< Yohane 9 >

1 Iye akuyendabe, anaona munthu wosaona chibadwire.
Kane oyudo owuotho odhi, noneno ngʼat moro mane osebedo muofu nyaka aa nywolne.
2 Ophunzira ake anamufunsa Iye kuti, “Rabi anachimwa ndani, munthuyu kapena makolo ake, kuti iye abadwe wosaona?”
Jopuonjre nopenje niya, “Rabi, en ngʼa ma notimo richo; ngʼatni koso jonywolne, momiyo nonywole muofu?”
3 Yesu anayankha kuti, “Sikuti iyeyu anachimwa kapena makolo ake, koma izi zinachitika kuti Mulungu aonetse ntchito zake mwa iyeyu.
Yesu nodwokogi niya, “Ngʼatni kata jonywolne ne ok otimo richo, to ma notimore mondo teko mar Nyasaye onenre e changne.
4 Ife tiyenera kugwira ntchito za Iye amene anandituma kukanali masana. Usiku ukubwera, pamene wina aliyense sadzagwira ntchito.
Nyaka wati tije mag Jal mane oora ka pod piny odiechiengʼ, nikech otieno biro maonge ngʼama nyalo tiyo.
5 Pamene Ine ndili mʼdziko lapansi, Ine ndine kuwunika kwa dziko lapansi.”
Ka pod an e piny, to an e ler mar piny.”
6 Atanena izi, Iye anathira malovu pansi ndi kukanda dothi, napaka matopewo mʼmaso a munthuyo.
Kane osewacho kamano, nongʼudho olawo piny, mi olosogo chwodho, kaeto oketo e wangʼ ngʼatno.
7 Yesu anamuwuza iye kuti, “Pita kasambe mʼdziwe la Siloamu” (mawu awa akutanthauza Wotumidwa). Choncho munthuyo anapita ndi kukasamba ndipo anabwerako akupenya.
Eka nowachone ngʼatno niya, “Dhiyo ilwok wangʼi e yawo mar Siloam” (tiende ni “Ote”). Omiyo ngʼatno nodhi moluoko wangʼe, kendo noduogo dala koneno.
8 Anzake ndi iwo amene anamuona iye poyamba akupempha anafunsa kuti, “Kodi uyu si munthu amene amapemphapempha uja?”
Jogwengʼ-gi gi joma nosenene motelo kokwecho nopenjo niya, “Donge ma e ngʼat mosebedo kakwechocha?”
9 Ena ananena kuti anali yemweyo. Ena anati, “Ayi, sakuoneka ngati yemweyo.” Koma iye mwini ananenetsa kuti, “Munthuyo ndine.”
Jomoko kuomgi nowacho ni mano en. Ji mamoko to nowacho niya, “Ooyo, ngʼatni chal mana kode.” Ngʼatno owuon to nowacho koramo niya, “En mana an.”
10 Iwo anafunsitsa kuti, “Kodi nanga maso ako anatsekuka bwanji?”
Negimedo penje niya, “Ka en kamano, to wengeni nokelo yawore nade?”
11 Iye anayankha kuti, “Munthu wina wotchedwa Yesu anakanda dothi ndi kupaka mʼmaso anga. Iye anandiwuza kuti ndipite ku Siloamu ndi kukasamba. Choncho ndinapita kukasamba, ndipo ndikuona.”
Nodwokogi niya, “Ngʼat miluongo ni Yesu noloso chwodho moro bangʼe oketo chwodhono e wengena. Nonyisa ni adhi Siloam aluok wangʼa, kendo ne adhi mi aluoko wangʼa, bangʼe ne aneno.”
12 Iwo anamufunsa iye kuti, “Ali kuti munthu ameneyu?” Iye anati, “Ine sindikudziwa.”
Negipenje niya, “Ere ngʼatno?” To nodwokogi niya, “Ok angʼeyo kuma entiere.”
13 Iwo anabwera naye munthu amene poyamba anali wosaona kwa Afarisi.
Ne gitero ngʼat machon ne muofuno ir jo-Farisai.
14 Tsono linali la Sabata tsiku limene Yesu anakanda dothi ndi kutsekula maso a munthuyu.
To chiengʼ mane Yesu olose chwodho kendo ochango wangʼ muofuno ne en chiengʼ Sabato.
15 Choncho Afarisi anamufunsanso iye momwe analandirira kuona kwake. Munthuyo anayankha kuti, “Iye anapaka matope mʼmaso anga, ndipo ine ndinakasamba, ndipo ndikuona.”
