< Yohane 20 >
1 Mmamawa tsiku loyamba la sabata, kukanali kamdimabe, Mariya wa ku Magadala anapita ku manda ndipo anaona kuti mwala unali utachotsedwa pa khomo la manda.
Ülycümne ts'ettiyne yiğıl, vacarıl, çakra miç'eer, Magdaleençena Mayram mağareene nyuq'vnesqa ayreele. Məng'ık'le g'aye mağarayne ghalençe g'avşu g'ooce.
2 Choncho anabwerera akuthamanga kwa Simoni Petro ndi wophunzira winayo, amene Yesu anamukonda, ndipo anati, “Iwo amuchotsa Ambuye mʼmanda, ndipo ife sitikudziwa kumene iwo amuyika Iye!”
Mana zaara g'adarxhun, Şimon-Pyoturneyiy I'says geer ıkkanne şene telebayne k'anyaqa qarı, manbışik'le eyhen: – Yişda Xərna mağareençe qıkkıvur, nyaqa qıkkiyid şak'le ats'a deş.
3 Choncho Petro ndi wophunzira winayo ananyamuka kupita ku manda.
Pyoturiy manasa teleba g'aqa qığeepç'ı, mağaraysqana avayk'an.
4 Onse awiri anathamanga pamodzi koma wophunzira winayo anamupitirira Petro, nafika ku manda moyambirira.
Mana q'öyürsana sacigee g'adaaxvan vooxhe. Şena teleba Pyoturele sik'ırra zaara ı'ğiykır, mağaraysqa ögil hiyxhar.
5 Ndipo mmene anawerama nasuzumira mʼkati mwa manda anaona nsalu zili potero koma sanalowemo.
Mana k'yorzul aqa ilyakkımee katanıke hav'una kafan ab g'ooce, vucme aqa ikkeç'e deş.
6 Kenaka Simoni Petro, amene anali pambuyo pake, anafika ndi kulowa mʼmanda. Iye anaona nsaluzo zili pamenepo,
Mang'uqar qihna Şimon-Pyotur qarı, mağareeqa ikkeç'e. Mang'uk'le avxuna kafaniy
7 pamodzinso ndi nsalu imene anakulungira nayo mutu wa Yesu. Nsaluyi inali yopindidwa pa yokha yosiyanitsidwa ndi inayo.
I'sayne vuk'lelqa gyuvxhuna desmal g'ooce. Desmal sav'u kafanıke curayba gyuvxhu vuxha.
8 Pomaliza wophunzira winayo, amene anafika ku manda moyambirira, analowanso mʼkati, iye anaona ndi kukhulupirira.
Manke mağaraysqa ögil qarına şena telebar aqa ikkeç'e. Mang'uk'le man g'acu, inyam ha'a.
9 (Iwo sanazindikire kuchokera mʼmalemba kuti Yesu anayanera kuuka kuchokera kwa akufa).
Manbışe I'sa hapt'ıynbışde yı'q'neençe oza qixhesva, Muq'addasne Otk'unee otk'unin ciga yugda vuk'leeqa k'eççu ıxha deş.
10 Kenaka ophunzira anabwerera ku nyumba zawo,
Qiyğa telebabı xaybışeeqa siviyk'al.
11 koma Mariya anayima kunja kwa manda akulira. Pamene akulira, anawerama ndi kusuzumira mʼmanda
Mayram mağareene nyuq'vnesne geeşe ulyorzul yixha. Mana geeşe-geeşe kyorzul mağarayne aqa ileeka.
12 ndipo anaona angelo awiri atavala zoyera, atakhala pamene panali mtembo wa Yesu, mmodzi kumutu ndi wina kumapazi.
Maa'ar cagvaran karbı ali'ına q'öyre malaaik g'ece. Manbışda sa I'sayn mayıt gixhxhiyne cigayne vuk'ulynane cigee, manasar g'elybınane cigee gyu'ur ıxha.
