< Yohane 2 >
1 Pa tsiku lachitatu munali ukwati mu Kana wa ku Galileya. Amayi ake a Yesu anali komweko,
Eso aduna aligili, Ga: ina moilai (Ga: lili sogega) amo ganodini ilia uda lasu hou hamosu. Yesu Ea ame amoga misi esalu.
2 ndipo Yesu ndi ophunzira ake anayitanidwanso ku ukwatiwo.
Lolo nasu ouligisu dunu da Yesu, Ea ado ba: su dunu, ilima misa: ne sia: i dagoiba: le, ilia misi esalu.
3 Vinyo atatha, amayi a Yesu anati kwa Iye, “Wawathera vinyo.”
Be waini hano huluane na dagoiba: le, Yesu Ea ame Ema amane sia: i, “Ilia waini huluane da na dagoiba: le ebelei.”
4 Yesu anayankha kuti, “Amayi, chifukwa chiyani mukundiwuza Ine? Nthawi yanga sinakwane.”
Be Yesu da bu adole i, “Na hawa: hamomu dia abuliba: le adosala: ? Na ilegei eso da hame doaga: i.”
5 Amayi ake anati kwa antchito, “Inu muchite chilichonse chimene akuwuzeni.”
Yesu Ea: me da hawa: hamosu dunuma amane sia: i, “Ea adosea dilia hamoma!”
6 Pamenepo panali mitsuko yamiyala yothiramo madzi isanu ndi umodzi, imene Ayuda amagwiritsa ntchito pa mwambo wodziyeretsa. Uliwonse unali ndi malita 100 kapena kupitirirapo.
Yu dunu ilia lobo dodofesu hou sema bagade dialu. Amo hou hamoma: ne ofodo da gafeyale gala dialu. Ofodo afae afae da hano100lidase (litres) agoane sogasalasea nabai ba: i.
7 Yesu anati kwa antchitowo, “Dzazani madzi mʼmitsukoyi,” ndipo iwo anadzaza ndendende.
Yesu da hawa: hamosu dunu ilima amane sia: i, “Amo ofodo gafeyale gala amoga hano sogasalawane, nabama!” Amalalu, ilia hano sogasalawane, ofodo da nabaidafa ba: i.
8 Ndipo Iye anatinso kwa iwo, “Tsopano tungani ndipo kaperekeni kwa mkulu waphwando.” Iwo anachita momwemo.
Amalalu, Yesu da ilima amane adole i, “Defea! Wali amo ofodoga hano dili, gaguli asili, lolo Nasu aowasu dunuma ima.” Ilia da Ea sia: i defele hamoi.
9 Mkulu waphwando analawa madziwo amene anasandulika vinyo, ndipo sanazindikire kumene vinyoyo anachokera, ngakhale kuti antchito amene anatunga madziwo amadziwa. Kenaka anayitanira mkwati pambali
Lolo Nasu ouligisu dunu da hano afadenene, bu waini hano hamoi, amo na ba: i. Waini da habidili misi, aowasu dunu da hame dawa: i (be hawa: hamosu dunu da hano dili iabeba: le dawa: i). Amalalu e da uda lamu dunuma amane wele sia: i,
10 ndipo anati, “Aliyense amatulutsa vinyo wokoma kwambiri poyambirira ndipo kenaka vinyo wosakoma pamene oyitanidwa atamwa kale wambiri; koma iwe wasunga wokoma mpaka tsopano.”
“Dunu huluane da hidadea waini hano ida: iwane sagole, fa: no ilima misi dunu da bagadewane na dagoiba: le, ilia da wadela: i waini hano sagosa. Be dia hou da hisu. Di da fa: nodafa waini baligili ida: iwane gala ninima iaha!”
11 Ichi chinali chizindikiro chodabwitsa choyamba chimene Yesu anachita ku Kana wa ku Galileya. Potero Iye anawulula ulemerero wake, ndipo ophunzira ake anamukhulupirira Iye.
Ga: ina moilai, Ga: lili soge ganodini, amoga Yesu da amo degabo gasa bagade musa: hame ba: su hou hamoi dagoi. E da Ea hadigi olelebeba: le, Ea ado ba: su dunu da Ea hou dafawaneyale dawa: i galu.
12 Zitatha izi Iye anatsikira ku Kaperenawo pamodzi ndi amayi ake, abale ake ndi ophunzira ake. Iwo anakhala kumeneko masiku owerengeka.
Amohaga fa: no, Yesu, Ea ame, Ea eya, amola Ea ado ba: su dunu, eso bagahame oualigimusa: , Gabena: iame moilaiga asi.