Omiyo jo-Farisai nopenje kaka nokelo neno. To ngʼatno nodwokogi niya, “Nende oketo chwodho e wengena, bangʼe aluoko mi koro aneno.”
16 Ena a Afarisi anati, “Munthu uyu siwochokera kwa Mulungu, pakuti sasunga Sabata.” Koma enanso anafunsa kuti, “Kodi munthu wochimwa angachite bwanji zizindikiro zodabwitsa ngati izi?” Choncho iwo anagawanika.
Moko kuom jo-Farisaigo nowacho niya, “Ngʼatni ok oa kuom Nyasaye, nimar ok orito Sabato.” Ji mamoko to nopenjo niya, “Ere kaka ngʼama jaricho nyalo timo tim hono machal kama?” Omiyo ne gipogore e kindgi giwegi.
17 Pomaliza iwo anatembenukiranso kwa munthu amene anali wosaona uja nati, “Kodi iwe unena chiyani za Iye poti ndi maso ako amene watsekula?” Munthuyo anayankha kuti, “Iye ndi mneneri.”
Eka negichako gidonjore gi muofuno, mi gipenje niya, “In manende ochangi, to iwacho angʼo kuome?” Ngʼatno nodwokogi niya, “En janabi.”
18 Ayuda sanakhulupirirebe kuti iye anali wosaona ndi kuti anayamba kuona kufikira atayitana makolo ake.
To jo-Yahudi ne pod ok oyie ni ngʼatni nonywol ka en muofu, kendo ni wengene noseyawore, nyaka negioro wach mondo oluong jonywol ngʼatno.
19 Iwo anafunsa kuti, “Kodi uyu ndi mwana wanu? Kodi iyeyu ndi amene mukunena kuti anabadwa wosaona? Nanga zikutheka bwanji kuti akuona?”
Ne gipenjogi niya, “Bende ngʼatni e wuodu ma uwacho ni nonywol muofu? Obet nade ni koro onyalo neno?”
20 Makolo anayankha kuti, “Ife tikudziwa kuti ndi mwana wathu, ndipo tikudziwa kuti anabadwa wosaona.
Jonywolgo nodwokogi niya, “Wangʼeyo ni ma en wuodwa, kendo wangʼeyo ni nonywole muofu.
21 Koma sitidziwa zimene zachitika kuti tsopano azipenya. Amenenso wamupenyetsa sitikumudziwa. Mufunseni ndi wamkulu; iye adziyankhira yekha.”
To kaka koro onyalo neno sani, kata ngʼama noyawo wengene, to wakia. Penjeuru, tinde oduongʼ. Obiro wacho wach kuome owuon.”
22 Makolo ake ananena izi chifukwa amaopa Ayuda, popeza Ayuda anatsimikiza kale kuti aliyense amene adzamuvomereza Yesu kuti anali Khristu adzatulutsidwa mʼsunagoge.
Jonywolne nowacho kamano nikech negiluoro jo-Yahudi, nimar noyudo jo-Yahudi osengʼado wach ni ngʼato angʼata ma nohul ni Yesu en Kristo ne ibiro riembi e sinagogi.
23 Ichi ndi chifukwa chake makolo ake anati, “Mufunseni iye ndi wamkulu.”
Mano emomiyo jonywolne nowacho niya, “Tinde oduongʼ, penjeuru.”
24 Iwo anamuyitanitsa kachiwiri munthu amene anali wosaonayo. Iwo anati, “Lemekeza Mulungu. Ife tikudziwa kuti munthu uyu ndi wochimwa.”
Negichako giluongo ngʼat ma nonywol ka en muofuno mi gikone niya, “Wach adier e nyim Nyasaye! Wan wangʼeyo ni ngʼatni en jaricho.”
25 Iye anayankha kuti, “Zakuti Iye ndi wochimwa kapena ayi, ine sindikudziwa. Ine ndikudziwa chinthu chimodzi. Ndinali wosaona koma tsopano ndikuona!”
Nodwokogi niya, “An akia kata ka en jaricho kata ka ok en. Gimoro achiel kende ema angʼeyo: Ni chon ne an muofu, to sani koro aneno!”
26 Kenaka anamufunsa kuti, “Kodi Iye anachita chiyani kwa iwe? Iye anatsekula motani maso ako?”
Eka negipenje niya, “Angʼo ma notimoni ma wangʼi oneno? Ere kaka noyawo wengeni?”
