< Yohane 8 >
1 Koma Yesu anapita ku phiri la Olivi.
Vbvrikunamv nyichar mvnwngngv naam bv vngnya toku, vbvritola Jisu Olib Moodw bv chaatoku.
2 Mmamawa Iye anaonekeranso ku Nyumba ya Mulungu kumene anthu onse anamuzungulira ndipo Iye anakhala pansi nawaphunzitsa.
Alu logonvgv arukamchibv nw Pwknvyarnvnaam bv vngkur toku. Nyi mvnwngngv vngkumla ninyia vngyumto, okv nw dootung tvvla bunua tamsar sarrap toku.
3 Aphunzitsi amalamulo ndi Afarisi anabweretsa mkazi amene anagwidwa akuchita chigololo. Iwo anamuyimiritsa patsogolo pa anthu ndipo
Pvbv tamsarnv vdwv okv Parisis vdwv nyimv ako yoomur nvgo naatungla boolwk nyato, okv bunu nyimv nvnga mvnwng gv kaagialo dakmuto.
4 anati kwa Yesu, “Aphunzitsi, mkazi uyu tinamugwira akuchita chigololo.
Bunu Jisunyi minto, “Tamsarnv, so nyimv angv yoomurla rila donv nga naatung pvnv.
5 Mʼmalamulo a Mose anatilamulira kuti akazi otere tiwagende ndi miyala. Tsopano Inu mukuti chiyani?”
Ngonugv Pvbv lo Moses gamkito svkvnv nyimv nga vlwngngv orkidubv. Vjak, no ogu vla mindunv?”
6 Iwo anagwiritsa ntchito funsoli ngati msampha, ndi cholinga choti apeze chifukwa cha kumuneneza Iye. Koma Yesu anawerama pansi ndi kuyamba kulemba pa dothi ndi chala chake.
Bunugv svbv minam si Jisunyi minkup gvrila gungnying lwkdubv vla minto. Vbvritola hv dumpo bawng gvrila ninyigv lakching lokv kvdwlo akor lvkminla dooyasuto.
7 Pamene iwo anapitirira kumufunsa, Iye anaweramuka ndipo anawawuza kuti, “Ngati wina wa inu alipo wopanda tchimo, ayambe iyeyo kumugenda ndi miyala mkaziyu.”
Bunu hoka daktola ninyia tvula tvvka dvdvnyato, hv mvngrwpala yikula baarapla bunua minto, “Nonu gv lokv akonv yvvla rimur rima pvnv hv ninyia vlwng orcholaka.”
8 Iye anaweramanso pansi ndi kulemba pa dothi.
Vbvrikunamv nw lvkodv dumpo bawng gvrila kvdw lo lvkminto.
9 Iwo atamva izi anayamba kuchoka mmodzimmodzi, akuluakulu poyamba, mpaka Yesu anatsala yekha ndi mkaziyo atayimirira pomwepo.
Vdwlo bunu sum tvvtokudw, bunu abwngyachok v vngcho gvlaila akin akinbv mvnwngngv vngyu nyatoku. Jisunyi akin dookubv okv nyimv nvngaka hoka dakbwng dubv bunu vngyu nyatoku.
10 Yesu anaweramuka ndipo anamufunsa iye kuti, “Akuluakulu aja ali kuti? Kodi palibe amene wakutsutsa?”
Hv atubongv mvngrw laila baarapla nyimv anga tvvkato, “Ogolo bunu? Nam miakaya jinv akoka dooku mai?”
11 Iye anati, “Ambuye, palibe ndi mmodzi yemwe.” “Inenso sindikukutsutsa iwe. Pita kuyambira tsopano usakachimwenso.”
Nw mirwksito, “Tamsarnv,” akoka dookuma. Vbvrikunamv, alvdo, Jisu minto, “Ngo ka nam miakaya madunv. Vngnyikuka, vbvritola lvkodv rimur kumabvka.”
12 Yesu atayankhulanso kwa anthu, anati, “Ine ndine kuwunika kwa dziko lapansi. Aliyense amene anditsata Ine sadzayenda mu mdima, koma adzakhala ndi kuwala kotsogolera anthu ku moyo.”
Jisu Parisis vdwa lvkodv mindvto. Nw minto, “Ngo nyiamooku gv loung ngv, yvvdw nga vngming gvdunv hv singnamlo loung yayabv rire okv vdwloka kanv arwnglo vngkar mare.”
13 Afarisi anamutsutsa Iye nati, “Iwe ukudzichitira umboni wa Iwe mwini, umboni wako siwoona.”
Parisis vdwv ninyia minto, “Vjak no atubogv lvgabv minsudo; no ogugo mindudw anyung kaama.”
