< Yobu 7 >

1 “Kodi munthu sakhala ndi ntchito yowawa pa dziko lapansi? Kodi masiku ake sali ngati munthu waganyu?
Nemde szolgálati ideje van a halandónak a földön, és mint a béres napjai olyanok a napjai!
2 Monga ngati kapolo wolakalaka mthunzi wa nthawi yamadzulo, kapena ngati munthu waganyu woyembekezera malipiro ake,
Mint rabszolga, ki liheg árnyék után, s mint a zsoldos, ki reményli munkabérét:
3 choncho ine ndapatsidwa nthawi yongovutika pachabe, ndiponso usiku wamasautso wapatsidwa kwa ine.
úgy kaptam én örökbe bajnak hónapjait és szenvedésnek éjszakáit rendelték nekem.
4 Ndikamagona ndimaganiza kuti, ‘Kodi kucha liti?’ Usikuwo umatalika ndipo sindigona tulo mpaka mmawa.
Ha lefeküdtem, azt mondom: mikor kelek fel, és nyúlik az este és jóllakom a hánykódással szürkületig.
5 Thupi langa ladzala mphutsi ndi zipsera, khungu langa langʼambika ndipo likutuluka mafinya.
Magára öltött húsom férget és porgöröngyöt, bőröm felfakadt s megevesedett.
6 “Masiku anga ndi othamanga kupambana makina wolukira nsalu, ndipo amatha wopanda chiyembekezo.
Napjaim gyorsabbak a vetélőnél, s remény nélkül enyésztek el.
7 Inu Mulungu kumbukirani kuti moyo wanga uli ngati mpweya; sindidzaonanso masiku achisangalalo.
Gondolj rá, hogy lehelet az életem, jót nem fog többé látni a szemem;
8 Amene akundiona tsopano akundiona; mudzandifunafuna koma sindidzapezekanso.
nem pillant meg engem nézőm szeme, szemeid rajtam vannak, de nem vagyok.
9 Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka, momwemonso munthu amene walowa mʼmanda sabwerera. (Sheol h7585)
Felhő elenyészett és eltűnt: úgy ki alvilágba száll, nem jöhet fel, (Sheol h7585)
10 Iye sadzabweranso ku nyumba kwake ndipo onse omudziwa adzamuyiwala.
nem tér vissza többé házába és nem ismer rá többé az ő helye.
11 “Nʼchifukwa chake ine sindidzakhala chete; ndidzayankhula mopsinjika mtima, ndidzadandaula mowawidwa mtima.
Én sem tartóztatom számat, hadd beszélek lelkem szorultában, hadd panaszkodjam lelkem keservében!
12 Kodi ine ndine nyanja kapena chirombo chamʼnyanja kuti inu mundiyikire alonda?
Tenger vagyok-e avagy szörnyeteg, hogy őrséget vetsz reám?
13 Pamene ndikuganiza kuti ndidzapeza chitonthozo pa bedi panga ndipo pogona panga padzachepetsa madandawulo anga,
Ha azt mondom: majd megvigasztal ágyam, panaszomat viselnem segít fekvőhelyem:
14 ngakhale nthawi imeneyo mumandiopseza ndi maloto ndi kundichititsa mantha ndi masomphenya,
akkor rémítgetsz engem álmokkal és látomások által ijesztesz engem.
15 kotero kuti ndimalakalaka kudzikhweza kapena kufa, kupambana kupirira zowawa zimene ndikuzimva mʼthupi mwanga.
Választotta lelkem a megfulladást, a, halált inkább csontjaimnál.
16 Ine ndatopa nawo moyo wanga; sindingakonde kukhala moyo nthawi zonse. Ndisiyeni ndekha pakuti moyo wanga ulibe tanthauzo.
Megvetettem: nem örökké élek; hagyj föl velem, mert lehelet a napjaim!
17 “Kodi munthu nʼchiyani kuti muzimuganizira chotere, kuti muzisamala zochita zake,
Mi a halandó, hogy nagyra tartod, s hogy reá fordítod szívedet,
18 kuti muzimusanthula mmawa uliwonse ndi kumamuyesa nthawi yonse?
és reá gondolsz reggelenként, perczenként megvizsgálod őt?
19 Kodi simudzaleka kumandizonda kuti ndipezeko mpata wopumula?
Meddig nem tekintesz el tőlem, nem eresztesz el, míg nyálam lenyelhetem?
20 Ngati ine ndachimwa, ndachita chiyani kwa Inu, Inu wopenyetsetsa anthu? Chifukwa chiyani mwachititsa kuti ndikhale ngati choponyera chandamale chanu? Kodi ndasanduka katundu wolemera kwa Inu?
Vétettem: mit cselekszem neked, emberőrző? Miért tettél engem támadásul magadnak, hogy önmagamnak terhére lettem?
21 Chifukwa chiyani simukundikhululukira zolakwa zanga ndi kundichotsera machimo anga? Pakuti posachedwa ndilowa mʼmanda; mudzandifunafuna ine koma simudzandionanso.”
S mit nem bocsátod meg; bűnömet s nem veszed el vétkemet? Mert most porban feküdném, keresnél engem és nem volnék.

< Yobu 7 >