< Yohane 4 >

1 Yesu atazindikira kuti Afarisi amva zoti Iye ankapeza ndi kubatiza ophunzira ambiri kupambana Yohane,
Manoor Iyesus Yohansiyere bogo ay ashuwotsi b́ danifwotsi b́ woshirwok'onat b́ gupirwok'o ferisawino etfwots shishbok'ri,
2 (ngakhale kuti Yesuyo sankabatiza, koma ophunzira ake).
Wotowaere gupirwots b́ danifuwotsi bako bí b́tookon gufatse.
3 Iye anachoka ku Yudeya ndi kubwereranso ku Galileya.
B́ jango keewetso ferisawiwots boshishtsok'o danb́k'rtsok'on Iyesus Yhud datso k'azt Gelil maants aani k'az bíam.
4 Ndipo Iye anayenera kudutsa mu Samariya.
Manokowere bíamor Semari weeron besho bín geyika b́tesh.
5 Iye anafika mʼmudzi wa Asamariya wotchedwa Sukari, pafupi ndi malo amene Yakobo anapatsa mwana wake Yosefe.
Mansh Ya'ak'ob b́naaysh Yosefsh b́ imts beyoku ganoke fa'u, Sikari ett s'egefu Semariy kituts b́weyi.
6 Chitsime cha Yakobo chinali pamenepo ndipo Yesu atatopa ndi ulendo anakhala pansi pambali pa chitsimecho. Nthawi inali pafupifupi ora lachisanu ndi chimodzi masana.
Manoknowere Yak'ob aats gop'o fa'e b́tesh, Iyesus werind sha'oke b́ mááwtsotse gop'man ganok beeb́dek'i, manoor gizewonwere shrt sa'atok'owi b́tesh.
7 Mayi wa Chisamariya atabwera kudzatunga madzi, Yesu anati kwa iye, “Kodi ungandipatse madzi akumwa.”
Manoor Semariy datsatsik wotts mááts iku aats kito gop'ok bweyi, Iyesuswere, «Úshet aatso taash ime!» bí eti
8 (Ophunzira ake nʼkuti atapita mʼmudzi kukagula chakudya).
Manoor b́ danifwots mish keewosh kito maand amtnibofa'o.
9 Mayiyo anati kwa Iye, “Inu ndinu Myuda ndipo ine ndine Msamariya. Bwanji mukundipempha madzi akumwa?” (Popeza Ayuda ndi Asamariya sankayanjana).
Semari dats ash wotts ashmanwere Iyesussh, «Nee n naaro ayhudi wotefetsat aawk'oneya tnaaro Semari wottsush ‹Úshi aatso taash ime!› etaat niatiri?» bí et, man bíetwere ayhudiwots Samrawino etefwotsnton ik woto bodeshawotsna.
10 Yesu anamuyankha kuti, “Koma iwe ukanadziwa mphatso ya Mulungu ndi Iye amene akukupempha madzi akumwa, ukanamupempha ndipo akanakupatsa madzi amoyo.”
Iyesuswere, «Ik'i imonat ‹Úshet aatso taash ime!› neesh etirwo koni b́wotstsok'o ndanink'e, bín k'oniyank'u neene bteshi, bíwere kash aatso neesh imank'e» bíet.
11 Mayiyo anati, “Ambuye, Inu mulibe kanthu kotungira madzi ndipo chitsime ndi chakuya. Kodi madzi amoyowo mungawatenge kuti?
Biwere hank'o etaat biaaniyi, «Doonzono! neewo bín kitet k'ac'o deshatsnere, gop'onuwere ayi dashan woke, eshe kash aatso eewkneya n datsiti?
12 Kodi Inu ndinu wamkulu kuposa kholo lathu Yakobo, amene anatipatsa chitsimechi ndipo iye ankamwanso monga anachita ana ake ndi ziweto zake?”
Nee gop'an imtso nonih Yak'obiyere bogfiya? Bína ett b́ nana'on, b́ minzwotswere gop'anitse úshrnee.»
