< Yohane 14 >

1 “Mtima wanu usavutike. Khulupirirani Mulungu; khulupirirani Inenso.
“Mvngdwk mvngkula doomabvka,” Jisu bunua minto. “Pwknvyarnvnyi mvngjwng laka okv ngaaka mvngjwng laka.
2 Mʼnyumba mwa Atate anga muli zipinda zambiri. Kukanakhala kuti mulibemo ndikanakuwuzani. Ine ndikupita kumeneko kukakukonzerani malo.
Ngo Abu gv naam tv karchung ngv awgo doodu, okv ngo nonugv lvgabv dooku riku mvpvripv jitebv vngjinv. Minggvdvnam si doorung mabolo ngo nonua svbv mima dvnvpv.
3 Ndipo ndikapita kukakukonzerani malo, ndidzabweranso kudzakutengani, kuti kumene kuli Ineko, inunso mukakhale komweko.
Okv ngo vngla nonugv lvgabv dooku riku nga mvpv ripvro kochingbv, ngo aakur reku okv ngo atuv nonua naareku, vbvrikubolo ngo ogolo doopvdw nonuka dooming gvreku.
4 Inu mukudziwa njira ya kumene Ine ndikupita.”
Nonu chindu ngoogv vngjiku mooku lo vnglwknv lamtv nga.”
5 Tomasi anati kwa Iye, “Ambuye ife sitikudziwa kumene Inu mukupita, nanga tingadziwe bwanji njirayo?”
Tomas ninyia minto, “Ahtu, ngonu chima noogv vngku lamtv nga; vkvlvgabv tolo chaalwk dubv oguaingbv ngonu lamtv nga chinyu dubv?”
6 Yesu anayankha kuti, “Ine ndine njira, choonadi ndi moyo. Palibe munthu angafike kwa Atate popanda kudzera mwa Ine.
Jisu ninyia mirwkto, “Ngo lamtv ngv, jvjv ngv, okv turnammv; ngo gvlokv vngmabv yvvka Abu gvlo vngnyu mare.
7 Mukanandidziwadi Ine, mukanadziwanso Atate anga. Kuyambira tsopano, mukuwadziwa ndipo mwawaona.”
Vjak nonu ngam chimpvku,” nw bunua minto, “Nonu ngoogv Abu nyika chinreku, okv vjak gvlokv nonuka ninyia chireku okv nonu ninyia kaakw pvku.”
8 Filipo anati, “Ambuye, tionetseni Atatewo ndipo ife tikhutitsidwa.”
Pilip ninyia minto, “Ahtu, Abunyi ngonua kaatam labv; si ngonu mvnwng gv mvngnamv.”
9 Yesu anayankha kuti, “Kodi iwe Filipo, ndakhala pakati panu nthawi yonseyi ndipo iwe sukundidziwabe? Aliyense amene waona Ine, waonanso Atate. Tsono ukunena bwanji kuti, ‘Tionetseni Atate?’
Jisu mirwkto, “Pilip, ngo nonua mvngchi kumanamgo lvkobv reming gvkwng kunam vka nonu ngam chimai?” Yvvdw ngam kaadudw hv Abu nyika kaadunv, vbvrikunamv ogulvgabv no Abunyi ngonua kaatam labv vla mindunv?
10 Kodi sukukhulupirira kuti Ine ndili mwa Atate, ndipo Atate ali mwa Ine? Mawu amene Ine ndiyankhula kwa inu si mawu anga okha koma ndi mawu Atate wokhala mwa Ine, amene akugwira ntchito yake.
Ngo Abu gvlo doodu okv Abu ngoogvlo doodu um Pilip no mvngjwng madunvre? Jisu ninyigv lvbwlaksu vdwa mintoku, “Ngoogv nonua gaam minam dvdv ngv, ngo gvlokv aama. Abu, ngoogvlo doonv ninyigv ridung nga atuv ridunv.
