< Yoswa 18 >
1 Atagonjetsa dziko lonse Aisraeli anasonkhana ku Silo ndipo anayimikako tenti ya msonkhano.
and to gather all congregation son: descendant/people Israel Shiloh and to dwell there [obj] tent meeting and [the] land: country/planet to subdue to/for face: before their
2 Koma pa nthawiyo nʼkuti mafuko asanu ndi awiri a Aisraeli asanalandire cholowa chawo.
and to remain in/on/with son: descendant/people Israel which not to divide [obj] inheritance their seven tribe
3 Ndipo Yoswa anati kwa Aisraeli, “Kodi mudikira mpaka liti kuti mulowe ndi kulanda dziko limene Yehova Mulungu wa makolo anu wakupatsani?
and to say Joshua to(wards) son: descendant/people Israel till where? you(m. p.) to slacken to/for to come (in): come to/for to possess: take [obj] [the] land: country/planet which to give: give to/for you LORD God father your
4 Sankhani amuna atatu kuchokera ku fuko lililonse ndipo ine ndidzawatuma kuti akayendere dzikolo ndi kukalilembera bwino kuti ndiligawe kukhala lawo. Akatero, abwererenso kwa ine.
to give to/for you three human to/for tribe and to send: depart them and to arise: establish and to go: walk in/on/with land: country/planet and to write [obj] her to/for lip: according inheritance their and to come (in): come to(wards) me
5 Aligawe dzikolo mʼzigawo zisanu ndi ziwiri; fuko la Yuda lidzakhale ndi dziko lake la kummwera ndi nyumba ya Yosefe ikhalebe mʼdziko lawo la kumpoto.
and to divide [obj] her to/for seven portion Judah to stand: stand upon border: area his from south and house: household Joseph to stand: stand upon border: area their from north
6 Mudzalembe mawu ofotokoza za zigawo zisanu ndi ziwiri za dzikolo, ndi kubwera nawo kwa ine. Tsono ineyo ndidzakuchitirani maere pamaso pa Yehova Mulungu wanu.
and you(m. p.) to write [obj] [the] land: country/planet seven portion and to come (in): bring to(wards) me here/thus and to shoot to/for you allotted here to/for face: before LORD God our
7 Alevi asakhale ndi dziko pakati panu, chifukwa gawo lawo ndi kutumikira Yehova pa ntchito ya unsembe. Ndipo Gadi, Rubeni ndi theka la fuko la Manase analandira kale cholowa chawo kummawa kwa Yorodani. Mose mtumiki wa Yehova ndiye anawapatsa.”
for nothing portion to/for Levi in/on/with entrails: among your for priesthood LORD inheritance his and Gad and Reuben and half tribe [the] Manasseh to take: recieve inheritance their from side: beyond to/for Jordan east [to] which to give: give to/for them Moses servant/slave LORD
8 Anthuwo akupita kukalembera dzikolo, Yoswa anawalangiza kuti, “Pitani mukayendere ndi kulembera dzikolo. Kenaka mukabwere kwa ine, ndidzakuchitirani maere kuno ku Silo pamaso pa Yehova.”
and to arise: rise [the] human and to go: went and to command Joshua [obj] [the] to go: went to/for to write [obj] [the] land: country/planet to/for to say to go: went and to go: walk in/on/with land: country/planet and to write [obj] her and to return: return to(wards) me and here to throw to/for you allotted to/for face: before LORD in/on/with Shiloh
9 Ndipo anthu anachoka ndi kukayendera dziko lonse. Iwo analemba bwinobwino mʼbuku za dzikolo, mzinda ndi mzinda. Analigawa magawo asanu ndi awiri, ndipo anabwerera kwa Yoswa ku misasa ya ku Silo.
and to go: went [the] human and to pass in/on/with land: country/planet and to write her to/for city to/for seven portion upon scroll: book and to come (in): come to(wards) Joshua to(wards) [the] camp Shiloh
10 Pambuyo pake Yoswa anawachitira maere ku Silo pamaso pa Yehova, ndipo fuko lililonse la Israeli analigawira dziko lake.
and to throw to/for them Joshua allotted in/on/with Shiloh to/for face: before LORD and to divide there Joshua [obj] [the] land: country/planet to/for son: descendant/people Israel like/as division their
11 Maere anagwera mabanja a fuko la Benjamini. Dziko limene anapatsidwa linali pakati pa fuko la Yuda ndi fuko la Yosefe:
and to ascend: rise allotted tribe son: descendant/people Benjamin to/for family their and to come out: casting(lot) border: area allotted their between son: descendant/people Judah and between son: descendant/people Joseph
12 Mbali ya kumpoto malire awo anayambira ku Yorodani nalowera chakumpoto kwa matsitso a ku Yeriko kulowera cha kumadzulo kwa dziko la ku mapiri ndi kukafika ku chipululu cha Beti-Aveni.
and to be to/for them [the] border: boundary to/for side north [to] from [the] Jordan and to ascend: rise [the] border: boundary to(wards) shoulder Jericho from north and to ascend: rise in/on/with mountain: hill country sea: west [to] (and to be *Q(K)*) outgoing his wilderness [to] Beth-aven Beth-aven
13 Kuchokera kumeneko malirewo analoza ku Luzi nadutsa mʼmbali mwa mapiri kummwera kwa Luzi (ndiye Beteli) ndipo anatsika mpaka ku Ataroti Adari, ku mapiri a kummwera kwa Beti-Horoni wa Kumunsi.
