< Yohane 18 >

1 Yesu atamaliza kupemphera, Iye anachoka ndi ophunzira ake ndi kuwoloka chigwa cha Kidroni. Kumbali inayo kunali munda wa Olivi, ndipo Iye ndi ophunzira ake analowamo.
I'see manva uvhuyle qiyğa telebabışika sacigee Qidronne q'adaaline manisa suralqa ılğeç'e. Maa sa bağ eyxhe. I'sayiy telebabı maqa ikkeebaç'e.
2 Tsopano Yudasi, amene anamupereka amadziwa malowo chifukwa Yesu ankakumana ndi ophunzira ake kumeneko.
I'sa hımva eyhesse telebabışika maqa arayle ıxha. I'sa merıng'une xılyaqa qelesde Yahudayk'led mançil-alla man ciga ats'anniy.
3 Choncho Yudasi anabwera ku munda, akutsogolera gulu la asilikali ndi akuluakulu ena ochokera kwa akulu a ansembe ndi Afarisi. Iwo anali atanyamula miyuni, nyale ndi zida.
Məxür Yahuda maqa sa deste eskeraaşika, sayib kaahinaaşine ç'ak'ınbışeyiy fariseyaaşe g'axuvuyne g'aravulyçeeşika arayle. Manbışde xıle bazirbı, ts'abı, silahbı eyxhe.
4 Yesu, podziwa zonse zimene zimati zichitike kwa Iye, anatuluka ndi kuwafunsa kuti, “Kodi mukufuna ndani?”
I'sayk'le vuk'lelqa qalesın ats'ava, Mana ögilqa qığeç'u, manbışike qiyghan: – Vuşune t'abala'a?
5 Iwo anayankha kuti, “Yesu wa ku Nazareti.” Yesu anati, “Ndine.” (Ndipo Yudasi womuperekayo anali atayima nawo pamenepo).
Mang'us alidghıniy qele: – Nazaretğançena I'sa. I'see manbışik'le eyhen: – Zı vorna. Mana merıng'une xılyaqa qelena Yahudar manbışika ıxha.
6 Pamene Yesu anati, “Ndine,” iwo anabwerera mʼmbuyo ndi kugwa pansi.
I'see manbışik'le «Zı vornava» uvhumee, manbı yı'q'əlqa qeepxha, ç'iyelqa gizyabaççe.
7 Iye anawafunsanso kuti, “Kodi mukumufuna ndani?” Ndipo iwo anati, “Yesu wa ku Nazareti.”
I'see meed manbışike qiyghanan: – Vuşune t'abal ha'a? Manbışe eyhen: – Nazaretğançena I'sa.
8 Yesu anayankha kuti, “Ine ndakuwuzani kuti Ndine. Ngati inu mukufuna Ine, asiyeni anthu awa apite.”
I'see alidghıniy qele: – Zı şok'le uvhuyn, Zı vornava. Zı t'abal ha'axhee, Zakanbı g'avkke, hudooracen.
9 Izi zinachitika kuti mawu amene Iye anayankhula akwaniritsidwe: “Ine sindinataye ndi mmodzi yemwe mwa iwo amene mwandipatsa.”
I'see ögil uvhuyn cuvab ixhecenva, man eyxhe. Mang'vee ögilycadniy uvhu: «Zas huvuynbışda nenacar agvales harsıl deş».
10 Kenaka Simoni amene anali ndi lupanga analitulutsa ndi kutema nalo wantchito wa wamkulu wa ansembe, nadula khutu lake la kudzanja lamanja. (Dzina la wantchitoyo ndi Makusi).
Şimon-Pyoturuqa g'ılınc ıxha. Man qığayşu xənne kaahinne nukarıle k'ena ı'xı', mang'un sağın k'ırı g'a'adaççen. Mane nukarın do Malx ıxha.
11 Yesu analamula Petro kuti, “Bwezera lupanga mʼchimake! Kodi Ine ndisamwere chikho chimene Atate andipatsa?”
Manke I'see Pyoturık'le eyhen: – G'ılınc cigeeqa gixhxhe! Dekkee Zas huvuyn əq'übayn k'ola ulymoğane?