11 Khulupirirani Ine pamene ndi kuti Ine ndili mwa Atate ndipo Atate ali mwa Ine. Koma ngati si chomwecho, khulupiriranitu Ine chifukwa cha ntchito zanga zodabwitsa.
Ngam mvngjwng laka ngo vdwlo abu ngoogvlo doodunv okv ngo Abu gvlo doodunv vla minam a. Ho malo, ngoogv rinam a kaagvrila mvngjwng tvka.
12 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene akhulupirira Ine adzachita zimene Ine ndakhala ndikuchita. Iye adzachita ngakhale zinthu zazikulu kuposa zimenezi, chifukwa ndikupita kwa Atate.
Ngo nonua jvjv nga minjidunv: yvvdw ngam mvngjwng dunv hv ngoogv rinam aingbv rire—am, hv kaiyanv goka rire, ogulvgavbolo ngo abu gvlo vngjinv.
13 Ndipo Ine ndidzachita chilichonse chimene inu mudzapempha mʼdzina langa kuti Atate alemekezedwe mwa Mwana.
Okv nonu ngoogv amin bv ogugo kooridw ngo rijire, Abu gv kairungnv jwkrw nga Kuunyilo gvlokv kaatam kunam lvgabv.
14 Ngati mudzapempha kanthu kalikonse mʼdzina langa, Ine ndidzachita.
Nonu ngoogv amin bv ngam ogugo kooridw, ngo um rijire.”
15 “Ngati mundikonda Ine, sungani malamulo anga.
“Nonu nga mvngjwng bolo, nonu ngoogv gamki nama tvjirijire.
16 Ine ndidzapempha Atate, ndipo adzakupatsani Nkhoswe ina kuti izikhala nanu nthawi zonse. (aiōn g165)
Ngo Abunyi koore, okv hv nonua ridur rianv kvvbigo jire, hv nonua dvbvsvngtambv dooming gvvre. (aiōn g165)
17 Nkhosweyo ndiye Mzimu wachoonadi. Dziko lapansi silingalandire Nkhosweyi chifukwa samuona kapena kumudziwa. Koma inu mumamudziwa pakuti amakhala nanu ndipo adzakhala mwa inu.
Hv Dow hv Pwknvyarnv gv jvjv nga kaatam rianv. Nyiamooku v ninyia naarwk nyumare, ogulvgavbolo hv ninyia chima vmalo kaakwma. Vbvritola nonu ninyia chindu, ogulvgavbolo hv nonu gvlo lvkobv doobwngdu okv nonu lo doodu.”
18 Ine sindikusiyani nokha kuti mukhale ana amasiye. Ine ndidzabweranso kwa inu.
“Vdwlo ngo vngro jeka, nonua ngo opin jvbv doomu mare; ngo nonu gvlo aakur reku.
19 Patsala nthawi yochepa dziko lapansi silidzandionanso koma inu mudzandiona. Popeza kuti Ine ndili ndi moyo, inunso mudzakhala ndi moyo.
Nyia mooku hv ngam ayungjvma nga kaapa kumare, vbvritola nonu ngam kaare; ogulvgavbolo ngo turre, okv nonu ka turre.
20 Tsiku limenelo inu mudzazindikira kuti Ine ndili mwa Atate, ndipo inu muli mwa Ine, ndipo Ine ndili mwa inu.
Vdwlo ho aluv lori kudw, nonu chinre ngo Abu gvlo doodu, okv nonu ngoogvlo doodu, ngo oguaingbv nonu gvlo doodudw ho apiabv.”
21 Iye amene amadziwa malamulo anga ndi kuwasunga ndiye amene amandikonda. Wokonda Ine adzakondedwa ndi Atate wanga ndipo Inenso ndidzamukonda ndikudzionetsa ndekha kwa iye.”
“Yvvdw ngoogv gamki nama torwk sudunv okv um tvduridunv hv ngam paknvrinvbv ridunv. Yvvdw ngam pakdunv um ngoogv Abu pakre; ngooka ninyia paktare okv ngo atuv ninyia kaatam sure.”
