< Yohane 12 >
1 Masiku asanu ndi limodzi Paska asanafike, Yesu anafika ku Betaniya, kumene kumakhala Lazaro, amene Yesu anamuukitsa kwa akufa.
Olusiku lwa katanu na imwi ichali ipasaka, Yesu agendele Bethania, anualiga Lazaro, unu asuluye okusoka mu bhafuye.
2 Kumeneko anamukonzera Yesu chakudya cha madzulo. Marita anatumikira pamene Lazaro anali mmodzi wa iwo amene anakhala nawo pa chakudyacho.
Mbe nibhamutekelayo ebyilo bya kegolo eyo na Martha nakeleketa, omwanya ogwo Lazaro aliga ali umwi ku bhaliya bheyanjile kubyilo amwi na Yesu.
3 Kenaka Mariya anatenga botolo la mafuta a nadi, onunkhira bwino kwambiri, amtengowapatali; Iye anadzoza mapazi a Yesu napukuta ndi tsitsi lake. Ndipo nyumba yonse inadzaza ndi fungo lonunkhira bwino la mafutawo.
Mbe Mariamu nagega ratli ya malange ago gakonjelwe kwa nardo inkonde eyobhulambu muno, namubhambaga Yesu ebhigele, na mukubhula ebhigele kwa jifwili jaye; inyumba yona niijula obhulange bha mafuta.
4 Koma mmodzi wa ophunzira ake, Yudasi Isikarioti, amene pambuyo pake adzamupereka anati,
Yuda Iskariote, umwi wa bhaliya abheigisibwa bhaye, unu aliga nenda okumulomela inuku Yesu, naika ati,
5 “Nʼchifukwa chiyani mafuta awa sanagulitsidwe ndipo ndalama zake nʼkuzipereka kwa osauka?” Mafutawo anali a mtengo wa malipiro a chaka chimodzi.
“Kubhaki amafuta ganu gatakakanibwe kwa dinali magana gasatu ni bhabhana abhataka?
6 Iye sananene izi chifukwa cha kuganizira osauka koma chifukwa anali mbava; ngati wosunga thumba la ndalama, amabamo zomwe ankayikamo.
Nawe aikile kutyo atali kubhafyila echigongo abhataka, kwokubha aliga mwifi: niwe omugumya wa isagwa gwa impilya aliga nagegamoga ebyo bhatulamoga okubha byaye wenyele.
7 Yesu anayankha kuti, “Mulekeni. Mafutawa anayenera kusungidwa mpaka tsiku loyika maliro anga.
Yesu anaika ati,”Mumusige atuleo echo alinacho kulwejo okulusi lwo kusikwa lwani.
8 Inu mudzakhala ndi osauka nthawi zonse, koma simudzakhala nane nthawi zonse.”
Omutaka mulinabho siku jona; nawe mutakubha nanye siku jona.”
9 Pa nthawi imeneyi gulu lalikulu la Ayuda linadziwa kuti Yesu anali kumeneko, ndipo linabwera, sichifukwa cha Iye yekha koma kudzaonanso Lazaro, amene anamuukitsa kwa akufa.
Mbe echise chinene cha Bhayaudi bhamenyele ati Yesu aliyo, nibhaja, atali kulwa, Yesu ela nawe bhamulole na Lazaro unu Yesu asuluye okusoka mu bhafuye.
10 Choncho akulu a ansembe anakonza njira yoti aphenso Lazaro,
Nawe abhakulu bha bhagabhisi nibhakola imbisike okumwita Lazaro;
11 pakuti chifukwa cha iye Ayuda ambiri amapita kwa Yesu ndi kumukhulupirira.
Kubha kubwaye bhafu Abhayaudi nibhagenda jebwe nibhamwikilisha Yesu.
12 Tsiku lotsatira, gulu lalikulu la anthu lomwe linabwera kuphwando linamva kuti Yesu anali mʼnjira kupita ku Yerusalemu.
