< Yoswa 10 >

1 Adoni-Zedeki mfumu ya ku Yerusalemu inamva kuti Yoswa wagonjetsa ndi kuwononga kotheratu mzinda wa Ai pamodzi ndi mfumu yake, monga anachitira ndi Yeriko ndi mfumu yake. Inamvanso kuti anthu a ku Gibiyoni anachita pangano la mtendere ndi Israeli ndipo amakhala pakati pawo.
Yelusaleme hina bagade amo Adounaisidege da Yosiua da Yeligou mugululi ea hina bagade fane legei amo defele A: iai mugululi, ea hina bagade medole legei, amo nabi dagoi. E da Gibione dunu da Isala: ili dunuma gousa: su hamone, ilia fi amo ganodini esala amola nabi.
2 Choncho iye ndi anthu ake anachita mantha aakulu, chifukwa Gibiyoni unali mzinda waukulu kwambiri, monga mzinda uliwonse wokhala ndi mfumu. Unali waukulu ndipo ankhondo ake anali olimba mtima.
Yelusaleme dunu fi da bagadewane beda: i. Bai Gibione da moilai bai bagade. Gibione da moilai huluane hina bagade gala amo defele galu. Ilia dadi gagui dunu da gasa bagade amola Gibione moilai ea defei da A: iai moilai defei baligiligai.
3 Chotsatira chake Adoni-Zedeki mfumu ya Yerusalemu inatuma uthenga kwa Hohamu mfumu ya Hebroni, Piramu mfumu ya Yarimuti, Yafiya mfumu ya Lakisi ndi Debri mfumu ya Egiloni.
Amaiba: le, Adounaisidege da Hibalone hina bagade Houha: me, Yamade hina bagade Ba: ila: me, La: igisi hina bagade Yafaia amola Egelone hina bagade Dibe ilima sia: adole iasi, amane,
4 Iye anatumiza mawu kuti, “Bwerani mudzandithandize kumenyana ndi Gibiyoni, chifukwa anthu ake achita pangano la mtendere ndi Yoswa ndi Aisraeli.”
“Nama fidila misa. Gibione moilai bai bagade dunu da Yosiua amola Isala: ili dunu ilima gousa: su hamoiba: le, na da Gibione doagala: musa: masunu.”
5 Mafumu asanu a Aamori aja, mfumu ya Yerusalemu, mfumu ya Hebroni, mfumu ya Yarimuti, mfumu ya Lakisi ndi mfumu ya Egiloni, anagwirizana. Iwo anasonkhanitsa ankhondo awo nazungulira mzinda wa Gibiyoni ndi kuwuthira nkhondo.
Amo A: moulaide hina bagade biyale gala amo Yelusaleme hina bagade, Yamade hina bagade, La: igisi hina bagade amola Egelone hina bagade, ilia da gilisili Gibione moilai bai bagade sisiga: le, doagala: i.
6 Koma anthu a ku Gibiyoni anatumiza uthenga kwa Yoswa ku misasa ya ku Giligala nati, “Musawataye anthu anu! Bwerani msanga mudzatipulumutse! Dzatithandizeni chifukwa mafumu a Aamori ochokera ku dziko la ku mapiri agwirizana kuti adzatithire nkhondo.”
Gibione dunu da Yosiua (Giliga: le abula moilaiga esalu) ema sia: adole iasi, “Nini mae fisima! Wahadafa nini gaga: la misa! Agolo sogega esala A: moulaide hina bagade huluane da gilisili ninima doagala: i dagoi.”
7 Choncho Yoswa ananyamuka kuchoka ku Giligala ndi gulu lake la ankhondo pamodzi ndi anthu ake olimba mtima.
Amaiba: le, Yosiua amola ea dadi gagui dunu huluane (noga: idafa dadi gagui amola da asi) da Giliga: le yolesi.
8 Yehova anati kwa Yoswa, “Usawaope, Ine ndawapereka mʼdzanja lako. Palibe ndi mmodzi mwa amenewa amene adzalimbe.”
Hina Gode da Yosiuama amane sia: i, “Ilima mae beda: ma. Na da dima hasalasu hou i dagoi. Dunu afae da dima bu gasawane gegemu hamedei ba: mu.”
