< Yohane 3 >
1 Ndipo panali Mfarisi wotchedwa Nekodimo, wa mʼgulu lolamulira la Ayuda.
Teo t’indaty mpiamo Fariseoo, i Nikodemosy ty tahina’e, mpifehe amo Jiosio,
2 Iye anabwera kwa Yesu usiku ndipo anati, “Rabi, ife tikudziwa kuti ndinu aphunzitsi wochokera kwa Mulungu, pakuti palibe amene angachite zizindikiro zodabwitsa zimene Inu mukuchita ngati Mulungu sali naye.”
niheo mb’amy Iesoà mb’eo hàleñe, le nanoa’e ty hoe: O Talè, fohi’ay te mpañòke hirik’ aman’ Añahare irehe; amy te tsy eo ty hahatafetetse o viloñe anoe’oo naho tsy aman’ Añahare.
3 Poyankha Yesu ananena kuti, “Zoonadi, Ine ndikukuwuza kuti, ngati munthu sabadwanso mwatsopano sangathe kuona ufumu wa Mulungu.”
Hoe ty natoi’ Iesoà aze: Eka! To o itaroñakoo, naho tsy asamake indraike t’indaty, le tsy hahaoniñe i Fifehean’ Añaharey re.
4 Nekodimo anati, “Kodi munthu angabadwenso bwanji atakalamba? Kodi angalowe kachiwiri mʼmimba ya amayi ake kuti abadwenso?”
Aa hoe t’i Nikodemosy ama’e: Aia ty hahatolia’ ondaty, ie fa bey? Hahafimoake an-tron-drene’e ao fañindroe’e hao re hasamake?
5 Yesu anayankha kuti, “Zoonadi, Ine ndikukuwuza kuti ngati munthu sabadwa mwa madzi ndi Mzimu Woyera, sangalowe mu ufumu wa Mulungu.
Tinoi’ Iesoà: Eka! to t’itaroñako t’ie tsy asamak’ ami’ty rano naho amy Arofoy le tsy hahazilike amy Fifehean’ Añaharey.
6 Thupi limabereka thupi, koma Mzimu amabereka mzimu.
Ze nasama’ ty nofotse ro nofotse, fe ze nasama’ i Arofoy ro arofo.
7 Iwe usadabwe chifukwa ndakuwuza kuti, ‘Uyenera kubadwanso.’
Ko ilatsà’o i nitaroñakoy ty hoe: Tsy mahay tsy asamake boak’ añ’abo nahareo.
8 Mphepo imawomba kulikonse kumene ikufuna. Ungathe kumva kuwomba kwake, koma sungathe kudziwa kumene ikuchokera kapena kumene ikupita. Nʼchimodzimodzi ndi amene abadwa ndi Mzimu Woyera.”
Mitiok’ amy ze nahi’e i tiokey, mahajanjiñe ty feo’e irehe, fe tsy oni’o ty nihirifa’e ndra ty handoaha’e; izay ka ze hene nasama’ i Arofoy.
9 Nekodimo anafunsa kuti, “Kodi izi zingatheke bwanji?”
Hoe ty natoi’ i Nikodemosy, Aia ty hahamete izay?
10 Yesu anati, “Iwe mphunzitsi wa Israeli, kodi sukuzindikira zimenezi?
Hoe ty natoi’ Iesoà: Ihe mpañoke Israele hao ro tsy maharendreke o raha zao?
11 Zoonadi, Ine ndikukuwuza kuti ife tiyankhula zimene tikuzidziwa ndi kuchitira umboni zimene taziona, komabe inu simuvomereza umboni wathu.
Eka! to t’itaroñako te volañe’ay o fohi’aio vaho talilie’ay o nitrea’aio, fe tsy antofe’ areo o taro’aio.
12 Ine ndikuyankhula kwa iwe zinthu za dziko lapansi ndipo sukukhulupirira. Nanga kodi udzakhulupirira bwanji ngati nditayankhula zinthu zakumwamba?