Olusiku lwa kabhili echise chinene bhaliga bhejile kumalwa. bhejile bhongwa ati Yesu kaja Yerusalemu,
13 Iwo anatenga nthambi za kanjedza ndi kupita kukakumana naye, akufuwula kuti, “Hosana! “Wodala Iye amene akubwera mʼdzina la Ambuye! “Yodala Mfumu ya Israeli!”
Bhagegele amatabhi gamakinda no kusoka anja nokugenda okumulamila nibhabhuma chikelele,”Hosana! ana libhando unu kaja kwa lisina lya Lata bhugenyi, Omukama wa Israeli.”
14 Yesu anapeza bulu wamngʼono ndi kukwerapo, monga kunalembedwa kuti:
Yesu nabhona omwana wa isikili nakalinyako lwa kutyo jandikilwe,
15 “Usachite mantha mwana wamkazi wa Ziyoni; taona mfumu yako ikubwera, itakhala pa mwana wabulu.”
“Utobhaya, muyala wa Sayuni; lola, Omukama wao kaja, alinyile omwana wa isikili
16 Poyamba ophunzira ake sanamvetsetse zonsezi. Koma pomwe Yesu analemekezedwa ndi pamene anazindikira kuti zinthu izi zinalembedwa ndipo kuti anamuchitira Iye.
Abheigisibwa bhaye bhatasombokewe emisango ja kubwambilo; Nawe Yesu nakusibwa, niwo nibhechuka okubha emisango jinu andikiwe ati bhakola emisango jinu kumwene.
17 Tsopano gulu la anthu lomwe linali naye pa nthawi imene amaukitsidwa Lazaro ku manda linapitiriza kuchitira umboni.
Mbe liijo lya bhanu abhobhaliga aamwi na Yesu omwanya nibhamubhilkila Lazaro okusoka mufwa, nibhamubhambalila ku bhandi.
18 Anthu ambiri, anapita kukakumana naye, chifukwa iwo anamva kuti Iye anachita chizindikiro chodabwitsachi.
Okubha liijo lya bhanu bhagendele okumulamila kwo kubha bhonguwe ati akolele echibhalikilsho echo.
19 Choncho Afarisi anati kwa wina ndi mnzake, “Taonani, palibe chimene mwachitapo. Anthu onse akumutsatira Iye!”
Abhafalisayo nibhaikana abhene kwa bhene, Lola, woli mutakutula kukola lyona; lola isi yagenda mumwene.”
20 Tsopano panali Agriki ena pakati pa amene anapita kukapembedza ku phwando.
Woli bhalio Abhayunani bhaliga amwi mwa bhaliya abhobhagendaga okulamya kumalya.
21 Iwo anabwera kwa Filipo, wochokera ku Betisaida wa ku Galileya, ndi pempho, nati, “Akulu, ife tikufuna kuona Yesu.”
Bhanu nibhamulubha Filipo, unu asokaga Bethsaida ya Galilaya, nibhamusabwa nibhaika ati,” Lata bhugenyi, ewse echenda okumulola Yesu;
22 Filipo anapita kukawuza Andreya; Andreya ndi Filipo pamodzi anakawuza Yesu.
Filipo nagenda namubwila ati Andrea; Andrea na Filipo nibhagenda nibhamubwila Yesu.
23 Yesu anayankha kuti, “Nthawi yafika yakuti Mwana wa Munthu alemekezedwe.
Yesu nabhasubya naika ati,”Omwanya gwakinga kulwejo omwana wa Adamu akusibwe.
24 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti, ‘Mbewu ya tirigu imakhala imodzi yokha ngati sikugwa mʼnthaka ndi kufa. Koma ngati imfa, imabereka mbewu zambiri.’
Ni chimali, chimali, nabhabwila ati, injuma ya ingano ikalema okugwa ku si nifwa, eiyanja awo yenyele; nawe ikafwa, eibhula amatwasho mafu.
25 Munthu amene amakonda moyo wake adzawutaya, pamene munthu amene amadana ndi moyo wake mʼdziko lino lapansi adzawusungira ku moyo wosatha. (aiōnios )
Unu kenda obhuanga bwaye alibhubhusha; nawe unu katamaganwa obhuanga bwaye mu si munu alibhuonya nolwo obhuanga bwa kajanende. (aiōnios )
26 Aliyense amene atumikira Ine ayenera kunditsata; ndipo kumene Ine ndili, wotumikira wanga adzakhalanso komweko. Atate anga adzalemekeza amene atumikira Ine.