9 Atayenda usiku wonse kuchokera ku Giligala, Yoswa anawathira nkhondo mwadzidzidzi.
Daeya wa: le ahoanoba hadigi, Yosiua amola ea dadi gagui dunu da Giliga: le fisili, Gibione moilai bai bagadega asi. Ilia da A: moulaide dunu ilima hedolowane doagala: loba, A:moulaide dunu da fofogadigi.
10 Yehova anachititsa mantha adani aja atangoona gulu lankhondo la Israeli. Choncho Aisraeli anagonjetsa Aamori ku Gibiyoni ndipo anawathamangitsa mu msewu wopita ku Beti-Horoni ndi kuwapha njira yonse yopita ku Azeka ndi Makeda.
Hina Gode da hamoiba: le, A:moulaide dunu da Isala: ili dadi gagui dunu ba: loba, bagade beda: iba: le hobea: i. Isala: ili dadi gagui da ili bagohame Gibione moilai bai bagadega medole legele, sefasi. Sefasili, ilia da goumi adobo logo amo Bede Houlone amoga sefasili, Asiga moilai amola Ma: gida moilaiga doaga: i.
11 Pamene ankathawa pamaso pa Israeli pa njira yochokera ku Beti-Horoni mpaka ku Azeka, Yehova anawagwetsera matalala akuluakulu kuchokera kumwamba ndipo ambiri mwa iwo anafa ndi matalala kuposa amene anaphedwa ndi lupanga la Israeli.
A: moulaide dunu da goumi logoga Isala: ili dadi gagui ilima hobeale ahoananoba, Hina Gode da hamoiba: le, gibu mugene da ilima sa: ili mae fisili Asiga ahoasu amoga sa: i. Amola mugene igi amoga medole legei idi da Isala: ili dunuga medole legei idi amo baligi dagoi.
12 Pa tsiku limene Yehova anapereka Aamori mʼmanja mwa Israeli, Yoswa ananena kwa Yehova pamaso pa Israeli kuti, “Iwe dzuwa, ima pamwamba pa Gibiyoni, mwezi ima pamwamba pa chigwa cha Ayaloni.”
Amo esoha Hina Gode da hamoiba: le, Isala: ili dunu da A: moulaide dunuma hasali. Amola amo esoha, Isala: ili dunu huluane ba: ma: ne, Yosiua da Hina Gode hamoma: ne amane sia: i, “Eso! Di Gibione moilaiga gadodili leloma. Oubi! Di A: iyalone Fago amoga gadodili leloma.”
13 Choncho dzuwa linayima, mwezinso unayima, mpaka dziko la Israeli litagonjetsa adani ake. Zimenezi zalembedwa mʼbuku la Yasari. Dzuwa linayima pamodzimodzi pakati pa thambo mlengalenga, osayendanso kwa tsiku lathunthu.
Amalalu, eso da mae asili, oulelu amola oubi da mae asili, oulelu. Isala: ili dunu da ilima ha lai hasali dagoiba: le fawane bu asi. Amo hou da Ya: isa buga ganodini dedei diala. Eso da mu dogoa amo ganodini lelu, eso afaega hame sa: i.
14 Sipanakhaleponso tsiku ngati limeneli kuyambira kale, tsiku limene Yehova anamvera munthu. Izi zinatero chifukwa Yehova ankamenyera nkhondo Aisraeli.
Amo hou amo Hina Gode da osobo bagade dunu ea sia: ne ba: su, musa: da hame ba: su amola fa: no amo hame ba: su. Hina Gode da Isala: ili fi fidima: ne gegei.
15 Kenaka Yoswa anabwerera pamodzi ndi Aisraeli onse ku misasa ku Giligala.
Amalalu, Yosiua amola ea dadi gagui dunu da Giliga: le abula diasu gilisisuga buhagi.