13 Iwo anamufunsa iye kuti, “Amayi, nʼchifukwa chiyani mukulira?” Iye anati, “Amuchotsa Mbuye wanga, ndipo ine sindikudziwa kumene iwo amuyika.”
Manbışe qiyghan: – Zəiyfa, nya'a geeşe? Mayrameeyid manbışik'le eyhen: – Yizda Xərna nyuq'vneençe qıkkıvur, nyaqa gixhxhıyid ats'a deş.
14 Atanena izi, iye anatembenuka ndipo anaona Yesu atayima potero koma iye sanazindikire kuti anali Yesu.
Man uvhu yı'q'əlqa ileekıyle qiyğa, I'sa maa ulyorzul g'ece. Yic mana I'sa ıxhay cek'le ats'axhxhe deş.
15 Iye anati, “Amayi, mukulira chifukwa chiyani? Ndani amene mukumufunafuna?” Poganiza kuti anali mwini munda, iye anati, “Bwana, ngati inu mwamuchotsa, ndiwuzeni kumene mwamuyika, ndipo ine ndikamutenga.”
I'see məng'ıke qiyghanan: – Zəiyfa, nya'a geeşe? Vuşune t'abal ha'a? Mayramık'le Mana bağban ıxhay ats'axhxha, eyhen: – Xərna, ğu Mana qıkkıxheene, nyaqayiy gixhxhı zak'le eyhe, zınar hark'ın Mana alyart'as.
16 Yesu anati kwa iye, “Mariya.” Anatembenukira kwa Iye nafuwula mu Chiaramaiki kuti, “Raboni!” (kutanthauza Mphunzitsi).
I'see məng'ık'le eyhen: – Mayram! Manar sayk'ı, I'sayk'le cühüt'yaaşine mizel eyhen: – Ravvuni! (Mə'əllimva eyhen vodun.)
17 Yesu anati, “Usandigwire Ine, pakuti sindinapite kwa Atate. Mʼmalo mwake pita kwa abale anga ndikukawawuza kuti, ndikupita kwa Atate ndi kwa Atate anunso, kwa Mulungu wanga ndi Mulungu wanunso.”
I'see məng'ı'k'le eyhen: – Zı ıqmaqqa, Zas Dekkısqa ılqeç'es ıkkan. Yizde çocaaşisqa hark'ın, manbışik'le eyhe: «Yizde Dekkıne – vuşde Dekkıne, Yizde Allahne – vuşde Allahne k'anyaqa ılqəə».
18 Mariya wa ku Magadala anapita kwa ophunzira ndi uthenga wakuti, “Ndamuona Ambuye!” Iye anawawuza iwo kuti Yesu ananena zinthu izi kwa iye.
Magdaleençena Mayram telebabışde k'anyaqa qarı, manbışik'le eyhen: – Zak'le yişda Xərna g'acu! Mang'vee cek'le hucoovayiy uvhu, man yuşan ha'an.
19 Madzulo a tsiku limenelo limene linali loyamba la Sabata ophunzira ake ali pamodzi, atatseka ndi kukhoma zitseko chifukwa choopa Ayuda, Yesu anabwera ndi kuyima pakati pawo nati, “Mtendere ukhale nanu!”
Ülycümne ts'ettiyne yiğıne, vacarne exhal, Yahudeeşine ç'ak'ınbışile qəvəyq'ənva, telebabınane cigayn akka qı'ı eyxhe. Sayır sayangara maqa I'sa arayle. Mana yı'q'nee ulyorzul eyhen: – Şos salam vuxhena!
20 Iye atatha kunena izi, anawaonetsa manja ake ndi mʼnthiti mwake. Ophunzira anasangalala kwambiri pamene anaona Ambuye.
Manıd uvhu, telebabışik'le Cun xıleppıyiy ak'vaa hagva. Telebabışik'ler yişda Xərna g'acu, şadeebaxhenbı.
21 Yesu anatinso, “Mtendere ukhale nanu! Monga Atate anandituma Ine, Inenso ndikukutumani.”
I'see manbışik'le meed eyhen: – Şos salam vuxhena! Dekkee Zı g'axuvuyn xhinne, Zınab şu g'uxoole.