12 Kenaka gulu la asilikali ndi olamulira wawo ndi akuluakulu a Ayuda anamugwira Yesu. Iwo anamumanga.
Məxür eskeraaşeyiy desteyne xərıng'vee Yahudeeşine g'aravulyçeeşika sacigee I'sa aqqı, g'el-xıl iyt'alan.
13 Poyamba anapita naye kwa Anasi amene anali mkamwini wa Kayafa, mkulu wa ansembe chaka chimenecho.
Mana ts'erre Hannanne k'anyaqa qıkkekka. Hannan Kayafayna abattey ıxha. Mane sen Kayafa xərna kaahiniy vor.
14 Kayafa anali amene analangiza Ayuda kuti kukanakhala kwabwino ngati munthu mmodzi akanafera anthu.
«Milletnemee sa İnsanın qik'uy yugdava» Yahudeeşine ç'ak'ınbışik'le uvhuna Kayafa ina vuc vor.
15 Simoni Petro ndi ophunzira wina ankamutsatira Yesu chifukwa ophunzira uyu amadziwika kwa mkulu wa ansembe. Iye analowa ndi Yesu mʼbwalo la mkulu wa ansembe
Şimon-Pyoturiy sa merna teleba I'sayne qihna əlyhəə vuxha. Xərne kaahinık'le mana teleba ats'ava, mana I'sayka sacigee xərne kaahinne məhleeqa ikkeç'e.
16 koma Petro anadikira kunja pa khomo. Ophunzira winayo amene amadziwika kwa mkulu wa ansembe, anatuluka ndi kuyankhula ndi mtsikana amene anali mlonda wa pa khomo ndi kumulowetsa Petro.
Pyoturmee g'ar akkayne k'ane ulyorzul ıxha. Mane gahıl xərne kaahinık'le ats'ana mana teleba g'aqa qığeç'u akkee ileezarne içiyka yuşan hı'ı, Pyotur aqa akkyayhe.
17 Mtsikanayo anafunsa Petro kuti, “Kodi iwe sindiwe mmodzi wa ophunzira a Munthu uyu?” Iye anayankha kuti, “Ayi, sindine.”
Akkee ileezarne içee Pyoturuke qiyghanan: – Deşxhee, ğunar mane İnsanne telebabışkenane vor? Pyoturee «De'eşva» eyhe.
18 Popeza kunkazizira, anyamata antchito ndi akuluakulu ena anasonkha moto wamakala namawotha atayimirira mozungulira. Petro nayenso anayimirira pamodzi ndi iwo namawotha nawo motowo.
Mık'adava nukaraaşeyiy g'aravulyçeeşe maa'ab ts'a halyaqqı, hiqiy-alla ulyobzur g'ümə abak'a vuxha. Pyoturur manbışde k'ane ulyorzul g'ümə arak'va ıxha.
19 Pa nthawi imeneyi, mkulu wa ansembe anamufunsa Yesu za ophunzira ake ndi chiphunzitso chake.
Mane gahıl Hannanee, kaahinaaşine ç'ak'ınbışde sang'vee, I'sayke telebabışdeyiy Vucee xət qa'ançine hək'ee qiyghan.
20 Yesu anayankha kuti, “Ine ndinayankhula poyera ku dziko lapansi. Nthawi zonse ndimaphunzitsa mʼsunagoge kapena mʼNyumba ya Mulungu kumene Ayuda onse amasonkhana pamodzi. Ine sindimanena kanthu mseri.
I'see mang'us alidghıniy qele: – Zı dyunyeyk'le dyugul hidi'ı uvhu, Yahudeeşin gırgınbı sabıyne sinagogbışeeyiy Allahne Xaasne xət qı'ı. Vuççud Zı dyugulenda uvhu deş.
21 Nʼchifukwa chiyani mukundifunsa Ine? Afunseni amene amamva. Zoonadi akudziwa zimene Ine ndinanena.”
Nya'a Zake qiyghan? Zı uvhuyn g'ayxhiyne insanaaşike qiyghne. Manbışik'le Zı uvhuyn karbı ats'anbı.
