinda yonse inakwana khumi ndi iwiri pamodzi ndi midzi yake.
O Katata, a me Nahalala, a me Simerona, a me Idala, a me Betelehema: he umikumamalua kulanakauhale, a me ko lakou mau kauhale.
16 Mizinda imeneyi pamodzi ndi midzi yake ndi imene mabanja a fuko la Zebuloni analandira.
Oia ka ainahooili o na keiki a Zebuluna ma ko lakou mau ohua; oia hoi na kulanakauhale a me na kauhale.
17 Maere achinayi anagwera mabanja a fuko la Isakara.
Ua puka mai ka ha o ka hailona ana no Isakara, no na mamo a Isakara, mamuli o ko lakou poe ohua.
18 Dziko lawo linaphatikiza zigawo izi: Yezireeli, Kesuloti, Sunemu,
O ko lakou mokuna aia ma Ie zereela, a me Kesulota, a me Sunema,
19 Hafaraimu, Sioni, Anaharati,
O Haparaima, a me Sihona, a me Anaharata,
20 Rabiti, Kisoni, Ebezi,
O Rabita, a me Kisiona, a me Abeza,
21 Remeti, Eni Ganimu, Eni Hada ndi Beti-Pazezi.
O Remeta, a me Eneganima, a me Enehada, a me Betepazeza.
22 Malirewa anakafikanso ku Tabori, Sahazuma ndi Beti-Semesi ndipo anakathera ku Yorodani. Mizinda yonse inalipo 16 ndi midzi yake.
A ua pili ka mokuna i Tabora, a me Sahazima, a me Betesemesa; a o ka welau o ko lakou mokuna aia ma Ioredane; he umikumamaona kulanakauhale a me ko lakou mau kauhale.
23 Mizinda imeneyi pamodzi ndi midzi yake ndiyo inali cholowa cha mabanja a fuko la Isakara.
Oia ka ainahooili o ka ohana a Isakara mamuli o ko lakou poe ohua; o na kulanakauhale a me na kauhale.
24 Maere achisanu anagwera mabanja a fuko la Aseri.
Ua puka mai ka lima o ka hailona ana no ka ohana a ka poe mamo a Asera, mamuli o ko lakou poe ohua.
25 Gawo lawo linaphatikiza Helikati, Hali, Beteni, Akisafu,
O ko lakou mokuna, o Helekata, a me Hali, a me Betena, a me Akesapa,
26 Alameleki, Amadi ndi Misali. Kumadzulo malire anafika ku Karimeli ndi Sihori Libinati.
O Alameleka, a me Amada, a me Miseala; a ua moe ae la ia i Karamela ma ke komohana, a me Sihoralibenata;
27 Kenaka anakhotera kummawa kulowera ku Beti-Dagoni nafika ku dziko la Zebuloni ndi ku chigwa cha Ifita Eli, ndipo anapita kumpoto ku Beti-Emeki ndi Neieli. Anapitirirabe kumpoto mpaka kukafika ku Kabuli,
Alaila, huli ia i ka hikina i Betedagona, a pili ia i Zebuluna a me ke awawa o Iipetaela ma ka akau o Betemeka, a me Neiela, a hiki aku i Kabula ma ka aoao hema;
28 Ebroni, Rehobu, Hamoni, ndi Kana, mpaka ku Sidoni Wamkulu.
A o Heberona, a me Rehoba, a me Hamona, a me Kana, a hiki i Zidona nui.
29 Kenaka malirewo anakhotera ku Rama ndi kupita ku mzinda wotetezedwa wa ku Turo. Kuchokera pamenepo malirewo anakhota kupita ku Hosa nakatulukira ku Nyanja, mʼchigawo cha Akizibu,
A huli ka mokuna i Rama, a i ke kulanakauhale ikaika o Turo; alaila huli ka mokuna i Hosa; a o kona welau aia ma ke kai, mai kona aoao a hiki i Akeziba.
30 Uma, Afeki ndi Rehobu. Mizinda yonse inalipo 22 pamodzi ndi midzi yake.
O Uma hoi a me Apeka, a me Rehoba; he iwakaluakumamalua kulanakauhale, a me ko lakou mau kauhale.
31 Mizinda yonseyi pamodzi ndi midzi yake ndiyo inali cholowa cha mabanja a fuko la Aseri.
Oia ka ainahooili o ka ohana a Asera mamuli o ko lakou poe ohua, oia na kulanakauhale a me na kauhale.
32 Maere achisanu ndi chimodzi anagwera mabanja a fuko la Nafutali.
Ua puka mai ke ono o ka hailona ana no ka poe mamo a Napetali, no ka poe mamo a Napetali, mamuli o ko lakou poe ohua.
33 Malire awo anayambira ku Helefu mpaka ku mtengo wa thundu wa ku Zaananimu, ndipo anapitirira nʼkukafika ku Adami Nekebu, Yabineeli mpaka ku Lakumi ndi kukathera ku Yorodani.
Aia ko lakou mokuna mai Halepa mai, mai Alona hoi a i Zaananima a me Adami, Nekeba, a me Iabenela a hiki i Lakuma; a o kona welau aia ma Ioredane.
