< Yohane 11 >
1 Tsopano munthu wina dzina lake Lazaro anadwala. Iye anali wa ku Betaniya, mudzi wa Mariya ndi mchemwali wake Marita.
to be then one be weak: ill Lazarus away from Bethany out from the/this/who village Mary and Martha the/this/who sister it/s/he
2 Mariyayo ndi yemwe uja amene anadzoza Ambuye ndi mafuta onunkhira napukuta mapazi ake ndi tsitsi lake. Lazaro wodwalayo anali mlongo wake.
to be then Mary the/this/who to anoint the/this/who lord: God ointment and to wipe off the/this/who foot it/s/he the/this/who hair it/s/he which the/this/who brother Lazarus be weak: ill
3 Choncho alongo ake anatumiza mawu kwa Yesu kuti, “Ambuye, uja amene Inu mumamukonda akudwala.”
to send therefore/then the/this/who sister to/with it/s/he to say lord: God look! which to love be weak: ill
4 Atamva izi, Yesu anati, “Kudwalako safa nako. Koma akudwala kuti Mulungu alemekezedwe; ndi kuti Mwana wa Mulungu alemekezedwe chifukwa cha matendawo.”
to hear then the/this/who Jesus to say this/he/she/it the/this/who weakness: ill no to be to/with death but above/for the/this/who glory the/this/who God in order that/to to glorify the/this/who son the/this/who God through/because of it/s/he
5 Yesu anakonda Marita, mchemwali wake ndi Lazaro.
to love then the/this/who Jesus the/this/who Martha and the/this/who sister it/s/he and the/this/who Lazarus
6 Koma atamva kuti Lazaro akudwala, Iye anakhalabe kumene anali masiku ena awiri.
as/when therefore/then to hear that/since: that be weak: ill then on the other hand to stay in/on/among which to be place two day
7 Kenaka anati kwa ophunzira ake, “Tiyeni tibwerere ku Yudeya.”
then with/after this/he/she/it to say the/this/who disciple to bring toward the/this/who Judea again
8 Ophunzira akewo anati, “Rabi, posachedwa pomwepa Ayuda anafuna kukugendani ndi miyala, koma Inu mukupitanso komweko?”
to say it/s/he the/this/who disciple Rabbi now to seek you to stone the/this/who Jew and again to go there
9 Yesu anayankha kuti, “Kodi sipali maora khumi ndi awiri pa tsiku? Munthu amene amayenda masana sapunthwa, popeza akuona chifukwa cha kuwala kwa dziko lapansi.
to answer (the/this/who *k*) Jesus not! twelve hour to be the/this/who day if one to walk in/on/among the/this/who day no to strike that/since: since the/this/who light the/this/who world this/he/she/it to see
10 Koma amene akuyenda usiku amapunthwa, chifukwa kuwalako alibe.”
if then one to walk in/on/among the/this/who night to strike that/since: since the/this/who light no to be in/on/among it/s/he
11 Iye atatha kunena izi, anapitirira kuwawuza iwo kuti, “Bwenzi lathu Lazaro wagona tulo; koma Ine ndikupita kumeneko kukamudzutsa.”
this/he/she/it to say and with/after this/he/she/it to say it/s/he Lazarus the/this/who friendly/friend me to sleep but to travel in order that/to to awake it/s/he
12 Ophunzira ake anayankha kuti, “Ambuye, ngati wagona adzapeza bwino.”
to say therefore/then the/this/who disciple (it/s/he *N(K)O*) lord: God if to sleep to save
13 Yesu ankayankhula za imfa yake koma ophunzira ake ankaganiza kuti amanena za tulo chabe.
to say then the/this/who Jesus about the/this/who death it/s/he that then to think that/since: that about the/this/who sleep the/this/who sleep to say
14 Ndipo kenaka anawawuza momveka kuti, “Lazaro wamwalira.
then therefore/then to say it/s/he the/this/who Jesus boldness Lazarus to die
15 Ine ndikukondwera chifukwa cha inu kuti kunalibe kumeneko; koma kuti mukakhulupirire tiyeni tipiteko.”
and to rejoice through/because of you in order that/to to trust (in) that/since: that no to be there but to bring to/with it/s/he
16 Pamenepo Tomasi, wotchedwa Didimo, anati kwa ophunzira anzake, “Tiyeni nafenso tipite, kuti tikafere naye pamodzi.”
to say therefore/then Thomas the/this/who to say: call Twin the/this/who fellow disciple to bring and me in order that/to to die with/after it/s/he
17 Yesu atafika, anapeza kuti Lazaro anali atagona mʼmanda masiku anayi.
to come/go therefore/then the/this/who Jesus to find/meet it/s/he four already day to have/be in/on/among the/this/who grave
18 Mudzi wa Betaniya unali pafupi ndi Yerusalemu pa mtunda wosachepera makilomita atatu,
to be then the/this/who Bethany near the/this/who Jerusalem as/when away from stadium fifteen
19 ndipo Ayuda ambiri anabwera kwa Marita ndi Mariya kudzawatonthoza pa imfa ya mʼbale wawo.
