< Yohane 6 >
1 Nthawi ina zitatha izi, Yesu anawolokera ku gombe la kutali la nyanja ya Galileya (iyi ndi nyanja ya Tiberiya),
So kochingbv, Jisu Galili Svpar vmalo, Tiberias Svpar vlaka minam a vngbola vngtoku.
2 ndipo gulu lalikulu la anthu linamutsata Iye chifukwa linaona zizindikiro zodabwitsa zimene anazichita pa odwala.
Nyi nyipam twngtv nvgo ninyia vngming gvto, ogulvgavbolo bunu ninyigv lvvmanv vdwa lamrwpadubv mvpuripu nama kaatoku.
3 Kenaka Yesu anakwera pa phiri nakhala pansi ndi ophunzira ake.
Jisu moodw gulo chaatoku okv ninyigv lvbwlaksu vdwa lvkobv dootung toku.
4 Tsopano phwando la Paska la Ayuda linali pafupi.
Vngbokunam Pumja ridw v nvchi toku.
5 Yesu atakweza maso ndi kuona gulu lalikulu la anthu likubwera kwa Iye, anati kwa Filipo, “Kodi tingagule kuti buledi kuti anthu awa adye?”
Jisu kaitkarla kaato okv nyipam v nw gvlo aadungdubv kaapato, vkvlvgabv nw Pilipnyi tvvkato, “Ngonu so nyi vdw sum dvgu dubv dvmunam lvgabv ogolo dvnam rvvpa nyuredw?”
6 Iye anafunsa izi kumuyesa chabe, pakuti Iye ankadziwa chimene ankayenera kuchita.
Hv svbv minam si Pilipnyi tvvka rungbv minto; minjvjvbolo hv chincho suto ogugo hv rise ngvdw.
7 Filipo anamuyankha Iye kuti, “Malipiro a miyezi isanu ndi itatu sangathe kugula buledi okwanira aliyense kuti adye!”
Pilip mirwkto, “Nyichar mvnwngnga achukgo dvmu dajvka, so si lokdwng lvngnyi go dinchirungre dvgudvbv dvnam rvvdubv.”
8 Mmodzi wa ophunzira ake, Andreya, mʼbale wa Simoni Petro, anati,
Ninyigv lvbwlaksu akonv, Andriu, Saimon Pitar gv boru bv rinv, angv minto,
9 “Pano pali mnyamata amene ali ndi buledi musanu wabarele ndi tinsomba tiwiri, kodi zingakwane onsewa?”
“Olo vka vmi ako vtwng tangu go okv ngui nvnyi go gvnvgo doopv. Vbvritola hv so nyi mvnwng gv lvgabv chirung mare.”
10 Yesu anati, “Awuzeni anthuwa akhale pansi.” Pamalo pamenepa panali udzu wambiri ndipo amuna amene anakhala pansi anali osachepera 5,000.
Jisu bunua minto, “Nyi vdwa dootung dubv mvtoka,” (Hoka achialvgo nvmwng ngv dooto.) Vkvlvgabv nyi mvnwngngv dootung nyatoku; hoka ho nyiga dvdv ngv hejar angu gubv ritoku.
11 Kenaka Yesu anatenga bulediyo, atayamika anagawira iwo amene anakhala pansi, chimodzimodzinso nsombazo monga momwe iwo anafunira.
Jisu vtwng nga naato, okv Pwknvyarnvnyi umbonyikv vto, okv hoka doonv nyi vdwa ortoku. Nw ngui haka vbvdvdvbv mvto, okv bunu mvnwngngv vdwgo dvla pvkudw dvgubv dubv dvtoku.
12 Ndipo atakhuta, Iye anati kwa ophunzira ake, “Tolani zotsala kuti pasawonongeke kanthu.”
Vdwlo bunu mvnwngngv dvji dubv dvto kudw, nw ninyigv lvbwlaksu vdwa minto, “Dvlv nga naakumto; akoka ornam orsubv ora momabvju.”
13 Choncho iwo anasonkhanitsa makombo nadzaza madengu khumi ndi awiri.
Vkvlvgabv bunu vtwng tangu nyi vdwgv dvkunam lokv dvtung dvngo dvlv mvnwngnga paapi vring gola anyigo naakum toku.
