< Yohane 12 >

1 Masiku asanu ndi limodzi Paska asanafike, Yesu anafika ku Betaniya, kumene kumakhala Lazaro, amene Yesu anamuukitsa kwa akufa.
Peesaxıle yixhılle yiğna ögil I'sa Bet-Anyeeqa, Vuce hapt'ıynbışde yı'q'neençe üç'ür qı'ına Lazar eyxhene cigeeqa qarayle.
2 Kumeneko anamukonzera Yesu chakudya cha madzulo. Marita anatumikira pamene Lazaro anali mmodzi wa iwo amene anakhala nawo pa chakudyacho.
Maa'ad I'saynemee otxhuniy hele ıxha. Marteeyid sufranılqa otxhanan haqqa ıxha. Lazarır I'sayka sacigee sufrayne hiqiy-allanbışde yı'q'nee eyxhe.
3 Kenaka Mariya anatenga botolo la mafuta a nadi, onunkhira bwino kwambiri, amtengowapatali; Iye anadzoza mapazi a Yesu napukuta ndi tsitsi lake. Ndipo nyumba yonse inadzaza ndi fungo lonunkhira bwino la mafutawo.
Mayramee mane gahıl sura litralqa ələən, geed gıranın, yugun evanan q'ış alyaat'u, I'sayne g'elybışilqa k'ya'a. Qiyğa məng'ee cene ç'ərbışika Mang'un g'elybı mətta'a. Xavcad q'ışşıne evayn alyaat'a.
4 Koma mmodzi wa ophunzira ake, Yudasi Isikarioti, amene pambuyo pake adzamupereka anati,
I'sayne telebabışde sang'vee, Mana merıng'une xılyaqa qelesde Kariotğançena Yahudee eyhen:
5 “Nʼchifukwa chiyani mafuta awa sanagulitsidwe ndipo ndalama zake nʼkuzipereka kwa osauka?” Mafutawo anali a mtengo wa malipiro a chaka chimodzi.
– Nya'a man q'ış xhebıd vəş dinarıs massa huvu, kar deşinbışis bit'al hidi'ı?
6 Iye sananene izi chifukwa cha kuganizira osauka koma chifukwa anali mbava; ngati wosunga thumba la ndalama, amabamo zomwe ankayikamo.
Mang'vee man cuvab kar deşinbışda haa'ava deş eyhe, sixnariy ıxhayke eyhe. Mang'usqa pılnana q'utye quvu vooxhe, mang'veeyid cus ıkkanne karas mançe pıl alyaat'a ıxha.
7 Yesu anayankha kuti, “Mulekeni. Mafutawa anayenera kusungidwa mpaka tsiku loyika maliro anga.
I'see eyhen: – Mana ı'ğiykar himee'e! Məng'ee man q'ış g'iyniyne yiğıs havacı ıxha. Məxür məng'ee Zı k'eyxhas ixhesın xhinnee qı'ı.
8 Inu mudzakhala ndi osauka nthawi zonse, koma simudzakhala nane nthawi zonse.”
Kar deşinbı gırgıne gahbışilycab şoka vuxhes, Zımee gırgıne gahbışil şoka ixhes deş.
9 Pa nthawi imeneyi gulu lalikulu la Ayuda linadziwa kuti Yesu anali kumeneko, ndipo linabwera, sichifukwa cha Iye yekha koma kudzaonanso Lazaro, amene anamuukitsa kwa akufa.
Gellesde Yahudeeşik'le I'sa maa'ar ıxhay ats'axhxhe. Manbı maqa I'sa g'acesvacar deş, Vucee hapt'ıynbışde yı'q'neençe üç'ür qı'ına Lazar g'aces abı.
10 Choncho akulu a ansembe anakonza njira yoti aphenso Lazaro,
Lazarır-alla gellesde Yahudeeşe hapk'ın, I'says inyam hı'ı. Mançil-alla kaahinaaşin ç'ak'ınbışis Lazar gik'as ıkkiykan.
11 pakuti chifukwa cha iye Ayuda ambiri amapita kwa Yesu ndi kumukhulupirira.
12 Tsiku lotsatira, gulu lalikulu la anthu lomwe linabwera kuphwando linamva kuti Yesu anali mʼnjira kupita ku Yerusalemu.
Qinne yiğıl bayrameeqa abıyne gellesde insanaaşik'le I'sa İyerusalimeeqa ayresva g'ayxhı.
