< Yona 2 >

1 Yona ali mʼmimba mwa chinsomba chija anapemphera kwa Yehova Mulungu wake.
Yunusee baluğne vuxhnenang'a cune Rəbbis Allahıs inəxübna düə haa'a:
2 Iye anati: “Pamene ndinali mʼmavuto anga ndinayitana Yehova, ndipo Iye anandiyankha. Ndili ku dziko la anthu akufa ndinapempha thandizo, ndipo Inu munamva kulira kwanga. (Sheol h7585)
Rəbb, zı dağamiyvalenang'a Valqa onu'u, Ğunad alidghıniy quvuyn. Zı ahaleençe ts'ir hav'u, Vak'le yizda ts'ir g'avxhuna. (Sheol h7585)
3 Munandiponya mʼnyanja yozama, mʼkati mwenimweni mwa nyanja, ndipo madzi oyenda anandizungulira; mafunde anu onse ndi mkokomo wake zinandimiza.
Ğu zı deryahne k'oralybışeeqa g'uvorxhul, Zı xhyanbışde yı'q'nee axu, Yiğın gırgın xhyanbıyiy dalğabı Zal ooğançe ılğeeç'u.
4 Ndinati, ‘Ine ndachotsedwa pamaso panu; komabe ndidzayangʼananso ku Nyumba yanu yopatulika.’
Manke zı uvhuyn: «Ğu zı Vake əq'əna qı'ı, Meed zak'le Yiğın muq'addasın xav İyerusalimee g'acesıncad».
5 Madzi wondimiza anandichititsa mantha, nyanja yozama inandizungulira; udzu wa mʼmadzi zinakuta mutu wanga.
Nafas əlyhəəsme xhyanbı zalqa qadı, K'oralybışeeqa qıkkı, Vuk'lelqad xavsiy alitk'ır.
6 Ndinatsikira kunsi ndithu, mʼtsinde mwa mapiri; mipiringidzo ya dziko inanditsekereza kosatha. Koma Inu munatulutsa moyo wanga mʼmandamo, Inu Yehova Mulungu wanga.
Suvabışde avqamee zı giç'una, İttehesu Ğu dunyeyn akkabı zal oğa it'umetxha. Ğumee yizda Rəbb Allah Yizın tan k'oralybışeençe g'attixhan hı'iyn.
7 “Pamene moyo wanga umachoka mwa ine, ine ndinakumbukira Inu Yehova, ndipo pemphero langa linafika kwa inu, ku Nyumba yanu yopatulika.
Yizda ı'mı'r k'yabat'amee, Zı Rəbb yik'el qali'ı, Yizda düə Valqa, Yiğne muq'addas xaalqa hipxhırna.
8 “Iwo amene amagwiritsitsa mafano achabechabe amataya chisomo chawo.
Şavaayiy nişiscad karaı'dəəne bütbışis ı'bəədat ha'a, Manbışe Ğu yik'el hixan ha'a, Colqana rəhı'm avaak'an haa'a.
9 Koma ine ndidzapereka kwa Inu nsembe ndikuyimba nyimbo yamayamiko. Chimene ndinalonjeza ndidzachikwaniritsa. Chipulumutso chimachokera kwa Yehova.”
Zımee şukur haa'ane mə'niybışika Vas q'urbanbı allya'as. Zı huvuyn cuvab cigeeqa qalya'asın. G'attivxhan haa'ana sa Rəbb Vuc vorna!
10 Ndipo Yehova analamula chinsomba chija, ndipo chinakamusanza Yonayo mʼmbali mwa nyanja.
Rəbbee baluğuk'le uvhuyng'a, mançin Yunus ghalençe xhyan deşde cigeeqa qığayhe.

< Yona 2 >