14 Pambuyo pake anthu ataona chizindikiro chodabwitsa chimene Yesu anachita, iwo anati, “Zoonadi uyu ndi Mneneri wakudzayo mʼdziko la pansi.”
Jisu gv svbv lamrwpanam rila kaatam nama kaala hoka nyi vdwv minto, “So si jvjvbv Nyijwk gurung Sichingmooku so aakujinv akonv!”
15 Yesu atadziwa kuti iwo amafuna kubwera kudzamuwumiriza kuti akhale mfumu, anachoka napita ku phiri pa yekha.
Bunu ninyia naatungla Dvbv bv mvlilala tvdu vla Jisu chintoku; vkvlvgabv nw atubongv moodw vdwbv vngyu toku.
16 Pofika madzulo, ophunzira ake anatsikira ku nyanja,
Vdwlo arium tokudw, Jisu gv lvbwlaksu vdwv svpar lo ilwk toku,
17 kumene iwo analowa mʼbwato ndi kuyamba kuwoloka nyanja kupita ku Kaperenawo. Tsopano kunali kutada ndipo Yesu anali asanabwerere kwa iwo.
svpw gulo aalwk toku, okv svpar lo Kaparnaum kiambv vngkorla vngtoku. Arium kanv toku, okv Jisu vjaklodvbv bunu gvlo aatv madvto.
18 Mphepo yamphamvu inawomba ndipo nyanja inalusa.
Vbvrikunamv kainv doori go rilwkto okv isi a kiokdubv mvtoku.
19 Iwo atayenda makilomita asanu kapena asanu ndi limodzi, anaona Yesu akuyandikira bwatolo, akuyenda pa madzi; ndipo anachita mantha.
Lwbwlaksu vdwv svpwa dula lvtw angu vmalo akv gubv dulwk toku vdwlo bunu Jisunyi isi aolo vngdung dubv, svpw nvchilo aadung dubv kaapa toku, okv bunu busu nyatoku.
20 Koma Iye anawawuza kuti, “Ndine, musaope.”
Jisu bunua minto, “Nonuno busu mabvka, si ngo sumabv!”
21 Ndipo iwo analola kumutenga mʼbwatomo, nthawi yomweyo bwatolo linafika ku gombe la nyanja kumene ankapita.
Vbvrikunamv bunu mvngpula ninyia svpw arwnglo aamu toku okv svpw lo bunugv vnglwkjiku mooku lo baapubv vngchi nyatoku.
22 Pa tsiku lotsatira gulu la anthu limene linatsala kumbali ina yanyanjayo linaona kuti panali bwato limodzi lokha, ndipo kuti Yesu sanalowe mʼbwatomo pamodzi ndi ophunzira ake, koma kuti ophunzirawo anapita okha.
Logo nvnga nyipam v svpar takdv gonvbv doonv vdwv oloka svpw ngv akin gumwng vla mvngdi nyatoku. Bunu Jisunyi ninyigv lvbwlaksu lvkobv vngma, vbvritola bunu ninyia kayupila vngyu ropvku vla chintoku.
23 Kenaka mabwato ena ochokera ku Tiberiya anafika pafupi ndi pamalo pamene anthu anadya buledi Ambuye atayamika.
Kvvbi svpw vdwv, Tiberias lokv, Jisu gv vtwng nga umbonyikv vro kochingbv nyi vdwa dvmuku mooku nvchi gv isi adarlo aakum nyatoku.
24 Nthawi yomwe gulu la anthu linaona kuti Yesu kapena ophunzira ake sanali pamenepo, ilo linalowanso mʼmabwatowo ndi kupita ku Kaperenawo kukamufunafuna Yesu.
Vdwlo nyipam v Jisu hoka dooma, ninyigv lvbwlaksu vdwvka dooma vla kaato kudw, bunu ho svpw vdw ho aanyatoku okv ninyia kaakarla Kaparnaumbv vngtoku.