Aa naho itaroñako raha an-tane atoio, fa tsy antofe’ areo, le aia ty hahatokisa’ areo te itaroñako rahan-dindìñe ao?
13 Palibe wina aliyense anapita kumwamba, koma yekhayo amene watsika kuchokera kumwamba, Mwana wa Munthu.
Toe tsy eo ty nionjoñe mb’andindìñe ey naho tsy i nizotso hirik’ andikerañey, toe i Ana’ Ondatiy.
14 Tsono monga Mose anapachika njoka mʼchipululu, moteronso Mwana wa Munthu ayenera kupachikidwa,
Manahake ty nañonjona’ i Mosè i mereñe am-patrambey añey, ro tsi-mete tsy hañengañe i Ana’ Ondatiy.
15 kuti aliyense amene akhulupirira Iye akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Soa te, hanan-kaveloñe nainai’e iaby naho tsy ho momoke ze miato ama’e. (aiōnios )
16 “Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi, kotero anapereka Mwana wake wobadwa yekha, kuti aliyense wokhulupirira Iye asatayike koma akhale ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Akore ty hakokoan’ Añahare ty voatse toy, kanao nitolora’e i lahy bako-toka’ey, soa tsy haito ze miato ama’e fa hanan-kaveloñe nainai’e. (aiōnios )
17 Pakuti Mulungu sanatume Mwana wake ku dziko lapansi, kuti akaweruze, koma kuti akapulumutse dziko lapansi.
Tsy nirahen’ Añahare mb’ ami’ty voatse toy hamàtse ty voatse toy i Anakey; fa t’ie ho fandrombahañe ty voatse toy.
18 Aliyense wokhulupirira Iye saweruzidwa, koma aliyense wosakhulupirira waweruzidwa kale chifukwa sanakhulupirire dzina la Mwana wobadwa yekha wa Mulungu.
Tsy hafàtse ze miato ama’e; fa nafàtse ka ty tsi-miato, amy te tsy natokisa’e ty tahina’ i Ana-dahi-bako tokan’ Añaharey.
19 Ndipo chiweruzo ndi ichi: kuwunika kunabwera mʼdziko lapansi, koma anthu anakonda mdima mʼmalo mwa kuwunikako, chifukwa ntchito zawo zinali zoyipa.
Zao o fàtseo, te nivotrak’ an-tane atoy i hazavàñey fe nitea’ ondatio o ieñeo te amy hazavàñey, ie raty sata.
20 Aliyense wochita zoyipa amadana ndi kuwunika, ndipo sabwera poyera chifukwa cha mantha kuti ntchito zake zingaonekere.
Heje’ ze hene mpanao ratio i hazavàñey, ie tsy miheo mb’amy hazavàñey tsy mone ho ventareñe o sata-rati’eo.
21 Koma aliyense wokhala mu choonadi amabwera ku kuwunika, kuti zionekere poyera zimene iye wachita zachitika kudzera mwa Mulungu.”
Fe mb’amo hazavàñeo ty manao to, hampidodeàñe o fitoloña’eo, t’ie nanoeñe aman’ Añahare.
22 Zitatha izi, Yesu ndi ophunzira ake anapita mʼmadera a ku midzi ya ku Yudeya, kumene Iye anakhala kanthawi akubatiza.
Ie añe, le nomb’an-tane’ Iehodà mb’eo t’Iesoà rekets’ o mpiama’eo le nitamañe añe miharo am’ iereo vaho nampilipotse.
23 Ndipo Yohane amabatizanso ku Ainoni kufupi ndi Salimu, chifukwa kumeneko kunali madzi ambiri ndipo anthu amabwererabwererabe kudzabatizidwa.
Nampilipotse e Ainone marine i Saleime añe ka t’i Jaona, amy t’ie maro rano, le nimb’ama’e mb’eo iareo vaho nampiliporeñe.
24 (Apa nʼkuti Yohane asanatsekeredwe mʼndende).