34 Tsono malirewo anakhotera kumadzulo kupita ku Azinoti-Tabori. Kuchoka kumeneko anapita ku Hukoki, modutsa Zebuloni cha kummwera, Aseri cha kumadzulo ndi mtsinje wa Yorodani cha kummawa.
Alaila, huli ka mokuna ma ke komohana i Azenotabora, a malaila aku hele ia i Hukoka, a moe ae la ia i Zebuluna ma ka aoao hema, a moe ae la ia i Asera ma ke komohana, a ia Iuda hoi ma Ioredane ma ka hikina o ka la.
35 Mizinda yotetezedwa inali Zidimi, Zeri, Hamati, Rakati, Kinereti,
Eia na kulanakauhale i paa i ka pa, o Zidima, a me Zera, a me Hamata, o Rakata, a me Kinareta,
O Adama, a me Rama, a me Hazora,
37 Kedesi, Ederi, Eni Hazori,
O Kedesa, a me Ederei, a me Enehazora,
38 Yironi, Migidali Eli, Horemu, Beti-Anati ndi Beti-Semesi. Yonse pamodzi inalipo mizinda 19 ndi midzi yake.
O Irona, a me Migedaleela, a me Horema, a me Betanata, a me Betesemesa; he umikumamaiwa kulanakauhale a me ko lakou mau kauhale.
39 Mizinda yonseyi pamodzi ndi midzi yawo ndiyo inali cholowa cha mabanja a fuko la Nafutali.
Oia ka ainahooili o ka ohana a Napetali ma ko lakou poe ohua; oia na kulanakauhale a me na kauhale.
40 Maere achisanu ndi chiwiri anagwera mabanja a fuko la Dani.
Ua puka mai ka hiku o ka hailona ana no ka ohana a ka poe mamo a Dana, mamuli o ko lakou poe ohua.
41 Gawo lawo linaphatikiza mizinda iyi: Zora, Esitaoli, Iri Semesi,
O ka mokuna o ko lakou ainahooili, o Zora a me Asetaola, a me Iresemesa,
42 Saalabini, Ayaloni, Itira,
O Saalabina, a me Aialona, a me Ietela,
O Elona a me Timenata, a me Ekerona,
44 Eliteke, Gibetoni, Baalati,
O Eleteka, a me Gibetona, a me Baalata,
45 Yehudi, Beni Beraki, Gati-Rimoni,
O Iehuda, a me Beneberaka, a me Gaterimona,
46 Me-Yarikoni ndi Rakoni, pamodzi ndi dera loyangʼanana ndi Yopa.
O Meiarekona, a me Rakona, a me ka mokuna imua o Iapo.
47 Anthu a fuko la Dani atalandidwa dziko lawo, anapita kukathira nkhondo Lesemu. Iwo anapha anthu ake onse, nawulandiratu mzindawo, kuwusandutsa wawo ndi kumakhalamo. Tsono anatcha mzindawo dzina loti Dani popeza ndilo linali dzina la kholo lawo.
Ua pilikia ka mokuna o na keiki a Dana; no ia mea, pii aku la na keiki a Dana e kaua aku i ko Lesema, a pio oia ia lakou, a pepehi lakou ia wahi me ka maka o ka pahi kaua, a lilo mai ia ia lakou, a noho lakou ilaila, a kapa aku lakou ia Lesema, o Dana, mamuli o ka inoa o Dana o ko lakou makuakane.
48 Mizinda yonseyi pamodzi ndi midzi yake ndiyo inali cholowa cha mabanja a fuko la Dani.
Oia ka ainahooili o ka ohana a ka poe mamo a Dana, mamuli o ko lakou poe ohua; oia mau kulanakauhale a me na kauhale.
49 Atatha kugawana zigawo zosiyanasiyana za dzikolo, Aisraeli anamupatsa Yoswa mwana wa Nuni chigawo chake.
A hoopau lakou i ka mahele ana i ka aina no na ainahooili, ma na mokuna, ua haawi aku la ka poe mamo a Iseraela i ainahooili no Iosua ke keiki a Nuna, iwaena o lakou.
50 Potsata zimene Yehova anawalamula, anamupatsa mzinda wa Timnati-Sera umene anawupempha. Mzindawu unali mʼdziko lamapiri la Efereimu. Iye anawumanga mzindawu ndi kukhazikikako.
E like me ke kauoha a Iehova, haawi lakou nona i ke kulanakauhale ana i noi mai ai, ia Timenasera ma ka mauna o Eperaima; a kukulu oia i ke kulanakauhale, a noho malaila.
51 Wansembe Eliezara, Yoswa ndi atsogoleri a mabanja onse a Israeli anagawa dziko lija zigawozigawo pogwiritsa ntchito maere pamaso pa Yehova. Izi zinachitika ku Silo pa khomo la tenti ya msonkhano. Choncho anamaliza kugawa dzikolo.
Oia na ainahooili a Eleazara ke kahuna, a me Iosua ke keiki a Nuna, a me ka poe koikoi o na makua o ka poe ohana a Iseraela, i mahele ai i ainahooili ma ka hailona ana, ma Silo, imua o Iehova, ma ka puka o ka halelewa o ke anainakanaka. Pela i pau ai ka mahele ana i ka aina.