25 Atamupeza mbali ina ya nyanjayo, iwo anamufunsa Iye kuti, “Rabi, mwafika nthawi yanji kuno?”
Vdwlo nyi vdwv Jisunyi svpar gv takdv gunvlo kaapa tokudw, bunu ninyia tvvkato, “Tamsarnv, vdwlo no so aapvnv?”
26 Yesu anawayankha kuti, “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti mukundifuna, osati chifukwa munaona zizindikiro zodabwitsa koma chifukwa munadya chakudya ndi kukhuta.
Jisu mirwksito, “Ngo nonua jvjv nga minpa jidunv: nonuno ngam makardu ogulvgavbolo nonu vtwng nga dvla okv nonugv mvngnam a dvkunam lvgalo, ngoogv lamrwpanam rinam a chinam lokvma.
27 Gwirani ntchito, osati chifukwa cha chakudya chimene chimawonongeka koma chifukwa cha chakudya chimene sichiwonongeka mpaka ku moyo wosatha, chimene Mwana wa Munthu adzakupatsani. Mulungu Atate anamusindikiza chizindikiro chomuvomereza.” (aiōnios )
Alvmanv gubv rijinv dvnam lvgabv rima bvka, vmabvya turbwngla svngya jinv dvnam lvgabv rilaka. So siinv Nyia Kuunyilo gv nonua dvnam jiji namv, ogulvgavbolo Pwknvyarnv Abu ninyia alvnvgobv tolwk laku mvu pvkunv.” (aiōnios )
28 Kenaka anamufunsa Iye kuti, “Kodi tichite chiyani kuti tigwire ntchito za Mulungu?”
Vkvlvgabv bunu ninyia tvvkato, “Pwknvyarnv gv mvnglwkbv rinam lvgabv ngonu ogugo rila sego bri?”
29 Yesu anayankha kuti, “Ntchito ya Mulungu ndi iyi: Kukhulupirira Iye amene anamutuma.”
Jisu mirwksito, “Pwknvyarnv gv nonua ritokv vla mvngnamv si ninyigv vngmunam anga mvngjwng laka vla.”
30 Choncho iwo anamufunsa Iye kuti, “Kodi mudzatipatsa chizindikiro chodabwitsa chotani kuti ife tichione ndi kukhulupirira Inu? Kodi mudzachita chiyani?
Bunu mirwksito, “Ogu lamrwpanam go no rila kaatam dubv ngonu um kaagvrila nam mvngjwng dubv? No ogugo ridubv?
31 Makolo athu akale anadya mana mʼchipululu; monga zalembedwa: ‘anawapatsa buledi wochokera kumwamba kuti adye.’”
Ngonugv abuapa vdwv chukrimooku lo manna nga dvto Darwknv Kitaplo minam aingbv, ‘Hv nyido mooku tolokv vtwng nga jito dvmu dubv.’”
32 Yesu anawawuza kuti, “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti si Mose amene ankakupatsani chakudya chochokera kumwamba, koma ndi Atate anga amene ankakupatsani chakudya chenicheni chochokera kumwamba.
“Ngo nonua jvjv nga minjidunv,” Jisu minto, “Moses nonua ogugo jipv kudw hv nyidomooku tolokv vtwng ma; so si ngoogv Abu nonua nyidomooku tolokv vtwng loda jenga jinv.
33 Pakuti chakudya cha Mulungu ndi Iye amene wabwera kuchokera kumwamba ndi kupereka moyo ku dziko la pansi.”
Pwknvyarnv gv vtwng jinammv hv yvvdw nyidomooku tolokv inv okv nyiamookua turnam jidu.”
34 Iwo anati, “Ambuye, kuyambira tsopano muzitipatsa buledi ameneyu.”
Bunu ninyia kooto, “Tamsarnv, so gv dvnam a ngonua lokia jilabv.”
35 Kenaka Yesu ananenetsa kuti, “Ine ndine chakudya chamoyo. Iye amene abwera kwa Ine sadzamva njala, ndipo iye amene akhulupirira Ine sadzamva ludzu.
Jisu bunua mintoku, “Ngo kunv turnam gv vtwng ngv, yvvdw ngoogvlo aadunv vdwloka kano kumare; yvvdw ngam mvngjwng dunv vdwloka tvngnwng kumare.