16 Mafumu asanu aja anathawa ndi kukabisala ku phanga la Makeda.
Be A: moulaide hina bagade biyale gala da hobeale, Ma: gida sogebi gele gelabo amo ganodini wamoaligi.
17 Koma Yoswa anamva kuti mafumu asanu awapeza akubisala ku phanga la Makeda.
Dunu eno da amo ba: i dagoi. Ilia wamoaligisu ilia da Yosiuama olelei.
18 Tsono Yoswa analamula kuti, “Mugubuduzire miyala ikuluikulu pa khomo la phangalo, ndipo muyike anthu ena kuti azilondera.
E amane sia: i, “Gele gelabo amo ea logo holei igi bagadega ga: sima. Ouligisu dunu amo logo ouligima: ne sia: ma.
19 Koma inu musakhaleko! Thamangitsani adani anu, muwathire nkhondo kuchokera kumbuyo ndipo musawalole kuti akafike ku mizinda yawo, pakuti Yehova Mulungu wanu wawapereka mʼmanja mwanu.”
Be dilia amogawi mae esaloma. Ninima ha lai amo sefasili ilia baligiga fane legema. Ilia moilai bai bagadega buhagimu logo hedofama. Dilia Hina Gode da fidibiba: le, dilia da amo dunu hasali dagoi.”
20 Kotero Yoswa ndi Aisraeli anapha anthu aja, kupatulapo ochepa amene anathawa nakabisala ku mizinda yawo.
Yosiua amola Isala: ili dunu da amo dunu fane legei dagoi. Be mogili da ilia moilai bai bagade gagoi amo ganodini hobeale, ilia hame fane legei.
21 Kenaka gulu lonse la ankhondo linabwerera bwinobwino kwa Yoswa ku misasa ya ku Makeda, palibe aliyense mu mzindamo amene anaputanso Aisraeli.
Amalalu, Yosiua ea dunu huluane da hahawane Ma: gida abula diasu gilisisuga bu misi. Amalalu, amo soge dunu huluane da beda: iba: le, Isala: ili dunuma lasogole sia: mu bagadewane beda: i galu.
22 Yoswa anati, “Tsekulani khomo la phangalo ndipo muwabweretse kwa ine mafumu asanuwo.”
Amalalu, Yosiua da amane sia: i, “Gele gelabo logo doasili, amo hina bagade biyale gala nama oule misa.”
23 Pamenepo mafumu asanu aja anatulutsidwa, mfumu ya ku Yerusalemu, mfumu ya ku Hebroni, mfumu ya ku Yarimuti, mfumu ya ku Lakisi, ndi mfumu ya ku Egiloni.
Amaiba: le, ilia da gele gelabo doasili, Yelusaleme, Hibalone, Yamade, La: igisi amola Egelone amoea hina bagade dunu gadili hiouginana asili,
24 Atabwera nawo kwa Yoswa, iye anayitana Aisraeli onse. Ndipo analamula akuluakulu ake amene anapita naye limodzi kuti, “Bwerani kuno ndipo apondeni pakhosi mafumuwa.”
Yosiuama oule misi. Amalalu, Yosiua da Isala: ili dunu huluane amola dadi gagui ouligisu dunu huluane da e sigi asi, amo ilia emo amo hina bagade dunu ilia gonomagi da: iya osa: la heda: ma: ne sia: i. Ilia amo hamoi dagoi.
25 Yoswa anawawuza kuti, “Musaope kapena kutaya mtima. Khalani amphamvu ndi olimba mtima popeza umo ndi mmene Yehova adzachitire ndi adani anu onse amene mudzamenyana nawo.”
Amalalu, Yosiua da ea dadi gagui hina dunuma amane sia: i, “Dilia mae beda: ma mae da: i dioma. Gasa bagadewane amola hahawane hamoma. Bai Hina Gode da dilima ha lai dunu huluane ninia wali hamoi defele hamomu.”
26 Kenaka Yoswa anawabaya ndi kuwapha mafumuwo ndipo anawapachika pa mitengo isanu ndipo anakhala pamenepo mpaka madzulo.