14 Yesu anayankha kuti, “Ngakhale Ine ndidzichitire umboni, umboni wangawu ndi woona, pakuti Ine ndikudziwa kumene ndinachokera ndi kumene ndikupita. Koma inu simukudziwa ndi pangʼono pomwe kumene ndinachokera kapena kumene ndikupita.
Jisu mirwksito, “Ma, ngo atubogv lvkwng nga minsu jvka, ngo ogugo mindudw hv jvjv ngv, ogulvgavbolo ngo chinsudo ngo ogolokv aapvnvdw okv ngo ogolo vngtv tvdunvdw. Nonu chima ngo ogolokv aapvnvdw vmalo ngo ogolo vngtv tvdunvdw.
15 Inu mumaweruza potsata maganizo a anthu chabe. Ine sindiweruza munthu wina aliyense.
Nonu ngam nyi adwnayak lokv chingching bv jwngkadakado; ngo yvvnyika jwngkadaka mapvnv.
16 Koma Ine ndikati ndiweruze, ndimaweruza molondola, chifukwa Ine sindili ndekha koma ndili ndi Atate amene anandituma.
Vbvritola ngo vbvrinam gubv rinv guilo, ngoogv jwngkadaka namv jvjvre, ogulvgavbolo so ngo akin mwngma; ngam vngmunv Abu ka ngam lvkobv reming gvdu.
17 Mʼmalamulo anu munalembedwa kuti umboni wa anthu awiri ndi wovomerezeka.
So si nonugv Pvbv lo lvkpv vdwlo kayatayanv anyi gonv tolwk minsu bolo, bunu ogugo minpvdw hv jvjv ngv,
18 Ine ndikudzichitira ndekha umboni; ndipo mboni inanso ndi Atate amene anandituma.”
Ngo atubogv lvgabv minsudo okv ngam vngmunv Abu ka ngoogv lvgabv mindvdo.”
19 Kenaka iwo anamufunsa Iye kuti, “Kodi Atate anuwo ali kuti?” Yesu anayankha kuti, “Inu simundidziwa Ine. Atate anganso simuwadziwa. Mukanandidziwa Ine, mukanawadziwanso Atate anga.”
Bunu tvvkato, “Ogolo no gv abu?” Jisu mirwksito, “Nonu ngamla ngoogv Abu nyika chima, nonu ngam chinv guilo, ngoogv Abu nyika nonu chinre.”
20 Iye anayankhula mawu awa pamene amaphunzitsa Nyumba ya Mulungu pafupi ndi malo amene amaponyapo zopereka. Komabe palibe amene anamugwira Iye, chifukwa nthawi yake inali isanakwane.
Jisu so mvnwngnga minto, Pwknvyarnvnaam lo karchung arwng lo morko lwkku jampa vvpvku hoka ninyigv tamsar sarnam aingbv. Okv yvvka ninyia naatung mato, ogulvgavbolo ninyigv dw ngv aatv madvto.
21 Kenakanso Yesu anawawuza kuti, “Ine ndikupita, ndipo mudzandifunafuna, koma mudzafa muli mʼmachimo anu. Kumene ndikupita, inu simungabwereko.”
Jisu lvkodv bunua minto, “Ngo vngro reku: nonu ngam kaakar reku, vbvritola nonu nonugv rimurlo silwk reku. Nonu vngnyu mare ngoogv vngkulo.”
22 Izi zinachititsa Ayuda kufunsa kuti, “Kodi adzadzipha yekha? Kodi ndicho chifukwa chake akuti, ‘Kumene ndikupita, inu simungabwereko?’”
Jius nyi kainv vdwv minto, “Hv mindu ninyigv vngjikolo ngonu vngnyu mare vla. Svbv minam si hv atubongv mvki sidubv mindu nvgo bri?”
23 Koma Iye anapitiriza kuti, “Inu ndi ochokera pansi pano. Ine ndine wochokera kumwamba. Inu ndinu anthu a dziko la pansi. Ine sindine wa dziko lapansi lino.
Jisu mirwkto, “Nonu so lvkwng gv Sichingmooku so gvngv, vbvritola ngo ao tolokv inv ngv. Nonu so Sichingmooku so gvngv, vbvritola ngo so Sichingmooku gvngvma.
24 Ine ndinakuwuzani kuti mudzafera mʼmachimo anu ngati simukhulupirira kuti Ine Ndine. Ndithu inu mudzafera mʼmachimo anu.”