36 Monga ndakuwuzani kale, ngakhale kuti mwandiona simukukhulupirirabe.
Vjak, ngo nonua mindunv nonuno ngam kaaroku vbvritola mvngjwng mare.
37 Zonse zimene Atate andipatsa zidzabwera kwa Ine, ndipo aliyense amene adzabwera kwa Ine sindidzamutaya kunja.
Nyichar mvnwngnga yvvnyi ngo Abu ngam jidu kudw ngogvlo aareku. Ngo vdwloka ngogvlo aanv nga dakkurla vngyu mare,
38 Pakuti Ine ndinatsika kuchokera kumwamba osati kudzachita chifuniro changa koma cha Iye amene anandituma Ine.
ogulvgavbolo ngo nyidomooku tolokv inam hv ngo atugv mvngwngbv ridu bvma vbvritola ngam vngmunv ninyigv mvngnambv ridubv.
39 Ndipo chifuniro cha Iye amene anandituma Ine nʼchakuti ndisatayepo ngakhale ndi mmodzi yemwe mwa onse amene Iye wandipatsa, koma kuti ndidzawaukitse kwa akufa pa tsiku lomaliza.
Okv so si ngam vngmunv ninyigv mvngnamv ngo ninyigv jinam mvnwng loka akonyika ngoomu marung dubv, vbvritola ngo bunua ataranya alulo bunua turrap modukubv.
40 Pakuti chifuniro cha Atate anga ndi chakuti aliyense amene aona Mwanayo namukhulupirira akhale ndi moyo wosatha, ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza.” (aiōnios )
Ngo Abu gv mvngnam v Kuunyilo nga kaanv mvnwngngv okv ninyia mvngjwngnv vdwv turbwngnv singnam ha paadubv. Okv ngo bunua ataranya alu lo turmu dukubv.” (aiōnios )
41 Pamenepo Ayuda anayamba kungʼungʼudza chifukwa anati, “Ine ndine chakudya chotsika kuchokera kumwamba.”
Nyi vdwv ninyia bvdung-bvdungbv japnyato, ogulvgavbolo hv minto “Ngo nyidomooku tolokv vtwng inv ngv.”
42 Iwo anati, “Kodi uyu si Yesu, mwana wa Yosefe, amene abambo ake ndi amayi ake timawadziwa? Nanga Iyeyu akunena bwanji kuti, ‘Ine ndinatsika kuchokera kumwamba?’”
Vkvlvgabv bunu minto, “So nyi si Jisu, Josep gv kuunyilo ngv, hv mari? Ngonu ninyigv abu nyila okv anvnyi chindu, vbvrikunamv vjak oguaingbv hv mindunvdw ngo nyidomooku tolokv ipvnv vla?”
43 Yesu anayankha kuti, “Musangʼungʼudze pakati panu.”
Jisu mirwksito, “Nonugv pingkolo bvdung-bvdungbv mimabvka.
44 Palibe munthu amene angabwere kwa Ine, ngati Atate amene anandituma Ine samubweretsa. Ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza.
Yvvka ngoogvlo aanyu mare vdwlo ngam vngmunv Abu ninyia ngoogvlo naalwk jima redw; okv ngo ninyia ataranya alulo turrap moreku.
45 Aneneri analemba kuti, “Onse adzaphunzitsidwa ndi Mulungu! Aliyense amene amamva Atate ndi kuphunzira kwa Iye amabwera kwa Ine.
Nyijwk vdwv lwkgapto, ‘Mvnwngnga Pwknvyarnv tamsarto.’ Yvvdw Abunyi tvvgap dunv okv ninyi gvlo chindunv ngoogvlo aadunv.
46 Palibe amene anaona Atate koma yekhayo amene achokera kwa Mulungu; yekhayo ndiye anaona Atate.
So si vbv minam angvma nyi gunv Abunyi kaapv nvgo vla; hv yvvdw Pwknvyarnv lokv aapvnv hv mvngchik Pwknvyarnvnyi kaanv ngv.