22 Ndi mawu amenewo Iye anawapumira ndipo anati, “Landirani Mzimu Woyera.
Manıd uvhuyle qiyğa, I'see manbışilqa uf av'u, eyhen: – Muq'addasın Rı'h aleet'e!
23 Ngati mukhululukira aliyense machimo ake, iwo akhululukidwa; ngati simuwakhululukira, iwo sanakhululukidwe.”
Şavneyiy şu bınahıle ılğeepç'ı, manbışda bınah havaakalasda, şavneyiy bınahıle şu ılyhıdeepç'ı, manbışda bınah havaakalas deş.
24 Koma Tomasi (otchedwa Didimo), mmodzi wa khumi ndi awiriwo, sanali ndi ophunzira pamene Yesu anabwera.
Yıts'ıq'vəne telebayna sa eyxhena Q'ömkale donana Tomas, I'sa arımee, manbışde k'ane ıxha deş.
25 Ophunzira enawo atamuwuza Tomasi kuti iwo anaona Ambuye, iye ananenetsa kuti, “Pokhapokha nditaona zizindikiro za misomali mʼmanja ake ndi kuyikamo chala changa mʼmene munali misomali ndi kukhudza dzanja langa mʼnthiti mwake, ine sindidzakhulupirira.”
Manesa telebabışe Tomasık'le «Yişda Xərna g'acuva» uvhumee, mang'vee eyhen: – G'adaxbışe Mang'une xılepbışik hı'iyn cigabı g'ıdecu, mançik zı t'ub sidyoot'eene, ak'vaaykıd xıl qidet'veene, şu eyhençilqa zı hayexhe deş.
26 Patapita sabata, ophunzira ake analinso mʼnyumbamo ndipo Tomasi anali nawo. Ngakhale makomo anali otsekedwa, Yesu anabwera nayima pakati pawo, ndipo anati, “Mtendere ukhale nanu!”
Molyne yiğıle I'sayn telebabı meeb xaa sacigeeqa sabımee, Tomasır manbışika eyxhe. Akkabı qı'ı ıxheeyid, I'sa aqa ikkeç'ena. Mana yı'q'nee ulyorzul eyhen: – Şos salam vuxhena!
27 Kenaka anati kwa Tomasi, “Ika chala chako apa; ona manja anga. Tambasula dzanja lako ndi kukhudza mʼnthiti mwanga. Leka kukayika, khulupirira.”
Mançile qiyğa Tomasık'le eyhen: – T'ub inyaqa hopke, Yizde xıleppışiqa ilekke. Xılid hotku, Yizde ak'vaalqa gixhxhe. İnyam deşda mexhe, inyamnana ixhe!
28 Tomasi anati kwa Iye, “Ambuye wanga ndi Mulungu wanga!”
Tomasee Mang'us alidghıniy qele: – Ğu yizda Rəbb, yizda Allah vor!
29 Kenaka Yesu anamuwuza kuti, “Kodi wakhulupirira chifukwa wandiona Ine? Ndi odala amene amakhulupirira ngakhale asanaone.”
I'see mang'uk'le eyhen: – Vak'le Zı g'acuynçil-allane inyam hı'ı? G'ıdecu inyam ha'anbı nimee baxtivarariy!
30 Yesu anachita zodabwitsa zambiri pamaso pa ophunzira ake zimene sizinalembedwe mʼbuku lino.
I'see telebabışde ulene ögil medın geed əlaamatbı hagu, manbı ine kitabee otk'un deş.
31 Koma izi zalembedwa kuti mukhulupirire kuti Yesu ndi Khristu, Mwana wa Mulungu, ndi kuti mukakhulupirira mukhale nawo moyo mʼdzina lake.
İnyaa otk'uninbı, mançil-alla otk'un, I'sa Masixh ıxhalqa, Allahna Dix ıxhalqa şu inyam he'ecen. Mang'une doyulqa inyam he'ee, şoqa gırgıne gahbışisda ı'mı'r vuxhes.