13 Iwo anatenga nthambi za kanjedza ndi kupita kukakumana naye, akufuwula kuti, “Hosana! “Wodala Iye amene akubwera mʼdzina la Ambuye! “Yodala Mfumu ya Israeli!”
Manbışe xurmayn bıtağbı alyaat'u ts'irbı ha'a, Mang'une ögilqa qığeebaç'e. Manbışe eyhen: – Hosanna! Rəbbine doyuka Qarıyng'us şukur vuxhena! İzrailyne Paççahıs şukur vuxhena!
14 Yesu anapeza bulu wamngʼono ndi kukwerapo, monga kunalembedwa kuti:
I'see q'udux t'abal hav'u, çil ilexa. Mane karbışde hək'ee Muq'addasne Otk'unee inəxüd otk'un:
15 “Usachite mantha mwana wamkazi wa Ziyoni; taona mfumu yako ikubwera, itakhala pa mwana wabulu.”
«Sionna yiş, qimeeqən! İleeke, yiğna Paççah sa q'uduxul alixı vor qöö!»
16 Poyamba ophunzira ake sanamvetsetse zonsezi. Koma pomwe Yesu analemekezedwa ndi pamene anazindikira kuti zinthu izi zinalembedwa ndipo kuti anamuchitira Iye.
Ts'etta telebabışilqa vuççud hiyxhar deş. Allahee I'sa axtı qı'iyle qiyğa, Mang'une vuk'lelqa qadıynbı, telebabışe yik'el qalya'a. Mançine hək'ee ögilycadniy Muq'addasne Otk'uniybışee otk'un.
17 Tsopano gulu la anthu lomwe linali naye pa nthawi imene amaukitsidwa Lazaro ku manda linapitiriza kuchitira umboni.
I'see Lazar nyuq'vneençe qort'ul hapt'ıynbışde yı'q'neençe üç'ür qı'iyne gahıl, Mang'une hiqiy-alla sadıyne milletın mançina gaf haa'a.
18 Anthu ambiri, anapita kukakumana naye, chifukwa iwo anamva kuti Iye anachita chizindikiro chodabwitsachi.
Milletık'le I'see man əlaamat haguva g'ayxhı ıxha, mançil-allad millet Mang'une ögilqa adayle.
19 Choncho Afarisi anati kwa wina ndi mnzake, “Taonani, palibe chimene mwachitapo. Anthu onse akumutsatira Iye!”
Mançil-alla Fariseyaaşe sana-sang'uk'le eyhen: – Vuççud yişde xılençe qöö deş. Gırgınbı Mang'uqab qihna əlyhəə!
20 Tsopano panali Agriki ena pakati pa amene anapita kukapembedza ku phwando.
Bayramıs İyerusalimqa ı'bəədatısva abıynbışde yı'q'nee Yunanarıb vuxhaynbı.
21 Iwo anabwera kwa Filipo, wochokera ku Betisaida wa ku Galileya, ndi pempho, nati, “Akulu, ife tikufuna kuona Yesu.”
Manbı Galileyayne Bet-Tsayda şahareençe eyxhene Filippne k'anyaqa hapk'ın, miz k'yaa'a: – Xərna, şak'le I'sa g'aces ıkkan.
22 Filipo anapita kukawuza Andreya; Andreya ndi Filipo pamodzi anakawuza Yesu.
Filipp arı, Andreyk'le eyhen. Andreyir Filippır hapk'ın, mana gaf I'says haa'a.
23 Yesu anayankha kuti, “Nthawi yafika yakuti Mwana wa Munthu alemekezedwe.
I'see alidghıniy qele: – İnsanne Duxayna axtı qexhena gah qabı.
24 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti, ‘Mbewu ya tirigu imakhala imodzi yokha ngati sikugwa mʼnthaka ndi kufa. Koma ngati imfa, imabereka mbewu zambiri.’
Zı şok'le hək'en eyhe, sa suk ç'iyelqa g'a'aypxhı qidevk'eene, vuccab aaxva. Mana qivk'veeme, geed şagav hele.
25 Munthu amene amakonda moyo wake adzawutaya, pamene munthu amene amadana ndi moyo wake mʼdziko lino lapansi adzawusungira ku moyo wosatha. (aiōnios g166)
Cuna ı'mı'r vukkanang'vee, mana avaak'an haa'as. İne dyunyel cune ı'mrena hidyaa'ang'veeme, mana gırgıne gahbışis havaces. (aiōnios g166)
26 Aliyense amene atumikira Ine ayenera kunditsata; ndipo kumene Ine ndili, wotumikira wanga adzakhalanso komweko. Atate anga adzalemekeza amene atumikira Ine.