47 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Iye amene akhulupirira ali nawo moyo wosatha. (aiōnios )
Ngo nonua jvjv nga minjidunv: yvvdw mvngjwng dunv hv turbwngnv singnam a paapv kunv. (aiōnios )
48 Ine ndine chakudya chamoyo.
Ngo kunv turnam gv vtwng ngv.
49 Makolo anu akale anadya mana mʼchipululu, komabe anafa.
Nonugv abuapa vdwv chukrimooku lo manna nga dvto, vbvritola bunu siroku.
50 Koma pano pali chakudya chochokera kumwamba, chimene munthu akadya sangafe.
Vbvritola nyidomooku tolokv inv vtwng ngv vbvridu um dvnv ngv simare.
51 Ine ndine chakudya chamoyo chochokera kumwamba. Ngati munthu adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi zonse. Chakudya chimenechi ndi thupi langa, limene Ine ndidzalipereka kuti anthu pa dziko lapansi akhale ndi moyo.” (aiōn )
Ngo turnv vtwng ngv nyidomooku tolokv ipvnv. Yvvdw so vtwng sum dvbolo, hv turbwngla singre. Ngoogv ninyia vtwng jiji namv ngoogv ayak v um ngo jidu ogulvgavbolo nyiamooku hv singdu kubv.” (aiōn )
52 Kenaka Ayuda anayamba kutsutsana kwambiri pakati pawo kuti, “Kodi munthu uyu angathe kutipatsa bwanji thupi lake kuti tidye?”
Si bunugv apumlo haachila larrap minsunam gubv rito. Bunu tvvka minsuto, “Oguaingbv so nyi si ninyigv ayakka ngonua dvmudubv vla jila nyuridw?”
53 Yesu anawawuza kuti, “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti ngati simungadye thupi la Mwana wa Munthu ndi kumwa magazi ake, simungakhale ndi moyo mwa inu.
Jisu bunua minto, “Ngo jvjv nga nonua minjidunv: nonu vdwlo nyia Kuunyilo gv ayakka dvma redw okv ninyigv oyi ha tvngma redw nonu atubongv turnama paamare.
54 Aliyense amene adya thupi langa ndi kumwa magazi anga ali ndi moyo wosatha ndipo Ine ndidzamuukitsa kwa akufa pa tsiku lomaliza. (aiōnios )
Yvvdw ngoogv ayakka dvridw okv ngoogv oyi ha tvngridw turbwngnv singnam ha paare, okv ataranya alulo ngo ninyia turrap moriku. (aiōnios )
55 Pakuti thupi langa ndi chakudya chenicheni ndipo magazi anga ndi chakumwa chenicheni.
Ogulvgavbolo ngoogv ayak v dvnam jvjv ngv; ngoogv oyi si tvngnam jvjv ngv.
56 Aliyense amene adya thupi langa ndi kumwa magazi anga amakhala mwa Ine, ndi Ine mwa iye.
Yvvdw ngoogv ayak ha dvdunv okv ngoogv oyi ha tvngdunv ngoogvlo doodunv, okv ngo ninyi gvlo doodunv.
57 Monga Atate amoyo anandituma Ine, ndipo ndili ndi moyo chifukwa cha Atatewo, chomwechonso amene adya thupi langa adzakhala ndi moyo chifukwa cha Ine.
Turbwngnv Abu ngam vngmuto, okv ninyigv lokv ngo ka turdunv. Ho apaiabv yvvdw ngoogv ayak ha dvdunv hv ngo gvlokv turbwngla doore.
58 Ichi ndiye chakudya chimene chinatsika kuchokera kumwamba. Makolo athu akale anadya mana ndi kufa, koma iye amene adya chakudya ichi, adzakhala ndi moyo nthawi yonse.” (aiōn )
Vbvrikunamv, si, nyidomooku tolokv inv vtwng ngv; so si nonugv abuapa vdwgv vtwng dvnam aingma, vbvritola koching so sitoku. Yvvdw so vtwng sung dvredw hv turbwngla svngre.” (aiōn )
59 Iye ankanena izi pamene ankaphunzitsa mʼsunagoge mu Kaperenawo.
Jisu sum Kaparnaum lo Jius kumkunaamlo ninyigv tamsar sarnam jvbv minto.