13 Yesu anayankha kuti, “Aliyense amene amamwa madzi awa amamvanso ludzu,
Iyesus hank'o ettni bish bíaaniy, «Aatshan úshetu jamo ando aaniy shashwitwee,
14 koma aliyense amene adzamwa madzi amene Ine ndidzamupatsa sadzamvanso ludzu. Ndithudi, madzi amene ndidzamupatsa adzakhala kasupe wamadzi wotumphukira ku moyo wosatha.” (aiōn g165, aiōnios g166)
Taa timet aatso úshetwonmo dúre dúrosh b́ jamon shashweratse, taa ti imet aatso dúre dúrosh kasho bítse t'up'et aatse b́ wotiti.» (aiōn g165, aiōnios g166)
15 Mayiyo anati kwa Iye, “Ambuye, patseni madzi amenewo kuti ndisadzamvenso ludzu ndi kumabwerabe kuno kudzatunga madzi.”
Máátsmanwere, «Doonzono! haniye hakon aatso taan b́shashwirawok'o aaninwere kitosh hanok twarawok'o oona neesha man naari aatso taash ime!» bí et.
16 Iye anamuwuza kuti, “Pita kayitane mwamuna wako ndipo ubwere naye.”
Iyesuswere, «Amr n kenihi s'eede aniwowe» bíet.
17 Iye anayankha kuti, “Ine ndilibe mwamuna.” Yesu anati kwa iye, “Wakhoza ponena kuti ulibe mwamuna.
Ashmanwere, «Keniho deshatse» etaat bíaaniy. Manoor Iyesus hank'owa bish bíet, «Keniho deshatse niettsoniye arikee,
18 Zoona nʼzakuti iwe wakhala pa banja ndi amuna asanu, ndipo mwamuna amene uli naye tsopano si wako. Zimene wanenazi ndi zoona.”
Uts kenihwotsi detsfne b́teshi, and neenton fa'a ashonwere n kenihiyaliye, manshe ariko keewurne» bí eti.
19 Mayiyo anati, “Ambuye, ine ndazindikira kuti Inu ndinu mneneri.
Máátsmanwe hank'o bísh bíet, «Doonzono! nee nebiyiyo nwottsok'o andee t dani,
20 Makolo athu ankapembedza mʼphiri ili koma inu Ayuda mumati malo amene tiyenera kupembedzera ali ku Yerusalemu.”
Nonihots guranatsene Ik'o bok'ofoni, itmó ‹Ashuwots Ik'o k'ono boosh b́ geyitiye Iyerusalemitsne› etfte.»
21 Yesu anati, “Mayi inu khulupirira Ine. Nthawi ikubwera pamene inu simudzapembedza Atate mʼphiri ili kapena mu Yerusalemu.
Iyesuswere hank'wa bish bíet, «Nee ashune! Guranatse wee Iyerusalemitse Ik'o nihosh sagado it k'azet aawo b́ weetwok'oyish taan amanowe,
22 Inu Asamariya mumapembedza chimene simukuchidziwa. Ife timapembedza chimene tikuchidziwa, pakuti chipulumutso nʼchochokera kwa Ayuda.
It it daanawoshe it sagadiri, noomo kashet weero b́weet ayhudiwotsoke b́wottsotse no dants Ik'oshe nosagadiri.
23 Koma nthawi ikubwera ndipo yafika kale tsopano pamene opembedza woona adzapembedza Atate mu mzimu ndi mʼchoonadi, pakuti opembedza otere ndiwo amene Atate akuwafuna.
Ernmó arikon Ik'osh sagadirwots, Ik'o nihosh arikonat Shayirn bosagadit aawo weetwe, dab andoor waare, Ik'o nihonwere b́geyirwo hank'on bísh sagaditwotsiye.
24 Mulungu ndi Mzimu, ndipo omupembedza Iye ayenera kumupembedza mu mzimu ndi mʼchoonadi.”
Ik'o shayire, bísh sagadirwotswere shayironat arikon sagado boosh geyife.»
25 Mayiyo anati, “Ine ndikudziwa kuti Mesiya (wotchedwa Khristu) akubwera. Akabwera, Iye adzafotokoza zonse kwa ife.”
Máátsmanwere «Krstosi eteetso Mesihiyo b́weetuwok'o danfee, bí b́ woor jam keewo noosh keewitwe» bi et.
26 Ndipo Yesu anamuwuza kuti, “Amene ndikukuyankhulane, ndine amene.”
Iyesuswere «Hamb! and neenton keeweyirwo taahe bíne» bí et.
27 Pa nthawi yomweyo ophunzira ake anabwerera ndipo anadabwa kupeza Iye akuyankhula ndi mayi. Koma palibe amene anamufunsa kuti, “Kodi mukufuna chiyani?” kapena, “Nʼchifukwa chiyani mukuyankhula naye?”