Şavusiy Zas g'ullux haa'as vukkan, Zaqar qihna qoracen. Zı nyaa ixhee, Yizda nukarır maa'ar ixhes. Şavaayiy Zas g'ullux hav'u, Yizde Dekkeeyib mang'us hı'rmat haa'as.
27 “Moyo wanga ukuvutika tsopano, kodi ndidzanena chiyani? Ndinene kuti Atate pulumutseni ku nthawi ino? Ayi. Chifukwa chimene Ine ndinabwera pa nthawi iyi ndi chimenechi.
Həşde Yizın yik' ulyoyk'al vod. Hucoo Zasse eyhes əxəyee? Deşxheene, «Dek, Zı ine gahıke g'attixhan he'evane!» eyhes? Zı ine gahınemeecar qarı.
28 Atate, lemekezani dzina lanu!” Kenaka mawu anabwera kuchokera kumwamba, “Ine ndalilemekeza, ndipo ndidzalilemekezanso.”
Dek, Yiğın do axtı qe'e! Manke xəənçe ses qayle: – Yizın do axtı qı'iyn, meedıd axtı qa'asın!
29 Gulu la anthu lomwe linali pamenepo litamva linati, “Kwagunda bingu,” ena anati, “Mngelo wayankhula kwa Iye.”
Maa'ab ulyobzurne sabaranbışe eyhen: – Xəybı g'əhətqı'. Mansanbışed eyhen: – Mang'uka malaaik yuşan hı'ı.
30 Yesu anati, “Mawu awa abwera chifukwa cha inu osati chifukwa cha Ine.
I'see manbışis alidghıniy qele: – Man ses Yizdemee deş, vuşdemee qadı.
31 Ino tsopano ndi nthawi yachiweruzo pa dziko lapansi; tsopano olamulira wa dziko lapansi adzathamangitsidwa.
İne dyunyeys məhkama alğahasda gah hipxhırna, in dyunye vuk'lek ıkkekkan iblis g'eheşşesda.
32 Koma Ine, akadzandipachika pa dziko lapansi, ndidzakokera anthu onse kwa Ine.”
Zı ooqa qa'amee, Zı gırgınbı Zalqa ts'ıts'a'as.
33 Iye ananena izi kuti aonetse mmene adzafere.
I'see mane cuvabıka Vuc nəxüriy qik'asva eyhe.
34 Gulu la anthu linayankha kuti, “Ife tinamva kuchokera mʼmalamulo kuti Khristu adzakhala kwamuyaya, nanga bwanji Inu mukunena kuti, ‘Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa?’ Kodi Mwana wa Munthuyu ndani?” (aiōn g165)
Milletın Mang'us alidghıniy qele: – Şak'le Q'aanune g'ayxhiyn, Masixh gırgıne gahbışis axvas. Nya'a Ğu manke «İnsanna Dix ooqa qa'asva» eyhe? İna İnsanna Dix vuşune? (aiōn g165)
35 Kenaka Yesu anawawuza kuti, “Inu mukhala ndi kuwunika kwa nthawi pangʼono. Yendani pamene mukanali ndi kuwunika, kuti mdima usakupitirireni. Munthu amene amayenda mu mdima sadziwa kumene akupita.
Manke I'see manbışik'le eyhen: – Sık'ınna gahnad Nur şol oğa ixhes. Nur vodnang'a iviykre, miç'axiyvalin şu uvqumaaqacen. Miç'axiyvalee iykarang'uk'le vuc nyaqa ark'ıniy ats'a eyxhen deş.
36 Khulupirirani kuwunika, pamene mukanali ndi kuwunika, kuti mukhale ana a kuwunika.” Yesu atamaliza kuyankhula izi, Iye anachoka nabisala kuti asamuone.
Nur vodnang'a Nurus inyam he'e, şu Nurun dixbı vuxhecenva. I'see manva uvhuyle qiyğa, mançe ark'ın dyugulexhena.
37 Ngakhale Yesu anachita zizindikiro zodabwitsa zonsezi pamaso pawo, sanamukhulupirirebe.
I'see manbışde ögil manimeen əlaamatbı hagveeyid, manbışe Mang'ulqa inyam ha'a deş.
38 Izi zinakwaniritsa mawu a mneneri Yesaya kuti: “Ambuye, wakhulupirira uthenga wathu ndani, ndipo ndi kwa yani komwe mkono wa Ambuye wavumbulutsidwa?”