Mbe tsy nafetsak’ an-drohy ao hey t’i Jaona.
25 Mkangano unabuka pakati pa ophunzira ena a Yohane ndi Ayuda ena pa zamwambo wodziyeretsa wa Ayuda.
Ie amy zao nifandietse amo fañaliovañeo o Tehodao naho o mpiamy Jaonao.
26 Iwo anabwera kwa Yohane anati, “Rabi, munthu uja munali naye mbali inayo ya mu mtsinje wa Yorodani, amene munamuchitira umboni, taonani naye akubatizanso, ndipo aliyense akupita kwa Iye.”
Aa le nimb’ amy Jaona iereo, nanao ty hoe: O Raby, i nindre ama’o alafe’ Iordaneiy, i nitalilie’oy, inao, ie ka ro mampilipotse, le kila mb’ama’e mb’eo.
27 Atamva zimenezi, Yohane anayankha kuti, “Munthu amalandira chokhacho chapatsidwa kwa iye kuchokera kumwamba.
Hoe ty natoi’ i Jaona: Tsy maha-rambe ndra inoñ’ inoñe t’indaty naho tsy natolots’aze boak’ andindìñe añe.
28 Inuyo ndinu mboni zanga kuti ine ndinati, ‘Ine sindine Khristu koma ndatumidwa patsogolo pa Iye.’
Inahareo ro valolombeloñe te nitaroñeko ty hoe, Tsy izaho i Norizañey, fa nahitrike ho fiaolo’e.
29 Mwini wake wa mkwatibwi ndi mkwati. Ndipo bwenzi lamkwati limadikira ndi kumvetsera iye, ndipo amakondwa akamva mawu a mkwatiyo. Ine changa ndi chimwemwe ndipo ndine wosangalala kwambiri.
Talè’ ty enga-vao ty mpañenga; mijohañe eo naho mitsendreñe aze ty rañe’ i mpañengay, le mahavaranehake aze ty fiarañanaña’ i mpañengay; izay ty mañeneke o haehakoo.
30 Nʼkoyenera kuti Iyeyo akule, ine ndichepe.
Mahity te ie ty haonjoñe vaho izaho ty hareke.
31 “Iye wochokera kumwamba ndi wapamwamba pa onse: iye wochokera mʼdziko lapansi ndi wa dziko lapansi, ndipo amayankhula monga mmodzi wa adziko lapansi. Iye wochokera kumwamba ndi wopambana onse.
Ambone’ ze he’e i hirik’ amboney. Le a ty tane toy ty hirik’an-tane atoy, vaho ty tane toy ro fisaontsie’e; lohà’ ze he’e i boak’ andindìñey.
32 Iye achita umboni pa zimene waziona ndi kuzimva, koma palibe avomereza umboni wake.
Ze nivazoho’e naho nijanjiñe’e ro taroñe’e; fe tsy eo ty mandrambe i taro’ey.
33 Munthu amene amawulandira akutsimikizira kuti Mulungu ndi woona.
I niantoke i taro’eiy ty namolitomboke te to t’i Andrianañahare.
34 Pakuti amene Mulungu wamutuma amayankhula mawu a Mulungu; Mulungu wamupatsa Mzimu Woyera mopanda malire.
Saontsie’ i nahitrin’ Añaharey o tsaran’ Añahareo, amy te tsy arañen’ Añahare ty fanolorañe i Arofoy.
35 Atate amakonda Mwana ndipo apereka zonse mʼmanja mwake.
Kokoan-dRae i Anakey vaho kila natolo’e am-pità’e.
36 Aliyense wokhulupirira Mwanayo ali ndi moyo wosatha, koma iye amene samvera Mwanayo sadzawuona moyo, pakuti mkwiyo wa Mulungu umakhala pa iye.” (aiōnios )
Aman-kaveloñe nainai’e ty miato amy Anakey; fe tsy hahaisake i haveloñey ty manjehatse i Anakey, ie mb’e fehe’ ty haviñeran’ Añahare. (aiōnios )