< Yohane 4 >
1 Yesu atazindikira kuti Afarisi amva zoti Iye ankapeza ndi kubatiza ophunzira ambiri kupambana Yohane,
Mafalisayu wapikiniriti handa Yesu kaweriti kankubatiza na kankuwapata wafundwa wavuwa kuliku Yohani.
2 (ngakhale kuti Yesuyo sankabatiza, koma ophunzira ake).
Kumbiti nakaka Yesu kawera ndiri kankubatiza ira wafundwa wakuwi ndo waweriti wankubatiza.
3 Iye anachoka ku Yudeya ndi kubwereranso ku Galileya.
Yesu pakapikaniriti aga, kalawa Yudeya kagenda Galilaya,
4 Ndipo Iye anayenera kudutsa mu Samariya.
pamwanja gwakuwi kalazimika kupitila Samariya.
5 Iye anafika mʼmudzi wa Asamariya wotchedwa Sukari, pafupi ndi malo amene Yakobo anapatsa mwana wake Yosefe.
Su kafikiti Sikari, lushi lumu lwa Samariya, pakwegera na lirambu lilii Yakobu lyakamupiti mwana gwakuwi Yosefu.
6 Chitsime cha Yakobo chinali pamenepo ndipo Yesu atatopa ndi ulendo anakhala pansi pambali pa chitsimecho. Nthawi inali pafupifupi ora lachisanu ndi chimodzi masana.
Na panu paweriti na linegu lya Yakobu. Yesu kaweriti katoka toziya ya mwanja, su kalivagiti pasi pampenku pa linegu. Iweriti ipata saa sita paliwala.
7 Mayi wa Chisamariya atabwera kudzatunga madzi, Yesu anati kwa iye, “Kodi ungandipatse madzi akumwa.”
Mdala Msamariya kiziti kuteka mashi na Yesu kamgambira, “Gunupi mashi nandi.”
8 (Ophunzira ake nʼkuti atapita mʼmudzi kukagula chakudya).
Wafundwa wakuwi wagenditi mulushi kuhemera shiboga.
9 Mayiyo anati kwa Iye, “Inu ndinu Myuda ndipo ine ndine Msamariya. Bwanji mukundipempha madzi akumwa?” (Popeza Ayuda ndi Asamariya sankayanjana).
Mdala uliya kamgambira, “Gwenga gwa Muyawudi, neni na Msamariya! Su guwezahashi kunduwa mashi ga kulanda?” Wayawudi hapeni watumii vikombi na vibakuli vyavihanganyikiti na vya wantu wa Samariya.
10 Yesu anamuyankha kuti, “Koma iwe ukanadziwa mphatso ya Mulungu ndi Iye amene akukupempha madzi akumwa, ukanamupempha ndipo akanakupatsa madzi amoyo.”
Yesu kamwankula, “Handa meguvimaniti mafupu ga Mlungu na gaa yakakuluwa mashi ga kulanda, megumluwi na yomberi mekakupi mashi ga ukomu.”
11 Mayiyo anati, “Ambuye, Inu mulibe kanthu kotungira madzi ndipo chitsime ndi chakuya. Kodi madzi amoyowo mungawatenge kuti?
Mdala uliya kalonga, “Mtuwa, gwenga gwahera shintu sha kutekera mashi na linegu ndo litalipa. Su, hagupati koshi mashi gana ukomu?
12 Kodi Inu ndinu wamkulu kuposa kholo lathu Yakobo, amene anatipatsa chitsimechi ndipo iye ankamwanso monga anachita ana ake ndi ziweto zake?”
Mbuyi gwetu Yakobu ndo yakatupiti linegu ali, yomberi na wana wakuwi pamuhera na mifugu yakuwi yoseri walanditi mashi aga. Ashi gwenga gulitumba kuwera mkulu kuliku Yakobu?”
13 Yesu anayankha kuti, “Aliyense amene amamwa madzi awa amamvanso ludzu,
Yesu kamwankula, “Woseri walanda mashi aga hawaweri na kwimiluwa kayi.
14 koma aliyense amene adzamwa madzi amene Ine ndidzamupatsa sadzamvanso ludzu. Ndithudi, madzi amene ndidzamupatsa adzakhala kasupe wamadzi wotumphukira ku moyo wosatha.” (aiōn , aiōnios )
Kumbiti yoseri yakalanda mashi ganumupa neni, hapeni kaweri na kwimiluwa kayi. Mashi ganumupa hagaweri mngati mwakuwi mbwiru ya mashi ga ukomu na kumupa ukomu wa mashaka goseri.” (aiōn , aiōnios )
15 Mayiyo anati kwa Iye, “Ambuye, patseni madzi amenewo kuti ndisadzamvenso ludzu ndi kumabwerabe kuno kudzatunga madzi.”