60 Pakumva izi ambiri a ophunzira ake anati, “Ichi ndi chiphunzitso chovuta. Angachilandire ndani?”
Ninyigv rigvnam nyi achialvgo sum tvvpa toku okv minto, “So tamsarnam si achialvbv rinyu manamgo. Yvv sum tvvria nyudubv?”
61 Pozindikira kuti ophunzira ake ankangʼungʼudza, Yesu anawafunsa kuti, “Kodi izi zikukukhumudwitsani?
Minpanvgo kaamajeka, Jisu chinto bunu soogv lvga nga bvdung-bvdungbv larmisidu nvgo vla vkvlvgabv hv bunua minto, “So si nonua topu monwng dubv mvdu nvgo lare?
62 Nanga mutaona Mwana wa Munthu akukwera kupita kumene Iye anali poyamba!
Vbvrikunamv, nonu nyia Kuunyilo nga ninyigv kvvlo doochoku mooku tolo chaakor dukubv kaanam gubv rikubolo?
63 Mzimu Woyera apereka moyo, thupi silipindula kanthu. Mawu amene ndayankhula kwa inu ndiwo mzimu ndipo ndi moyo.
Turnam ogugo jinv si Pwknvyarnv gv Dow ngv; nyi gv jwkrw si vdwloka ogu mvnwng loka rinv nyuma. Ngoogv nonua gamchar minam vdwv turnam naalwk jinv Pwknvyarnv gv Dow ngv.
64 Komabe alipo ena mwa inu amene sakukhulupirira.” Pakuti Yesu ankadziwa kuyambira pachiyambi ena mwa iwo amene samakhulupirira ndi amene adzamupereka Iye.
Vbvritola nonu megonv mvngjwngma.” (Jisu atoklokv chinchoto bunugv lokv yvvdw mvngjwng majinv okv yvvdw ninyia koa kujinv.)
65 Iye anapitiriza kunena kuti, “Ichi ndi chifukwa chake ndinakuwuzani kuti palibe wina angabwere kwa Ine pokhapokha Atate atamuthandiza.”
Okv hv mindvto, “So siinv anyung ngv ngo nonua mintoku vdwlo Abu ninyia vbv rinyu dubv mvvma dvdvlo yvvka ngoogvlo aanyu mare.”
66 Kuyambira nthawi imeneyi ophunzira ake ambiri anabwerera ndipo sanamutsatenso Iye.
Vbv minam lvkwngbv, Jisu gv rigvnam achialvgo vngkur nyatoku okv ninyia lvkoka vngming gvkuma.
67 Yesu anafunsa khumi ndi awiriwo kuti, “Kodi inu mukufuna kuchokanso?”
Vkvlvgabv ninyigv lvbwlaksu vring gola anyi vdwa tvvkato, “Okv nonu—nonu ka topu duku bri?”
68 Simoni Petro anamuyankha Iye kuti, “Ambuye, ife tidzapita kwa yani? Inu muli ndi mawu amoyo wosatha. (aiōnios )
Saimon Pitar ninyia mirwksito, “Ahtu vbvbolo ngonu yvvnyi vngming gvdu kubv? Turbwngnv singnam a jinv gamchar v no gvlo doodu. (aiōnios )
69 Ife tikhulupirira ndi kudziwa kuti Inu ndinu Woyerayo wa Mulungu.”
Okv ngonu vjak mvngjwngdu okv chindu no darwk mvngchiknv Pwknvyarnv gvlokv aanv.”
70 Kenaka Yesu anayankha kuti, “Kodi Ine sindinakusankheni inu khumi ndi awiri? Komabe mmodzi wa inu ndi mdierekezi.”
Jisu mirwksito, “Ngo nonu vring gola anyia darpvnv, ngo darmare? Vbvritola nonugv lokv akonv uyudvbv go!”
71 (Iye amanena Yudasi, mwana wa Simoni Isikarioti amene ngakhale anali mmodzi mwa khumi ndi awiriwo, anali woti adzamupereka).
Hv Judas gv lvkwng nga minto, Saimon Iskeriot gv kuunyilo. Judas, lvbwlaksu vring gola anyi lokv jeka, Jisunyi koa tvduku.