< Yohane 16 >

1 “Ine ndakuwuzani zonsezi kuti musadzakhumudwe.
«Hambe, jaman itsh t keew it imnetiyatse it giwawok'owa etaatniye.
2 Iwo adzakuchotsani mʼsunagoge mwawo. Kunena zoona, nthawi ikubwera imene aliyense amene adzakuphani adzaganiza kuti akutumikira Mulungu.
Ayhudiyots Ik' k'oni mootse kishder iti gishitno, mank'o itn ud'itu jamwots dab́ Ik'osh bofinirwok'o boosh bí arit aawo weetwe.
3 Iwo adzachita zoterozo chifukwa sanadziwe Atate kapena Inenso.
Hanowere bok'alir nihono taano bodanawotsene.
4 Ine ndakuwuzani izi kuti nthawi ikadzafika mudzakumbukire kuti Ine ndinakuchenjezani kale. Ine sindinakuwuzeni izi poyamba paja chifukwa ndinali nanu.”
Han itsh tkeewiriye bíaawo b́bodor itsh eeg tkeewtsok'o gaw itdekishe.» Jaman haniyere shin itsh keewo tk'aziye itnton t teshtsotsne.
5 “Tsopano Ine ndikupita kwa Iye amene anandituma koma palibe wina mwa inu akundifunsa kuti, ‘Kodi mukupita kuti?’
«Andmó taan woshtsok amishee, b́wotiyalor ititse ‹Eewke niameti› err taan aatitwo aaliye.
6 Muli ndi chisoni kwambiri chifukwa ndakuwuzani zimene.
Jaman itsh t keewtsotse it nibo shiyanon s'eenwtsere.
7 Komatu ndakuwuzani zoona. Ine ndikuti kuli bwino kwa inu kuti ndichoke. Ngati sindichoka, Nkhosweyo sidzabwera kwa inu, koma ngati Ine ndipita, ndidzamutumiza kwa inu.
Taamó arikon aroniye itsh tietiriye, ti amo itsh k'anefe, taa amo t k'azal kup'shitwo itook waratse, taa tiamalmó bín itsh deyitwe.
8 Iye akabwera, adzatsutsa dziko lapansi za uchimo, zachilungamo ndi zachiweruzo.
Bí b́woor morri jangosh, kááw woti jango, angshi jangosho datsatsi ashuwotsi wok'asitwe.
9 Za uchimo, chifukwa anthu sakhulupirira Ine.
Morri jango b́ kitsitiye taan amano bok'azirwoshe.
10 Za chilungamo, chifukwa Ine ndi kupita kwa Atate, kumene simudzandionanso.
Kááw woti jango kish b́ kitsitiye niho maants tiametwonat haniye haniyak taan bek'o it k'azetwoshe,
11 Za chiweruzo, chifukwa wolamulira dziko lino lapansi waweruzidwa tsopano.
Angshi jango kish b́kitsit datsan keewtsoats angshetsoshe.
12 “Ine ndili ndi zambiri zoti ndiyankhule nanu, koma simungathe kuzilandira tsopano.
«Itsh t keewitwo andoor ay keewo detsfe, ernmó and itatse b́mangiti,
13 Koma pamene Iye, Mzimu wachoonadi, abwera, adzakutsogolerani mʼchoonadi chonse. Iye sadzayankhula mwa Iye yekha, adzayankhula zokhazo zimene wamva ndipo Iye adzakuwuzani zimene zikubwera.
Arik wotts Shayiro b́ woor ar jamo maants itn jishitwe. Bí b́ keewitwo b́ shishtsoni bako b́tokk woto b́ k'aztsotse bí shinomaants wotit keewo itsh keewitwe.
14 Iye adzalemekeza Ine chifukwa adzatenga za Ine nadzakudziwitsani.
Tik wottsotse de'er itsh b́keitwotse taan mangitwe.
15 Zonse za Atate ndi zanga. Ichi nʼchifukwa chake Ine ndanena kuti Mzimu Woyera adzatenga kwa Ine zanga kuti muzidziwe.”
Nihok wotts jamo tikee, ‹Tik wottso de'er itsh keewitwe› ti et manshe.
16 Yesu anapitiriza kuyankhula kuti, “Mwa kanthawi kochepa, simudzandionanso, ndipo patatha nthawi pangʼono mudzandionanso.”
«Muk'i it teshiyakon taan be'atste, ando muk'i it teshiyakon taan bek'etute.»
17 Ena a ophunzira ake anati kwa wina ndi mnzake, “Kodi Iye akutanthauza chiyani ponena kuti, ‘Mwa kanthawi kochepa, simudzandionanso,’ ndi ‘ndipo patatha nthawi pangʼono mudzandionanso,’ ndiponso ‘chifukwa ndikupita kwa Atate?’”
B́ danifwotsitse ik ikwots, «Han, ‹Muk'i b́ teshihakon taan be'atste, ando muk'i it teshihakon taan bek'etute, ando aani nihomaants ametuwe› b́ etiru keewo eebi?» ett boatsatseyo bo aateyi.
18 Iwo anapitiriza kufunsana kuti, “Kodi akutanthauza chiyani, ‘kanthawi kochepa?’ Ife sitikumvetsetsa chimene Iye akuyankhula.”
«Eshe han ‹Muk'i b́teshihakon› bí etiru keewo eebi? B́ keewiru keewo danatsone» ett anansh dek't́ boaateyi.