Mdala uliya kamgambira, “Mtuwa, gunupi mashi aga! Shakapanu hapeni numuluwi kayi na hapeni nizi kayi panu kuteka mashi.”
16 Iye anamuwuza kuti, “Pita kayitane mwamuna wako ndipo ubwere naye.”
Yesu kamgambira, “Gugendi gwakamshemi mpalu gwaku gwizi nayomberi.”
17 Iye anayankha kuti, “Ine ndilibe mwamuna.” Yesu anati kwa iye, “Wakhoza ponena kuti ulibe mwamuna.
Mdala uliya kamwankula, “Neni nahera mpalu,” Yesu kamgambira, “Gutakula weri pagutakuliti gwahera mpalu.
18 Zoona nʼzakuti iwe wakhala pa banja ndi amuna asanu, ndipo mwamuna amene uli naye tsopano si wako. Zimene wanenazi ndi zoona.”
Guyugwa na wapalu wamuhanu, yomberi yagulikala nayu vinu, mpalu gwaku ndiri. Gung'ambira nakaka.”
19 Mayiyo anati, “Ambuye, ine ndazindikira kuti Inu ndinu mneneri.
Mdala uliya kamgambira, “Mtuwa, mona gwenga gwa mbuyi gwa Mlungu.
20 Makolo athu ankapembedza mʼphiri ili koma inu Ayuda mumati malo amene tiyenera kupembedzera ali ku Yerusalemu.”
Wambuyi wangu wa Samariya wamguwiriti Mlungu mulugongu alu, su mwenga Wayawudi mlonga kuwera Yerusalemu ndo pahala pa kumwabudu Mlungu.”
21 Yesu anati, “Mayi inu khulupirira Ine. Nthawi ikubwera pamene inu simudzapembedza Atate mʼphiri ili kapena mu Yerusalemu.
Yesu kamgambira, “Mdala, gunjimira, shipindi shankwiza ndo sheni wantu hapeni wamguwira Tati mulugongu alu ama ku Yerusalemu.
22 Inu Asamariya mumapembedza chimene simukuchidziwa. Ife timapembedza chimene tikuchidziwa, pakuti chipulumutso nʼchochokera kwa Ayuda.
Mwenga Wasamaliya muvimana ndiri nakaka yawamguwira, kumbiti twenga Wayawudi tumumana yatumguwira, toziya ulopoziya wiza kulawa kwa Wayawudi.
23 Koma nthawi ikubwera ndipo yafika kale tsopano pamene opembedza woona adzapembedza Atate mu mzimu ndi mʼchoonadi, pakuti opembedza otere ndiwo amene Atate akuwafuna.
Kumbiti shipindi shankwiza na kayi shisoka kala, peni wawamguwira nakaka, hawamguwili Tati kwa likakala lya Rohu, wantu wamguwira hangu ndo Tati yakawafira.
24 Mulungu ndi Mzimu, ndipo omupembedza Iye ayenera kumupembedza mu mzimu ndi mʼchoonadi.”
Mlungu ndo Rohu, na wantu hawawezi hera kumwabudu nakaka kwa likakala lya Rowu gwakuwi.”
25 Mayiyo anati, “Ine ndikudziwa kuti Mesiya (wotchedwa Khristu) akubwera. Akabwera, Iye adzafotokoza zonse kwa ife.”
Mdala ulii kamgambira, “Nuvimana kuwera Kristu Mlopoziya yakasyagulitwi hakizi na pakiza hakatugambiri twenga kila shintu.”
26 Ndipo Yesu anamuwuza kuti, “Amene ndikukuyankhulane, ndine amene.”
Yesu kamgambira, “Neni, ndo yantakula na gwenga.”
27 Pa nthawi yomweyo ophunzira ake anabwerera ndipo anadabwa kupeza Iye akuyankhula ndi mayi. Koma palibe amene anamufunsa kuti, “Kodi mukufuna chiyani?” kapena, “Nʼchifukwa chiyani mukuyankhula naye?”
Shipindi shila shilii wafundwa wa Yesu wawuyiti na waweriti na likangasha likulu pawamwona Yesu pakatakula na mdala. Kwehera yumu pakati pawu yakamgambiriti mdala ulii, “Gufira shishi?” Ama kumkosiya Yesu, “Iwera hashi gwankutakula na mdala ayu?”