Vkvlvgabv ngo nonua minpa pvkunv nonuno silwkre nonugv rimurlo. Okv nonu sireku nonugv rimurlo vdwlo nonu ‘Ngo Yvvkudw Ngo’ um nonu mvngjwng maridw.”
25 Iwo anafunsa kuti, “Ndinu ndani?” Yesu anayankha kuti, “Monga Ine ndakhala ndikunena nthawi yonseyi,
Bunu tvvkato, “No yvvla?” Jisu mirwksito, “Atuk lokv ngo nonua ogugo minpvdw.
26 ndili ndi zambiri zoti ndinene zoweruza inu. Koma Iye amene anandituma ndi woona, ndipo chimene Ine ndamva kuchokera kwa Iye, ndi chimene ndimaliwuza dziko lapansi.”
Ngo nonugv lvga nga minse ngv awgo doodu, awgo nonua mia sengv. Ngam vngmunv angv, ogubv rijeka jvjv ngv, okv ngo nyiamookua mintamdu ninyi gvlo tvvnam dvdv nga mwngchik.”
27 Iwo sanazindikire kuti Iye amawawuza za Atate ake.
Bunu Jisunyi ninyigv Abu gv lvga nga bunua mindunv vla tvchin mato.
28 Choncho Yesu anati, “Inu mukadzapachika Mwana wa Munthu, pamenepo mudzadziwa kuti Ine Ndine. Mudzadziwa kuti sindichita kalikonse pa Ine ndekha koma ndimayankhula zokhazo zimene Atate anandiphunzitsa.
Vkvlvgabv hv bunua minto, “Vdwlo nonu Nyia Kuunyilo nga tungcha rikudw, ho nonu chinre ‘Ngo Yvvkudw Ngo;’ vbvrikubolo nonu chireku ngo atunvgv chinampanam lokv oguguka rima, vbvritola ngo mindu Abu gv mintoka vla minam a ngo mimwngdunv.
29 Iye amene anandituma Ine ali nane pamodzi. Iye sanandisiye ndekha popeza nthawi zonse ndimachita zomwe zimamukondweretsa Iye.”
Okv yvvdw ngam vngmunv hv ngam lvkobv redunv; hv ngam akinbv kayuma, ogulvgavbolo ngo lokia ninyigv mvnglwkbv ridunv.”
30 Pamene Iye ankayankhula zimenezi, ambiri anamukhulupirira.
Achialv nvgo Jisunyi so mvnwng sum mindubv tvvnv vdwv mvngjwng nyatoku.
31 Kwa Ayuda amene anamukhulupirira, Yesu anati, “Ngati inu mutsatira chiphunzitso changa, ndithu ndinu ophunzira anga.
Vkvlvgabv Jisu ninyia mvngjwngnv vdwa minto, “Nonu ngoogv tamsar nama tvvnvrinv gubv ribolo, nonu jvjvbv ngoogv lvbwlaksu v;
32 Tsono mudzadziwa choonadi, ndipo choonadicho chidzakumasulani.”
nonu jvjv nga chinreku okv jvjv ngv nonua ajarabi moriku.”
33 Iwo anamuyankha Iye kuti, “Ife ndife zidzukulu za Abrahamu ndipo sitinakhalepo akapolo a wina aliyense. Kodi mukunena bwanji kuti, ‘Ife tidzamasulidwa?’”
“Ngonu Abraham gv husi hv,” bunu mirwkto, “okv ngonu yvv gvka nyirabv rikw manv. Vbvrinamv noogv nonua ajarabi kunam gubv mvreku vla minammv oguv?”
34 Yesu anayankha kuti, “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wochita tchimo ndi kapolo wa tchimolo.
Jisu bunua minto, “Ngo jvjv nga nonua minjidunv: nyichar mvnwngngv yvvdw rimur dunv hv rimur gv nyirabv ridunv.
35 Pajatu kapolo alibe malo wokhazikika mʼbanja, koma mwana ndi wa mʼbanjamo nthawi zonse. (aiōn )
Nyira ngv vpinlo doobwng madunv, vbvritola kuunyilo ngv doobwng nvgobv ridunv. (aiōn )
36 Nʼchifukwa chake ngati Mwana adzakumasulani, mudzakhala mfulu ndithu.
Kuunyilo ngv nonua ringlin mooku bolo, vbvrikunamv nonu jvjvrungbv ajarabi kunamv.
37 Ine ndikudziwa kuti inu ndinu zidzukulu za Abrahamu. Chonsecho inu mwakonzeka kundipha Ine, chifukwa mawu anga alibe malo mwa inu.