22 Yesu atanena izi, mmodzi wa akuluakulu amene anali pafupi anamumenya kumaso. Iye anafunsa kuti, “Mayankhidwe awa ndi woti ndi kuyankha mkulu wa ansembe?”
I'sa cuvab uvhu ç'əvxhayle qiyğa, maa ulyobzurne g'aravulyçeeşine sang'vee Mang'une aq'vays ı'xiyxə. G'aravulyçee qiyghanan: – Xərne kaahinıs məxüdne cuvab qelen?
23 Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine ndanena kanthu kolakwika, chitirani umboni chimene ndalakwa. Koma ngati ndanena zoona, nʼchifukwa chiyani mwandimenya?”
I'see mang'us alidghıniy qele: – Zı qorkura yuşan hidi'ıxhee, eyhe, neniy qotkuda ittevhu? Qotkuda uvhuxheeyid, nya'a Zas ı'xiyxə?
24 Kenaka Anasi anamutumiza Iye, ali womangidwabe, kwa Kayafa, mkulu wa ansembe.
Qiyğa Hannanee I'sa g'el-xıl ayt'ılcar, xənne kaahinne Kayafayne k'anyaqa g'ıxele.
25 Pamene Simoni Petro anali chiyimirire kuwotha moto, anafunsidwa kuti, “Kodi iwe si mmodzi wa ophunzira ake?” Iye anayankha kuti, “Ayi, sindine.”
Şimon-Pyotur g'ar ts'ayisnee ulyorzul g'ümə arak'va ıxha. Mang'uke qiyghanan: – Deşxheene, ğunar Mang'une telebabışdane vor? Mang'vee «De'eşva» alidghıniy qele.
26 Mmodzi wa antchito a mkulu wa ansembe, mʼbale wa munthu amene anadulidwa khutu ndi Petro anamutsutsa iye kuti, “Kodi sindinakuone iwe pamodzi ndi Iye mʼmunda muja?”
Xərne kaahinne nukaraaşina sa, Pyoturee ı'xı' k'ırı g'a'aççuyne insanna xını, maa'ar ıxha. Mane nukaree Pyoturuke qiyghan: – Mang'uka sacigee zak'le ğu dişdiy bağee g'acu?
27 Petro anakananso, ndipo pa nthawi yomweyo tambala analira.
Pyoturee meed gardanaqa alyaat'a deş. Mane gahıl dadal hook'a.
28 Kenaka Ayuda anamutenga Yesu kuchoka kwa Kayafa ndi kupita ku nyumba yaufumu ya bwanamkubwa wa Chiroma. Tsopano kunali mmamawa, ndipo polewa kudetsedwa monga mwa mwambo Ayuda sanalowe mʼnyumba yaufumuyo; iwo anafuna kuti adye Paska.
Qiyğa Yahudeeşine ç'ak'ınbışe I'sa Kayafayne k'anençe Pilatne sarayeeqa qıkkekka. Miç'eed qexhe. Allahne ögil mı'q'ı' qimeebaxhecenva, Peesaxıne otxhuniyked oxhanas əxecenva, manbı co sarayeeqa ikkeebaç'e deş.
29 Choncho Pilato anatuluka napita kwa iwo ndipo anati, “Kodi ndi milandu yanji imene mukumuzenga munthu uyu?”
Mançil-allar Pilat g'aqa manbışde k'anyaqa qığeç'u, eyhen: – Nena bınahne İng'ulqa g'iviyxhe?
30 Iwo anayankha kuti, “Ngati Iye akanakhala kuti si wolakwa, ife sitikanamupereka kwa inu.”
Manbışe Pilatıs alidghıniy qele: – Mang'ul bınah devxhaynxhiy, Mana vasqa qeles deşdiy.
31 Pilato anati, “Mutengeni inu eni ake ndi kumuweruza Iye monga mwa malamulo anu.” Ayuda anatsutsa nati, “Koma tilibe ulamuliro wakupha aliyense.”
Pilatee manbışik'le eyhen: – Mana şosqa alyart'u, vuşde q'aanunbışis sik'ı Mang'us cazaa g'ats'aak'vne. Yahudeeşine ç'ak'ınbışe Pilatık'le eyhen: – Şaqa vuşumecar gik'asda icaaza deşda.