Manoor b́ danifwots bo amtsoke aanat boweyi, Iyesus máátsunton b́ keeweyirwotse bo adi, wotowa bako, «Eege ngeyiri? Wee binton eegishe n keeweyiri?» ett bín attso konwor aali b́ tesh.
28 Kenaka mayiyo anasiya mtsuko wamadzi, nabwerera ku mzinda ndipo anati kwa anthu,
Maniye hakon máátsman b koro k'azk'rat́ kito maants amat́ ash ashosh hank'o bieti,
29 “Tiyeni mukaone munthu amene wandiwuza ine zilizonse zimene ndinazichita. Kodi ameneyu sangakhale Khristu?”
«T k'alts jamó taash keewts asho waar s'iilere! daneraka biye Krstosi wotifek'úna?»
30 Iwo anatuluka mʼmudziwo ndi kupita kumene kunali Iye.
Ashuwotswere kitotse kesht Iyesus maants boami.
31 Pa nthawi imeneyi ndi kuti ophunzira ake akumukakamiza kuti, “Rabi idyani.”
Manoor b́ danifwots Iyesussh, «Danifonó! ik jago mishok'o moowe» ett bok'oni.
32 Koma Iye anawawuza kuti, “Ine ndili ndi chakudya choti ndidye chimene inu simukuchidziwa.”
Bimó, «It danawo taa t meyiru móó detsfe» bíet.
33 Ndipo ophunzira ake anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Kodi alipo wina amene anamubweretsera Iye chakudya?”
Mansh b́ danifwots, «Asho bísh misho dek'waatso fa'ak'úna?» bo eti.
34 Yesu anati, “Chakudya changa ndikuchita chifuniro cha Iye amene anandituma Ine ndi kumaliza ntchito yake.
Iyesuswere boosh hank'owo bí et, «Tiko mishoniye taan woshtso ettso k'alona ett b́ finono s'eentsone.
35 Kodi inu simunena kuti, ‘Kwatsala miyezi inayi ndipo kenaka kukolola?’ Ine ndikukuwuzani kuti, tsekulani maso anu ndipo muyangʼane mʼminda! Mbewu zacha kale kuti zikololedwe.
It ‹Haniyak awd shasho orere, maniye hakone maay k'ees'o b́bodeti› etirutosha? Taamó ‹Aab kaaw de'er mááykatswots k'es'osh bobodtsok'o s'iilere› etirwe itsha.
36 Ngakhale tsopano amene akukolola akulandira malipiro ake, ndipo akututa mbewu ku moyo wosatha kuti wofesa ndi wokolola asangalale pamodzi. (aiōnios g166)
K'es'irwo bí angi k'awntso dek'etwe, dúre dúri bewosh wotit shuwo ko'itwe, mansha shokirwonat, k'es'irwonton tohar gene'uwitúne. (aiōnios g166)
37 Nʼchifukwa chake mawu akuti, ‘Wina amafesa ndipo wina amakolola’ ndi woona.
Hnk'o b́ wottsotse ‹Iko shoketwe, k'osho k'es'etwe› eteetso arikee.
38 Ine ndinakutumani kukakolola zimene simunagwirire ntchito. Ena anagwira ntchito yolemetsa ndipo inu mwatuta phindu la ntchito yawo.”
Taawere it bíats it shamberawo it k'es'etwok'o itn woshere, k'oshwots finon bomaawi, itmo bomawtsatse shuwo it meyi.»
39 Asamariya ambiri ochokera mʼmudziwo anakhulupirira Iye chifukwa cha umboni wa mayiyo wakuti, “Iye anandiwuza ine zonse ndinazichita.”
Máátsunwere «T k'alts jamo taash keewure» etaat b gawtsok'on kit manitsere ankat Samari dats ashuwots bín bo amani.
40 Choncho Asamariya atabwera kwa Iye, anamuwumiriza Iye kuti akhale nawo, ndipo Iye anakhala nawo masiku awiri.
Samari datsatsi ashuwots Iyesusok bo waatsok'on bonton b́ beetuewk'o bok'oni, bíwere git aawo manoke b́ teshi.
41 Ndipo chifukwa cha mawu ake, ena ambiri anakhulupirira.
Bí aap'atse tuutsatse k'osh ankat ashonwere bín bo amani.