Ngo chindu nonu Abraham gv husi hv. Vbvrirung gvrila nonu ngam mvki dubv rikwdo, ogulvgavbolo nonu ngoogv tamsar nama torwk simare.
38 Ine ndikukuwuzani zimene ndaziona pamaso pa Atate, ndipo inu mukuchita zimene mwazimva kwa abambo anu.”
Ngo, ngoogv abu ogugo kaatam pvdw ho lvgabv mindunv, vbvritola nonu ridu nonugv abu nonua ogugo minpv pvdw.”
39 Iwo anayankha kuti, “Ife abambo athu ndi Abrahamu.” Yesu anati, “Inu mukanakhala ana a Abrahamu, bwenzi mukuchita zinthu zimene Abrahamuyo ankachita.
Bunu mirwkto, “Ngonugv abuv Abraham.” Jisu mirwksito, “Nonu jvjvbv Abraham gv Kuu gubolo, nonuka hv ogugo ripvdw ho apiabv rire.
40 Koma mmene zililimu, inu mwatsimikiza kundipha Ine, munthu amene ndinakuwuzani choonadi chimene Ine ndinachimva kuchokera kwa Mulungu. Abrahamu sanachite zinthu zoterezi.
Ngoogv rinam mvnwngngv ngo ogugo Pwknvyarnv gvlokv tvvpvdw nonua jvjv nga minji dubv vla ripvnv, vjvka nonu ngam mvkidubv rikwdo. Abraham svkv aingbv rimato!
41 Inu mukuchita zinthu zimene abambo anu amachita.” Iwo anatsutsa kuti, “Ife si ana amʼchigololo, Atate amene tili nawo ndi Mulungu yekha.”
Nonu nonugv abu gv rinam apiabv ridungdo.” “Pwknvyarnv mvngchik ngonugv Abu doonv ngv,” bunu mirwkto, “okv ngonu ninyigv kuunyilo jvjv ngv.”
42 Yesu anawawuza kuti, “Mulungu akanakhala Atate anu, inu mukanandikonda Ine, pakuti Ine ndinachokera kwa Mulungu ndipo tsopano ndili pano. Ine sindinabwere mwa Ine ndekha.
Jisu bunua minto, “Jvjvbv Pwknvyarnv nonugv Abu bv rinv guilo, nonu ngam ayare, ogulvgavbolo ngo Pwknvyarnv gvlokv aanv ngv okv vjak ngo si doodu. Ngo atubogv jwkrw lokv aasuma vbvritola hv nga vngmupvnv.
43 Nʼchifukwa chiyani simukumvetsetsa mawu anga? Chifukwa chake nʼchakuti simungathe kumva zoyankhula zanga.
Ngo ogugo mindudw nonu ogubv chima dunv? So si ogulvgavbolo nonu ngoogv doin ha tvvya nwngmado.
44 Inu ndinu ana a mdierekezi. Iye ndiye abambo anu ndipo mukufuna kuchita zimene abambo anuwo amakhumba. Iye anali wakupha kuyambira pachiyambi, sanasunge choonadi, pakuti mwa iye mulibe choonadi. Pamene Iye anena bodza, amayankhula chiyankhulo chobadwa nacho, popeza ndi wabodza ndipo ndi bambo wa mabodza.
Nonuno Uyudvbv gv kuu ngv, okv nonu abu gv mvngjimvngro kolo rinwngnv. Atuk lokv hv gwngrw gwnv okv vdwloka jvjvgv takbv aakw manv, ogulvgavbolo hoka ninyigvlo jvjv achuk guka dooma. Vdwlo nw mvridw, nw ninyigv riching bv ridunv, ogulvgavbolo nw mvkinv okv mvnv mvnwng gv abuv.
45 Koma chifukwa ndikuwuzani choonadi, inu simukundikhulupirira Ine!
Vbvritola ngo jvjv nga minjidu, vkvlvgabv nonu ngam mwngjwng madunv.
46 Ndani mwa inu angatsimikize kuti ndine wochimwa? Ngati Ine ndikunena choonadi, nʼchifukwa chiyani simukundikhulupirira?
Nonu gvlokv akonv yvvla ngam rimur nvgobv vla gungnying lwkla gaknyu jinv? Ngo jvjv nga mindu bolo, vbvrikunamv nonu ogubv ngam tvvjing madunv?
47 Munthu wochokera kwa Mulungu amamva zimene Mulungu amanena. Chifukwa chimene simumvera nʼchakuti, inuyo sindinu ochokera kwa Mulungu.”