Amalalu, Yosiua da amo hina bagade biyale gala medole legele, ilia da: i hodo ifa biyale gala amoga hegoa: nesi. Ilia da amogawi hegoa: nesili dialu, eso dabe galu bu lai.
27 Dzuwa litalowa, Yoswa analamula kuti awachotse pa mitengo ija ndi kuwaponya mʼphanga limene ankabisalamo. Pa khomo pa phangalo anayikapo miyala ikuluikulu imene ilipo mpaka lero.
Eso dabe amoga Yosiua da sia: beba: le, ilia da hina bagade dunu amo ilia da: i hodo ifaga fadegale, gele gelabo amo ganodini musa: hina bagade da wamoaligi amoga ha: digi. Ilia da gele bagade bagohame amoga gele gelabo ea logo holeiga dedeboi. Amo gele da wali eso amaiwane diala.
28 Tsiku lomwelo Yoswa analanda mzinda wa Makeda. Iye anapha anthu a mu mzindamo ndi mfumu yake ndipo sanasiye aliyense wamoyo. Yoswa anachita ndi mfumu ya ku Makeda monga anachitira ndi mfumu ya Yeriko.
Yosiua da amo esoga, Ma: gida moilai bai bagade amola ea hina bagade doagala: le, fedele lai. Dunu huluane amo ganodini esalu e da medole legei. Dunu afae esalebe hame ba: i. E da Yeligou hina bagade ema hamoi defele, Ma: gida hina bagadema hamoi.
29 Kenaka Yoswa ndi Aisraeli onse anapitirira kuchokera ku Makeda nakafika ku Libina ndi kuthira nkhondo mzindawo.
Amalalu, Yosiua amola ea dadi gagui dunu da Ma: gida fisili, Libina moilai bai bagadega doagala: i.
30 Yehova anaperekanso mzindawo ndi mfumu yake mʼmanja mwa Aisraeli. Ndipo Yoswa anapha onse amene anali mu mzindamo. Palibe amene anatsala wamoyo. Ndipo Yoswa anachita ndi mfumu ya Libina monga anachitira ndi mfumu ya Yeriko.
Hina Gode da fidibiba: le, Isala: ili dunu da amo moilai amola ea hina bagade hasali. Ilia dunu afae amoma hame asigiwane, huludafa fane legei. Ilia da Yeligou hina bagade ema hamoi amo defele Libina hina bagadema hamoi dagoi.
31 Kenaka Yoswa ndi Aisraeli onse anapitirira kuchokera ku Libina kupita ku Lakisi. Iye anazungulira mzindawo ndi kuwuthira nkhondo.
Amalalu, Yosiua da Libina fisili, La: igisi moilai bai bagade amo sisiga: le, doagala: i.
32 Yehova anapereka Lakisi kwa Israeli; ndipo Yoswa anawulanda pa tsiku lachiwiri. Monga anachita ndi mzinda wa Libina, Yoswa anapha anthu onse okhala mu mzinda wa Lakisi, ndipo palibe amene anatsala ndi moyo.
Eso ageyaduga, Hina Gode da fidibiba: le, Isala: ili dunu da La: igisi hasali. Ilia da Libina amoga hamoi defele dunu afae moilai ganodini amoma hame asigiwane, huludafa fane legei.
33 Nthawi imeneyi nʼkuti Horamu mfumu ya Gezeri itabwera kudzathandiza Lakisi koma Yoswa anamugonjetsa pamodzi ndi asilikali ake ndipo palibe anatsala wamoyo.
Houla: me (Gise moilai bai bagade hina bagade) da La: igisi dunu fidimusa: misi, be Yosiua da e amola ea dadi gagui dunu hasali. Dunu afae esalebe hame ba: i.
34 Kenaka Yoswa ndi Aisraeli onse anapitirira kuchokera ku Lakisi nakafika ku Egiloni. Iwo anazungulira mzindawo ndi kuwuthira nkhondo.
Amalalu, Yosiua amola ea dadi gagui dunu da La: igisi fisili, Egelone moilaiga asili, amo moilai sisiga: le, doagala: i.
