< Yoswa 12 >

1 Aisraeli anagonjetsa dziko lonse la kummawa kwa Yorodani, kuyambira ku chigwa cha Arinoni mpaka ku phiri la Herimoni pamodzi ndi dera lonse la kummawa kwa Araba. Iwo anatenga dzikoli kukhala lawo, ndipo mafumu a dzikoli anali awa:
La ngamakhosi amazwe anqotshwa ngabako-Israyeli njalo alezabelo ezathunjwa empumalanga yeJodani, kusukela eDongeni lwase-Arinoni kusiya entabeni yaseHemoni, okugoqela lonke icele langempumalanga ye-Arabha:
2 Sihoni mfumu ya Aamori, amene ankakhala mu Hesiboni. Iye analamulira kuyambira ku Aroeri mzinda umene uli mʼmphepete mwa mtsinje wa Arinoni, mpaka ku mtsinje wa Yaboki, umene uli mʼmalire mwa Aamori, kuphatikizanso theka la dziko la Giliyadi.
USihoni inkosi yama-Amori, wayebusa eHeshibhoni. Wayebusa kusukela e-Aroweri emaphethelweni oDonga lwase-Arinoni, kusukela phakathi laphakathi kodonga kusiyafika emfuleni uJabhoki, oyiwo umngcele wama-Amoni. Lokhu kwakugoqela ingxenye yeGiliyadi.
3 Iye ankalamuliranso dera la chigwa cha Yorodani kuyambira ku Nyanja ya Kinereti, kummawa ndi kumatsika mpaka ku Beti-Yesimoti, mzinda umene unali kummawa kwa Nyanja ya Mchere ndi kutsikabe kummwera mpaka pa tsinde pa phiri la Pisiga.
Wayebusa njalo empumalanga ye-Arabha kusukela olwandle lweKhinerethi kusiyafika olwandle lwe-Arabha (uLwandle lweTswayi) kusiya eBhethi-Jeshimothi, eningizimu phansanyana kwemithezuko yasePhisiga:
4 Ogi mfumu ya mzinda wa Basani, amene anali mmodzi mwa otsala mwa Arefaimu. Iye ankakhala ku Asiteroti ndi Ederi.
Lelizwe lika-Ogi inkosi yaseBhashani, omunye wamaRefayi okucina owayebusa e-Ashitharothi le-Edreyi.
5 Dera la ufumu wake linafika ku phiri la Herimoni, ku Saleka ndi dziko lonse la Basani mpaka ku malire ndi anthu a ku Gesuri Makati. Ufumu wake unaphatikizanso theka la Giliyadi mpaka ku malire a mfumu Sihoni ya ku Hesiboni.
Wabusa eNtabeni yaseHemoni, eSalekha, iBhashani yonke kusiya emngceleni wabantu beGeshuri leMahakhathi, lengxenye yeGiliyadi kusiya emngceleni kaSihoni inkosi yeHeshibhoni.
6 Mose mtumiki wa Yehova ndi Aisraeli anawagonjetsa ndipo anapereka dziko lawo kwa anthu a fuko la Rubeni, fuko la Gadi ndi theka la fuko la Manase kuti chikhale cholowa chawo.
UMosi inceku kaThixo, labako-Israyeli babanqoba. UMosi inceku kaThixo wanika ilizwe labo abakoRubheni labakoGadi lengxenye yesizwana sakoManase ukuthi libe ngelabo.
7 Yoswa ndi Aisraeli onse anagonjetsa mafumu onse okhala kumadzulo kwa mtsinje wa Yorodani kuyambira ku Baala-Gadi, ku chigwa cha Lebanoni mpaka ku phiri la Halaki, kumapita cha ku Seiri. Yoswa anagawira dzikolo mafuko a Israeli kuti likhale cholowa chawo.
La yiwo amakhosi elizwe lelo uJoshuwa labako-Israyeli abalithumbayo eceleni elisentshonalanga yeJodani, kusukela eBhali-Gadi esiGodini seLebhanoni kusiya eNtabeni yeHalakhi ekhangele eSeyiri (amazwe abo uJoshuwa wawanika njengelifa ezizwaneni zako-Israyeli kusiya ngezigaba zezizwana zabo,
8 Dziko limeneli linali dera la ku mapiri, chigwa cha kumadzulo, chigwa cha Yorodani, ku matsitso a kummawa, ndi dziko la chipululu la kummwera. Amene ankakhala mʼdzikoli anali Ahiti, Aamori, Akanaani, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi. Mafumu ake anali awa:
indawo elamaqaqa, amawatha asentshonalanga, i-Arabha, lemithezukweni yezintaba, inkangala leNegebi, amazwe amaHithi, ama-Amori, amaKhenani, amaPherizi, amaHivi, lamaJebusi): La ayengamakhosi:
9 mfumu ya Yeriko imodzi mfumu ya Ai (kufupi ndi Beteli imodzi
inkosi yeJerikho, eyodwa inkosi ye-Ayi (eduze leBhetheli), eyodwa
10 mfumu ya Yerusalemu imodzi mfumu ya Hebroni imodzi
inkosi yeJerusalema, eyodwa inkosi yeHebhroni, eyodwa
11 mfumu ya Yarimuti imodzi mfumu ya Lakisi imodzi
inkosi yeJamuthi, eyodwa inkosi yeLakhishi, eyodwa
12 mfumu ya Egiloni imodzi mfumu ya Gezeri imodzi
inkosi ye-Egiloni, eyodwa inkosi yeGezeri, eyodwa
13 mfumu ya Debri imodzi mfumu ya Gederi imodzi
inkosi yeDebhiri, eyodwa inkosi yeBhethi-Gaderi, eyodwa
14 mfumu ya Horima imodzi mfumu ya Aradi imodzi
inkosi yeHoma, eyodwa inkosi ye-Aradi, eyodwa
15 mfumu ya Libina imodzi mfumu ya Adulamu imodzi
inkosi yeLibhina, eyodwa inkosi ye-Adulami, eyodwa
16 mfumu ya Makeda imodzi mfumu ya Beteli imodzi
inkosi yeMakheda, eyodwa inkosi yeBhetheli, eyodwa
17 mfumu ya Tapuwa imodzi mfumu ya Heferi imodzi
inkosi yeThaphuwa, eyodwa inkosi yeHeferi, eyodwa
18 mfumu ya Afeki imodzi mfumu ya Lasaroni imodzi
inkosi ye-Afekhi, eyodwa inkosi yeLasharoni, eyodwa
19 mfumu ya Madoni imodzi mfumu ya Hazori imodzi
inkosi yeMadoni, eyodwa inkosi yeHazori, eyodwa
20 mfumu ya Simuroni Meroni imodzi mfumu ya Akisafu imodzi
inkosi yeShimron Meroni, eyodwa inkosi ye-Akhishafi, eyodwa
21 mfumu ya Taanaki imodzi mfumu ya Megido imodzi
inkosi yeThanakhi, eyodwa inkosi yeMegido, eyodwa
22 mfumu ya Kadesi imodzi mfumu ya Yokineamu ku Karimeli imodzi
inkosi yeKhedeshi, eyodwa inkosi yeJokhiniyamu eseKhameli, eyodwa
23 mfumu ya Dori ku Nafoti Dori imodzi mfumu ya Goyini ku Giligala imodzi
inkosi yeDori (eNafothi Dori), eyodwa inkosi yeGoyimi eseGiligali, eyodwa
24 mfumu ya Tiriza imodzi mafumu onse pamodzi analipo 31.
inkosi yeThiza, eyodwa. Amakhosi angamatshumi amathathu lanye esewonke.

< Yoswa 12 >