(and *k*) much (then *no*) out from the/this/who Jew to come/go to/with (the/this/who *N(k)O*) (about *k*) Martha and Mary in order that/to to encourage it/s/he about the/this/who brother (it/s/he *k*)
20 Pamene Marita anamva kuti Yesu akubwera, anapita kukakumana naye. Koma Mariya anatsala ku nyumba.
the/this/who therefore/then Martha as/when to hear that/since: that (the/this/who *k*) Jesus to come/go to go meet it/s/he Mary then in/on/among the/this/who house: home to sit down
21 Marita anati kwa Yesu, “Ambuye, mukanakhala muli kuno, mlongo wanga sakanamwalira.
to say therefore/then the/this/who Martha to/with the/this/who Jesus lord: God if to be here no if (to die *N(k)O*) the/this/who brother me
22 Koma ine ndikudziwa kuti ngakhale tsopano Mulungu adzakupatsani chilichonse chimene mudzamupempha.”
but and now to know that/since: that just as/how much if to ask the/this/who God to give you the/this/who God
23 Yesu anati kwa iye, “Mlongo wako adzauka.”
to say it/s/he the/this/who Jesus to arise the/this/who brother you
24 Marita anayankha kuti, “Ine ndikudziwa kuti adzauka pa kuukanso pa tsiku lomaliza.”
to say it/s/he (the/this/who *no*) Martha to know that/since: that to arise in/on/among the/this/who resurrection in/on/among the/this/who last/least day
25 Yesu anati kwa iye, “Ine ndine kuuka ndi moyo. Wokhulupirira Ine, angakhale amwalira adzakhala ndi moyo.
to say it/s/he the/this/who Jesus I/we to be the/this/who resurrection and the/this/who life the/this/who to trust (in) toward I/we and if to die to live
26 Aliyense amene ali ndi moyo ndi kukhulupirira Ine sadzamwalira. Kodi iwe ukukhulupirira izi?” (aiōn )
and all the/this/who to live and to trust (in) toward I/we no not to die toward the/this/who an age: eternity to trust (in) this/he/she/it (aiōn )
27 Marita anamuwuza Iye kuti, “Inde Ambuye, ine ndikukhulupirira kuti ndinu Khristu, Mwana wa Mulungu, amene abwera mʼdziko lapansi.”
to say it/s/he yes lord: God I/we to trust (in) that/since: that you to be the/this/who Christ the/this/who son the/this/who God the/this/who toward the/this/who world to come/go
28 Ndipo iye atanena izi anabwerera ndi kukayitana mchemwali wake Mariya namuyankhula monongʼona pambali, nati, “Aphunzitsi abwera ndipo akukuyitana.”
and (this/he/she/it *N(k)O*) to say to go away and to call Mary the/this/who sister it/s/he quietly to say the/this/who teacher be present and to call you
29 Mariya atamva izi, anayimirira mofulumira napita kwa Iye.
that (then *no*) as/when to hear (to arise *N(k)O*) quickly and (to come/go *N(k)O*) to/with it/s/he
30 Tsopano nʼkuti Yesu asanalowe mʼmudzi, koma anali akanali pa malo pamene Marita anakumana naye.
not yet then to come/go the/this/who Jesus toward the/this/who village but to be (still *no*) in/on/among the/this/who place where(-ever) to go meet it/s/he the/this/who Martha
31 Ayuda amene ankamutonthoza Mariya mʼnyumba, anaona mmene iye anayimira mofulumira ndi kutuluka kunja, iwo anamutsata akuganizira kuti ankapita ku manda kukalirira kumeneko.