35 Anawulanda tsiku lomwelo ndipo anapha aliyense amene anali mu mzindawo monga momwe anachitira ku Lakisi.
Amo eso afaega ilia da moilai lai. Ilia da La: igisi fi ilima hamoi defele, dunu huluanedafa medole legei.
36 Kenaka Yoswa ndi Aisraeli onse anachoka ku Egiloni nakafika ku Hebroni ndi kukawuthira nkhondo.
Amalalu, Yosiua amola ea dadi gagui dunu da Egelone moilai fisili, agolo sogega asili, Hibalone moilai bai bagadega doagala: i.
37 Iwo analanda mzindawo napha ndi lupanga mfumu yake pamodzi ndi onse amene ankakhala mʼmenemo. Monga anachita ndi mzinda wa Egiloni, kuti sanasiye aliyense ndi moyo, anachitanso chimodzimodzi ndi mzinda wa Hebroni.
Ilia da Hibalone lale, amo hina bagade dunu, amogai esalebe dunu huluane amola dunu huluane moilai sisiga: le ganodini esalu, medole legei. Yosiua ea sia: beba: le, ilia da Egelone moilai amoma hamoi defele, amo moilai gugunufinisi. Dunu afae amo ganodini esalebe hame ba: i.
38 Pambuyo pake Yoswa ndi Aisraeli onse anatembenukira mzinda wa Debri ndi kukawuthira nkhondo.
Amalalu, Yosiua amola ea dadi gagui da sinidigili, Dibe moilaiga doagala: i.
39 Iwo analanda mzindawo ndi midzi ndi kupha mfumu yake pamodzi ndi onse okhala mʼmenemo. Anachita ndi mzinda wa Debri pamodzi ndi mfumu yake zofanana ndi zimene anachita ndi mzinda wa Libina ndi wa Hebroni.
E da amo moilai, ea hina bagade amola dunu huluane moilale sisiga: le dialu amo ganodini esalu lai dagoi. Yosiua da Hibalone, Libina amola ela hina bagade dunu ilima hamoi defele, e da Dibe amola ea hina bagade amoma hamoi. E da ilia dunu huluane medole legei dagoi.
40 Motero Yoswa anagonjetsa dziko lonselo. Anapha mafumu onse a dera la kumapiri, dera la kummawa, dera la kumadzulo mʼmphepete mwa phiri, ndiponso dera la ku magomo, kummwera. Iye sanasiye wina aliyense wamoyo. Anapha onse amene anali moyo monga momwe Yehova Mulungu wa Israeli analamulira.
Yosiua da soge huluane hasali. E da hina bagade huluane, amo agolo soge hina bagade, eso mabadi soge hina bagade, eso dabe agolo fonobahadi hina bagade amola hafoga: i soge ga (south) dialebe hina bagade huluane fane legei. E da dunu huludafa medole legei dagoi. Bai Isala: ili Hina Gode da amo hamoma: ne sia: beba: le.
41 Yoswa anawagonjetsa iwo kuyambira ku Kadesi Barinea mpaka ku Gaza, ndiponso kuchokera ku chigawo chonse cha Goseni mpaka ku Gibiyoni.
Yosiua da soge huluane lai. Amo da ga (south) Ga: idese Bania asili Ga: isa (amo da wayabo bagade bega: ), Gousiene soge huluane ga (north) asili, Gibione moilai bai bagadega doaga: i.
42 Yoswa anagonjetsa mafumu onsewa ndi kulanda dziko lawo kamodzinʼkamodzi chifukwa Yehova Mulungu wa Israeli anawamenyera nkhondo.
Isala: ili Hina Gode da ili fidimusa: gegeiba: le, Yosiua da amo hina bagade amola ilia soge huluane hasali dagoi.
43 Pambuyo pake Yoswa ndi Aisraeli onse anabwerera ku misasa yawo ku Giligala.
Amalalu, Yosiua amola ea dadi gagui dunu da Giliga: le abula diasu gilisisuga buhagi.

< Yoswa 10 >