28 Kenaka mayiyo anasiya mtsuko wamadzi, nabwerera ku mzinda ndipo anati kwa anthu,
Su, mdala uliya kaileka vulu yakuwi, kagenda mulushi na kuwagambira wantu,
29 “Tiyeni mukaone munthu amene wandiwuza ine zilizonse zimene ndinazichita. Kodi ameneyu sangakhale Khristu?”
“Mwizi mloli muntu yakang'ambiriti vitwatira vyoseri vyantenditi. Hashi, iwezikana yomberi kawera Kristu yakasyagulitwi na Mlungu?”
30 Iwo anatuluka mʼmudziwo ndi kupita kumene kunali Iye.
Wantu walawa mulushi, wamgendera Yesu.
31 Pa nthawi imeneyi ndi kuti ophunzira ake akumukakamiza kuti, “Rabi idyani.”
Shipindi shila shiriya wafundwa waweriti wankumuhiga Yesu, “mfunda, gulii shiboga!”
32 Koma Iye anawawuza kuti, “Ine ndili ndi chakudya choti ndidye chimene inu simukuchidziwa.”
Su Yesu kawankula, “Neni nana shiboga shamshimana ndiri.”
33 Ndipo ophunzira ake anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Kodi alipo wina amene anamubweretsera Iye chakudya?”
Wafundwa wakuwi walitakuziyana weni, “Hashi, kwana muntu yoseri yakamjegiriti shiboga?”
34 Yesu anati, “Chakudya changa ndikuchita chifuniro cha Iye amene anandituma Ine ndi kumaliza ntchito yake.
Yesu kawagambira, “Shiboga shaneni ndo kugajimira gakafira ulii yakantumiti neni na kumalira lihengu lyakanupiti kutenda.
35 Kodi inu simunena kuti, ‘Kwatsala miyezi inayi ndipo kenaka kukolola?’ Ine ndikukuwuzani kuti, tsekulani maso anu ndipo muyangʼane mʼminda! Mbewu zacha kale kuti zikololedwe.
Mwenga mtakula, ‘Kunkali myezi ya msheshi hera, shipindi sha kubenanga hashisoki.’ Su nukugambirani, mloli marambu, viboga vinu vipiya kala na viwera kala kubenanga!
36 Ngakhale tsopano amene akukolola akulandira malipiro ake, ndipo akututa mbewu ku moyo wosatha kuti wofesa ndi wokolola asangalale pamodzi. (aiōnios )
Yakabena viboga kankupata shibenamgongu na kankujojinira viboga kwa mashaka goseri, su yumonga yakayala na ulii yakabena hawanemeleri pamuhera. (aiōnios )
37 Nʼchifukwa chake mawu akuti, ‘Wina amafesa ndipo wina amakolola’ ndi woona.
Kutakula aku kwa nakaka, ‘Yumu kayalaga na yumonga kabenaga.’
38 Ine ndinakutumani kukakolola zimene simunagwirire ntchito. Ena anagwira ntchito yolemetsa ndipo inu mwatuta phindu la ntchito yawo.”
Neni nuwatumiti mwenga mwakabeni viboga mulirambu mtenda ndiri lihengu, wamonga watenditi lihengu kulii na mwenga muna mota kulawirana na lihengu lyawatenditi.”
39 Asamariya ambiri ochokera mʼmudziwo anakhulupirira Iye chifukwa cha umboni wa mayiyo wakuti, “Iye anandiwuza ine zonse ndinazichita.”
Wasamariya wavuwa mulushi lulii wamjimiriti Yesu toziya mdala uliya katakuliti, “Kang'ambiriti neni shintu shoseri shantenditi.”
40 Choncho Asamariya atabwera kwa Iye, anamuwumiriza Iye kuti akhale nawo, ndipo Iye anakhala nawo masiku awiri.
Su Wasamariya pawamgendiriti Yesu, wamuluwiti yomberi kalikali pamuhera na womberi na Yesu kalikaliti kulii mashaka mawili.
41 Ndipo chifukwa cha mawu ake, ena ambiri anakhulupirira.
Wantu wavuwa wamjimiriti toziya ya ujumbi wakuwi,
42 Iwo anati kwa mayiyo, “Ife sitikukhulupirira chifukwa cha mawu ako okha, koma tsopano ife tadzimvera tokha, ndipo tikudziwa kuti munthu uyu ndithu ndi Mpulumutsi wa dziko lapansi.”
na womberi wamgambira mdala uliya, “Vinu twenga tujimira, toziya ndiri ya shilii shagutakuliti, ira toziya twenga tumpikanira twaweni na tuvimana kuwera nakaka ndo Mlopoziya gwa pasipanu.”