the/this/who therefore/then Jew the/this/who to be with/after it/s/he in/on/among the/this/who home and to encourage it/s/he to perceive: see the/this/who Mary that/since: that soon to arise and to go out to follow it/s/he (to think *N(K)O*) that/since: that to go toward the/this/who grave in order that/to to weep there
32 Mariya anafika pamalo pamene panali Yesu ndipo atamuona, anagwa pa mapazi ake ndipo anati, “Ambuye mukanakhala muli kuno mlongo wanga sakanamwalira.”
the/this/who therefore/then Mary as/when to come/go where(-ever) to be (the/this/who *k*) Jesus to perceive: see it/s/he to collapse it/s/he (to/with *N(k)O*) the/this/who foot to say it/s/he lord: God if to be here no if me to die the/this/who brother
33 Yesu ataona iye akulira, ndi Ayuda amene anabwera naye akuliranso, anakhudzidwa kwambiri ndi kuvutika mu mzimu.
Jesus therefore/then as/when to perceive: see it/s/he to weep and the/this/who to assemble it/s/he Jew to weep be agitated the/this/who spirit/breath: spirit and to trouble themself
34 Iye anafunsa kuti, “Kodi mwamuyika kuti?” Iwo anayankha kuti, “Ambuye tiyeni mukaone.”
and to say where? to place it/s/he to say it/s/he lord: God to come/go and to perceive: see
to weep the/this/who Jesus
36 Pamenepo Ayuda anati, “Taonani mmene Iye anamukondera Lazaro!”
to say therefore/then the/this/who Jew look! how! to love it/s/he
37 Koma ena a iwo anati, “Iye amatsekula maso a munthu wosaona, kodi sakanakhoza kuletsa kuti munthu uyu asamwalire?”
one then out from it/s/he to say no be able this/he/she/it the/this/who to open the/this/who eye the/this/who blind to do/make: do in order that/to and this/he/she/it not to die
38 Yesu atakhudzidwanso kwambiri anafika ku manda. Manda akewo anali phanga ndipo anatsekapo ndi mwala.
Jesus therefore/then again be agitated in/on/among themself to come/go toward the/this/who grave to be then cave and stone to lay on upon/to/against it/s/he
39 Yesu anati, “Chotsani mwala.” Marita mlongo wa womwalirayo anati, “Koma Ambuye, nthawi ino wayamba kununkha, pakuti wakhala mʼmenemu masiku anayi.”
to say the/this/who Jesus to take up the/this/who stone to say it/s/he the/this/who sister the/this/who (to decease *N(k)O*) Martha lord: God already to stink fourth for to be
40 Kenaka Yesu anati, “Kodi Ine sindinakuwuze kuti ngati iwe ukhulupirira, udzaona ulemerero wa Mulungu?”
to say it/s/he the/this/who Jesus no to say you that/since: that if to trust (in) to see: see the/this/who glory the/this/who God
41 Choncho iwo anachotsa mwalawo. Kenaka Yesu anayangʼana kumwamba ndikuti, “Atate, Ine ndikukuthokozani chifukwa mumandimvera.
to take up therefore/then the/this/who stone (whither to be the/this/who to die/be dead to lay/be appointed *K*) the/this/who then Jesus to take up the/this/who eye above and to say father to thank you that/since: that to hear me
42 Ine ndimadziwa kuti Inu mumandimvera nthawi zonse, koma Ine ndanena izi chifukwa cha anthu amene ayima pano, kuti iwo akhulupirire kuti Inu munandituma Ine.”
I/we then to perceive: know that/since: that always me to hear but through/because of the/this/who crowd the/this/who to stand around to say in order that/to to trust (in) that/since: that you me to send
43 Yesu atanena izi, Iye anayitana ndi mawu ofuwula kuti, “Lazaro, tuluka!”
and this/he/she/it to say voice/sound: voice great to shout Lazarus come out/outside(r)
44 Munthu womwalirayo anatuluka, womangidwa miyendo ndi manja ndi nsalu za ku manda, ndi nkhope yake yokulungidwa nsalu. Yesu anawawuza kuti, “Mʼmasuleni, ndipo muloleni apite.”