Omunu woona akankolela anye, nandubhe; anye nili eyo omukosi wani labhaga. Omunu woone alankolela, Lata alimuyana echibhalo.
27 “Moyo wanga ukuvutika tsopano, kodi ndidzanena chiyani? Ndinene kuti Atate pulumutseni ku nthawi ino? Ayi. Chifukwa chimene Ine ndinabwera pa nthawi iyi ndi chimenechi.
Wolyanu omwoyo gwani gwasulumbala: anye enaikaki?'Lata, nuukishe omwanya gunu'? Nawe kulwejo nikingila mumwanya gunu.
28 Atate, lemekezani dzina lanu!” Kenaka mawu anabwera kuchokera kumwamba, “Ine ndalilemekeza, ndipo ndidzalilemekezanso.”
Lata, ulikushe lisina lyao.”Mbe lilaka nilija okusoka mulwile niyaika ati,”Nalikusha anye enilikusha lindi.”
29 Gulu la anthu lomwe linali pamenepo litamva linati, “Kwagunda bingu,” ena anati, “Mngelo wayankhula kwa Iye.”
Mbe ebhise byaliga bhimeleguyu yeyi nage nibhogwa nibhaika ati, kugwajuma. Abhandi nibhaika ati,”Malaika aika nage.”
30 Yesu anati, “Mawu awa abwera chifukwa cha inu osati chifukwa cha Ine.
Yesu nasubya naika ati,”Lilaka linu litejile kulwanye nawe ni kubwemwe.
31 Ino tsopano ndi nthawi yachiweruzo pa dziko lapansi; tsopano olamulira wa dziko lapansi adzathamangitsidwa.
Wolyanu okulamula kwa isi inu ilio: Wolyanu omukulu wa isi inu kesibwa anja.
32 Koma Ine, akadzandipachika pa dziko lapansi, ndidzakokera anthu onse kwa Ine.”
Anye nakayanikwa ingulu ya isi, ndifutila bhona kwanye.”
33 Iye ananena izi kuti aonetse mmene adzafere.
Aikile kutyo nolesha okufwa kunu kajokufwa.
34 Gulu la anthu linayankha kuti, “Ife tinamva kuchokera mʼmalamulo kuti Khristu adzakhala kwamuyaya, nanga bwanji Inu mukunena kuti, ‘Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa?’ Kodi Mwana wa Munthuyu ndani?” (aiōn )
Elikofyanya nibhamusubya ati,”eswe chonguwe mubhilagilo ati Kristo kabhalio kajanende. Kawe owaikaki,' Omwana wa Adamu ayanikwe ingulu'? Onu omwana wo munu niga?” (aiōn )
35 Kenaka Yesu anawawuza kuti, “Inu mukhala ndi kuwunika kwa nthawi pangʼono. Yendani pamene mukanali ndi kuwunika, kuti mdima usakupitirireni. Munthu amene amayenda mu mdima sadziwa kumene akupita.
Mbe Yesu nabhabwila ati, “Obwelu bhuchalio amwi nemwe mwanya mutoto Nimulibhate muchali no bwelu, echisute chisige okubhagwatila. Oyo kalibhatila muchisute atakumenya enukaja.
36 Khulupirirani kuwunika, pamene mukanali ndi kuwunika, kuti mukhale ana a kuwunika.” Yesu atamaliza kuyankhula izi, Iye anachoka nabisala kuti asamuone.
Woli muchali no bwelu, mwikilishe obwelu mubhe bhana bho bwelu.”Yesu ejile amala okwaika nagenda jae niibhisa bhasiga kumulola.
37 Ngakhale Yesu anachita zizindikiro zodabwitsa zonsezi pamaso pawo, sanamukhulupirirebe.
Yesu akolele ebhibhalikisho byafu imbele yebwe, bhatamwikilisishe.