32 Izi zinachitika kuti mawu a Yesu amene anayankhula kusonyeza mtundu wa imfa imene Iye anati adzafe nayo akwaniritsidwe.
Məxüd I'see Vuc nəxüriy q'ik'asva uvhuyn ixhecenva eyxhe.
33 Kenaka Pilato anapita mʼkati mwa nyumba yaufumu nayitanitsa Yesu, ndipo anamufunsa kuti, “Kodi iwe ndi mfumu ya Ayuda?”
Pilat meer cune sarayeeqa ikkeç'u, I'sa qort'ul eyhen: – Yahudeeşina Paççah Ğune?
34 Yesu anafunsa kuti, “Kodi amenewo ndi maganizo anu wokha? Kapena kuti ena anakuwuzani za Ine?”
I'see alidghıniy qele: – Ğu man valed-alqanane eyhe, deşxhee mebınbışene vak'le Yizde hək'ee uvhu?
35 Pilato anayankha kuti, “Kodi iwe ukuganiza kuti ine ndine Myuda? Ndi anthu ako ndi akulu a ansembe ako amene akupereka iwe kwa ine. Kodi walakwanji?”
Pilatee eyhen: – Zı Yahudeençe deş vor. Ğu yizde xılyaqa yiğne milletıniy kaahinaaşine ç'ak'ınbışe quvu. Eyhe, Ğu hucooyiy hı'ı?
36 Yesu anati, “Ufumu wanga si wa dziko lapansi lino. Ukanakhala wa pansi pano, antchito anga akanachita nkhondo kulepheretsa Ayuda kundigwira. Koma tsopano ufumu wanga ndi wochokera kumalo ena.”
I'see mang'us alidghıniy qele: – Yizda Paççahiyvalla ine dyunyeykena deş vob. Yizda Paççahiyvalla ine dyunyeykena vuxhanaxhiy, Yizde yəqqı'linbı Yahudeeşine ç'ak'ınbışde xılyaqa qımelecenva saç'ivkasınbıniy. Yizda Paççahiyvallame inçena deş vob.
37 Pilato anati, “Kani ndiwe mfumu!” Yesu anayankha kuti, “Inu mwalondola ponena kuti, Ine ndine mfumu. Kunena zoona, Ine ndinabadwa chifukwa cha chimenechi, ndipo nʼchifukwa chake ndinabwera mʼdziko lapansi, kudzachitira umboni choonadi. Aliyense amene ali mbali yachoonadi amamvera mawu anga.”
Pilatee Mang'uk'le eyhen: – Ğu manke Paççahne? I'see alidghıniy qele: – Ğu qotkuda eyhe. Zı hək'ene karbışda şahaadat haa'asva uxu, ine dyunyelqa qarı. Vuşuyiy hək'ene sural Zal k'ırı alixhxhesın.
38 Pilato anafunsa kuti, “Kodi choonadi nʼchiyani?” Ndi mawu awa iye anapitanso kwa Ayuda ndipo anati, “Ine sindikupeza mlandu mwa Iye.
Pilatee Mang'uke qiyghan: – Hək'en sura vodunne? Man qiyghıniyle qiyğa, mana meer Yahudeeşisqa qığeç'u, manbışik'le eyhen: – Zak'le Mang'ul nəxbınacab bınah g'ooce deş.
39 Koma ndi mwambo wanu kuti pa nthawi ya Paska, ine ndikumasulireni wamʼndende mmodzi. Kodi mufuna ndikumasulireni ‘Mfumu ya Ayuda?’”
Şoqa ədat vod, Peesaxnang'a zı vuşdemee sa insan g'ekkan. Həşder şos ıkkanxhee, vuşdemee «Yahudeeşina Paççah» g'aykkas?
40 Iwo anafuwula nati, “Ameneyu ayi! Mutipatse ife Baraba!” Barabayo anali wachifwamba.
Manbışe alidghıniy qeleng'a, ts'irbı hı'ı eyhen: – Mana deş, Barabba g'aykke! Barabbamee g'uldur ıxha.

< Yohane 18 >