and to pass from there [the] border: boundary Luz [to] to(wards) shoulder Luz [to] south [to] he/she/it Bethel Bethel and to go down [the] border: boundary Ataroth-addar Ataroth-addar upon [the] mountain: mount which from south to/for (Lower) Beth-horon (Lower) Beth-horon Lower (Beth Horon)
14 Ndipo malirewo analowanso kwina, analunjika kummwera kuchokera kumadzulo kwake kwa phiri loyangʼanana ndi Beti-Horoni, mpaka ku mzinda wa Kiriyati Baala (ndiye Kiriati Yearimu), mzinda wa anthu a fuko la Yuda. Amenewa ndiye anali malire a mbali ya kumadzulo.
and to border [the] border: boundary and to turn: turn to/for side sea: west south [to] from [the] mountain: mount which upon face: surface Beth-horon Beth-horon south [to] (and to be *Q(K)*) outgoing his to(wards) Kiriath-baal Kiriath-baal he/she/it Kiriath-jearim Kiriath-jearim city son: descendant/people Judah this side sea: west
15 Malire a kummwera anayambira mʼmphepete mwenimweni mwa Kiriati Yearimu napita kumadzulo mpaka kukafika ku akasupe a Nefitowa.
and side south [to] from end Kiriath-jearim Kiriath-jearim and to come out: extends [the] border: boundary sea: west [to] and to come out: extends to(wards) spring water Nephtoah
16 Malire anatsikira mʼmphepete mwa phiri loyangʼanana ndi chigwa cha Beni Hinomu, kumpoto kwa chigwa cha Refaimu. Anapitirira kutsikira ku chigwa cha Hinomu kummwera kwa chitunda cha Ayebusi mpaka ku Eni Rogeli.
and to go down [the] border: boundary to(wards) end [the] mountain: mount which upon face: surface Valley son: child (Topheth of son of) Hinnom which in/on/with Valley (of Rephaim) (Valley of) Rephaim north [to] and to go down Valley (Topheth of) Hinnom to(wards) shoulder [the] Jebusite south [to] and to go down En-rogel En-rogel
17 Kenaka anakhotera kumpoto kupita ku Eni-Semesi, kupitirira mpaka ku Geliloti amene amayangʼanana ndi pokwera pa Adumimu. Kenaka malire anatsikira ku Mwala wa Bohani, mwana wa Rubeni.
and to border from north and to come out: extends En-shemesh En-shemesh and to come out: extends to(wards) Geliloth which before ascent Adummim and to go down stone Bohan son: child Reuben
18 Anabzola cha kumpoto kwa chitunda cha Beti Araba ndi kutsikabe mpaka ku chigwa cha Yorodani.
and to pass to(wards) shoulder opposite [the] (Beth)-arabah north [to] and to go down [the] (Beth)-arabah [to]
19 Anabzolanso cha kumpoto kwa chitunda cha Beti-Hogila kukafika cha kumpoto ku gombe la Nyanja ya Mchere kumene mtsinje wa Yorodani umathirirako, cha kummwera kwenikweni. Awa anali malire a kummwera.
and to pass [the] border: boundary to(wards) shoulder Beth-hoglah Beth-hoglah north [to] (and to be outgoing *Q(K)*) [the] border: boundary to(wards) tongue: bar sea [the] Salt (Sea) north [to] to(wards) end [the] Jordan south [to] this border: boundary south
20 Yorodani ndiye anali malire a mbali ya kummawa. Awa anali malire a dziko limene mabanja a fuko la Benjamini analandira.
and [the] Jordan to border [obj] him to/for side east [to] this inheritance son: descendant/people Benjamin to/for border her around to/for family their
21 Mabanja a fuko la Benjamini anali ndi mizinda iyi; Yeriko, Beti-Hogila, Emeki Kezizi,
and to be [the] city to/for tribe son: descendant/people Benjamin to/for family their Jericho and Beth-hoglah Beth-hoglah and Emek (Emek)-keziz
22 Beti-Araba, Zemaraimu, Beteli
and Beth-arabah [the] Beth-arabah and (Mount) Zemaraim and Bethel Bethel
and [the] Avvim and [the] Parah and Ophrah
24 Kefari-Amoni, Ofini ndi Geba, mizinda khumi ndi awiri ndi midzi yake
and Chephar ([the] (Chephar)-ammoni *Q(K)*) and [the] Ophni and Geba city two ten and village their
25 Panalinso Gibiyoni, Rama, Beeroti,
Gibeon and [the] Ramah and Beeroth
and [the] Mizpeh and [the] Chephirah and [the] Mozah
27 Rekemu, Iripeeli, Tarala,
and Rekem and Irpeel and Taralah
28 Zera Haelefu, mzinda wa Ayebusi (ndiye kuti Yerusalemu) Gibeya ndi Kiriati, mizinda 14 ndi midzi yake. Limeneli ndilo dziko limene mabanja a fuko la Benjamini analandira kuti likhale lawo.
and Zela Haeleph and [the] Jebus he/she/it Jerusalem Gibeah Kiriath-jearim city four ten and village their this inheritance son: descendant/people Benjamin to/for family their