Yvvdw Pwknvyarnv gvlokv aadunv Pwknvyarnv gv gamchar vdwa tvvdunv. Nonu, ogubvrijeka, Pwknvyarnv lokvma, okv vkvlvgabv nonuno tvya madunv.”
48 Ayuda anamuyankha Iye kuti, “Kodi ife sitikulondola ponena kuti Inu ndi Msamariya ndi wogwidwa ndi chiwanda?”
Bunu Jisunyi tvvkato, “Ngonugv nam samaritan go okv no uyuvram gvnvgo vla minam v minjwk mapvnvre?”
49 Yesu anati, “Ine sindinagwidwe ndi chiwanda, koma ndimalemekeza Atate anga, koma inu mukundinyoza.
Jisu mirwksito, “Ngoogvlo uyuvram dooma, ngo Abunyi mvngdv dunv okv nonu ngam miakaya dunv.
50 Ine sindidzifunira ndekha ulemu; koma alipo wina amene amandifunira, ndipo Iyeyo ndiye woweruza.
Ngo atubogv lvgabv mvngdvnam makar madunv. Vbvritola hoka um makarnv ako doodu okv hv ngogvbv jwngkadakayadu.
51 Ine ndikukuwuzani choonadi, munthu akasunga mawu anga, sadzafa konse.” (aiōn )
Ngo jvjv nga nonua minjidunv: yvvdw ngoogv tamsar nama tvvdunv hv vdwloka simare.” (aiōn )
52 Pamenepo Ayuda anafuwula kuti, “Tsopano ife tadziwadi kuti Inu ndi wogwidwa ndi chiwanda! Abrahamu anafa ndiponso aneneri, koma Inu mukunena kuti, ‘Ngati munthu asunga mawu anga, sadzafa.’ (aiōn )
Bunu ninyia minto, “Vjak ngonu jvjvbv mvngduku no gvlo uyuvram doorungdo! Abraham siroku, okv nyijwk vdwvka siroku, vjvka no mindu yvvdw no gv tamsar nama tvvrinv hv vdwloka simare vla. (aiōn )
53 Kodi ndinu wa mkulu kuposa abambo athu Abrahamu? Iye anafa, ndiponso aneneri onse. Inu mukuganiza kuti ndinu yani?”
Ngonugv abu Abraham siroku; no Abrahamnyi kaiyanv gubv mvngsu dunvre? Okv nyijwk vdwvka siroku. No atuv yvv vla mvngsudunv?”
54 Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine ndidzilemekeza ndekha, ulemu wangawo ndi wosatanthauza kanthu. Atate anga amene inu mukuti ndi Mulungu wanu, ndiye amene amandilemekeza Ine.
“Ngo atuv mvngdv subolo, ho mvngdv namv ogu arv doomare. Ngam mvngdvnv angv ngoogv Abu—nonugv Pwknvyarnv vla minam angv.
55 Ngakhale kuti inuyo simukumudziwa, Ineyo ndikumudziwa. Ngati Ine nditanena kuti sindikumudziwa, Ineyo nditha kukhala wabodza ngati inuyo, koma Ine ndimamudziwa ndipo ndimasunga mawu ake.
Nonu vdwloka ninyia chimato, vbvritola ngo ninyia chindu. Ngo ninyia chima vla minbolo, ngo nonugv apiabv mvvki nvgobv ripvnvpv. Vbvritola ngo ninyia chirung dunv, okv ninyigv gamchar a tvvdunv.
56 Abambo anu Abrahamu anakondwera poyembekezera kubwera kwanga. Iwo anandiona ndipo anasangalala.”
Nonugv abu Abraham ngoogv aaji nama kaanwngla mvngpula kaacho toku okv himpu toku.”
57 Ayuda anati kwa Iye, “Inu sumunafike nʼkomwe zaka makumi asanu, ndipo mukuti munamuona Abrahamu!”
Bunu ninyia minto, “No vjak anying chamngu goka svngtv madv—okv no Abrahamnyi kaapv nvlv?”
58 Yesu anayankha kuti, “Ine ndikukuwuzani choonadi, Abrahamu asanabadwe, Ine Ndine!”
Jisu mirwksito, “Ngo jvjv nga nonua minjidunv, Abrahamnyi bvngtv madvbv, ‘Ngoonv.’”
59 Pamenepo iwo anatola miyala kuti amugende, koma Yesu anabisala, nachoka mozemba mʼNyumba ya Mulungu.
Vbvrikunamv bunu ninyia vlwng ordubv vla naarap toku, vbvritola Jisu atubongv tosisito okv Pwknvyarnvnaam a vngyu toku.