42 Iwo anati kwa mayiyo, “Ife sitikukhulupirira chifukwa cha mawu ako okha, koma tsopano ife tadzimvera tokha, ndipo tikudziwa kuti munthu uyu ndithu ndi Mpulumutsi wa dziko lapansi.”
Ashmanshowere «Hniye hakon bín no amanitiye nee noosh n keewtsoshaliye no notookon noshishtsonat arikon datsani kashitwo bín b́wottsok'o no dantsotsne.» boeti.
43 Patatha masiku awiri Iye anachoka napita ku Galileya.
Iyesus Semariy datsatse git aawo b́ teshihakon Gelil datso maantsan bíami.
44 (Tsopano Yesu mwini ananena kale kuti mneneri salandira ulemu mʼdziko lake).
Bí b́ tookon «Nebiyiwo b́ took datsatse mangiyerakee» ett keewre b́tesh.
45 Iye atafika ku Galileya, Agalileya anamulandira. Iwo anali ataona zonse zimene anazichita mu Yerusalemu pa phwando la Paska, pakuti iwonso anali komweko.
Gelil maants b́bodtsok'onmó Gelil dats ashuwots mangon bín bodek'i, han b́wotwere Fazig baliwots Iyerusalem maants amt boteshor bi manoke b́ k'alts jamo bek't boteshtsotsná.
46 Iye anakafikanso ku Kana wa ku Galileya, kumene anasanduliza madzi kukhala vinyo. Ndipo kumeneko kunali nduna ina ya mfumu imene mwana wake wamwamuna anali chigonere akudwala ku Kaperenawo.
Maniye hakon Iyesus aatso weyini biro maants b́wonits datsu Gelil datsatse fa'a K'aan kitu maants aani aanat b́weyi, manoor K'frnahomn b́ na'o b́shirotse shodtso mengsti mootse naash iko fa'e b́ tesh.
47 Munthu uyu atamva kuti Yesu wafika ku Galileya kuchokera ku Yudeya, anapita kwa Iye, namupempha kuti apite akachiritse mwana wakeyo, amene anali pafupi kufa.
Bíwere Iyesus Yihud datsatse Gelil datsats b́wowo shisht b́ maants bíam, K'frnahom maants ood'r ayidek't shodt k'irosh etirwo b́ na'o bísh b́kashiytwok'o Iyesusi b́k'oni.
48 Yesu anawawuza iwo kuti, “Anthu inu pokhapokha mutaona zizindikiro zodabwitsa, simudzakhulupirira.”
Iyesuswere «It adits keewonat milikito it bek'ala bako eegonor amaneratste!» bíet.
49 Nduna ya mfumuyo inati, “Ambuye tiyeni mwana wanga asanafe.”
Naashmanúwere «Doonzono! t na'o b́ k'irftsre oona neesha kaari ood'e» bíet.
50 Yesu anayankha kuti, “Pita. Mwana wako adzakhala ndi moyo.” Munthuyo anakhulupirira mawu a Yesu ndipo ananyamuka.
Iyesuswere «N moo maants amee! n na'o kashon fa'e» bíet. Ashmanwere Iyesus aap'tso amanat b́ moo maants bíami.
51 Iye ali pa njira, antchito ake anakumana naye, namuwuza kuti mwana wanu uja wachira.
Bíamfere b́guutswots weerindatse daatsdek't «N na'o kashwtsere» ett bísh keew bok'ri.
52 Iye atafunsa kuti ndi nthawi yanji imene mwana wake anapeza bwino, iwo anati kwa iye, “Malungo anamusiya iye dzulo pa ora lachisanu ndi chiwiri.”
Bíwere b́ na'o b́ shamp'ts sa'ato boon bíaati. Bowere «Oots shawat sa'atatse atsik'es'o bínfakshb́k'riye» boet.
53 Ndipo bamboyo anazindikira kuti iyi inali nthawi yomweyo imene Yesu anati kwa iye, “Mwana wako adzakhala ndi moyo.” Choncho iye ndi onse a pa banja lake anakhulupirira.
Nihonwere, Iyesus «N na'o kashon fa'e» bíettso manoori sa'aton b́wottsok'owo danb́k'r, mansh manots aawon detst bínat b́maa ashon Iyesusi aman bok'ri.
54 Ichi ndiye chinali chizindikiro chodabwitsa chachiwiri chimene Yesu anachita atafika ku Galileya kuchokera ku Yudeya.
Aditshan Iyesus Yhud datsatse Gelil datsomants waat b́k'alts gitloniye.

< Yohane 4 >