43 Patatha masiku awiri Iye anachoka napita ku Galileya.
Pagapititi mashaka mawili, Yesu kawukiti paliya na kugenda Galilaya.
44 (Tsopano Yesu mwini ananena kale kuti mneneri salandira ulemu mʼdziko lake).
Mana Yesu mweni katakuliti, “Mbuyi gwa Mlungu hapeni kapananwi ligoya muisi yakuwi.”
45 Iye atafika ku Galileya, Agalileya anamulandira. Iwo anali ataona zonse zimene anazichita mu Yerusalemu pa phwando la Paska, pakuti iwonso anali komweko.
Pakafikiti Galilaya, wantu wa paliya wamshemiriti, toziya pawaweriti mumsambu gwa Pasaka kulii Yerusalemu wawonaga vitwatira vyoseri vyakatenditi Yesu shipindi sha msambu.
46 Iye anakafikanso ku Kana wa ku Galileya, kumene anasanduliza madzi kukhala vinyo. Ndipo kumeneko kunali nduna ina ya mfumu imene mwana wake wamwamuna anali chigonere akudwala ku Kaperenawo.
Su Yesu kawuyiti kayi Kana mumkowa gwa Galilaya, pahala pakagalambuziti mashi kuwera divayi. Afisa gwa sirikali kaweriti paliya mwana gwakuwi kaweriti kalwala ku Kafarinaumu.
47 Munthu uyu atamva kuti Yesu wafika ku Galileya kuchokera ku Yudeya, anapita kwa Iye, namupempha kuti apite akachiritse mwana wakeyo, amene anali pafupi kufa.
Pakapikaniriti handa Yesu kankwiza Galilaya pakalawila Yudeya, kamgendiriti yomberi na kumgambira kagendi Kaferinawumu na kamuponiziyi mwana gwakuwi, yakaweriti sambira kahowa.
48 Yesu anawawuza iwo kuti, “Anthu inu pokhapokha mutaona zizindikiro zodabwitsa, simudzakhulupirira.”
Yesu kamgambira, “Pamwona ndiri malangaliru na mauzauza, hapeni mjimiri!”
49 Nduna ya mfumuyo inati, “Ambuye tiyeni mwana wanga asanafe.”
Afisa ulii kamwankula, “Mtuwa, tugendi pamuhera vinu, mwana keni howi.”
50 Yesu anayankha kuti, “Pita. Mwana wako adzakhala ndi moyo.” Munthuyo anakhulupirira mawu a Yesu ndipo ananyamuka.
Yesu kamgambira, “Gugendi, mwana gwaku hakaweri mkomu!” Muntu uliya kavimaniti visoweru vya Yesu, su kagenda zakuwi.
51 Iye ali pa njira, antchito ake anakumana naye, namuwuza kuti mwana wanu uja wachira.
Pakaweriti kankali kamunjira kuwuya ukaya kaliwoniti na wantumintumi wakuwi pawamjegera visoweru, “Mndemba gwakuwi kawera mkomu!”
52 Iye atafunsa kuti ndi nthawi yanji imene mwana wake anapeza bwino, iwo anati kwa iye, “Malungo anamusiya iye dzulo pa ora lachisanu ndi chiwiri.”
Kawakosiya shipindi gaa mwana gwakuwi pakaweriti mkomu na womberi wamwankula, “Iweriti saa saba paliwala lishu nshimba kupyupa paimlekeziyiti.”
53 Ndipo bamboyo anazindikira kuti iyi inali nthawi yomweyo imene Yesu anati kwa iye, “Mwana wako adzakhala ndi moyo.” Choncho iye ndi onse a pa banja lake anakhulupirira.
Tati uliya kaliholiti kuwera shipindi shiliya ndo Yesu pakamgambiriti, “Mwana gwaku hakaweri mkomu.” Su mweni pamuhera na kaya yakuwi yoseri wamjimira Yesu.
54 Ichi ndiye chinali chizindikiro chodabwitsa chachiwiri chimene Yesu anachita atafika ku Galileya kuchokera ku Yudeya.
Liuzauza ali ndo lya pili lyakatenditi Yesu pakaweriti kankulawa Yudeya na kugenda Galilaya.