Man karbı, Yeşaya peyğambaree uvhiynbı xhinne, eyxhe: «Rəbb, şi uvhuynçilqa şavaane inyam hı'ı? Şavusne Rəbbina guc gyaagu?»
39 Pa chifukwa cha ichi iwo sanakhulupirire, chifukwa Yesaya ananenanso kuti:
Manbışisse inyam ha'as əxə deşdiy, Yeşaya peyğambaree menne cigee inəxüd uvhuva:
40 “Iye wachititsa khungu maso awo ndi kuwumitsa mitima yawo, kotero kuti iwo sangathe kuona ndi maso awo, kapena kuzindikira ndi mitima yawo, kapena kutembenuka kuti Ine ndikanawachiza.”
«Allahee manbışin uleppı bı'rq' qı'ı, yik'bıd g'ayelqa sak'al hı'ı, uleppışika g'ımececenva, yik'bışisıd haymeexhecenva, Mang'ulqab sivmiyk'alcen manbı yug qee'eva».
41 Yesaya ananena izi chifukwa anaona ulemerero wa Yesu ndi kuyankhula za Iye.
Yeşayayk'le I'sayna axtıvalla g'avcuynçil-alla, man cuvab uvhu Mang'une hək'ee yuşan hı'ı.
42 Komabe pa nthawi yomweyi ambiri ngakhale atsogoleri anakhulupirira Iye. Koma chifukwa cha Afarisi iwo sanavomereze chikhulupiriro chawo chifukwa amaopa kuti angawatulutse mʼsunagoge;
Ç'ak'ınbışde geebınbışe I'salqa inyam he'eeyid, man manbışe ats'axhya'a deş. Fariseyaaşe co sinagogeençe g'e'eebaşeva, manbı qəvəyq'ən vooxhe.
43 pakuti iwo amakonda kuyamikiridwa ndi anthu kuposa kuyamikiridwa ndi Mulungu.
Manbışis Allahee deş, insanaaşe cos q'iymat huvu vukkiykan.
44 Kenaka Yesu anafuwula nati, “Munthu aliyense amene akhulupirira Ine, sakhulupirira Ine ndekha, komanso Iye amene anandituma Ine.
I'see axtıda eyhen: – Zalqa inyam ha'ang'vee Zalqa deş, Zı G'axuvuyng'ulqa inyam ha'a.
45 Iye amene waona Ine, waonanso Iye amene anandituma Ine.
Zı g'eceng'uk'le Zı G'axuvuna g'ece.
46 Ine ndabwera mʼdziko lapansi monga kuwunika, kotero palibe amene amakhulupirira Ine nʼkumakhalabe mu mdima.
Zalqa inyam ha'ana vuşucar miç'axiyvalee ımaxvacenva, Zı dyunyelqa Nur xhinnee qarı.
47 “Ndipo munthu amene amva mawu anga koma osawasunga, Ine sindimuweruza. Pakuti Ine sindinabwere kudzaweruza dziko lapansi, koma kudzapulumutsa.
Şavuk'leyiy Zı uvhuyn g'ayxhı man hidi'ı, Zı mana muhaakima ha'as deş. Zı dyunye muhaakima ha'asva deş, man g'attixhana'asva qarı.
48 Iye amene akana Ine ndipo salandira mawu anga ali ndi womuweruza. Tsiku lomaliza mawu amene ndiyankhulawa adzamutsutsa.
Zı əq'əna qı'ına, Yizın cuvab k'ane qıdya'ana sa karan muhaakima ha'as. Manıd Zı uvhuyn cuvab vod. Nekke qiyğiyne yiğıl mana mançin muhaakima ha'as.
49 Pakuti Ine sindiyankhula mwa Ine ndekha, koma Atate amene anandituma amandilamulira choti ndinene ndi momwe ndinenere.
Zı Zaled-alqa deş uvhu, Zı g'axuvuyne Dekkee hucooyiy eyhesva, nəxüdiy eyhesva Zalqa əmr hav'u.
50 Ine ndikudziwa kuti lamulo lake ndi moyo wosatha. Choncho chilichonse chimene Ine ndinena ndi chimene Atate andiwuza.” (aiōnios g166)
Zak'le ats'an, Mang'una əmr gırgıne gahbışisda ı'mı'r vobna. Mançil-allad Dekkee Zak'le nəxüdiy uvhu, Zı həməxüdıd eyhen. (aiōnios g166)

< Yohane 12 >