19 Yesu anadziwa kuti ankafuna kuti amufunse za zimenezi, choncho anawafunsa kuti, “Kodi mukufunsana wina ndi mnzake chimene Ine ndimatanthauza pamene ndinati, ‘Mwa kanthawi kochepa simudzandionanso,’ ndi ‘patatha nthawi pangʼono mudzandionanso?’
Iyesuswere bín aatosh bogeyirwok'o dank'rat hank'o boosh bíet, «It atsatseyo it aateyirwo, ‹Muk'i b́ teshiyakon taan be'atste, ando aani múk'ibteshiyakon taan bek'etute, › ti ettsosheya?
20 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti inu mudzalira ndi kubuma pomwe dziko lapansi lidzakhale likukondwera. Inu mudzamva chisoni, koma chisoni chanu chidzasandulika chimwemwe.
Ariko aron itsh etirwe, it eepetutee, kuhitutee, datsanmó genee'uwitwee, it shiyanitute, ernmó it shiyano gene'o maants woneetwe.
21 Mayi akamabereka mwana amamva ululu chifukwa nthawi yake yafika; koma mwana wake akabadwa amayiwala ululu wake chifukwa cha chimwemwe chake chakuti mwana wabadwa mʼdziko lapansi.
Máátsu bshuwor b shambi aawo b́bodtsotse shiyanitwaniye, bshuwihakonmó datsats na'i marmat'o bshuwetsotse bgene'utsatse tuutson bali b kic'o gawratsaniye.
22 Chimodzimodzinso ndi inu. Tsopano ino ndi nthawi yanu yomva chisoni, koma Ine ndidzakuonaninso ndipo inu mudzasangalala, ndipo palibe amene adzachotsa chimwemwe chanu.
Mank'o and it shiyanitute, ernmó taa aani iti bek'etwe, it mac'onwere gene'uitwe, it gene'uwere itatse dek'etwo aaliye.
23 Tsiku limenelo inu simudzandipemphanso kalikonse. Ine ndikukuwuzani zoona kuti Atate anga adzakupatsani chilichonse chimene mudzapempha mʼdzina langa.
«Manots aawots tiyoke eegor k'onratste, ariko arikon itsh etirwe niho tshútson it k'oniyal jam keewo itsh ímetwe.
24 Mpaka tsopano simunapemphe kalikonse mʼdzina langa. Pemphani ndipo mudzalandira, ndipo chimwemwe chanu chidzakhala chathunthu.
Han b́ borfetsosh t shútson eegor ik keewo k'onrafa'atee, it k'oniyal itsh imetwe, mannowere it gene'uo s'een wotitwe.
25 “Ngakhale ndakhala ndikuyankhula mʼmafanizo, nthawi ikubwera imene Ine sindidzagwiritsanso ntchito mafanizo otere koma ndidzakuwuzani momveka za Atate anga.
«Andish b́borfetso jewron itsh keewre, haniyako jewron itsh t keeweraw aawo weetwe, ernmó niho jangosh jam keewo kishde itsh keewitwe.
26 Tsiku limenelo inu mudzapempha mʼdzina langa. Ine sindikunena kuti ndidzapempha Atate mʼmalo mwanu ayi.
Manots aawots tshútson k'onitute, taawere ‹Niho it jangosh k'onitwe› eraatse.
27 Atate mwini anakukondani chifukwa inu mwandikonda Ine ndipo mwakhulupirira kuti Ine ndinabwera kuchokera kwa Atate.
Man eegoshe niho b́tookon iti b́shuntsoshe, nihonwere iti b́shunir taan it shuntsonat Ik'oke twatsok'o it amantsotsne.
28 Ine ndinabwera kuchokera kwa Atate ndi kulowa mʼdziko lapansi. Tsopano ndikulisiya dziko lapansi kubwerera kwa Atate.”
Nihoke keshat datsats waare, ando aaniy datsani k'ayr nihok ametuwe.»
29 Kenaka ophunzira ake anati, “Tsopano mukuyankhula momveka bwino ndi mopanda mafanizo.
B́danifwotswere hank'owa boet, «Hamb! andee jewron b́woterawon shanone n keewi,
30 Tsopano ife tikuona kuti Inu mumadziwa zinthu zonse ndi kuti sipafunika wina aliyense kukufunsani. Mwa ichi ife takhulupirira kuti Inu munachokera kwa Mulungu.”
Nee jamo n dantsok'onat nee konnwor neesh aato t'intso b́geyirawok'o and t'iwintsdek'roone, mansh Ik'oke keshat n waatsok'o amanirwone.»
31 Yesu anawafunsa kuti, “Kodi tsopano mwakhulupirira?”
Iyesuswere boosh hank'o ett bíaaniy, «Andmó amanertya?
32 Koma nthawi ikubwera ndipo yafika, pamene inu mudzabalalitsidwa, aliyense ku nyumba yake. Inu mudzandisiya ndekhandekha. Koma Ine sindili ndekha, pakuti Atate anga ali nane.
It ik ikets it kaat kaaton bad'arr tiyali k'ayitk'rit sa'ato weetwe, b́ sa'atonwere andbodre, ernomó niho taanton b́wottsotse tiyaltanaliye.
33 “Ine ndakuwuzani izi kuti mwa Ine mukhale nawo mtendere. Mʼdziko lapansi mudzakhala nawo mavuto. Koma limbikani mtima! Ine ndaligonjetsa dziko lapansi.”
Han itsh tkeewir tiats deshar jeeno it datsitwok'owa etaatniye, datsanatse it befetsosh gondbek'o itaatse'faee, ernmó shatk'ayere, taa datsani da'adek're.»

< Yohane 16 >