22 Kenaka Yudasi (osati Yudasi Isikarioti) anati, “Koma Ambuye, nʼchifukwa chiyani mukufuna kudzionetsa nokha kwa ife, osati ku dziko lapansi?”
(Judas Iskariotnyi miyamabv) Judas gunv minto, “Ahtu, no atuv ngonua kaatamre okv nyiamookua kaatam sumare, hv oguaingbv ritv dunv?”
23 Yesu anamuyankha kuti, “Ngati wina aliyense andikonda Ine, adzasunga mawu anga. Atate wanga adzamukonda, ndipo Ife tidzabwera ndi kukhala naye.
Jisu ninyia minrwkto, “Yvvdw ngam pakdunv hv ngoogv tamsar nama tvduridunv. Ngoogv Abu ninyia pakre, okv ngo la Abu ninyi gvlo aala lvkobv dooming gvvre.
24 Iye amene sandikonda Ine sasunga mawu anga. Mawu awa amene mukumva si anga ndi a Atate amene anandituma Ine.
Yvvdw ngam pakma dunv ngoogv tamsar nama tvvmarima dunv. Okv nonugv tvvnam ngoogv tamsar namv ngo gvngvma, vbvritola ngam vngmunv Abu gvlo naapvnv.”
25 “Ndayankhula zonsezi ndikanali nanu.
“Ngo nonua minpvkunv nonuam lvkobv doodula.
26 Koma Nkhosweyo, Mzimu Woyera, amene Atate adzamutumiza mʼdzina langa adzakuphunzitsani zinthu zonse, ndipo adzakukumbutsani zonse zimene ndinakuwuzani.
Ridur rianv, Darwknv Dow, Abu gv ngo amin bv imu kujinam v, nonua tamsarre okv ngoogv nonua minam dvdv nga mvngpa more.”
27 Ine ndikukusiyirani mtendere. Ndikukupatsani mtendere wanga. Ine sindikukupatsani monga dziko lapansi limaperekera. Mtima wanu usavutike ndipo musachite mantha.
“Nonua ngo sarsopoyo nama lvkobv kayu jido; so si ngo atugv sarsopvyo nama nonua jipvnv. Um ngo nyiamooku gv rinam aingbv jima. Mvngdwk mvngkula doomabvka; Busu mabvka.
28 “Inu munamva Ine ndikunena kuti, ‘Ine ndikupita ndipo ndidzabweranso kwa inu.’ Mukanandikonda, mukanasangalala kuti Ine ndikupita kwa Atate, pakuti Atate ndi wamkulu kuposa Ine.
Nonu ngam nonua ‘Ngo vngjinv, vdubv tvvdu, vbvritola ngo nonu gvlo aakur reku,’ nonu ngam pakdu bolo, ngoogv Abu gvlo vngnam ha nonu mvngpure; ogulvgavbolo hv ngam kaiyanv.
29 Ine ndakuwuzani tsopano zisanachitike, kuti zikadzachitika mudzakhulupirire.
Ngo nonua mintam chodunv so gv ogumvnwng si ritv madvbv, vkvlvga vdwlo si rirekudw nonu mvngjwng reku.
30 Ine sindiyankhulanso nanu zambiri nthawi yayitali popeza wolamulira dziko lapansi akubwera. Iye alibe mphamvu pa Ine,
Ngo nonua awgo raami sidubv rinyuma, ogulvgavbolo nyiamookua rigvdakgv nvngv aariku. Hvkvgv jwkrw ngv ngam rigum lamare,
31 koma kuti dziko lapansi lizindikire kuti Ine ndimakonda Atate ndi kuti ndimachita zokhazokha zimene Atate wandilamulira Ine. “Nyamukani; tizipita.”
vbvritola nyiamookuv chirung laka ngo Abunyi pakdunv; vkvlvgalo ngo ogumvnwng ngam ridunv ninyigv ngam minam dvdv nga.” “Aatoka, klvi so mooku lokv vngla kuju.”

< Yohane 14 >