27 Iye anayankha kuti, “Ine ndakuwuzani kale ndipo inu simunamvetsetse. Chifukwa chiyani mukufuna mumvenso? Mukufuna kuti inu mukhale ophunzira akenso?”
Nodwokogi niya, “Donge ne asenyisou, to ok uyie. Udwaro winje kendo nangʼo? Koso un bende udwaro doko jopuonjrene?”
28 Pamenepo anamunyoza ndipo anati, “Iwe ndiye ophunzira wa munthuyu! Ife ndife ophunzira a Mose!
Kuom mano, ne giyanye mangʼeny kagiwacho niya, “In e japuonjrene! Wan to wan jopuonjre Musa.
29 Ife tikudziwa kuti Mulungu anayankhula kwa Mose, koma za munthu uyu, ife sitikudziwa ngakhale kumene akuchokera.”
Wangʼeyo ni Nyasaye nowuoyo gi Musa, to ngʼatni to wakia kata mana kuma oaye.”
30 Munthuyo anayankha kuti, “Tsopano izi ndi zodabwitsa! Inu simukudziwa kumene akuchokera, komabe iye watsekula maso anga.
Ngʼatno nodwokogi niya, “Mano en wach miwuoro! Ukia kuma oaye to en ema noyawo wengena?
31 Ife tikudziwa kuti Mulungu samvera wochimwa. Iye amamvera munthu woopa Mulungu amene amachita chifuniro chake.
Wangʼeyo ni Nyasaye ok winj jaricho. Owinjo mana ngʼatno matimo dwarone.
32 Palibe amene anamvapo za kutsekula maso a munthu wobadwa wosaona. (aiōn g165)
Nyaka nene pok nowinji ngʼat moyawo wangʼ ngʼat mane onywol ka en muofu. (aiōn g165)
33 Ngati munthu uyu akanakhala wosachokera kwa Mulungu, palibe chimene Iye akanachita.”
Ka dine bed ni ngʼatni ok noa kuom Nyasaye, to ok dine otimo gimoro.”
34 Pamenepo anayankha kuti, “Iwe unabadwa mu uchimo kotheratu; bwanji ukuyesa kutiphunzitsa ife!” Ndipo anamutulutsa kunja.
Omiyo negidwoke niya, “In nonywoli e chuny richo, koro ere kaka inyalo bukori ni ipuonjowa!” Bangʼ mano negiriembe oko.
35 Yesu anamva kuti anamutulutsa kunja ndipo pamene anamupeza anati, “Kodi ukukhulupirira Mwana wa Munthu?”
Yesu nowinjo ni ne oseriemb ngʼatno oko, omiyo kane oyude, nopenje niya, “Bende iyie kuom Wuod Dhano?”
36 Munthuyo anafunsa kuti, “Kodi, Ambuye, ameneyo ndi ndani? Ndiwuzeni kuti ndimukhulupirire Iye?”
Ngʼatno nopenjo niya, “Jaduongʼ, Wuod Dhano to en ngʼa? Nyisago mondo ayie kuome.”
37 Yesu anati, “Iwe wamuona tsopano. Zoonadi ndiye amene akuyankhula nawe.”
Yesu nodwoke niya, “Eri koro isenene; kendo en ema owuoyo kodini.”
38 Pamenepo munthuyo anati, “Ambuye, ndikukhulupirira,” ndipo anamulambira Iye.
Ngʼatno nowachone niya, “Ruoth, ayie,” kendo nolame.
39 Yesu anati, “Ndinabwera pansi pano kudzaweruza kuti osaona aone ndi openya asaone.”
Eka Yesu nowacho niya, “Asebiro e piny mondo angʼadne bura, mondo joma muofni onen, to joma neno olokre muofni.”
40 Afarisi ena amene anali pafupi naye anamva akunena izi ndipo anafunsa kuti, “Chiyani? Kodi ndife osaonanso?”
Jo-Farisai moko mane ni kode nowinje kowacho kamano mi openje niya, “Iwacho angʼono? Kare wan bende wan muofni?”
41 Yesu anati, “Mukanakhala osaona, simukanachimwa; koma tsopano popeza mukuti mumaona, ndinu ochimwabe.”
Yesu nowachonegi niya, “Ka dine bed ni un muofni, to dine ok ubedo joketho nikech richo; to nikech uketoru ni uneno, koro kethou osiko.”

< Yohane 9 >