13 Nthawi ya Paska ya Ayuda itayandikira, Yesu anapita ku Yerusalemu.
Baligisu Lolo Nasu gilisimu da gadeneiba: le, Yesu da Yelusaleme moilai bai bagadega asi.
14 Mʼbwalo la Nyumba ya Mulungu Iye anapeza anthu akugulitsa ngʼombe, nkhosa ndi nkhunda ndipo ena akusintha ndalama pa matebulo.
Debolo Diasu ganodini, E da dunu ilia bulamagau, sibi, amola musuni bidi lalebe ba: i. Eno dunu ilia fafai amoga fili, muni afadenene iasu hou hamonanebe ba: i.
15 Chifukwa cha zimenezi Iye anapanga chikwapu cha zingwe ndipo anatulutsa onse mʼbwalo la Nyumbayo, pamodzi ndi nkhosa ndi ngʼombe; Iye anamwaza ndalama zawo ndi kugudubuza matebulo.
Amalalu, Yesu da efega fegasu hamone, ohe fi, bulamagau, amola sibi huluane gadili sefasi. E da muni bidi lasu dunu ilia fafai delegili fasili, ilia muni fage huluane gugudili fasi.
16 Kwa amene amagulitsa nkhunda, Iye anati, “Tulutsani izi muno! Osasandutsa Nyumba ya Atate anga msika!”
E da sio bidi lasu dunuma amane sia: i, “Sio huluane gadili gaguli masa! Na Ada ea diasu bidi lama: ne diasu agoane hamomu da defea hame! Yolesima!”
17 Ophunzira ake anakumbukira kuti zinalembedwa kuti, “Kudzipereka kwanga ku nyumba yanu kudzandiphetsa.”
Amalalu, Ea ado ba: su dunu da Gode Sia: Dedei amo bu dawa: i, amane, “Gode! Na dogo ganodini, Dia Diasu amoma asigi hou da lalu agoane nesa.”
18 Kenaka Ayuda anamufunsa Yesu kuti, “Kodi mungationetse chizindikiro chodabwitsa chotani chotsimikizira ulamuliro wanu wochitira izi?”
Yu ouligisu dunu da Yesuma amane adole ba: i, “Di da abuliba: le amo hou hamonanebela: ? Amo olelema: ne, di da adi dawa: digima: ne olelesu ninima olelema: bela: ?”
19 Yesu anawayankha kuti, “Gwetsani Nyumba ya Mulunguyi ndipo Ine ndidzayimanganso mʼmasiku atatu.”
Yesu E bu adole i, “Dilia amo Debolo Diasu mugulusia, Na da eso udiana amoga bu hiougili dagomu.”
20 Ayuda anayankha kuti, “Zinatenga zaka makumi anayi kumanga Nyumbayi, kodi Inu mungayimange masiku atatu?”
Ilia da fofogadigili amane sia: i, “Ola! Musa: dunu ilia ode 46 agoanega amo diasu gagui galu. Di da habodane eso udiana amoga bu gaguma: bela: ?”
21 Koma Nyumba ya Mulungu imene amanena linali thupi lake.
Be Yesu da Debolo Diasu Ea hou hame olelei. E da Ea da: i hodo da diasu agoane sia: i.
22 Iye ataukitsidwa kwa akufa, ophunzira ake anakumbukira zimene Iye ananena ndipo anakhulupirira Malemba ndi mawu amene Yesu anayankhula.
Amaiba: le, fa: nowane, Yesu E bogole, bu wa: legadoloba, Ea fa: no bobogesu dunu da amo sia: bu dawa: i galu. Dawa: beba: le, ilia Gode Sia: Dedei bu dawa: le, Yesu Ea sia: i dafawaneyale dawa: i.
23 Tsopano Iye ali mu Yerusalemu pa phwando la Paska, anthu ambiri anaona zizindikiro zodabwitsa zimene amachita ndipo anakhulupirira dzina lake.
Yesu da Baligisu Lolo Nasu amoha Yelusaleme moilai bai bagadega esaloba, dunu bagohame Ea gasa bagade dawa: digima: ne olelesu ba: beba: le, Ea hou dafawaneyale dawa: i.
24 Koma Yesu sanawakhulupirire iwo, pakuti amadziwa anthu onse.
Be Yesu da osobo bagade dunu ilia hou huluane dawa: beba: le, ilia lalegagui hou dafawaneyale hame dawa: i.
25 Iye sanafune umboni wa wina aliyense popeza amadziwa zomwe zinali mʼmitima mwa anthu.
Eno dunu da osobo bagade dunu ilia hou Ema olelemu da hamedeidafa. Bai Hisu, enoga mae oleleiwane, liligi huluane osobo bagade dunu ilia dogo ganodini dialebe, dawa: i galu.