(and *k*) to go out the/this/who to die/be dead to bind the/this/who foot and the/this/who hand graveclothes and the/this/who face it/s/he handkerchief to wrap around to say it/s/he the/this/who Jesus to loose it/s/he and to release: permit it/s/he to go
45 Choncho Ayuda ambiri amene anabwera kudzamuchereza Mariya ndi kuona zimene Yesu anachita anamukhulupirira Iye.
much therefore/then out from the/this/who Jew the/this/who to come/go to/with the/this/who Mary and to look at (which *NK(o)*) to do/make: do (the/this/who Jesus *k*) to trust (in) toward it/s/he
46 Koma ena a iwo anapita kwa Afarisi ndi kukawawuza zimene Yesu anachita.
one then out from it/s/he to go away to/with the/this/who Pharisee and to say it/s/he which to do/make: do (the/this/who *ko*) Jesus
47 Kenaka akulu a ansembe ndi Afarisi anayitanitsa msonkhano wa akulu olamulira. Iwo anafunsa kuti, “Kodi ife tikuchita chiyani? Pano pali munthu uyu akuchita zizindikiro zodabwitsa zambiri.
to assemble therefore/then the/this/who high-priest and the/this/who Pharisee council and to say which? to do/make: do that/since: since this/he/she/it the/this/who a human much to do/make: do sign
48 Ngati ife timuleka kuti apitirize chotere, aliyense adzamukhulupirira Iye, ndipo kenaka Aroma adzabwera ndi kudzatenga malo athu pamodzi ndi dziko lathu.”
if to release: leave it/s/he thus(-ly) all to trust (in) toward it/s/he and to come/go the/this/who Roman and to take up me and the/this/who place and the/this/who Gentiles
49 Kenaka mmodzi wa iwo, dzina lake Kayafa, amene anali mkulu wa ansembe chaka chimenecho, anayankhula kuti, “Inu simukudziwa kanthu kalikonse!
one then one out from it/s/he Caiaphas high-priest to be the/this/who year that to say it/s/he you no to know none
50 Inu simukuzindikira kuti kuli bwino kwa inu kuti munthu mmodzi afe mʼmalo mwa anthu kusiyana ndi kuti mtundu wonse uwonongeke.”
nor (to count *N(k)O*) that/since: that be profitable (you *N(K)O*) in order that/to one a human to die above/for the/this/who a people and not all the/this/who Gentiles to destroy
51 Iye sananene izi mwa iye yekha, koma monga mkulu wa ansembe chaka chimenecho ananenera kuti Yesu anayanera kufera mtundu wa Ayuda,
this/he/she/it then away from themself no to say but high-priest to be the/this/who year that to prophesy that/since: that to ensue (the/this/who *k*) Jesus to die above/for the/this/who Gentiles
52 ndipo osati mtundu okhawo komanso kwa ana ena a Mulungu onse obalalikana, kuti awabweretse pamodzi ndi kuwapanga kukhala amodzi.
and no above/for the/this/who Gentiles alone but in order that/to and the/this/who child the/this/who God the/this/who to scatter to assemble toward one
53 Choncho kuyambira tsiku limeneli iwo anakonzekera za kuti amuphe.
away from that therefore/then the/this/who day (to plan *N(k)O*) in order that/to to kill it/s/he
54 Chifukwa cha ichi Yesu sanayendenso moonekera pakati pa Ayuda. Mʼmalo mwake Iye anapita ku chigawo cha kufupi ndi chipululu, ku mudzi wa Efereimu, kumene Iye anakhalako ndi ophunzira ake.
(the/this/who *no*) therefore/then Jesus no still boldness to walk in/on/among the/this/who Jew but to go away from there toward the/this/who country near the/this/who deserted toward Ephraim to say: call city and there (to stay *N(k)O*) with/after the/this/who disciple (it/s/he *k*)
55 Nthawi ya Paska wa Ayuda itayandikira, ambiri anakwera kupita ku Yerusalemu kuchokera ku madera a ku midzi chifukwa cha mwambo wa kuyeretsedwa Paska asanafike.
to be then near the/this/who Passover lamb the/this/who Jew and to ascend much toward Jerusalem out from the/this/who country before the/this/who Passover lamb in order that/to to purify themself
56 Iwo anapitiriza kumufunafuna Yesu, ndipo pamene ankayimirira mʼbwalo la Nyumba ya Mulungu anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Kodi ukuganiza chiyani? Kodi Iye sabwera konse kuphwando?”
to seek therefore/then the/this/who Jesus and to say with/after one another in/on/among the/this/who temple to stand which? to think you that/since: that no not to come/go toward the/this/who festival
57 Koma akulu a ansembe ndi Afarisi anapereka lamulo kuti ngati wina aliyense adziwe kumene kunali Yesu, iye akawawuze kuti akamugwire.
to give then (and *k*) the/this/who high-priest and the/this/who Pharisee (commandment *N(K)O*) in order that/to if one to know where? to be to disclose that to arrest/catch it/s/he