38 Izi zinakwaniritsa mawu a mneneri Yesaya kuti: “Ambuye, wakhulupirira uthenga wathu ndani, ndipo ndi kwa yani komwe mkono wa Ambuye wavumbulutsidwa?”
Gukumila omusango gwo mulagi Isaya, aikile ati Lata bhugenyi niga ekilisishe emisango jebwe? No kubhoko kwa Lata bhugenyi kwa sululiwe ga?”
39 Pa chifukwa cha ichi iwo sanakhulupirire, chifukwa Yesaya ananenanso kuti:
Nikwo bhatekilisishe, kubha Isaya aikile lindi,
40 “Iye wachititsa khungu maso awo ndi kuwumitsa mitima yawo, kotero kuti iwo sangathe kuona ndi maso awo, kapena kuzindikira ndi mitima yawo, kapena kutembenuka kuti Ine ndikanawachiza.”
“Abhaofushe ameso, nakola emitima jebwe bhasige kulola kwa meso gebwe no kumenyegesha ne mitima jebwe nibhekilisha anye nikebheulisha
41 Yesaya ananena izi chifukwa anaona ulemerero wa Yesu ndi kuyankhula za Iye.
Isaya aikile ati emisango jinu kwokubha alolele likusho la Yesu naika emisango jaye.
42 Komabe pa nthawi yomweyi ambiri ngakhale atsogoleri anakhulupirira Iye. Koma chifukwa cha Afarisi iwo sanavomereze chikhulupiriro chawo chifukwa amaopa kuti angawatulutse mʼsunagoge;
Nawe, nolwo mubhakulu bhafu bhamwikilisishe Yesu; Nawe kwokubha Abhafarisayo bhatekilisishe bhataja kuilisibwa na sinagogi.
43 pakuti iwo amakonda kuyamikiridwa ndi anthu kuposa kuyamikiridwa ndi Mulungu.
Bhendaga echibhalo cha bhanu kukila echibhalo cha Nyamuanga.
44 Kenaka Yesu anafuwula nati, “Munthu aliyense amene akhulupirira Ine, sakhulupirira Ine ndekha, komanso Iye amene anandituma Ine.
Yesu naikila ingulu naika ati,”Unu kanyikilisha naye, atakwikilisha anye tali unu antumile anye,
45 Iye amene waona Ine, waonanso Iye amene anandituma Ine.
Unu kandola anye kamulola unu antumile.
46 Ine ndabwera mʼdziko lapansi monga kuwunika, kotero palibe amene amakhulupirira Ine nʼkumakhalabe mu mdima.
Anye nejile kubha bwelu bwa isi bhuli munu unu kanyikilisha anye atakwikala muchisute.
47 “Ndipo munthu amene amva mawu anga koma osawasunga, Ine sindimuweruza. Pakuti Ine sindinabwere kudzaweruza dziko lapansi, koma kudzapulumutsa.
Akabha omunu woona atakugwata emisango jani nawe atakujigwata, anye nitakumulamila; okubha nitejile okulamula isi nawe nikishe isi.
48 Iye amene akana Ine ndipo salandira mawu anga ali ndi womuweruza. Tsiku lomaliza mawu amene ndiyankhulawa adzamutsutsa.
Unu kalema anye atakwikilisha emisango jani, unu kamulamula: Omusango gunu naika nigwo gulimulamula ku lusiku lwo bhutelo.
49 Pakuti Ine sindiyankhula mwa Ine ndekha, koma Atate amene anandituma amandilamulira choti ndinene ndi momwe ndinenere.
Okubha anye nitaikile kwo mutima gwani Nawe ni Lata unu antumile, nawe omwene andagiliye jinu ndaika na jinu ndaika.
50 Ine ndikudziwa kuti lamulo lake ndi moyo wosatha. Choncho chilichonse chimene Ine ndinena ndi chimene Atate andiwuza.” (aiōnios )
Anye nimenyele echilagilo chaye ni bhuanga bwa kajanende nawe jinu enaika anye, lwa kutyo Lata ambwiliye, nikwo enaika kwebwe.” (aiōnios )